BON KALINDO LERO PA 16 JULY 2024 |

  Рет қаралды 37,885

DZIWE TV

DZIWE TV

Күн бұрын

Пікірлер: 150
@user-lz4kc5ob1t
@user-lz4kc5ob1t Ай бұрын
Ife tamupasa kale mai kaliyati president of utm
@user-ig9ip8jq7v
@user-ig9ip8jq7v Ай бұрын
Watching from S A port Elizabeth timakunyadilani bwana pitilizani kuti imilira Mr Bon kalindo l Salute u bwana
@EnittaDavison
@EnittaDavison Ай бұрын
Umatiymilra iweyo ulemu wako bon 🔥🔥🔥🔥👏👏👏👏👏👏
@justinmakiyi4189
@justinmakiyi4189 Ай бұрын
As UTM and Malawi as whole country we are luck having this guy as somehow a prophet or advisor to the difference parties. The choice is in our hands to take the advise or leave them. But one day we shall remember Him. That's the free advise indeed. Regards
@GreyJecky
@GreyJecky Ай бұрын
True
@user-fi7ko7bl6f
@user-fi7ko7bl6f Ай бұрын
😅😅 zapana ndithu ndipo sanati and who is Manganya??? U don't know Bonnnnnn Kalindooooo mwana oopsa kwambiri ndiponso mumumva, the DC mwana woyankhulira pa mchombo pa Malawi, alibe mantha ndipo saopa Unyolo kaya mfuti😅😅😅
@Lazarus-qo1sl
@Lazarus-qo1sl Ай бұрын
President wathu wathu amangoyima pachilungamo🎉
@user-bd5kw8oq1r
@user-bd5kw8oq1r Ай бұрын
@@Lazarus-qo1sl president wa zitsilu zokhazokha ndi mbuli zophumzila koma makolo awo fees anagowononga ngati mmene DPP inawonongera dzikoli
@VungaQueen
@VungaQueen Ай бұрын
Mmmmmmmm inu Bon Kalindo musiye nde zitsilu tili ambili inu anthu abwino Kharani km siwani kt choyipa chitsata Mwini nadutsa sindinyoza ine
@christopherphiri8476
@christopherphiri8476 Ай бұрын
Born kalindo will help UTM if anything engenge him to assist he is a man of action Christopher phiri from Zambia
@FatimanickisJaffer
@FatimanickisJaffer Ай бұрын
DC born kalindo more fire 🎉
@SteveSamson-t9d
@SteveSamson-t9d Ай бұрын
following kalindo Diiiiiìiiiiiiii siìiiiiiiiiiiii
@user-dp7bc7yy6s
@user-dp7bc7yy6s Ай бұрын
Awa ndiye amkamuna a UTM zili ndiinu kunyozera km Bon ndiye walangiza.
@MisheckAselo
@MisheckAselo Ай бұрын
The DC, Mr booooooon kalindo 🎉🎉🎉
@TooNajahInsideKoshah
@TooNajahInsideKoshah Ай бұрын
Iwe ndiye president wathu wathu
@DalitsoTwalick
@DalitsoTwalick Ай бұрын
Thanks my president for ur information
@user-yk5qd6sk8e
@user-yk5qd6sk8e Ай бұрын
the dc 🎉🎉 mwana ooopsa kwambili
@user-mh7cc8up4i
@user-mh7cc8up4i Ай бұрын
Kodi a UTM mukuitana athu kwana chifukwa ninji Kodi menemo mulibeathu oti angayendese chipani ?bwinonazotu ndalama inampha mwanawamuthu zayekha ananyika sima m'mazi
@vincentkhunsanama584
@vincentkhunsanama584 Ай бұрын
Yeah, the DC is not making mistake to advice the utm fam big up the DC
@JosephLemani-qq1is
@JosephLemani-qq1is Ай бұрын
Mwayankhula bwino bon kalindo ena akufuna kugwetsa chipani cha UTM koma bola abwelele komwe anachokela
@user-bd5kw8oq1r
@user-bd5kw8oq1r Ай бұрын
Inetu ndimaganiza Kuti boni kalindo ndi mamuna koma ayi eti ndi wamkazi or kuganiza kwake ndimadabwa nako aaah lero ndamumvetsetsa ndi mkazi paja amavalaso ma browsers amamangaso tsitsi 😅😅😅😅😅 koma MCP yamulela bwinji because popanda MCP sibwenzi ali miss kalindo lero ayi akuyenera ponyoza MCP uku ndlama zikulowa kuchokera kwa anthu a ndale opposition 😅😅😅😅😅 uyithokoze MCP ukuchita bwino kwambili keep it up moto kuti buuu Satana akugwila ntchito yowatsogolela anthu ku moto ndi pakamwa kulankhula sosakondweretsa ambuye work up time is almost finished Jesus Christ is coming soon get ready before we die
@JusticeNyirenda
@JusticeNyirenda Ай бұрын
Thanks for the information about Jesus, but the rest is senseless
@user-bd5kw8oq1r
@user-bd5kw8oq1r Ай бұрын
@@JusticeNyirenda so it's better not to take part to these people we can die in sins we are in the last days all things must come to pass like economy James 5 the whole chapter famine, wars, disease all these they contribute financial crises all over the world Mathew 24 vs 5 to 8 then you will here about the national Sunday Law to combat all the crisses mentioned above by force in the name climate change and the pope will rule the world for 3 and half years but he will be overflow by all nations when they will see that no change but hypocrisy leading people to destruction and people will be against him work up time is almost finished Jesus Christ is coming soon get ready before we die follow Jesus not politicians ndi abodza Ngati omwe akuchulikitsa machimo awo pa social media
@ElizaJames-by8ef
@ElizaJames-by8ef Ай бұрын
African man ❤❤❤
@FrancisNyayi
@FrancisNyayi Ай бұрын
Muzibwereza mau aoooooopsya kwambiri 😅😅😅 ndi iiiiiii
@KondwaniBilliat-t4g
@KondwaniBilliat-t4g Ай бұрын
A DC tikupempha Mulungu wa kumwamba akupaseni moyo wautali ndi ntchito zanu zabwino pitilizani tilipambuyo panu nga!nga!nga!!!!!!!
@EdwinMabviko
@EdwinMabviko Ай бұрын
Unayankhula zimenezo ,galu iwe!!!
@user-zr7wk4oq2x
@user-zr7wk4oq2x Ай бұрын
Very sensible message bwana #DC♥️🔥🔥🔥
@ChimwemweKondowe-nj4lx
@ChimwemweKondowe-nj4lx Ай бұрын
Good advice Mr President
@KennedyPhiri-h9h
@KennedyPhiri-h9h Ай бұрын
The DC we are with you Mr president wa anthu osawuka ❤❤
@user-fi7ko7bl6f
@user-fi7ko7bl6f Ай бұрын
Wolimbana ndi Boooo Kalindo oooo the DC atembenuke ndipo azilume kunsana more 🔥🔥🔥 Kalindooooo the DC 😅😅
@LuckyMhlanga-m1u
@LuckyMhlanga-m1u Ай бұрын
Kalindo you are true
@HajjiSufiyani
@HajjiSufiyani Ай бұрын
Pitilizani. Kutisogolela. Ndithu kuyakhula koveka bwana
@user-xm3zl5cg6x
@user-xm3zl5cg6x Ай бұрын
Ndizona osangotenga zili zonse km a Malawi asanhhe
@user-wu8kp7ui5j
@user-wu8kp7ui5j Ай бұрын
The DC 🔥🔥🔥🔥🔥
@AliajoeAliajoe-vv1wo
@AliajoeAliajoe-vv1wo Ай бұрын
Great man
@violetpotani
@violetpotani Ай бұрын
Eeeish koma information mumayipeza 😅😅😅anthuwa bwenzi atangokhala coz akunyozeka
@Judah-zb6sl
@Judah-zb6sl Ай бұрын
The DC ❤🎉🎉🎉🎉🎉
@ErickMambelera
@ErickMambelera Ай бұрын
Umakwana kalindo
@WanangwaVwalika
@WanangwaVwalika Ай бұрын
More fire!!
@eliaschinoko2086
@eliaschinoko2086 Ай бұрын
The Dc Booooooooooooooooooooooooooooooooooon Kalindo 🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🎉🎉🎉🎉🎉🎉🎉🎉🎉
@OmrahGeraldOmrahGerald
@OmrahGeraldOmrahGerald Ай бұрын
❤❤❤❤ The DC kungalula
@davidmzee2205
@davidmzee2205 Ай бұрын
Nde mwati Pepe Kale ?😂😂
@annamazingashaibuh6276
@annamazingashaibuh6276 Ай бұрын
The DC kkkkkkkkk🔥🔥🔥🔥
@KingLunda-u1t
@KingLunda-u1t Ай бұрын
Big man hooooooo
@Lemankais
@Lemankais Ай бұрын
Bon ndi kampani simunthu wamba
@SteveZimba-e8s
@SteveZimba-e8s Ай бұрын
Gwiritsani ntchito malangizo amene wakupatsani DC osazitaya muononga chipani chanu chabwino bwino
@ExcitedBreakingWaves-oh3zb
@ExcitedBreakingWaves-oh3zb Ай бұрын
Ng''alula m'bale.
@user-oy6dl1pv9e
@user-oy6dl1pv9e Ай бұрын
Following kwa Diiiiiiiiiiiisiiiiiiiiiiiiiiiiii
@SanidaChirwa
@SanidaChirwa Ай бұрын
Ing'alilen fada ,osaopa ay Malawi ndiwathu uyu
@FelixKazembe-wi5zb
@FelixKazembe-wi5zb Ай бұрын
Ndizosantheka kutuluka anthu onse chipani" choti mudziwe chipani cha UTM chamwazikana! Pepho langa ndiloti osalawo asachuluke zomwe zitapangise chipani kuchepa mphavu...manganizo anga.😢
@sulleahmnyimbili1362
@sulleahmnyimbili1362 Ай бұрын
Thanks for the advice Mr kalindo
@FionaKhoma
@FionaKhoma Ай бұрын
Akunamizana kwambili athu amenewa mcp ikutula udindo pasi
@Raph-kayRaph-kay-g5v
@Raph-kayRaph-kay-g5v Ай бұрын
Utm samalani ndi kabambe ndi brocko yati musabwerere Ku DPP matchera chenjerani mafana
@Pangolinimw
@Pangolinimw Ай бұрын
The DC 🎉🎉🎉🎉🎉
@BrightNkhoma-xz4bg
@BrightNkhoma-xz4bg Ай бұрын
❤❤❤❤ ukupangila sogolo lowala DC
@CHEWATCHMAIDAH
@CHEWATCHMAIDAH Ай бұрын
It's true
@DONNEXKhama-bk1gy
@DONNEXKhama-bk1gy Ай бұрын
Ur right the DC akapusa kulowa mikangano
@user-sk3ld2ss7s
@user-sk3ld2ss7s Ай бұрын
Boni kalindo ndi chilata chopanda kanthu, chomangosokosera...
@Maliko-bp1xn
@Maliko-bp1xn Ай бұрын
Mukulankhula zooonadi
@PetroMatias
@PetroMatias Ай бұрын
Ndinzoonadi asangotora munthu
@user-be5fc3ed1i
@user-be5fc3ed1i Ай бұрын
The DC mwana wowopsya kwambiri Bon kalindo
@chirwaellace1093
@chirwaellace1093 Ай бұрын
The DC mnyamata oopya kwambiri 😅😅
@EmmanuelMalata-r4j
@EmmanuelMalata-r4j Ай бұрын
Mumatiyimilira bwana❤
@YolliyajeerasYeeras
@YolliyajeerasYeeras Ай бұрын
Mwana ooooooooooopsa kwambili
@RuthMoto
@RuthMoto Ай бұрын
Mukhalise comrade Bon kalindo
@user-pt8wb4vw6r
@user-pt8wb4vw6r Ай бұрын
Amp alibe nawe nthito kambwe iwe chisilu
@AwetuAmidu-u2j
@AwetuAmidu-u2j Ай бұрын
Wayankhula bwino bon
@user-pb6wb3iz7z
@user-pb6wb3iz7z Ай бұрын
Well narrated
@BrightNkhoma-xz4bg
@BrightNkhoma-xz4bg Ай бұрын
Athu opusa kwambiiri akuona ngat tikugona......... Our president Bon Kalindo 🇲🇼🇲🇼🇲🇼 😂😂😂😂 pepekale
@user-mk4ju6iw7c
@user-mk4ju6iw7c Ай бұрын
Mwathandidxa akafunakunyodxela anyodxele okha
@SHABBASELEMANI-o8d
@SHABBASELEMANI-o8d Ай бұрын
Ati PEPE KALE... koma DC
@FionaKhoma
@FionaKhoma Ай бұрын
We folow
@jacksonmaster2288
@jacksonmaster2288 Ай бұрын
Kalindo UTM amaikonda kwambili
@EstherBailoni
@EstherBailoni Ай бұрын
DC , tiye Nazo usaope
@DICODIDICODI
@DICODIDICODI Ай бұрын
No☝️THE DC
@richardjumah198
@richardjumah198 Ай бұрын
UTM malangizo a ulele awa please
@user-rr7je1zi8t
@user-rr7je1zi8t Ай бұрын
Kuti nkhaaaa wabwela bon kalindo
@KondwaniBilliat-t4g
@KondwaniBilliat-t4g Ай бұрын
Backward never forward ever ❤
@PeterNamphwanya
@PeterNamphwanya Ай бұрын
Chi booooon kalindooooooo🎉🎉🎉🎉🎉
@HusseinAdamLidezo
@HusseinAdamLidezo Ай бұрын
The DC
@user-ck7eb7tb7v
@user-ck7eb7tb7v Ай бұрын
Sakumudziwa Boooon Kaliindo
@user-do2cs8nf4b
@user-do2cs8nf4b Ай бұрын
Bola mwachenjez ali ndi khutu ambve
@Momweekly
@Momweekly Ай бұрын
Well spoken
@MecyMalothi
@MecyMalothi Ай бұрын
The D C our pangolin
@jumahgeorge
@jumahgeorge Ай бұрын
Following
@OwamiSimeon
@OwamiSimeon Ай бұрын
Born kalindo the deceeee
@user-rr5nq2uo6i
@user-rr5nq2uo6i Ай бұрын
Big up the DC
@AnyumbaJulias
@AnyumbaJulias Ай бұрын
Ulemu wako iweyo bon kalindo
@user-zl5wv8ix8u
@user-zl5wv8ix8u Ай бұрын
Kalindoo akunena dzoona
@jumahgeorge
@jumahgeorge Ай бұрын
The DC more 🔥
@JohnWindford-jv8ls
@JohnWindford-jv8ls Ай бұрын
Kma azipumako Tizimvako zina.
@marcelolemos1484
@marcelolemos1484 Ай бұрын
THE DC
@ClementJosephy
@ClementJosephy Ай бұрын
Inuyo munavaya patali ana achepa,... Eeeeee
@BrightonKamwendo-db1ci
@BrightonKamwendo-db1ci Ай бұрын
Mau onveka zeeed mbuyanga
@GiftJulius-ro9ev
@GiftJulius-ro9ev Ай бұрын
Kabambe simunthu ..
@MaxwellKananji-r5d
@MaxwellKananji-r5d Ай бұрын
Makamaka pamene wanena kut pakufunika mery chilima amutenge kut agwile naye ntchito pamenepo Mr DC mwanena zoona ndipo mzimu wa SKC utha kuusa mumtendele
@Extratremendouszeus
@Extratremendouszeus Ай бұрын
Chifukwa chamkazi wakeyo? Mukunama ....za Mulungu amaweruza yekha ndipo sapanga pangano ndimunthu...Za dziko lapansi musaphatikize Mulungu
@FelixKazembe-wi5zb
@FelixKazembe-wi5zb Ай бұрын
Ndichaka amalawi dale zimativuta chifukwa mumafuna anthu omwewo azipanga dale. banja lonse abambo akakhala president mwanaso akufunaso wu president omweyo ayi😂😂😂😂 dale sichoncho.
@user-hq6dq7zr1e
@user-hq6dq7zr1e Ай бұрын
Auzeni a utm azinyozela wokha
@TalazanGamah
@TalazanGamah Ай бұрын
We follow
@lydiagadama4887
@lydiagadama4887 Ай бұрын
The Dc
@YusufIbrahim-w1g
@YusufIbrahim-w1g Ай бұрын
Boooon kalindo is not sepro man is big man chizulo chat ambawi Allah bless him
@RhodaNombo
@RhodaNombo Ай бұрын
Mmatiimilila the dç
@oskidooscar7468
@oskidooscar7468 Ай бұрын
Aaaaaaaaaa awa amaopa manganya ndamzawo
@Raph-kayRaph-kay-g5v
@Raph-kayRaph-kay-g5v Ай бұрын
Manganya nkanyama kanji? Phwala lako wamva
@oskidooscar7468
@oskidooscar7468 Ай бұрын
@@Raph-kayRaph-kay-g5v manganya olo nda bambo ako angafanane iwenso chisilu et Manganya is a vp of malawi You like it or not
@TemwaKabisa
@TemwaKabisa Ай бұрын
The DC 🎉🎉🎉🎉🎉❤❤
@MosesShaibu-ee8hn
@MosesShaibu-ee8hn Ай бұрын
Pepekale ameneyo wakumalawi?kapenawaku ithiopia
@JosephyMagombo-t7d
@JosephyMagombo-t7d Ай бұрын
The DC ✊️
@stormchatepa134
@stormchatepa134 Ай бұрын
bwana nyo
@ellensambo6323
@ellensambo6323 Ай бұрын
❤❤❤
WANG'ALURA UKU AKUPHUNZITSA SAKUOPA ALIYENSE  |
29:10
DZIWE TV
Рет қаралды 6 М.
Please Help Barry Choose His Real Son
00:23
Garri Creative
Рет қаралды 21 МЛН
Harley Quinn's revenge plan!!!#Harley Quinn #joker
00:59
Harley Quinn with the Joker
Рет қаралды 24 МЛН
7 Days Stranded In A Cave
17:59
MrBeast
Рет қаралды 82 МЛН
Times Exclusive featuring Bon Kalindo - 6 January 2024
1:03:20
Times 360 Malawi
Рет қаралды 247 М.
BON KALINDO LERO PA  21 AUGUST  2024 |
16:53
DZIWE TV
Рет қаралды 29 М.
Vice President Chilima's visit to the SVTP (Chichewa Interview)
1:47
Shire Valley Transformation Programme
Рет қаралды 57 М.
Olo Anthu A Ku Kasiya MCP Sakuyifuna - Comrade Ntanyiwa
21:24
Nyasa VoiceBox
Рет қаралды 24 М.
BON KALINDO LERO PA 22 AUGUST 2024 |
17:14
DZIWE TV
Рет қаралды 20 М.
Artimiza Revela Esquema De Venâncio Mondlane no Novo Partido
16:18
ONELANI ACHAKWERA  AKUPALASA NJINGA | KUPEPELUKA PANJINGA |
9:22
MICHAEL USI  KUDYA PA CHIYIMILIRE ONELANI  |
16:00
DZIWE TV
Рет қаралды 9 М.
Please Help Barry Choose His Real Son
00:23
Garri Creative
Рет қаралды 21 МЛН