A ZIKHALE NG'OMA UKU NDIYE KWATENTHA🙌🙌🙌 TAMVANI MFUNDO ZOMWE ABWELA NAZO

  Рет қаралды 39,020

HOT 265

HOT 265

23 күн бұрын

Пікірлер: 540
@UseniMailosi
@UseniMailosi 21 күн бұрын
Malawi chikangawa party
@MaxWell-d7o
@MaxWell-d7o 21 күн бұрын
😂😂😂
@Allan-bk1
@Allan-bk1 21 күн бұрын
😂😂😂😂😂
@ackimchindimba9912
@ackimchindimba9912 21 күн бұрын
Mudyeleni apapa ndalama ziyamba kuphweka bas ndi kampeniyi tiyeni tiwadyele koma tonse ndikudziwa kuti ndife APM
@corretabanda7685
@corretabanda7685 21 күн бұрын
Nyama za mmanyumba mwanu. God is good and his eyes can see even in the heart of everyone. It will not work in the Name of Jesus
@anniedennis7127
@anniedennis7127 21 күн бұрын
Ng'ona zodya anthu zingalamulire anthu
@user-wq3dh1ly2o
@user-wq3dh1ly2o 20 күн бұрын
Olo patavuta bwanji simungalamulileso dziko la malawi chifukwa munataya chipangano ambuye sangalole kuti mutilamulile anthu akupha inu
@Sammy-vb1ed
@Sammy-vb1ed 21 күн бұрын
Mudzina la yesu krist ndikupemphera kut uone zowawawa zikhale
@MeleckDennis-vg3bv
@MeleckDennis-vg3bv 21 күн бұрын
Zopusa zokhazokha mfiti za anthu,kwanu kwathapo agalu inu
@JumaGadaff
@JumaGadaff 14 күн бұрын
Bwana kuvota tidzavota koma dziwani kuti muli ndi mulandu ku chikangawa zikomo mulungu ankhale Nanu amen 🙏🙏🙏🙏
@user-wu4tl2yn9e
@user-wu4tl2yn9e 21 күн бұрын
Before kuvota aliyense azizakumbuka kuchikangawa
@CatherineDesire
@CatherineDesire 21 күн бұрын
Eish ndipo 😭😭😭
@BrunoMbewe-xj1yy
@BrunoMbewe-xj1yy 19 күн бұрын
Ndangothokoza kuti mene mumampephelamo mu Mpephero lanu nonse simuna mutchulemo Yesu khristu.Zaoneka kuti inuyo mwazi wayesu simunauziwe mene munagwilira ntchito, pitilizani kugwira ntchito zakumidimazo.
@Gmtmphats124gy
@Gmtmphats124gy 21 күн бұрын
Akanakhala kuti mulungu amalanga mpompo mpompo akanakuthilan moto pasokhano wanu omweo
@ChristopherKawilam
@ChristopherKawilam 21 күн бұрын
Ngat boza bro
@giftmaliwa2385
@giftmaliwa2385 21 күн бұрын
Za make Dzana this new generation
@spargomw
@spargomw 21 күн бұрын
Zikhale Ng'oma😂😂😂😂 tsitsi muzipesako tisamakugemuleni zonse😂😂
@PatriciaMbewe-xn7ke
@PatriciaMbewe-xn7ke 21 күн бұрын
😂😂😂😂😂
@MaryNyirenda-nq3mh
@MaryNyirenda-nq3mh 21 күн бұрын
Kukhwima afiti
@nadiahPhiri
@nadiahPhiri 21 күн бұрын
Umfiti sizinthu
@ephraimmbiza9727
@ephraimmbiza9727 19 күн бұрын
Most important thing is that you know yourself that you will not come back in government
@user-cd4df3vg4y
@user-cd4df3vg4y 21 күн бұрын
Dzigawenga dzawanthu anthu akupha inuuu ng'ona zomwe mwachita pakupha abale athu asanu ndi anayi aja kuchikangawa dziko lonse lapansi ladziwa choonadi chifukwa ma German aja anenana zonse kuti black box inali ku palace.Ndipo anenaso kuti ndichiwembu chomwe munakonza.Pomwe inu muli pheee kufuna kutiuza bodza, ife tadziwa kale ndipo muyaluka
@AminaPhiri-pp9tw
@AminaPhiri-pp9tw 21 күн бұрын
Mukumbukeni chilima amene munamupha uja azikhale ng.oma ndipo zimu wake ukufinyeni ndipo khalira pomwe
@sanlakedickson6780
@sanlakedickson6780 21 күн бұрын
ana asatana awa Mzimu wa chilima ukuvutitsani
@juntoiman
@juntoiman 21 күн бұрын
Pathako panu nonse Zikhale Ng'oma pantumbo pako wamva
@user-eg8wx8oi5z
@user-eg8wx8oi5z 21 күн бұрын
Now it makes sense kod nkhumbai Nd mtumbuka eti😂😂
@kinggasperagain
@kinggasperagain 21 күн бұрын
Kweni Malawi inasoka ivinthe kuwina waka nbwe chikurya waka ndalama
@PaulMwaona-kh1fj
@PaulMwaona-kh1fj 21 күн бұрын
Ubwino wake achinyamata alipo ambili kunjaku,apapa pachulukana makolo otamba
@HassanMbalaka-gb5sv
@HassanMbalaka-gb5sv 21 күн бұрын
Palinyimbo inayake amat paulendooo paulendooo aaaayeee paulendoooo. Awakwao kwantha
@BittonRashid
@BittonRashid 20 күн бұрын
Aye aye paulendo tulinkwaula tulinkwaula kkkkkkk mfundo
@user-sh1rj3ol3t
@user-sh1rj3ol3t 21 күн бұрын
But tu Laz has failed Malawians way more than APM
@ustintembo
@ustintembo 21 күн бұрын
Ndipo inu mmm..
@peterjoshua2595
@peterjoshua2595 19 күн бұрын
100% sure
@user-fi7ko7bl6f
@user-fi7ko7bl6f 21 күн бұрын
Mukuzinamiza agalu Inu za kumachende, azimai nonse Nyini zanu zamanu,mugawane nonse phwala limodzi limodzi agalu okupha
@user-yp5cj2xb9y
@user-yp5cj2xb9y 21 күн бұрын
😂😂😂😂 koma 😂😂
@SphiweMalata
@SphiweMalata 21 күн бұрын
😂😂😂eeeh koma tikuyenda otopa kale
@PreciousBandah-l2r
@PreciousBandah-l2r 16 күн бұрын
Makape inu
@MisheckAselo
@MisheckAselo 21 күн бұрын
Ndimamva chisoni ndi anthu apanda nzeru ndikumanamiza anthu, mwaba zakwana azikhale ng'oma 😮
@zondanitzulumusicfly.5202
@zondanitzulumusicfly.5202 21 күн бұрын
Adziwa kuti babiloni is falling.
@rabisonpias5131
@rabisonpias5131 21 күн бұрын
“Akuti kumabwera ndalama “ ndalama za misonkho yanu zomwe zija ndi zimenezo. M’malao momagura mankhwala mzipatalaa , akungotafuna ndi Ma families awo
@IssacMateyo
@IssacMateyo 21 күн бұрын
Amuna mutu wake ometa ngati chiboliwo Muthu osokonezayo zazi
@EphraimNaveya-hz1du
@EphraimNaveya-hz1du 13 күн бұрын
Za ziiiiiii afiti simungazawine muli ndi magazi kale
@ChilangoNdalama
@ChilangoNdalama 21 күн бұрын
Suiona vote yanga Chaka chamawa ndangokudyera aise
@JuniorHala-vf9ov
@JuniorHala-vf9ov 21 күн бұрын
Viskulu vinu kwacha ninkhuni mpakana kupemphela pamusonkhano apo naumo wanthu wakutambulila namwe kuzomelezganga kwacha chitima chikukolana kweni in fact Mose imwe mukukondwa na mcp Mavi yinu
@joyahmedjoma4615
@joyahmedjoma4615 20 күн бұрын
Ine kunkhara iwe president bola ndifele kokuno ku south Africa wallah wosantha kuyankhura ngat iwe paliolo lenu mwenjo
@LekkttarKhembo-or1tx
@LekkttarKhembo-or1tx 18 күн бұрын
Zitsiru za Malawi zikhale chakwera nonse ndinu osadura ndipo mumanukha kabudula mwanumo mukutinyasa tu
@BeliLikhola
@BeliLikhola 16 күн бұрын
muuzeni chilungamo ameneyo, chigawenga ameneyo
@user-uc9qk7ci2v
@user-uc9qk7ci2v 21 күн бұрын
Taonani zinkhopezo ungokhala ngatinsonkhano wa afititu
@user-kh2bi8rk1d
@user-kh2bi8rk1d 21 күн бұрын
Kkkkkkkkkkkkkkkkkkkkmmmm
@Fatima-f5c
@Fatima-f5c 21 күн бұрын
Misokhano yanuyo muzipangila m,manyumba mwanumo Koma kunjaku ndithu tikugendani 2025 iwa alia
@yunuschiutula
@yunuschiutula 21 күн бұрын
😂😂
@user-lp8wj3vq4x
@user-lp8wj3vq4x 21 күн бұрын
Sure
@hesbaluku7281
@hesbaluku7281 21 күн бұрын
😂😊
@kingsleyhopematchaya5184
@kingsleyhopematchaya5184 21 күн бұрын
Mugenda kangati mmalo mogwira tchito kt zikuthandizeni koma kakaka zithu zoti sizikupatsani ndalama kagendeni tione amene akakhale ku chipatala ndani
@Blessings-td4cr
@Blessings-td4cr 20 күн бұрын
Mpake muzipangira munyumba campaign,,, chibadwireni mfiti sindinkaidziwa ,,koma Malawi tiona zithu.
@YohaneChitseko
@YohaneChitseko 20 күн бұрын
Manje mapephero amene chabe mulungu sangamve anthu okupha ngati inu
@chrisboyce2
@chrisboyce2 21 күн бұрын
Umphawi ndi matenda Zoonadi ( ife kuno ku Ntcheu sitikupanga nawo zimenezi popeza ABIYENI ndi aja munatichotsera aja ...)
@ChikumbutsoDzukwa
@ChikumbutsoDzukwa 21 күн бұрын
Munamizana udya Galu amawawa muziona this is new generation
@lucianogeoffrey4275
@lucianogeoffrey4275 21 күн бұрын
Koma mzimu wa Chilima uli pambuyo panu muyambila kugwa ku convention komko agalu inuu😢😢
@user-wg8tp8in1v
@user-wg8tp8in1v 21 күн бұрын
Apa ponkha ndikupempha Chonde Azikhale asasankhidwe pampandowo
@BrightNyoni-yd4ip
@BrightNyoni-yd4ip 20 күн бұрын
Gulu iwe usamaseweletsa dzina la yesu nkhumba iwe
@BashiruIbrahima-h6z
@BashiruIbrahima-h6z 21 күн бұрын
Kodi awa udindo wawo uja akuwuona kuchepa?? I'm feel sorry kwa manganya
@henryphiri6100
@henryphiri6100 21 күн бұрын
Manganya ndi mbuzi.amuthanso ngati saulos.nzeru za ma Rwanda amenewa nzoipa
@Sammy-vb1ed
@Sammy-vb1ed 21 күн бұрын
The savage politicians, we as malawians we don't need you anymore. Anthu atsankho, kupha komanso katangale.
@MarriamBakalie
@MarriamBakalie 21 күн бұрын
Manganya beware upita ngati chilima those r the same people who killed chilima with the same position they r nt happy with u take care
@ShabaniKuswere
@ShabaniKuswere 21 күн бұрын
Aaaa! Tadzingopani zanuzo zotchula Bible_zo ai siyani ndichibwana chachikulu
@GraceZumazuma
@GraceZumazuma 21 күн бұрын
Chikangawa party, okupha Inu muganiza asakudziwa ndani
@Zamwano
@Zamwano 21 күн бұрын
Ma suit ake amenewo chingawine ichoo 😅
@millionsenenje5010
@millionsenenje5010 21 күн бұрын
Mr Kamuyambeni ndiinu bambo wanga koma pena pake mhhhhhhh
@MusaKazembe-b1d
@MusaKazembe-b1d 17 күн бұрын
They are not even ashamed 😮
@CharlesMongola-jw7sk
@CharlesMongola-jw7sk 20 күн бұрын
Pepani mfundo zanu zopusazo musaphenso Manganya,afiti inu
@user-tw2zf7bj3e
@user-tw2zf7bj3e 21 күн бұрын
Manganya waziwonera wekha kuti iweyo komanso utm sakufunani uziganizile
@RobertChisenga-ci2mq
@RobertChisenga-ci2mq 21 күн бұрын
Do you think karonga's ndizitsilu? Poti kukaronga kuliso mbudzi ndizomwe zilikumenekozo
@IshumaliMakajunior
@IshumaliMakajunior 20 күн бұрын
Ndipo lnu mukanadziwa mene tikuvera
@JackNagoli
@JackNagoli 21 күн бұрын
Let them talk guys ndipo apange ma plan awowo km ubiwno wake malawi siwaathu atatu tiyeni tikakumane chaka chamawa basi khani ndi vote not to talk too much angochedwa nazo
@user-mq2or1lz8h
@user-mq2or1lz8h 21 күн бұрын
😢😢😢😢oooh he has confirmed that this is serious business 😢😢😢rip SKS
@FrancisNyayi
@FrancisNyayi 21 күн бұрын
My pipo tiyenda bwanji 😢 koma able
@SolomonNjolomole
@SolomonNjolomole 21 күн бұрын
Akulu awa ndi achitsilu kwambiri ndi azizawo onsewo kumeneko
@CatherineDesire
@CatherineDesire 21 күн бұрын
Xx2
@frankndawandawa6666
@frankndawandawa6666 21 күн бұрын
kutiseweretsatu Amalawi uku akuona ngat taiwala kale nthawi yomweyi
@pacharokoloviko1694
@pacharokoloviko1694 19 күн бұрын
Mayankhulidwe ake amenewa anthu aphanako uku
@FrancisNyayi
@FrancisNyayi 21 күн бұрын
Mayo mayo chitumbuka sitikunva yankhurani chichewa
@CannyMpehla-d1s
@CannyMpehla-d1s 21 күн бұрын
koma malawi waoladi ng'omaso ikhale vp kkkkkkkk
@user-mq2or1lz8h
@user-mq2or1lz8h 21 күн бұрын
😢😢😢😢 mpakana kumutchula mulungu nyasi ngati?😢😢😢😢😢😢
@DeliaKaduya
@DeliaKaduya 21 күн бұрын
Azimai opusa inu mxiew, kuziwachera achamanu ife tidakagonabe, Kuvotera MCP kuli ngati kuyenda maliseche koma utavala panti, mpakaso zikhale nkukhaka VP ndiye zamapipotu! Shupiti zanu
@user-ot8no9ex2z
@user-ot8no9ex2z 21 күн бұрын
Azakuvoterani ndi ambuyanu ndithu nsonkhani umakhala ndi anthu awiliwo kuousatu uko bwanji manyazi zimvereni chisoni
@LindaNkwazi
@LindaNkwazi 18 күн бұрын
U r still remembering chikangawa
@user-ph3zy9ox7d
@user-ph3zy9ox7d 21 күн бұрын
Inu munthuyu ngoopsa chonchi😮 is he a human being??
@TroubleKatsala-jp2li
@TroubleKatsala-jp2li 21 күн бұрын
Anthuwa apengamisala simukuona zimene akuchita tiyeni tiwadyele koma vote osawapatsa
@georgemponda
@georgemponda 21 күн бұрын
Mbuli izi😂😂😂😂 Zikhalebg'oma nde panja penipeni
@VictoriaWilly
@VictoriaWilly 21 күн бұрын
Kunamizana ndi kosavuta, zinamizanani
@alexgweje8610
@alexgweje8610 21 күн бұрын
Mulibe manyanzi anthu okupha inu 😢
@GanizaniKamvazaana
@GanizaniKamvazaana 18 күн бұрын
Aaaa dzitsiru dza athu kunamizana kukhwapa kwanu nonse
@sharifujoe7633
@sharifujoe7633 21 күн бұрын
Uyu sikhale ngoma same like idi ameen
@isaihmagani5697
@isaihmagani5697 16 күн бұрын
Apa akunena zoona Zikhale Pali zambiri zakhara zuchitika, nde kusankha mwachibwana MCP pa mpando itha kuchokapo
@HopeMakoka
@HopeMakoka 21 күн бұрын
Akabwerstsa ndalamazo landirani guys Koma zodzalamuliranso awa mmmmmm Kumwamba kudzatsika pansi
@Sammy-vb1ed
@Sammy-vb1ed 21 күн бұрын
Azikhaleo kwaona nkhopeyo ngati muru wamanyi afisi 😂😂😂😂😂😂.
@user-ee6be5kl5o
@user-ee6be5kl5o 21 күн бұрын
Ndiye. MCP aaaaa!!!!! Mwauponda ndithu2025 muziona kwanu kwatha anthu anakupatsani mpata koma mwalephera zinthu muzaka 4 amalawi sangapa nge misiteki kawiri
@user-fq4kv8dj4t
@user-fq4kv8dj4t 21 күн бұрын
Chikoka mulibemo olo nzozo mbola maturity mbola eeesh mudyeleni
@CatherineDesire
@CatherineDesire 21 күн бұрын
,🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤸🤸🤸🤸🤸mama ine ndakomoka
@user-oq5rg5mz7q
@user-oq5rg5mz7q 21 күн бұрын
Kusawa zoveselatu nanuso, agalu eni eni
@user-hl3st3cc4v
@user-hl3st3cc4v 21 күн бұрын
Kodi khope zimenezo zikuyakhula apazi pamodzi ndi zikhale ng,oma zamasana kapena zautsiku mmmmm anthu andalama olo kuwezuka
@user-hm9nc7lz6e
@user-hm9nc7lz6e 21 күн бұрын
Ndi zausiku mumuone or zikhameyo khope yace ngati chidzukwa
@Extratremendouszeus
@Extratremendouszeus 20 күн бұрын
Dziko linaola...nduna yosapesa😅😅😅😅😅😅
@WilliamBandaWili
@WilliamBandaWili 21 күн бұрын
Mmmmm izo ndi ng'ona zikuruzikuru zikudyani
@user-kh2bi8rk1d
@user-kh2bi8rk1d 21 күн бұрын
Msonkhano wanji wopangira mnyumba?? 😂😂😂😂
@WhiteRichard-cw2fo
@WhiteRichard-cw2fo 21 күн бұрын
Zikhale Ng'oma muti chani apaa tiyeni uko 😂😂😂
@WilliamblackvPaul
@WilliamblackvPaul 21 күн бұрын
Kwinaku ndingatukwane
@user-yb3su3hi9f
@user-yb3su3hi9f 21 күн бұрын
Ofunika kuwatukwana kumene. Onsewo panyero pawo
@MsondaBanda
@MsondaBanda 21 күн бұрын
Kumpoto kulije development, kufuma kale awo wangazenga kumpoto nimbani? No dpp, no udf , no utm, pali vifukwa apo,
@user-do2cs8nf4b
@user-do2cs8nf4b 21 күн бұрын
Simudzawina mizimu yonse yomwe munayipha ija ili pakati panupo anthu oyipa inu
@lame8
@lame8 21 күн бұрын
Alandila ma 20 pin zikuchita kuonesa. Kuwatengela anthu ku Hotel kobisika angolowobela manja chifukwa cha ndalama😢
@EllenPhiri-xt8pt
@EllenPhiri-xt8pt 20 күн бұрын
Mbamva ndi afiti awa sangawine tangonani anthu ndi anthu amabanja mwawo okhaokha amenewo
@alfrededwinmadziataika5869
@alfrededwinmadziataika5869 21 күн бұрын
Sapesa Adana ndimadzi..😮😮😮😮😮
@BrightNyoni-yd4ip
@BrightNyoni-yd4ip 20 күн бұрын
Anthu akupha inu mukungo Taya thawi yanu
@HalisonSolomon
@HalisonSolomon 15 күн бұрын
MBUZI ZAWANTHU ZAMANU PANSI MUNYERA MUONA
@jamesgama5489
@jamesgama5489 21 күн бұрын
Kwachaaa! Wachani mulibe manyazi eti!!.
@thondoyaenterprise3795
@thondoyaenterprise3795 21 күн бұрын
Chimphongo , chonenepa , cha kuda , chilibiiii chi ZIKHALE N'GOMA.
@KhalideNerve-mu1eq
@KhalideNerve-mu1eq 21 күн бұрын
Manganya come and see what you have done ✅
@user-wd9yd1bg9n
@user-wd9yd1bg9n 21 күн бұрын
Zikhareyo akutha kuona kuti mmmm apa pavuta , olo zikhaleyo sanafune kubwera
@wisdomwizzie9944Jahblessevery1
@wisdomwizzie9944Jahblessevery1 21 күн бұрын
Ngat u MP amugwesa gwesa ana zaka zambirimbiri lero nkumat Vp kkkkkk mudyeleni ameneyo ine olo ya u MP sazaiwonaso kuno
@user-lk3ki9hi3k
@user-lk3ki9hi3k 21 күн бұрын
Anthu a Karonga amenewo.......mukupepusidwa ndichani
@lawrencekauwa8005
@lawrencekauwa8005 20 күн бұрын
Kkkkkkk,,,, to be a supporter 🙌
BON KALINDO KWAUZA DR CHAKWELA LERO PA 2 August 2024
15:46
HOT 265
Рет қаралды 13 М.
ПРОВЕРИЛ АРБУЗЫ #shorts
00:34
Паша Осадчий
Рет қаралды 7 МЛН
Пранк пошел не по плану…🥲
00:59
Саша Квашеная
Рет қаралды 6 МЛН
Получилось у Миланы?😂
00:13
ХАБИБ
Рет қаралды 4,5 МЛН
Why Is He Unhappy…?
00:26
Alan Chikin Chow
Рет қаралды 51 МЛН
GWEDE-GWEDE KUZUKUTA MOSAOPA 🙌🙌🔥1 August 2024
21:03
Khothi la ICC likumufuna Zikhale Ng'oma; Mbava zovala ma suit ku Malawi
8:01
BLANTYRE NDILANDE A DR MICHAEL USI ATOKOTA🙌🙌🙌
15:46
CRUISE 5 WITH LUCIUS CHIKUNI PART 1   08 May 2022
58:54
Joab Frank Chakhaza
Рет қаралды 13 М.
TIMES EXCLUSIVE - 22 SEPTEMBER 2018 - DR KEN ZIKHALE NG'OMA
49:07
Times 360 Malawi
Рет қаралды 20 М.
Hello Zikhale Ng'oma! Kunali anzanu a nkhanza kuposa inu, anamwalira.
10:49
kumalawi kuno ndani wandale angamake??
1:01:32
Malawian Cameras
Рет қаралды 94 М.
ПРОВЕРИЛ АРБУЗЫ #shorts
00:34
Паша Осадчий
Рет қаралды 7 МЛН