APM Sanaluze Zisankho Mu 2019 Ndi Mu 2020 - Innocent Mutholo

  Рет қаралды 15,106

Nyasa VoiceBox

Nyasa VoiceBox

Ай бұрын

On Nyasa VoiceBox, Innocent Mutholo, says that in his opinion, when he analyses the number of votes cast for APM in 2019 and 2020, APM won the election free and fair.
Pa Nyasa VoiceBox, Innocent Mutholo, wati malinga ndi maganizo ake, pamene amasanthula mavoti a APM mu 2019 ndi 2020, APM adapambana pachisankhocho mwaufulu.
#malawi

Пікірлер: 100
@user-eh1mg3ww6d
@user-eh1mg3ww6d 27 күн бұрын
Apapa chofunika tilape mulungu akhululukile Malawi chifukwa chakwela akadapanda kulamulila dziko la Malawi dziko la Malawi kukanakhala khondo yoopya chifukwa athu amafuna chakwela kwambili ndipo mulungu adalola kuti ateteze Malawi kusakhale khondo koma chakwela alamulile kuti athu adziwe kuti sakwela si muthu oyenela kutumikila dziko ndipo amaene amafuna chakwela aona okha kuti chakwela si muthu
@chrisneySwanepoel-yu5vd
@chrisneySwanepoel-yu5vd 27 күн бұрын
Ndiye anthu akalore kut munthu mmodz yekha galunso ndiwuyo akabwerese nkhondo
@user-eh1mg3ww6d
@user-eh1mg3ww6d 27 күн бұрын
@@chrisneySwanepoel-yu5vd ambuye atithandize
@TopoTopo-bm4vw
@TopoTopo-bm4vw 26 күн бұрын
Zowonadi
@user-te3ps3kf2t
@user-te3ps3kf2t 26 күн бұрын
Very true,amalawi avutika mokwaila,chifukwa cha adindo anjiru,mwaona zimene amapanga Mulungu, disorganized of Ministers chifukwa mulungu anakwiya,zonsezo Mulungu akuona,tionana 2025 sitilola zopusa zilizonse kudzikolanthu la Malawi
@isaaczuze
@isaaczuze 28 күн бұрын
Uku ndiye kuyankhula kwenikweni kwas chilungamo ..... Mr game changer ayi ndithu mumaziwa kuyankhula kwambili
@paulbanda9638
@paulbanda9638 27 күн бұрын
I by myself personally I agree with this man, game changer he is 100%right, anaba boma a tonse alliance,
@user-is5dl7np9g
@user-is5dl7np9g 27 күн бұрын
Zoonad kwambiri Mr. Gama changer💪💪
@marryphili5419
@marryphili5419 27 күн бұрын
Koma chakwera mulungu akuwone Malawi panopa wukuvesa chisoni Kuti wudye mavuto okhaokha
@MorrisMapiri
@MorrisMapiri 25 күн бұрын
50+1 must be abolished
@yohanedaudi1740
@yohanedaudi1740 27 күн бұрын
Very true
@PhilipMatolino
@PhilipMatolino 27 күн бұрын
Im agree with you game changer
@user-mm3es3ph7h
@user-mm3es3ph7h 4 күн бұрын
Come on Brother man game changer.
@user-jj7oz4lo9t
@user-jj7oz4lo9t 20 күн бұрын
I agree with you Game changer🎉
@JMB804
@JMB804 27 күн бұрын
God remember us🙌🏾
@FelixMatebule
@FelixMatebule 27 күн бұрын
Uku ndiye kukamba Mr game changer continue fighting for Malawi, Malawi open your eyes
@MikeTheu-ic2dt
@MikeTheu-ic2dt 17 күн бұрын
❤❤❤❤❤ zowona DPP Vot kujoni Kuno kwatopesa mwina tingabwere kwa2
@ivychithyoka1551
@ivychithyoka1551 16 күн бұрын
And God remains big judge even if earthly judges rule otherwise
@spargomw
@spargomw 28 күн бұрын
Ma Judge aku Malawi ndi adyera, amagwira ntchito akuyang'ana Umphawi wawo😂😂😂😂😂. Alipo oweluza wa Chilungamo ndiye Mulungu basi.Ma judge nawoso akayankha Milandu pamaso pa Mulungu.Kazilandiran ndithu ma Envelope'wo nd zomwe zikakhale Mboni zanu kumwamba
@timothymhone2340
@timothymhone2340 22 күн бұрын
Ngwira tnchito akupasa ndalama msatiputsitsepo apa
@user-pj3qi7gb3s
@user-pj3qi7gb3s 23 күн бұрын
Keep it up brother
@chifundocharles2348
@chifundocharles2348 26 күн бұрын
That judgement was not fair indeed
@user-op3nx5qt4q
@user-op3nx5qt4q 23 күн бұрын
Chulungamo ukuyenda ngati madzi okumva wamva osamva asamve ndipo tikumvutika kwambiri kuno ku malawi chifukwa cha MCP Chakwera Chakwera ndi Chilima UTM 😢😢😢 Abuye chitanawoni anthu amenewa
@ibrahmdoka7486
@ibrahmdoka7486 27 күн бұрын
Manyaka aboma...mbuli zenizeni zankhanza
@user-pt5wn7nu1d
@user-pt5wn7nu1d 27 күн бұрын
Tikufuna anthu ngati inu
@FranklinNdovi
@FranklinNdovi 10 күн бұрын
Two blind persons can not lead each other properly for both of them are unable see what is ahead of them.
@juliochiwalo
@juliochiwalo 25 күн бұрын
Ngakhale mayi Jane Ansah anenanso kuti APM ndi amene anawina ndipo chisankho chinayenda bwino
@hanifahmponda8711
@hanifahmponda8711 27 күн бұрын
God bless you malawi wafika pa Zimbabwe lelo 2025 kumvota no ID ngati akufuna dzimenedzo polembetsa mamvoti popo pakakhale elembetsa ma ID chilinga aleyetse atsalephele kumvota chifukwa cha alibe ID dzikalepheka apo bolani vote ilepheleke adzilamula popanda kumvota kutsiyana kuti atibele tikuwona Maso anthu alephela chimene akufuna adzilamulilbe chiyani kuwopa mulandu bwanji
@ChifundoNinje
@ChifundoNinje 20 күн бұрын
💪💪💪🔥🔥🔥
@user-gn4mx2es3k
@user-gn4mx2es3k 4 күн бұрын
Totally true
@WitnessMaulidi
@WitnessMaulidi 18 күн бұрын
Osawopa Bwana tili nanu
@user-xh1ve5ym3l
@user-xh1ve5ym3l 27 күн бұрын
Zowona big brother 🙏💕♥️
@chrischiwere7279
@chrischiwere7279 27 күн бұрын
Zoonadi zolanda
@ivychithyoka1551
@ivychithyoka1551 16 күн бұрын
Gooooio !!!!!
@user-gn4mx2es3k
@user-gn4mx2es3k 4 күн бұрын
Alekeni athana okhaokha a tonse alliance wo. Ayamba kale.
@user-cy7gd1go6y
@user-cy7gd1go6y 27 күн бұрын
Fire 🔥🔥 plus 💪💪
@YasinMusa-ym8lp
@YasinMusa-ym8lp 27 күн бұрын
Kunena soona malawi wata boma lamalawi rochimtisa manyasi chivukwachani kumalawi kukukanika 🇱🇾😭
@MonicaChunga-wg6xz
@MonicaChunga-wg6xz 15 күн бұрын
Mutichitire chifundo mulungu pautsogoleri uwu
@GanieAlidih-gu7no
@GanieAlidih-gu7no 28 күн бұрын
💪🏼💪🏼💪🏼💪🏼💪🏼
@user-st6bt5vv9c
@user-st6bt5vv9c 25 күн бұрын
Achule awa achoka basi tizikavota ngati amalawi zoona ndithu
@LovemoreSalima
@LovemoreSalima 24 күн бұрын
Ndizoona. Anaberadi
@user-oq7hi3hd4p
@user-oq7hi3hd4p 27 күн бұрын
Amen
@user-te3ps3kf2t
@user-te3ps3kf2t 27 күн бұрын
True,
@TracyZiyaya-nz4pd
@TracyZiyaya-nz4pd 25 күн бұрын
Maka maka chilima mulungu athane nawe ndipo unapanga zonyasa kwambiri ku dziko lino lamalawi
@IssaKapalamula
@IssaKapalamula 14 күн бұрын
Munthuyo ndi sapota wa dpp, ndiye mukuona ngati anganene za nzelu?
@EmmanuelGasiten-fo5dr
@EmmanuelGasiten-fo5dr 23 күн бұрын
Mulungu awalange ma Judge amenewa.
@ivychithyoka1551
@ivychithyoka1551 16 күн бұрын
Speak Game changer!!!!!?
@user-oc9vl9xz8e
@user-oc9vl9xz8e 27 күн бұрын
Kodi monse munayambila muja kuti mupita pa mseu muzapitapo liti pomwe zinthu zikupitilila kuwonongeka???
@user-st6bt5vv9c
@user-st6bt5vv9c 25 күн бұрын
TIZALOWA AMBIRI PAMSEU
@NicholasJames-cb7du
@NicholasJames-cb7du 27 күн бұрын
Big man bwanji simutumiza ma audio a dj munyanane pepani ngat ndalakwisa kufusa
@nyasavoicebox
@nyasavoicebox 27 күн бұрын
Simukulakwitsa tiyesela tiziponya mungoti tipatsa ka mpata pang’ono
@MasiyeDayton
@MasiyeDayton 27 күн бұрын
Kkkkkkk game change ❤
@BistonNjobvu
@BistonNjobvu 27 күн бұрын
Koma antnhu amaziwa kutsata nkhani
@ivychithyoka1551
@ivychithyoka1551 16 күн бұрын
Eeeeeeee Apm anaberedwa
@BensonMalaulo
@BensonMalaulo 27 күн бұрын
Mumakwana Mr game changer
@user-qm1ri6cr6w
@user-qm1ri6cr6w 26 күн бұрын
Zen zen
@JosephMwambe-rz2oy
@JosephMwambe-rz2oy 17 күн бұрын
Zoona zimezo
@uchizJoelMumba
@uchizJoelMumba 27 күн бұрын
Ndiye ngati ukulimbana ndi majaji mbale wanga ndi dpp yakowo mulipamabvuto ndithu amene akutumawo akupweteketsa mbale wanga
@user-mm3es3ph7h
@user-mm3es3ph7h 4 күн бұрын
MCP, yawonga zambiri.
@user-nj5vu8cd5l
@user-nj5vu8cd5l 25 күн бұрын
Kodi APM , mukunena galu wakupha ma albinos ndi kuba ndi chisale
@DIRECTORJARVMACK
@DIRECTORJARVMACK 16 күн бұрын
Mukuganiza ngati mwanatu mesa achakwera amamufufuza sanamupedze ndi mulandu uliwose
@amiduclement2142
@amiduclement2142 20 күн бұрын
Kodi ku mcp kuribe wina wazeru
@SolokingChimzy-yt7dj
@SolokingChimzy-yt7dj 27 күн бұрын
Chakwela Ali ngat Hule wa pa saloon yemwe amazazionesa ngt munthu wabwino koma Ali ooopsa kuposa hule yemwe Ali ku Bar
@homeremedys3748
@homeremedys3748 27 күн бұрын
Panopa MCP yayamba kuchotsela masiku, DPP yayamba kuwengela masiku
@BertharrySecurity
@BertharrySecurity 27 күн бұрын
Chilungamo chimawawa,Koma mnthu wayankhula chilungamo uyu.
@paulbanda9638
@paulbanda9638 27 күн бұрын
Chi christu nthawi zina sichiri bwino, a chakwera ndi a khristu, zikuchitikazi ndi panichimeti kwa amalawi onse, chakwera ndi tonse alliance ndiakuba anaba boma kuli ndalama kukhala bwanji
@phillipstamaley7901
@phillipstamaley7901 21 күн бұрын
Chakwela woyeeee mcp m'paka 2063
@SALIMASSAN-vr8ld
@SALIMASSAN-vr8ld 27 күн бұрын
Ndip iwey ulem wak srs chilungam chikuveka bwin kwambir
@RaymondKaumba
@RaymondKaumba 10 күн бұрын
Galu iwe
@user-xy9vz6jj4u
@user-xy9vz6jj4u 27 күн бұрын
MA judge pawo pawo ndthu
@MonicaChunga-wg6xz
@MonicaChunga-wg6xz 15 күн бұрын
Chitsime chakudya chimaoneka chikaphwa
@user-do2cs8nf4b
@user-do2cs8nf4b 27 күн бұрын
Mulungu akuwona zonsezi tsiku la 40 lidzawakwanila anthu amenewa
@IsaacMusa-py2jm
@IsaacMusa-py2jm 27 күн бұрын
Mau amphanvu 👊 👊
@gladysbonongwe1038
@gladysbonongwe1038 27 күн бұрын
Dzuka Malawi dzuka
@Chiso2019
@Chiso2019 27 күн бұрын
A munthalika amagona kwambili that's why analandidwa dziko....nanuso mukuyankhula kwambili koma action zilo
@ShabaniKuswere
@ShabaniKuswere 27 күн бұрын
Kupewa sikupusa anapewa nkhondo
@user-eh1mg3ww6d
@user-eh1mg3ww6d 27 күн бұрын
Ndipo ndizoonadi mulungu samalakwitsa amafuna athu amuone chakwela kuti si muthu oyenela kutumikila Malawi
@ibrahmdoka7486
@ibrahmdoka7486 27 күн бұрын
Umafuna Peter apange nkhondo mbuziwe
@ibrahmdoka7486
@ibrahmdoka7486 27 күн бұрын
A judge amenewo tidzawamanga
@SolomonNjolomole
@SolomonNjolomole 27 күн бұрын
Kuyankhula kwabwanj uku mumafuna ayambitse nkhondo?
@gladysbonongwe1038
@gladysbonongwe1038 27 күн бұрын
Majaji ndi amene ayika amalawi pamoto
@IssakeMateyo
@IssakeMateyo 27 күн бұрын
Kkkkkkk
@user-ky8eq5ek1p
@user-ky8eq5ek1p 27 күн бұрын
Zoonadi munthu wamkulu
@uchizJoelMumba
@uchizJoelMumba 27 күн бұрын
Galu wa dpp kulila mobangula ndiye sunati ukanalila mcp 2025 boma kale
@mafukenimasangwi5487
@mafukenimasangwi5487 27 күн бұрын
Dzinazi osamatengela kut bambo anu anali a mcp kapena a dpp koma kumaona kut nziko mwathu zinthu zikuyenda? kapena ayi ngati mumamwa tea sikuti ndi azibale anu nso onse akumwa tea ayi akuvutika mukatengala ku muziti simunaati muziwe kut azibale anunso ali mugulu lomwelo lomva zowawa
@FelleCasim
@FelleCasim 26 күн бұрын
Zitsilu za nyau inu wamzelu angavotele mcp panomso?
@DIRECTORJARVMACK
@DIRECTORJARVMACK 16 күн бұрын
Kumalikonda dziko lako osati umoyo wako ayi anthu akumva kuwawa
@marryphili5419
@marryphili5419 27 күн бұрын
Malawi panopa akuvesa chisoni machine opanga mapassport sakugwira ntchito panopa machine wopangira ma ID akuvutaso Koma chakwera wuziwe komwe wuliko Kuti wulamuliro wako ndi mulungu yemwe ndiwokwiya ndi iwe
@SolokingChimzy-yt7dj
@SolokingChimzy-yt7dj 27 күн бұрын
kkkkkkkk......Nebukadinezera uyu
@DIRECTORJARVMACK
@DIRECTORJARVMACK 16 күн бұрын
Ku Lilongwe kuli machine 8 opangila ma id pomwe ma district ena ndi zero
@Littlefair7
@Littlefair7 27 күн бұрын
Mutholo ndi anzako achina Ben Longwe mupeze zochita, what you're doing is not activism, this is stupidity of its highest order, mwasanduka oyankhukira zipani, zopusazi tasiyani, ngati mukufuna u activist pitani ku school mukaphunzire osati kumasokosa ndi zopusa zanuzi.
@EvanceEdson-fz1vn
@EvanceEdson-fz1vn 21 күн бұрын
Akunena chilungamo, chilungamo chimawawa. Why 50+1, why alliance yet anakana a mec fresh vote registration? Don't you see kut the same rules of 2019, could apply for the fresh 2020 election
@user-mf7hf7we2u
@user-mf7hf7we2u 28 күн бұрын
Simungavumeleze
@LilianKachala-yz2xf
@LilianKachala-yz2xf 27 күн бұрын
Mau Amphamvu ngati amenewa tamva ndithu
A UDF Mdani Wanu Number One Si MCP - Concerned Citizen
18:18
Nyasa VoiceBox
Рет қаралды 2,6 М.
A UTM Nthawi Yakwana Mubwelele Komwe Munachoka - Bon Kalindo
14:26
Nyasa VoiceBox
Рет қаралды 58 М.
Countries Treat the Heart of Palestine #countryballs
00:13
CountryZ
Рет қаралды 29 МЛН
1❤️#thankyou #shorts
00:21
あみか部
Рет қаралды 88 МЛН
I Built a Shelter House For myself and Сat🐱📦🏠
00:35
TooTool
Рет қаралды 36 МЛН
Ku Boma Penapake Mulankhula Mwachibwana Kwambili - Bon Kalindo
16:32
The Times Malawi Report: CCPF Impresses South African Officials
2:51
JOHN KAPITO WATOPA NAYE CHAKWERA. Ityoke ityoke Osabisa mau // PART 1
33:23
Malamulo Akuti Chani Wa Chiwili Kwa Mtsogoleri Akamwalila?
6:01
Nyasa VoiceBox
Рет қаралды 30 М.
KAFUKUFUKU PA IMFA YA ACHILIMA
30:18
Jimmy
Рет қаралды 50 М.
JOHN KAPITO WATOPA NAYE CHAKWERA. Ityoke ityoke// PART 2
27:18
MALAWI TODAY
Рет қаралды 41 М.
Countries Treat the Heart of Palestine #countryballs
00:13
CountryZ
Рет қаралды 29 МЛН