No video

Enock Chihana kuulura poyela zinsisi zomwe chilima anamuuza asanamwalire zokhunza Tonse Alliance

  Рет қаралды 230,227

Makosana

Makosana

Ай бұрын

Пікірлер: 409
@StanleyMkulama
@StanleyMkulama 22 күн бұрын
Akatundu awa!!!!! He is so courageous!!! speaking with no Fear,, he sounds like Chilima in his Bond of courageous.
@MasausoMsiska-rz3id
@MasausoMsiska-rz3id Ай бұрын
Munthu koma uyu speaking without fear....Big up Mr chihana
@lloydjeremiah2250
@lloydjeremiah2250 Ай бұрын
eeee kma this man is so courageous
@user-fz3gu2ez1o
@user-fz3gu2ez1o 26 күн бұрын
Eeeeee Koma SKC 😭😭😭😭 Ine imfa iyiyi.. Imandiwawa.. eeeeee
@JesusChristFollowers-ez9zu
@JesusChristFollowers-ez9zu Ай бұрын
Mr. Chihana is man of his word, ndipo zikupanga prove that he is the son of his father. Amenewa ndi amene anathema ndi kamuzu, apa chakwera akuchoka, ndavomereza anthufe sitimafa koma maonekedwe athu ndi amene amasintha
@arnoldkaikenkayange
@arnoldkaikenkayange Ай бұрын
Afford my vote
@magex887
@magex887 18 күн бұрын
Koma ndiye.big up chihana❤
@iconiclife6811
@iconiclife6811 22 күн бұрын
So powerful bwana We need this Energy in our country honestly achinyamata ambiri akufuna ngati iziiii
@HopeJaffari
@HopeJaffari Ай бұрын
Ramaphosa wanthu waku Malawi 💪💪
@NoluvuyoMatutu
@NoluvuyoMatutu Ай бұрын
😂😂😂😂even me I thought like that ndtaona pic yake poyamba
@memoryziyaya2593
@memoryziyaya2593 Ай бұрын
true ..they are resembling very 😅
@kusekejere
@kusekejere 28 күн бұрын
SKC has gone leaving a message that malawi is the land with possibilities but the problem are the leaders. What a humble guy. Rest well sir
@jonasmunthali848
@jonasmunthali848 Ай бұрын
I didn't know dis guy can talk lyk dis🙌🙌🙌🙌🙌🔥🔥🔥🔥🔥
@hopesato
@hopesato 28 күн бұрын
Anthu akwiya mkoz
@jonasmunthali848
@jonasmunthali848 28 күн бұрын
@@hopesato ndaonaso🙌
@luciatembo-e4f
@luciatembo-e4f 28 күн бұрын
Straight wise proud of you chihana🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥
@papelariareis.e.
@papelariareis.e. 5 күн бұрын
This guy is very strong 💪 🎉🎉🎉
@amandamoyo7156
@amandamoyo7156 Ай бұрын
God protect Mr Chihana....we love u
@HappyAbyssinianCat-xt2bm
@HappyAbyssinianCat-xt2bm Ай бұрын
Km ndi zoona chakwera popanda chilima sukanawina galu iwe chakwera unapanga ndiwolotse ndikakutafune galu iwe chakwera dzimaso dzako unatiphera ngoni wathu
@catherinesilverio-d5w
@catherinesilverio-d5w Ай бұрын
Pankongo pake ameneyu ndipo mabala awawa sazapola taaaa
@user-ky4ce9gb6j
@user-ky4ce9gb6j Ай бұрын
Ndipo dziko lino analitembenuza dziko lino
@user-rf4br1fv2z
@user-rf4br1fv2z Ай бұрын
Ndiye chilima popanda chakwera adakhala vp tisamalakhule mbali imodzi chilima tu adali vp from 2014 up to 2024 ineyo ndimafuna nditadziwa zomwe adapanga kapena ankadikila adzakhale President kuti inuyo mudzayamve kusangalala to me i don't know thanks God ineyo ndimadziyimila from nyumba ya maudzu to mansion bra inuyo dikuilani chiloma wina kuti moyo wanu udzasithe
@DJBless1506
@DJBless1506 18 күн бұрын
@@user-rf4br1fv2z chilima anakhala vice president chakwera kulibe kapena wadya chamba eti?
@MikeMerecah
@MikeMerecah Ай бұрын
Kuno kwa msundwe keep it up chihana we need truith,
@DN-mp8pp
@DN-mp8pp Ай бұрын
We need fearless leaders like you! Ndipo ma leaders ena atengelepo phunzilo, learn to be fearless like Chihana osamangokhala phwiiii osalankhula
@AgnessMzengo
@AgnessMzengo Ай бұрын
Wise leader...... Tell them
@lyiemax
@lyiemax Ай бұрын
Powerful, proud of you Honourable Chihana
@fostersimbi8820
@fostersimbi8820 Ай бұрын
Didn't know this guy amayankhula mwamphamvu chonchi ❤🔥
@FelixChimsNyirenda
@FelixChimsNyirenda Ай бұрын
Tell them the truth don't be afraid 😨 GOD will guide and protect you, we relay behind your your back.
@chrisneySwanepoel-yu5vd
@chrisneySwanepoel-yu5vd 29 күн бұрын
Voice iyiyi itha kundipangisa kuyamba kusapota afford 💪💪💪💪
@WilliamNyirenda-xq4km
@WilliamNyirenda-xq4km 27 күн бұрын
Koma ajoinane ndi utm ndili mumbuyo mwao
@tsanzomwanya
@tsanzomwanya 22 күн бұрын
Akut Chisilu chilichonse Chitha kukhala nduna
@kennedybanda
@kennedybanda Ай бұрын
Even the bible itself says do not touch my anointed ones.
@user-nf3ik3ff6y
@user-nf3ik3ff6y Ай бұрын
Good Messnge Mr Enock Chihana❤
@EmmanuelMlinganiza-bm7li
@EmmanuelMlinganiza-bm7li 27 күн бұрын
Enock Chihana (Akatundu aboma) 🎉🎉🎉🎉 Thawi yakwana 🎉🎉🎉🎉
@user-cn3gi2vf5n
@user-cn3gi2vf5n Ай бұрын
You are the great man thanks for the truth
@WilliamNhlane-fd9hi
@WilliamNhlane-fd9hi Ай бұрын
Good leader
@tawongamhango7335
@tawongamhango7335 22 күн бұрын
Chihana we dont want hate speech be like you father who never preach hate speech
@YohaneMuonja
@YohaneMuonja 26 күн бұрын
Am not a politician and am from kumwera but ilove ana achihana personally.Courage ya nyoo
@dalsonkaluwa6575
@dalsonkaluwa6575 26 күн бұрын
Mwana wa Simbi ya Moto 🔥🔥🔥💪
@JoelMphoka
@JoelMphoka 25 күн бұрын
Watching from Soweto Johannesburg. Powerful.
@user-jv7xw1fo6c
@user-jv7xw1fo6c 24 күн бұрын
Sadzagona tulo wopha chilima
@josephphiri7481
@josephphiri7481 28 күн бұрын
Great leader 🎉mr chihana keep up
@sylvesteralfred8355
@sylvesteralfred8355 Ай бұрын
Lero ndiye kuli kung'aluladitu sizinaoneke
@EstherDebwe
@EstherDebwe 24 күн бұрын
Kuli zinthutu👐
@augustMag
@augustMag Ай бұрын
Haaaa mwatipha basi tonse Amalawi mukanamuuza zoona mwanao kuti fisi ndi fisi sangasithe mawaanga 😭😭😭😭
@RamzyMsukwa
@RamzyMsukwa 27 күн бұрын
The guy fearless and speak energetic
@ritanjolomole2076
@ritanjolomole2076 Ай бұрын
All the best Aford
@yvescadet8524
@yvescadet8524 Ай бұрын
Congratulations honorable chiana
@DaveChirwa-s4j
@DaveChirwa-s4j 27 күн бұрын
I lv it.
@user-nv3rf7bl7r
@user-nv3rf7bl7r Ай бұрын
A chilima asanduka kamupeni pano 😢😢😢 ambuye nkhondo ndiyanu chilichose mukudziwa ndinu
@user-tk6qh9zs7h
@user-tk6qh9zs7h Ай бұрын
Zomvetsatu chisoni kwambiri. Ndikanakonda a ku Banja akanaketsa Zopusa zimenezo. Chidziwika ndi chakuti SKC ndi CHIHANA were not Friends. Ngati zomwe akunenazo ndi zoona tione umboni wake. Atiuze nthawi, tsiku komanso Audio or ma message olemba. Musaiwale kuti ndi yomweyinso anabweretsa nkhani yonama ku Nyumba ya Malamulo atafunsidwa za umboni anakanika kupereka. SKC awuza bwanji iyeyo kusiya kuuza utm members?. CHIHANA ndi ONAMA kwambiri
@user-nv3rf7bl7r
@user-nv3rf7bl7r Ай бұрын
@@user-tk6qh9zs7h ndipo inu koma ambuye akuwona zomwe akupangazi ziwabwelela wokha kapeni ngati yavuta kungosiya mbanji elsh
@mishecksipolo7153
@mishecksipolo7153 Ай бұрын
Palibe wasanduka campaign apa ,akungokamba chilungamo period
@viennasamuel2976
@viennasamuel2976 Ай бұрын
Ndipo live akunenazo ndizoona ikakhala campaignyopangila munthu nawonso apanga ya kamuzu iyaaaa
@user-nv3rf7bl7r
@user-nv3rf7bl7r Ай бұрын
@@mishecksipolo7153 musalowetse ndale pa imfa yamunthu muziganiza mofatsa musanayankhule nyasi zanuzo inu simulungu
@wymankamanga-xd5pv
@wymankamanga-xd5pv 26 күн бұрын
achihana uko muli uko Pala pangawa mwayi mwizeko ku nkhatabay mkondezi area I beg
@smashingogden4236
@smashingogden4236 Ай бұрын
We soldier on!... very brave mr chihana junior 💪🏼🇲🇼... speak it like it is....
@ruthkundwe7448
@ruthkundwe7448 29 күн бұрын
No rest for the wicked
@PemphelaniTcheza
@PemphelaniTcheza Ай бұрын
Chilungamo sanong'onotu 😢😢with heart broken
@karenn2969
@karenn2969 12 күн бұрын
True voice of a leader, thus why he was the first to demand enquiries into the death of Chilima
@ClaraMkandawire-d2k
@ClaraMkandawire-d2k 26 күн бұрын
Kuyankhula koma ukuuu aaaaseeeee👊😂
@PatrickKabudula
@PatrickKabudula Ай бұрын
You are not alone mr
@SigoMw
@SigoMw Ай бұрын
Ndipo simunati akanantchulidwabetu chilima mpaka mpaka muphulikeee amfiti inu
@user-jm8kw9gw2d
@user-jm8kw9gw2d Ай бұрын
Aford the mother of all political parties in Malawi, it's your time Big Man, mcp is afraid of you in Jesus name
@shonmike-su7qk
@shonmike-su7qk 28 күн бұрын
Mcp inalakwitsa kwambiri kuphwanya lonjez ndipo izizi zimenez amalawi zatikwiitsa kwambiri from molongolo Tanzania
@user-ko1lk3br4r
@user-ko1lk3br4r 22 күн бұрын
Km Inu simudzalowapo mboma truth
@tumpalechihana5073
@tumpalechihana5073 Ай бұрын
Our own leader
@NysonStandy
@NysonStandy 29 күн бұрын
Go ahead mr Cihana
@WAZAKILIBANDA
@WAZAKILIBANDA 29 күн бұрын
Kumeneko nde kulankhula dad🥰🥰🥰🥰🥰
@MirriamKambale
@MirriamKambale 29 күн бұрын
Chakwerayutu si m'busa anthunu mangosokoneza munthu uja ndi nthakati. Mfwiti ya tyala iliye na mzeru ingaphepese yai after those words pray hard angakusowetse
@user-dh8ho2qt4h
@user-dh8ho2qt4h 21 күн бұрын
❤❤❤ love you dad. We all cry our vice president chilima.😢😢😢
@WilliamNyirenda-xq4km
@WilliamNyirenda-xq4km 27 күн бұрын
Viphalileni bwana viwanthu voina mitu ivi you are my vote
@MadalitsoTamayenda-ez5pj
@MadalitsoTamayenda-ez5pj 27 күн бұрын
Powerful voice
@JusticeDamalekani
@JusticeDamalekani 13 күн бұрын
Akamuna awa❤ osati akapamba enawa😢
@user-oc9vl9xz8e
@user-oc9vl9xz8e Ай бұрын
Kumeneku ndiye kuyankhula Kwa Mtsogoleli wadziko kuyankhula mosaipa wina aliyense
@PiliraniMalemia
@PiliraniMalemia Күн бұрын
God is watching from a distance
@RoseTaika
@RoseTaika 6 күн бұрын
So courageous
@user-ty4pq5ub3q
@user-ty4pq5ub3q 29 күн бұрын
RIP CHILIMA....😢😢. Auzeni live live..akapukuu ..nduna zokuda mbuuuuuuu
@unstorice4045
@unstorice4045 Ай бұрын
Appreciate you chihana🎉🔥🔥🔥🐐
@ConnexMtika
@ConnexMtika 15 күн бұрын
Ilov AFORD leader fearless
@OsimanIbnAkim
@OsimanIbnAkim Ай бұрын
Your the best speach 💪💪
@PemphelaniTcheza
@PemphelaniTcheza Ай бұрын
We have lost a great leader SkS because useless party mcp😢😢
@WilsonMillion-p2u
@WilsonMillion-p2u 11 күн бұрын
Ndiye cadet wachabechabe uzithupsya amalawi kuya nkhula chilungamo.apa ngakhale wina azinama koma imfa ya chilima ipase phunziro
@RespectMbewe
@RespectMbewe Ай бұрын
Speak out Mr Chihana
@chcmzuzudiocese5916
@chcmzuzudiocese5916 18 күн бұрын
Chakufwa Chihana weniweni
@ChisomoKalimba
@ChisomoKalimba 9 күн бұрын
Mudzamwalira osalamulirako dziko inu! Chifukwa chachimtima chasanje
@louisbonongwe8537
@louisbonongwe8537 Ай бұрын
Whoever has a hand on SKC will never have peace and enjoy his days of life.
@Issahkabichi7.
@Issahkabichi7. Ай бұрын
Ana achibwanaa
@williamchimpesa
@williamchimpesa 29 күн бұрын
For sure
@KennedyChitunda
@KennedyChitunda 28 күн бұрын
In Jesus name Amen
@wilkeyskapanga7510
@wilkeyskapanga7510 23 күн бұрын
True
@isaaczuze
@isaaczuze 3 күн бұрын
Enock chihana akunena zoona ...amasuleni agaluwa ..chimwendo ndiye akuzimva kwambili ndipo ndi munthu amane amakonza ziwembu zonse za chakwera
@LouisNgowera
@LouisNgowera Ай бұрын
Ndayamba afford basi😂😂😂
@cynthiakamunga8045
@cynthiakamunga8045 Ай бұрын
😂😂😂
@user-dh8ho2qt4h
@user-dh8ho2qt4h 21 күн бұрын
😂😂😂
@EmmanuelGasiten-fo5dr
@EmmanuelGasiten-fo5dr Ай бұрын
No SKC, indeed no MCP
@CharlesChilinde
@CharlesChilinde 25 күн бұрын
Kuulula nzinsinsi za chulungamo timauula miniwake ali ndimoyo osatizi izi menenezo ayi ulekeni Mzimu wa chilma uuse mu mtendere osati zonena mbweeeee pezani zina zonena osati kutukwana anzanu .😅😅😅
@lonelychakhala8449
@lonelychakhala8449 20 күн бұрын
Maliro aja trapeze zolankhula pa campaign popanda maliro aja fundo tinalibe fundo zake zimenezi zingatukule Malawi?
@CatherineChalema
@CatherineChalema 19 күн бұрын
Umbuli wazika mizu pa Malawi! Kwawo safa agalu awa komanso ngozi saidziwa. School ija ndiyabwino umbuli chihana chonsecho akudziwa kuti munthu anafa pa ngozi🚮
@FannyKumwenda-u4h
@FannyKumwenda-u4h 9 күн бұрын
My vote
@GraceZumazuma
@GraceZumazuma Ай бұрын
Chilungamo osamaopa chakwera aziziwa
@martinBPhiri
@martinBPhiri 29 күн бұрын
Nanga zoona tizingomva zoti a Chilima adandiuza 😅😅😅 usiyeni Mzimu wa Vice President wathu uwuse mumtendere
@McbeaulzJere-g7u
@McbeaulzJere-g7u Ай бұрын
Ndifera ndembera no2
@NeemaMatewere
@NeemaMatewere Ай бұрын
Thanks for the information
@MaloneBanda
@MaloneBanda 23 күн бұрын
Big up 💥💥💥
@janetbyson
@janetbyson 21 күн бұрын
Chakwela mfiti kobasi waiwala kuti anakupangila campaign Chilima analakwa chani
@clearbooks355
@clearbooks355 29 күн бұрын
Well spoken
@ZahnoorMilan
@ZahnoorMilan 17 күн бұрын
Powerful talk
@tanishadias
@tanishadias Ай бұрын
Go deeper Enock chihana
@user-cx8gk5en6h
@user-cx8gk5en6h 28 күн бұрын
I respect this guy
@johnkatapeh7182
@johnkatapeh7182 Ай бұрын
Kkkkkk chitsiru chinachake ndi nduna,,,,moto buuuuuuu
@maxwellofficialmusicartist1881
@maxwellofficialmusicartist1881 19 күн бұрын
Chilungamo chonsechi bwana mumasuga mukudziwa etii 😢
@faidaceciliaYekha
@faidaceciliaYekha 28 күн бұрын
Kumakhala munthu wolimba mtima ngati chihana💪
@sweedenBanda
@sweedenBanda 21 күн бұрын
Nice ndzaknda
@Jacjilinesawu
@Jacjilinesawu 6 күн бұрын
Koma yaaaa❤
@sofananamtsina
@sofananamtsina Ай бұрын
Ngati mulibe chokamba ndibwino kudekha coz zimenezi si fundo zoti zingatukule dziko ayi, mpake Malawi ali otsalira kwambiri kamba kosowa fundo .
@Jbzgambojunior
@Jbzgambojunior Ай бұрын
Mbuzi iwe
@user-mq7ou5xp5m
@user-mq7ou5xp5m 29 күн бұрын
Machende ako iweo osabweletsa fundo yako
@GiftKumbambe
@GiftKumbambe 29 күн бұрын
Ndizomwe akunenazo kapena akuchita kuwuzidwa
@SHENCOHNSOLOMBA
@SHENCOHNSOLOMBA 13 күн бұрын
Dolo 🎉
@ELLIOTNALIKATA
@ELLIOTNALIKATA 5 күн бұрын
Chakwela wanyema mu 18 an box mu thawi yoonjezela then refer lee mkuzaimba penate... Mu thawi yonjezela
@GiftJDavison-ru4kq
@GiftJDavison-ru4kq 22 күн бұрын
ZIKAMBANI ZOMWE MUZACHITIRE ANTHU , MAKUTU ANU
@MichealDPhiri
@MichealDPhiri Ай бұрын
Kkkkkkkkk 😂😂😂 ati kambuku koma amalawi munasiya mantha
@paulnyondo7572
@paulnyondo7572 Ай бұрын
Koma chakwera azibibira muthrauza ndithu .
@HassanYusufu-q4f
@HassanYusufu-q4f 9 күн бұрын
Ulemu wanu bg
小蚂蚁被感动了!火影忍者 #佐助 #家庭
00:54
火影忍者一家
Рет қаралды 52 МЛН
Inside Out 2: Who is the strongest? Joy vs Envy vs Anger #shorts #animation
00:22
Jumping off balcony pulls her tooth! 🫣🦷
01:00
Justin Flom
Рет қаралды 33 МЛН
Tamale Mirundi  JR ali mu maziga 🥹🥹
32:05
Kasuku Live
Рет қаралды 20 М.
Tamale Mirundi; Mukulu we ayogedde obudde bwe obwasembye ku nsi.
20:03
Zomwe Zinachitika Kut Ndege Isowe
5:19
Sam Malvitha
Рет қаралды 220 М.
小蚂蚁被感动了!火影忍者 #佐助 #家庭
00:54
火影忍者一家
Рет қаралды 52 МЛН