Bon Kalindo lero pa 11 July kufotokoza mopanda kuopa aliyense - “MUNDIMVA NDIPO SINATI”

  Рет қаралды 31,001

Makosana

Makosana

23 күн бұрын

Пікірлер: 81
@user-ix2ux5ss1b
@user-ix2ux5ss1b 21 күн бұрын
More fire mukutiimilira bwana! Ife timasowa mpata oyankhura zakukhosi kwathu. God bless you and protect you. Amalawi tikuvutika
@JowasiMasina-fy8ji
@JowasiMasina-fy8ji 21 күн бұрын
Mukazava kuti boma lawanyera ndi zimenezo anavako kuti Koma Malawi ayi ndithu komaso kamuzu samapaga zimenezo ayi amati zithu zikamakwela iyeyo amakambolana ndi anuwake kamphani kuti atsitseko anthu ake alibe ndalama ndiye inu mukuzitega bwanji zimenezo kodi dziko la Malawi mwalitani tamakumbukirani komwe munali azanufeso tikuva kuwawa ngati munkhavera inu muja kuli mulungu kumwamba zonse mukupagazo akuziwona ndithu tsiku lina lidzakwana la 40👏👏
@EversDman
@EversDman 20 күн бұрын
Bon kalindo wathu wathu 🔥🔥🔥💯
@LuyoloTlhapane
@LuyoloTlhapane 14 күн бұрын
A pule athu ❤❤❤god protect your mr born mmatiimilila
@PeterKasiya
@PeterKasiya 20 күн бұрын
Boniiiiiiiii kalindoooooooooo Mwana owopswa kwambili
@MomeryPhiri
@MomeryPhiri 20 күн бұрын
❤❤❤❤❤❤❤ love it
@user-kk4uj8ko8k
@user-kk4uj8ko8k 21 күн бұрын
bon kalindo sukunama luchenza. Lijoni ikupanga khazakwambili longopackngi 1ooooo u lube amakumanga kuselo
@user-xm5cq1fb8g
@user-xm5cq1fb8g 20 күн бұрын
Ulemu wanu big❤❤❤❤❤
@user-dj6rc3lc4t
@user-dj6rc3lc4t 20 күн бұрын
Inu ndinu Muthu wankulu kalindo Bon mumakwana
@UthmanKapungu
@UthmanKapungu 21 күн бұрын
Fire!!!!!!!!!! Bon kalindo nazoni tatopa ife
@neemahkapatamoyo9563
@neemahkapatamoyo9563 20 күн бұрын
Kkkk koma abare zowona mchenga omwewo omwe analenga Mulungu mwini nthaka zowona mpaka kumagulitsa ayi zikomo dziko ili 🙌🙌🙌🙌🙌🙌🙌
@AffickChaona
@AffickChaona 17 күн бұрын
❤❤❤❤❤
@DauglassNkhoma-dj9lp
@DauglassNkhoma-dj9lp 20 күн бұрын
😂😂Boni kalindo wangadula kkkkk boooo towopa kubwelako kumalawi
@FarookRaphael
@FarookRaphael 21 күн бұрын
More fire komanso mukuyankhula ngat chinyanja service channel Africa
@user-be5fc3ed1i
@user-be5fc3ed1i 20 күн бұрын
Ndipangeso replay pakanyimboko kandisangalasa bwanji kkkk koma uyu ndi pangolin 😂😂😂😂😂😂
@FlorryVugy
@FlorryVugy 20 күн бұрын
A president Bon mumatiyimilira😂😂😂😂😂 Sikusinja ndi gwenembe😂😂😂😂
@user-wm4rs4kd7d
@user-wm4rs4kd7d 21 күн бұрын
@user-lg6ym4hz3w
@user-lg6ym4hz3w 21 күн бұрын
Kkkkkkkkkk ana ofewa odya mipungu nthawi ya mayeso apolice akungosilira
@user-hq8fw5hz2l
@user-hq8fw5hz2l 20 күн бұрын
Awa ndie mawu
@Shelifibraheem
@Shelifibraheem 21 күн бұрын
Big up bro
@user-hx6jl2jq9j
@user-hx6jl2jq9j 20 күн бұрын
Aaaaa yai awawa akufuna kuti tiyiwale kunlankhula za chilima. Agalu a anthu ndithu
@PrinceBlessings-bv5bs
@PrinceBlessings-bv5bs 21 күн бұрын
😂😂😂😂😂 lero wayaka moto kalindo❤❤❤❤❤ a opposition please chitanipo kanthu awawa aikanika dziko olo manyazi alibe
@EllinaBitto
@EllinaBitto 21 күн бұрын
Bulaza wathu❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤
@FwasanMwenefumbo-zq7sg
@FwasanMwenefumbo-zq7sg 21 күн бұрын
The DC 🔥
@user-be5fc3ed1i
@user-be5fc3ed1i 20 күн бұрын
Awa ndi machine poyankhula the DC mwana wowopsya kwambiri 😂😂😂
@HelenamoisésLisboaMoisésLisboa
@HelenamoisésLisboaMoisésLisboa 21 күн бұрын
Ambuye akudalitsen
@PeterMaulana-qk5uq
@PeterMaulana-qk5uq 21 күн бұрын
Ooh...ambuye dalisani anthu amene akumenyela ufulu m'malawi chonde musalore kt mbava za mcp zilamulire dziko lathuli AMen!!
@NdawaPhillipfortunePhakatie
@NdawaPhillipfortunePhakatie 20 күн бұрын
Motor 💥 kalindoooo
@user-zt3gv7md6x
@user-zt3gv7md6x 19 күн бұрын
Zoona amwene
@FrankMilias-og3js
@FrankMilias-og3js 20 күн бұрын
Kulankhula mosaopa nyooo sss winiko
@BernadettaTengula
@BernadettaTengula 20 күн бұрын
Koma ine uyu ndimasowa pomuyika ,,ati chifukwa cha udindo😂😂😂
@JoyceChitsulo-mw7wg
@JoyceChitsulo-mw7wg 21 күн бұрын
Makosana apa nde mwapita
@ericlarks8165
@ericlarks8165 20 күн бұрын
,🔥🔥🔥🔥
@benjulius6070
@benjulius6070 20 күн бұрын
😂😂😂😂😂😂
@BlessingsKalonga
@BlessingsKalonga 20 күн бұрын
Aliyese ndi wakuba koma kusagwidwa Judgement day tidikire oweruza
@user-kx4cj7iu9q
@user-kx4cj7iu9q 20 күн бұрын
Dc
@D.RJALLI-qo6yd
@D.RJALLI-qo6yd 20 күн бұрын
Ine ndikudana ndi ma opposition akumalawi ndi agalu kobasi makamaka dpp ikungoyang'anila wosalangula khatu kumbonà lamasuso ngati ili ndiye boma adzalipesa bwanji dpp tadzukani ife tampudzilapo ndipo talapa mamisiteki athu bwelani nditu mutiwombole kwa agalu awa
@VincentMalika-w7x
@VincentMalika-w7x 21 күн бұрын
Ndipo eeeeee tikudziwona kuno tikulemba mayeso apolici ache akupemphaso dzokudza zakudya zath
@EdwardMukholi
@EdwardMukholi 21 күн бұрын
Kkkkkkkkkk koma chakwera ndiye ndiye zikuchoka kuti zimenezi
@RamseyWasi
@RamseyWasi 21 күн бұрын
Blasa, Malawi saadzatheka mpaka kale kale. This is my second SMS to you mr Dangerous Child (DC) My opinion: Kungosiiya utsogoleri wa anthu osawukawu.chfkwa or titatan,kusawukaako sikudzaatha.
@SmartMoles
@SmartMoles 20 күн бұрын
Zofunikila kulangura mwayangure kumene
@BlessingsKalonga
@BlessingsKalonga 20 күн бұрын
Ubwino wake ukuzimenyera wekha khondo uzalemera wekha
@ChisomoamitoniSauzandeamiton
@ChisomoamitoniSauzandeamiton 20 күн бұрын
bwana ng'alurani ndithu tili nanu nanu
@JuliusMunthali-z7j
@JuliusMunthali-z7j 21 күн бұрын
Awuzeni
@directorkfuture118
@directorkfuture118 20 күн бұрын
Ameneyo asamwe mowa 😂😂😂
@gerrardgladstone2473
@gerrardgladstone2473 21 күн бұрын
Akuti kufuna kumangidwaaaaa 🤣🤣🤣
@user-dm6xq6cp1m
@user-dm6xq6cp1m 20 күн бұрын
Ai zikomo 🥱
@HendersonDziwa
@HendersonDziwa 20 күн бұрын
Dzelu zachepa kkkk
@maxwellcaptain3937
@maxwellcaptain3937 21 күн бұрын
Kalindo samaopa😂😂
@TshepoModise-xs4qu
@TshepoModise-xs4qu 21 күн бұрын
Koma nkhaza zake mpaka licence ya mnchenga Mmmm zovuta bwanji eeee
@user-tw5iw7gf2v
@user-tw5iw7gf2v 20 күн бұрын
😂😂😂😂 mpaka muchenga license
@ChrispinEdward
@ChrispinEdward 20 күн бұрын
Bwanawe pafika boma umuthu walimbe akungo funa kumupanikiza Muthu osawuka kut azikhala ndima strees bas komano azidikile kut Pali mwambi waphala lakaka ukaza fika pomva kukoma limakhakut lathamo mupoto
@MathpeterLemon-ls1ns
@MathpeterLemon-ls1ns 20 күн бұрын
Ati kutitola kapena chani
@DaudiAbdullah-o5l
@DaudiAbdullah-o5l 20 күн бұрын
Mumatiyimilila
@nicholasmutano6017
@nicholasmutano6017 21 күн бұрын
Uyuyu ndi mandrax sichamba, akufuna titani tilowele kuti si misala iyi?
@user-yl3lg5fk8f
@user-yl3lg5fk8f 20 күн бұрын
Koma amalawi tinalakwanji kt tizunzike,,,galu uyu wazunza miyoyo ya anthu osalakwa,,chitsiru cha m'busa munthu opanda conscious
@PeterGrant-ih1sr
@PeterGrant-ih1sr 20 күн бұрын
Athuawa atakhala alipo okwana 4 ziko muno athuwa atasitha ndithu😂😂😂😂
@harrisbanda5891
@harrisbanda5891 21 күн бұрын
Mpakana tizigulisana mchenga wamudziko lathu zoona?, kusavukatu uku sopano aati!?, chaza ndiyan choti tizikhala ndi linces yovuwulila mchenga ?, ndepoti amalawi mumkafuna kusintha zinthu , zimene mumkafuna kwa abusa zija mzimenezi😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂❤❤ , mo 🔥🔥🔥🔥🔥🔥 mcp kkkkkk
@ikmusic-s9f
@ikmusic-s9f 21 күн бұрын
koma nde eeee mpaka licence mchenga
@pempheroraynnoxmpesi8713
@pempheroraynnoxmpesi8713 17 күн бұрын
😂😂😂😂msusi olo nthuli amatayapotu a dpp
@user-ls5zj8qn6k
@user-ls5zj8qn6k 21 күн бұрын
Koma uyu inu kkkk ati apolice osilila mpunga wa nyama 😂😂😂😂 ayi zikomo
@wangachindeya8577
@wangachindeya8577 21 күн бұрын
Bigiliman naweni
@sir-wanton-2001
@sir-wanton-2001 21 күн бұрын
Kkkkk Kkkkk uyu akazankhala president azamujaje nda uyu ndi dolo
@YonaMartin-kb3do
@YonaMartin-kb3do 21 күн бұрын
😂😂😂😂 akavoterana ndi amawo yemweyo kupuma palibe
@AaronLitete
@AaronLitete 20 күн бұрын
Kkkkk boma lopusa
@user-ky8us1ff5b
@user-ky8us1ff5b 21 күн бұрын
😅😅😅😅
@CaptainNyenga
@CaptainNyenga 20 күн бұрын
😂😂😂😂😂 koma DC
@lytonmaseko4534
@lytonmaseko4534 20 күн бұрын
😂😂 kung'alulatu
@user-vn1wq6wg6i
@user-vn1wq6wg6i 21 күн бұрын
K.K😂
@YohaneMbewe-u4k
@YohaneMbewe-u4k 20 күн бұрын
😂😂😂😂
@AnthoniohMazengera
@AnthoniohMazengera 19 күн бұрын
Hahahahahahahahahaha😂😂😂
@Aluwenkareem-ev3ro
@Aluwenkareem-ev3ro 20 күн бұрын
😂🤣😂🤣
@PhillipMtonga-g7o
@PhillipMtonga-g7o 21 күн бұрын
🤣🤣🤣🤣🤣🤣 zamanyazi kuntonse alliance
@GiftKulture
@GiftKulture 20 күн бұрын
🤣🤣🤣🤣 mipunga
@BenjaminKayembe-j7j
@BenjaminKayembe-j7j 21 күн бұрын
km eeee awawa ndsbwsna gayz mmmmmm amakwana km
@Kachelephiri
@Kachelephiri 20 күн бұрын
Awa.akulila.ayesetse.2025.azawinekwawo.ump.kwawo.kma.ngatiakukanakwawo.ndiakanene.jilose.tingamuvele.galu.wachabechabe.
@ChristopherKawilam
@ChristopherKawilam 20 күн бұрын
Uku nyoza bon kalindo,, zeru ulibe iwe uku Kanika kulemba kumene galu iwe
@ChristopherKawilam
@ChristopherKawilam 20 күн бұрын
Yamba wapita Kaye Ku school ya mkaka uziwe kulemba...... galu iwe
@user-wz6jy3re8n
@user-wz6jy3re8n 21 күн бұрын
😂😂😂😂😂😂
@MadalitsoManyozo
@MadalitsoManyozo 21 күн бұрын
😂😂😂😂😂😂😂😂
@myheartforkids2876
@myheartforkids2876 21 күн бұрын
😂😂😂😂😂
MANGANYA VS AKWENI - KWAPHULIKASO INA KU UTM
13:37
Makosana
Рет қаралды 33 М.
World’s Largest Jello Pool
01:00
Mark Rober
Рет қаралды 93 МЛН
Best KFC Homemade For My Son #cooking #shorts
00:58
BANKII
Рет қаралды 67 МЛН
DEFINITELY NOT HAPPENING ON MY WATCH! 😒
00:12
Laro Benz
Рет қаралды 64 МЛН
Slow motion boy #shorts by Tsuriki Show
00:14
Tsuriki Show
Рет қаралды 9 МЛН
PATRICIA KALIAT WABWENZA MOTO KACHIKENASO
12:51
Makosana
Рет қаралды 19 М.
Putin vows 'mirror measures' if US deploys missiles in Germany | VOANews
2:38
Maloto A Bon Kalindo (Part 2) - Bon Kalindo
14:17
Nyasa VoiceBox
Рет қаралды 109 М.
Top U.S. & World Headlines - July 29, 2024
10:31
Democracy Now!
Рет қаралды 176 М.
Meet the Press NOW - July 29
49:59
NBC News
Рет қаралды 945 М.
World’s Largest Jello Pool
01:00
Mark Rober
Рет қаралды 93 МЛН