No video

DALITSO KABAMBE CHIFUKWA CHANI ADATULUKA DPP.

  Рет қаралды 11,296

HOT 265

HOT 265

Күн бұрын

Пікірлер: 38
@LovelyGalaxy-rb7yl
@LovelyGalaxy-rb7yl Ай бұрын
Ayende bwno mwana waukape Awona ngati akapeza upele ku UTM, KOMA AXIWE KUTI NDIMWANA PANDALE 😅😅😅
@esaMoha-dm4kj
@esaMoha-dm4kj Ай бұрын
ngani yankulla and yakt ankufunna nkumugulla ndi m c p nkoma saneena nkandu ankabambe
@user-lw4hw9ce4w
@user-lw4hw9ce4w Ай бұрын
APM akuzasosora aswiswiri onse awo achoke alibe meaning ku dpp
@ThomasChiwaya-qx9mf
@ThomasChiwaya-qx9mf Ай бұрын
Ine mau ambiri ndilibe kom Peter mulungu adalise amalaw tinaphuzir bas kut chikuni chachikulu chimasunga moto bas
@ephraimphalawala4720
@ephraimphalawala4720 Ай бұрын
At this stage, we need to concentrate on National Interest and not political. Mavuto akula ku Malawi. Malawi must unite first to defeat MCP. That's top on the agenda. Politics ndi maudindo later.
@user-db3mh9wr9v
@user-db3mh9wr9v Ай бұрын
Kabambe wachita bwino akhale President wa UTM basi best wishes DK
@ephraimphalawala4720
@ephraimphalawala4720 Ай бұрын
DPP my vote
@OmegahThipa
@OmegahThipa Ай бұрын
Ngakhale anthu ambiri angayike maganizo awo motani, Ndichisankho chawo koma sikuti DPP ingagwedezeke palibe (APM 2025 boma akutenga
@JayoneAmbitious
@JayoneAmbitious Ай бұрын
Kabambe apanga phuma peter anafunika awatenge akabambe kukhala vp wao after 2or 3 years akanapanga resin kuwasiila akabambeo km paokha sangawine
@lungisanishezi1023
@lungisanishezi1023 7 күн бұрын
Pali ndale zoopsya dpp ndi a katundu,akudzaphatikizana dpp ndi utm
@gifttembo2306
@gifttembo2306 Ай бұрын
DPP ndiyochenjera akudziwa kuti utm ikhala pa mgwirizano ndi dpp and akufuna adzachithetse mphamvu chipani cha utm in the coming yrs. pomuika madalitso kabambe as vice president
@user-lu8px7td6p
@user-lu8px7td6p Ай бұрын
Akufuna udindo wa uprezident
@user-nj4ob8jw6y
@user-nj4ob8jw6y Ай бұрын
Mbabva iyiyi sidatuluke ku DPP, koma a Peter Mutharika amutuma kuti akayimile ku UTM cholinga ndichofuna kukatenga mabvoti a UTM kukapeleka ku DPP. Chonde a Malawi chenjerani
@AndrewSimakweli
@AndrewSimakweli Ай бұрын
Akabambe si andale
@StiveKantiki
@StiveKantiki Ай бұрын
Sanalakwise Ali Malawi momuno kulikose kumene angalowele akatumikila amalawi
@adamu1287
@adamu1287 Ай бұрын
Komano kunena zoona kabambe simunthu wandale
@actuarialscience2283
@actuarialscience2283 Ай бұрын
Ameneyu ndi wandale. I don't believe he has left DPP. Why? Here is the reason: HE ENDORSED APM.
@user-zo3bf3ec3g
@user-zo3bf3ec3g Ай бұрын
Muyendako bwino koko
@ChrisEnos-to5uv
@ChrisEnos-to5uv Ай бұрын
Uyu sanatuluke ku Dpp achita kumutuma
@user-dc7qq9yz3v
@user-dc7qq9yz3v Ай бұрын
Akamati mfulumila ndiumeneu
@bornface4786
@bornface4786 Ай бұрын
This is not a right time for the Kabambe to move we can he doesn't lo Malawi
@user-hb2hr5oc9l
@user-hb2hr5oc9l Ай бұрын
vuto anthu ambili sakufuna kunthandiza Malawi Koma Kuba ndalama Za boma akakhala pa udindo
@AlfredNazombe-me2ly
@AlfredNazombe-me2ly Ай бұрын
Muononga dziko ndiinu amene achinyamata simuziwa chomwe mukuchita munasonkhana mu 2020 lero ndi izi mumazitenga ngat otsogola lero mukuzinzika
@user-ml2vw1dc9c
@user-ml2vw1dc9c Ай бұрын
Achinyamata akutulula kamba koti APM sapeleka mpata kwachinyamata ndiye ataya chikhulupililo
@user-vl8uw8mc3u
@user-vl8uw8mc3u Ай бұрын
Kuthamangila udindo.saphulapo kanthu awa
@AntonyEdwinMuyila-ij4sx
@AntonyEdwinMuyila-ij4sx Ай бұрын
There is no future for the youth in Dpp.
@user-bp1cu2rb4f
@user-bp1cu2rb4f Ай бұрын
Kape iwe:Palibe chomwe uli.Galubwakoooo.Kachipanda ka peter bwenzi ulingati ndani?
@yasitafuphiri-nw2he
@yasitafuphiri-nw2he Ай бұрын
This is a plot for DPP 😢, APM will make him his running mate Kutuluka DPP ,kudzagwiranso ntchito ndi DPP yomweyo😮?? Pali nzeru apa??
@eliffagondewe8214
@eliffagondewe8214 Ай бұрын
Kabambe anatuluka kalekale ku Dpp, the thing is iyeyu Ali ngati nankhumwa amafuna president komaso ndiwa phuma nde no wonder palibe move apa ndi APM koma iyeyu wafuna you can see ma meeting ambiri adpp samapitako.. Ayende bwino
@MatthewsJohn-kv8fj
@MatthewsJohn-kv8fj Ай бұрын
Kuba bas ndizimene akufuna anthu kufinya mukaka ng'ombe yakuwanda kare
@user-bz4fs6gv8v
@user-bz4fs6gv8v Ай бұрын
Uyu amutuma serious
@JustineAdani
@JustineAdani Ай бұрын
y⁷
@JaneMoyo-ws2di
@JaneMoyo-ws2di Ай бұрын
MOTi ku UTM kulibe oti angaimile u president? Zikukhala bwanji? UTM say NO to Kabambe ( UTM presidency).
@user-qp8kh2hj9o
@user-qp8kh2hj9o Ай бұрын
Musavutike wakuuzani ndani zomwe mukunenazo
@user-qp8kh2hj9o
@user-qp8kh2hj9o Ай бұрын
Aliko kabambe akutaya nthawi uyo
@user-mw3kj4qz7b
@user-mw3kj4qz7b Ай бұрын
Let just Mary chilima stand guys to heal the heart s of Malawi
@user-nj4ob8jw6y
@user-nj4ob8jw6y Ай бұрын
Kabambe ndiwe mbabva wakuba. Udaba ndarama zambiri, zankhani nkhani. If u think that u r clever, Ukunama. U will never become president of UTM, never. Ndiwe mwana wa ng'ono pa ndale ku Malawi kuno.
ZOMWE ZIDALI KU NSOKHANO WA DPP 29 August 2024
24:21
HOT 265
Рет қаралды 2,1 М.
WILL IT BURST?
00:31
Natan por Aí
Рет қаралды 30 МЛН
나랑 아빠가 아이스크림 먹을 때
00:15
진영민yeongmin
Рет қаралды 4,5 МЛН
白天使选错惹黑天使生气。#天使 #小丑女
00:31
天使夫妇
Рет қаралды 15 МЛН
RFK Jr. drops out, endorses Trump: FULL SPEECH
48:21
FOX 4 Dallas-Fort Worth
Рет қаралды 1,7 МЛН
Inside Iran: The proxy war on the brink of erupting | Four Corners
46:29
ABC News In-depth
Рет қаралды 725 М.
Nancy vs Che Nkope - Zipungu
15:07
CHE NKOPE
Рет қаралды 8 М.
WILL IT BURST?
00:31
Natan por Aí
Рет қаралды 30 МЛН