This is true and he was warrior and may his saul rest in peace 😢😢😢😢😢😢😢. Chakwera akutinyasa. Chakwera ndiopa kwambiri ndipo akulitenga dzikori ngat ndilamake.
@sulleahmnyimbili13627 күн бұрын
Rest well SKC, thanks for the information
@patrickmacheso50628 күн бұрын
Well spoken Mr Man,, tikufuna anthu olimba mtima ngati inuyo Mr,, Mmene mukuyankhula chonchi ma Members a MCP akusakani bwana.
@AliceChipeta-pc3nb8 күн бұрын
Mzimu wachilima mmmm ndi waukali
@Kilocssreaction9 күн бұрын
Amene akudana ndi voice iyi machende ake ndichakwera manyi ake
Chilungamo ndi mwano amene ikumukhuza nkhani imeneyi audio iyi sakupuma nawo bwino akuwona ngati awanyoza koma ayi wayankhula chilungamo Zimveka bs any time chilungamo chizatuluka
@user-wb5ym2qm6y4 күн бұрын
Komaditu a Huwa Mkaka adalankhula kuti ndale za kuMalawi timapanga ndi usiku.
@babranzima81209 күн бұрын
Idalidi nyambo pama plan athuwadi😢😢
@Pangolinimw9 күн бұрын
😢😢😢😭😭😭 mcp ndi yakumpa
@nephitalychitedze21188 күн бұрын
Kusokosera pano sikuthandiza china chilichonse nkhani ndiyakuti. Ngati muli ndi umboni pitani ku Court. Sizomangosokosera zotibweretsera misozi ayi... RIP my Veep SKC
@OFG-th3st8 күн бұрын
Chippewa chija Ndichoopsa😢
@Hong_sing8 күн бұрын
Excellent 😭😭😭😭😭
@kubengovender69969 күн бұрын
We are together big man!!
@MillieMalakam6 күн бұрын
Cakwela ndiwosalakwa anavomeleza kt cilima zayimila koma nduna xakezi ndizimene zikumuzocelesa kt azipanga zoipa koma mcp must go akazizi achabecabe afiti osekelera
@KelvinPhiri7508 күн бұрын
zosakhala bwino...i do know when we will change a s a country 😭
@CharlesBanda-kv8bh8 күн бұрын
Ndiwe chitsiru amene ukutukwanawe udikire uwone cho me mulungu amanita ndizitsiru ngati iwe
@KelvinJpchimphepo-sh6nc2 күн бұрын
Umbuli wakudanawo osaziwa chimene akuchita
@SaidiMdoka-pn3zm9 күн бұрын
Mfiti yayikulu ndi Chakwela m'busa wonyenga
@FortuneAndrew-nb2im8 күн бұрын
Respected may his soul rest in peace
@reymondpetermaster56973 күн бұрын
Skc rest in peace, only God knows about your early departure.
@chitanibenito11096 күн бұрын
Mawu onse amayankhura a mcp aphelezera anthuwa ngakupha basi ngakhale zi siru za anthu ena zikubakira as if they don’t see wat is happening n it’s just only few people amene akumusokoneza president.
Vuto lanu a Malawi 🇲🇼 Kusankha kwanu kuti mumulande Boma Peter Mthalika.....wakwiya mzimu wa Bingu,Munya muzingophana shupiti....
@andrewmaluwa27138 күн бұрын
aaa uja adationjeza kwambili APM, nkhaza zomwe ma cadet amachita zija muona ngati tayiwala? aliyense adzafatu including APM yo, osamalakhula motumbwa, dzikoli si la amuthalika, chakwela naye 2025 akadzaluza ndekuti amalawi samufuna osati adzidzati andilanda boma
@PRECIOUSMKUTE8 күн бұрын
Lero akutifuna okhatu. Ankatinyoza
@sokojane40158 күн бұрын
Zinthu zimayenda bwino only with Bingu. Munthu uja aaaa anathesa njala ndipo zinthu zambiri zimaoneka ndi maso. Bingu wa Mthalika miss him always@@PRECIOUSMKUTE