GWEDEGWEDE LERO NDE KUNALI KUGUDULA NDIWO ZAGULU | ZITHUNZI ZA ANDUNA KUNO |

  Рет қаралды 22,557

DZIWE TV

DZIWE TV

22 күн бұрын

Пікірлер: 35
@kadijachilwan967
@kadijachilwan967 20 күн бұрын
Apolice amaonjeza nkhanza pansewu😢
@AlexKaunda-ny2eg
@AlexKaunda-ny2eg 20 күн бұрын
Zikhale ng'oma ma bombasa wagulakoso 😂😂😂 wausilu iwe
@giftmasenti5732
@giftmasenti5732 20 күн бұрын
A Traffic police ambiri za miyoyo ya anthu alibe nazo ntchito nde ndizimenezo
@B1Chitatata
@B1Chitatata 20 күн бұрын
Salute
@wilisonbornface4282
@wilisonbornface4282 20 күн бұрын
Live from south Africa cape town
@SolomonNjolomole
@SolomonNjolomole 20 күн бұрын
Munadza makosana ❤❤
@mathewsmdzanja3276
@mathewsmdzanja3276 20 күн бұрын
I salute mibawa
@gracemkandawire8769
@gracemkandawire8769 20 күн бұрын
Powerful GwedeGwede,,bambo banda
@AnaffSayamika-uh6vg
@AnaffSayamika-uh6vg 20 күн бұрын
Mumakwana guys 💥
@CatherineDesire
@CatherineDesire 20 күн бұрын
Chipewa cha khwangwala kuteloko amafuna anyemere kaye kuti adutse ndi mwana wodwala ,utsilu dyera
@StevieChikaonda
@StevieChikaonda 20 күн бұрын
Muli ndi mtopola guyz😊
@SurprisedDrumKit-ql7rj
@SurprisedDrumKit-ql7rj 20 күн бұрын
Za police mbuzi zaanthu izi kma kuba ndikupempha
@ishmaelchirwa9303
@ishmaelchirwa9303 19 күн бұрын
Anduna akutsotsola ulusi pano akuti kuionesa 😂
@MerryWayson
@MerryWayson 20 күн бұрын
Sitidya ndale kkkk ndimakunyadilani kwambiri Mibawa TV
@Homeofpeace321
@Homeofpeace321 20 күн бұрын
Nkaka akulembaso MSCE
@AlexKaunda-ny2eg
@AlexKaunda-ny2eg 20 күн бұрын
😢😢😢😢 apolice apamalawi vuto ndi umphawi anthuni
@user-gw2zb8pf7n
@user-gw2zb8pf7n 20 күн бұрын
Mwanayo anali ndi 1 month and 3 weeks mgalimoto ndinali MO ine😢
@NaduMbewe-zz6iw
@NaduMbewe-zz6iw 20 күн бұрын
Kkkkkk
@user-xx4jb9se3z
@user-xx4jb9se3z 19 күн бұрын
Zoonadi apolice amaonjeza
@AlexKaunda-ny2eg
@AlexKaunda-ny2eg 20 күн бұрын
Chakwera mumuudzeso kuti opha nzake afeso chifukwa chakwera anapha chilima my boss he call chakwera bull dog😂😂
@wilisonbornface4282
@wilisonbornface4282 20 күн бұрын
Steve ndi Selina mativesa kukoma
@MosesShaibu-ee8hn
@MosesShaibu-ee8hn 20 күн бұрын
Madokotalanso ali ndivutolawo munthu akumuwona ali pamzele komakungobwelawinawake wawudindo amakudusila chifukwachani winayusi munthu kodi?
@InnocentnMbale-zq8pk
@InnocentnMbale-zq8pk 20 күн бұрын
Kkkk chipanda kuyankhula bwezi ali mumaguza omwewo kkkk
@HarryMasamba
@HarryMasamba 20 күн бұрын
Kkkkkkkkkkkkkkkkkkk Komatsu dzina izi
@user-eh1mg3ww6d
@user-eh1mg3ww6d 20 күн бұрын
Ndipo apolice akumalawi ndinu otembelekdwa ndipo mukulephela kugwila mbava koma kulimbana ndi athu osalakwa
@LucianoKapepuza-sy9wx
@LucianoKapepuza-sy9wx 20 күн бұрын
Nawo a MCP asatile malamulo a gwirizano wawo kuti apite s Utm asogoleke nawo
@user-lc3sw8iz2g
@user-lc3sw8iz2g 20 күн бұрын
Ku malawi zimathera tikufufuza.
@dumisanimoyo3152
@dumisanimoyo3152 20 күн бұрын
Tisakubisileni apolice alowa chiwewe kusaka ndalama
@user-jn7bt1uy5s
@user-jn7bt1uy5s 20 күн бұрын
Mbambande mibawa
@user-bc2mu2ns5n
@user-bc2mu2ns5n 20 күн бұрын
Futso nkhumati kodi sopano kubako mwathana Nako?
@OfwaMwambila
@OfwaMwambila 20 күн бұрын
If u stopped by the police officers on the road in ur 🚗 .who is supposed to follow the other? 4me i don't go out to a police office who stopped me coz i had no intention of stopping.u stop me,u come to me &tell me why you stopped me not me coming to ask u
@CatherineDesire
@CatherineDesire 20 күн бұрын
Va police palibe vomwe vikuchita vimangodziwa kupempha ndrama pamseu ndikumanga mbava yoti anthu aigwira kare anthu eniake,ndipo vitengelepo phunziro mwina vingayambe kugwira ntchito bwino vipewa va mbalevo
@AlasonPaulo-ht7zb
@AlasonPaulo-ht7zb 20 күн бұрын
Zoonadi Inu muli bwino kwambili
@gwatandingo9502
@gwatandingo9502 20 күн бұрын
Wanga kufa mwana chifukwa cha wa police wandigwira nayeso adzafera pompo ineyoso natopa nawo mbuzi zimenezo pofunika osamawanyengelera😢😢
@WysonYohan
@WysonYohan 20 күн бұрын
Malawi tingogulisa tigawane ndlama bc
Mama vs Son vs Daddy 😭🤣
00:13
DADDYSON SHOW
Рет қаралды 45 МЛН
Pleased the disabled person! #shorts
00:43
Dimon Markov
Рет қаралды 28 МЛН
Zifukwa Zomwe Zingapangitse MCP Kuchoka M'Boma - Concerned Citizen
11:18
Released After Sadc Summit
10:55
Global Spot On TV📺 (We Spot Globally)
Рет қаралды 478
ZA CHIPANI CHA KONDWANI NANKHUMWA  KUNO PDP ZIVERENI NOKHA |
20:30
EXCLUSIVE INTERVIEW WITH BON KALINDO
59:52
Zodiak Malawi
Рет қаралды 53 М.
EXCLUSIVE INTERVIEW WITH MICHAEL USI (MANGANYA) Part 2
58:38
BON KALINDO LERO PA  31 JULY 2024 |
17:12
DZIWE TV
Рет қаралды 39 М.
Gwedegwede
34:25
Mibawa Studios
Рет қаралды 8 М.