Chakwela asowe fiti yothelatu UTM ganizani mofasa musakonde ndalama kumbukani tsogoleli wanu chilima upangili omwe analinawo sitikufuna kuti kupita kwachilima ndizinalake lithe ayi mukuziwabwino zomwe amafuna chilima still I remember S K C ambuye sungani mizimuyawo 😭😭😭💔💔💔
@Musa1828-l5d11 күн бұрын
Chakwera pamtumbo pakę anaba ndalama za fertilizer asamatipusitse azipusitsa zitsiru zake zomwezo
@user-uv5rf4zt5q11 күн бұрын
Malawi is lacking good leadership that's why is the poorest country in the world.
@user-le9su3mt7r8 күн бұрын
Chakwela satana wohipa ziko lamu nyeraaa
@user-xu9rh1lm8o11 күн бұрын
Asamango namidzila covid19
@WestonGawaza11 күн бұрын
UTM,mapulezident awa mayi chirima, mwana wachilima , Brayani Banda UTM awa ndi mapulesident a malawi, mukawasiya awa chipani chapita ndimazi, kongo kabira analowa ali ndi 31 years mundinkhulupirire , yeremiya, davidi, anali ana kaliyati ankhale muzati wa UTM, BY BY
@saadisadie312511 күн бұрын
Ayi kabira analowa Ali ndi28
@DanielVictor-pi5fj11 күн бұрын
Tikufuna Timothy mtambo
@sharifujoe763311 күн бұрын
Fredo yomweyo
@TiyanjaneLuka-e2l8 күн бұрын
😢😢😢😢Hey
@user-le9su3mt7r8 күн бұрын
Chakwela mbuzi yamuthu
@kubengovender699611 күн бұрын
Big up brother man!!
@Homeofpeace32111 күн бұрын
Am still worried about Chilima, Chakwela Anapaga Zolakwa Kwambili, Sangamuphe Munthu Chonchija
@user-qp8kh2hj9o11 күн бұрын
Kwambiri ndipo ine zimandiwawa mpaka lero pano bwenzi chilima atatiyankhula zokhuza comvension imeneyi hmm😢
@JafaliAkimu-ll1bf11 күн бұрын
chakwera asanamizire zimenezo chakwera ndi chitsiru chamunthu chigawenga
@user-jn2oc3cn3q10 күн бұрын
Mwakweza ferteleza tsopano mukuti tizigwilitsa ntchito manyowa ayi zikomo Bola la chakwera
@goodwilljeza841911 күн бұрын
Adah iweyo Bass limenero bwanji Koma?????
@MisheckNtanbalika11 күн бұрын
Mukufuna kt azaimile chifukwa mukuziwa kt Ali ndi mphavu xokupha aliyese odana ndichipanichi
@user-ii2sh1mz3r11 күн бұрын
President Chakwera akanabwera ndi chipani china osati MCP , nichifukwa chake mbiri yakale ya MCP ikumukhuza, but instead of kutukwana a president let us pray for our country, kutukwana sikusintha zinthu guys,
@brainsmkumbwa626711 күн бұрын
Wathamanga kukasiya ma pepela opikisana nawo pa udindo wapulezidenti chifukwa akudziwa kuti munthu yekhayo amene akanalimba mtima kuti apikisane naye wamupha kale (Chilima)changucho sichina koma kusangalala
Zaboza zimenezo kugwa kwa kwacha nanga. Zautsilu bas
@allansili-rc9gc11 күн бұрын
Covid 19 mpaka liti kod akuba inu
@FrancisNyayi11 күн бұрын
Hahaha covid
@user-kg5lf6bd1g11 күн бұрын
Patumbo pake chakweyo nyelo wake
@user-ti8ds7iq8z11 күн бұрын
Mmene anayambila za covid Muja mpaka liti
@dondamissonchdziwe395811 күн бұрын
Pongopha Chilima uja basi, Chakwera waluza, Chakwera must go
@user-em1qi8kj9h11 күн бұрын
Inu mudzikhala ndi manyazi ponena za covid....palibe anthu opasa manyazi ngati inu every statement of economics development....koma mukafuna Kuba ndalamazo Palibe za covid anthu onyansa mitima
@user-nb8wg3fh4u11 күн бұрын
Patumbo pako chakwela
@user-nf3ik3ff6y11 күн бұрын
MCP ndiyakupha
@user-yq1mc3nm1f11 күн бұрын
Utm uchitsiru mmmm
@HarryKandani11 күн бұрын
Blaming covid 19 mpaka pano? Abusa aku bagamoyo alibe nzeru za usogoleri
@phillipphiri21198 күн бұрын
Next time go straight to the point,Tizionera Zama parish Mmalo mwa za UTM