Nde ndiwe mtsogoleli nkumawopa kukumana ndi anthu omwe ukuwasogolera pali zabwino pamenepa ndiyankheniko
@GracePendame23 күн бұрын
Yomweyo apapa ndiye ziribwino
@Chifundokapondodza-f6d23 күн бұрын
Mwapanga zanthengo wapatari kwambiri
@emmaculatemenzeiwa21 күн бұрын
It's not too late it's a united movement ❤
@user-qp8kh2hj9o23 күн бұрын
SKC forever in our hearts ❤❤❤❤❤❤
@user-wq9ex2sf3b23 күн бұрын
UTM for life from Zambia 🇿🇲
@TroubleMuthala23 күн бұрын
That's nice 👍
@ThomasMwandila-tn7cf23 күн бұрын
Mama mwayankhura nthaks
@SydneySibande-z6k23 күн бұрын
Very wise Leaders of UTM and all members, Leave crodiles alone to eat themselves,RIP Baba Saulos Chilima
@Vaps-king23 күн бұрын
I can feel the pain inside her speech 😢
@user-zr7wk4oq2x23 күн бұрын
We're a little bit happy now 🙏
@TopoTopo-bm4vw23 күн бұрын
I like it 👍
@henryphiri610023 күн бұрын
Kaliati ndinu a experience ku ndale musalore Manganya kukupusitsani.ndiwazitsutso
@JeanyMdedza23 күн бұрын
Good idea
@EagerChicken-qj6xu23 күн бұрын
Komabe ndikukhulupilira kuti mwini wake sakadakhalanso ndi maganizo obwelelanso ku chipani cha dpp. Kuli aford udf konso ndi zipani zina. Think twice .f,
@user-qp8kh2hj9o23 күн бұрын
Zoona nkhani ikumveka bwino ndithu palibe chifukwa chibwelera ku DPP
@HassanIssaAbdulKarim23 күн бұрын
Strong woman . Courageous. Fearless. Few we have .
@user-fi7ko7bl6f23 күн бұрын
Lululuuuuuuuuiuuuuu mwachita bwino kwasiya atombolomboyo a MCP aziphana okha okha. Very soon freedom is coming tomorrow mwachita bwino kutuluka . Lero ndigona bwino iiiiii infa ya Dr Chilima aaaayosaiwalika😭😭😭😭
@HakeemJossam23 күн бұрын
look sharp 🎉
@MphatsoSteven-r8n23 күн бұрын
Mwachita bwino kutulukamo mutonse mai Patricia kaliat mwalankhula bwino kwambili🎉👏👏👏👏
@KhamaRaysonYoyora-nj9so23 күн бұрын
Good development
@HaroonAlibarara21 күн бұрын
Zili bwino ndinthu utm oyeee🎉🎉🎉🎉
@MonicaSembo17 күн бұрын
SKC made me to join politics
@misheckjanuary169623 күн бұрын
Zathapo 🤗
@user-xx4jb9se3z22 күн бұрын
Kaliati morefire mai inuyo MULUNGU adzikudalitsani ine utm my vote
@user-nz9ty3ih1v23 күн бұрын
kkkk kuteloko apa paseweredwa game kungoti apange gwilizano ndi DPP UDF ndi a FOD
@julietbanda520323 күн бұрын
Manganya ndiwa mcp,mayi Patricia kaliat congratulations for your speech
@HastingsMaclondonmuhoko20 күн бұрын
Good decision
@SuzgoMunthali23 күн бұрын
Mukatuluka 2023 bwezi chilima alipo Lero Koma Palibe yomwe amaziwazamawa only God knows
@Extratremendouszeus23 күн бұрын
Amwene...chilima samamva
@tiyowoyechiparton278523 күн бұрын
Muphese ma lawyer pano 😂😂😂
@user-vf2fo1mb2c23 күн бұрын
Yebo chomene mwawanthu 😅❤MWN
@Leo-fj6gz23 күн бұрын
Mwabwela inuyo 🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥💪🏾💪🏾💪🏾🇲🇼
@alexgweje861022 күн бұрын
Mwachedwa inu mukadapanga izi nthawi imene Chilima adakali ndi moyo anthu amkakuuzani kuti mutuluke Alliance koma kusamva inu bwelerani ku Dpp basi
@MAGIEWAJOHN20 күн бұрын
Ai zikomo kwambiri mwachita bwino ndithu ambuye adzikutsogorerani ndithu
Mary wachita bwino kuzisiya, ndalama anakamudyera iya
@FrancisBanda-g9v21 күн бұрын
Osada nkhawa ninthawi ikubwera 2025 kwakhala minyezi yocepa mai
@HussainKabila23 күн бұрын
💔💔💔💔🤪🤪🤪🤪😭😭zosangala mwachita bho kwambili osaopa
@SbueSbusiso23 күн бұрын
Osaopa tili pambuyo pa utm
@Inayake23 күн бұрын
Manganya ndi wa MCP, he is not a genuine member of UTM, Hon. Kaliati I salute you!!
@RobertGoliat-gt2qh23 күн бұрын
Bwererani komwe mudachokera congrats UTM
@IdrisaKapinga23 күн бұрын
Zapamwamba hvy🎉
@FredrickKachingwe23 күн бұрын
Utm motto ku buuuu
@webstermbewe839523 күн бұрын
Thanks
@atupelemposa478623 күн бұрын
Utmost for life
@HopefulCoralReef-tx4vx23 күн бұрын
Achita bwino ndithu potuluka chipani cha MCP or blood part
@actuarialscience228323 күн бұрын
Ndalowanso UTM 😊😂
@user-un4pm4yt5i23 күн бұрын
Congrats UTM
@SamuelAntone-mz6nq22 күн бұрын
Tili momo UTM tikavotabe basi kya tikaluza kya tiwina tilimomo ife
@user-du9qs4tb6u23 күн бұрын
UTM you have to move manganya
@user-es4jt6ds8m22 күн бұрын
Macheal utsi asapiteso Ku UTM please guys
@joicemumba360823 күн бұрын
Amen
@ChikondiBJosaya-pr1zu22 күн бұрын
Apa ndiye DPP 2025 wooo
@andyngola354222 күн бұрын
Mcp ikhale yokha, all the best
@ChikumbutsochantzMakumba23 күн бұрын
Ntchana chete😂
@emmanuelkamwagha936423 күн бұрын
Good
@AufiThera23 күн бұрын
Mulungu wayankha the DC 💪 alandile ulem
@MemoryGalaonga21 күн бұрын
Chipani cha utm chachinyata
@BiCyfer-pp8ke22 күн бұрын
Kkkk km amai awa
@user-fn5pu5zw5t22 күн бұрын
Osabwelelanso ku DPP please
@ChisomoamitoniSauzandeamiton23 күн бұрын
aaaa@a🤭 chavuta ndi chani kuti (UTM) ituluke mu tose
@Extratremendouszeus23 күн бұрын
Ingodikira uvotere MCP
@WysonMalack23 күн бұрын
Mhuuu aaa ine nkhani ya a Chilima omandivetsa chisoni mukayankhura kungotchurapo a Chilima sindipilira Loma kututsa misozi naso manga basi ndipo ndimati adaferanjiii? Mzimu wawo uziusa mu ntendere mpaka kumuvula kohala maliseche mhuuuu Malawi mchiyani?
@BenedictChikaoneka23 күн бұрын
Akuluakulu achipani basi omwewo? Tizipani tinati koma guys