Hot Current Nduna Yoona Zachitetezo Cha Mdziko Wamukalipira Brian Banda

  Рет қаралды 147,733

MJ-MODAH MALAWI TV

MJ-MODAH MALAWI TV

Жыл бұрын

Пікірлер: 412
@fedson2050
@fedson2050 11 ай бұрын
This Hot Current palibe chimene tatola ngat ife ma Listeners ndim'mene akuyakhira wakubayo
@bi8942
@bi8942 Жыл бұрын
A Brian tamubooleni mimbayo zikhale ng'oma mwina mimbayo iphwe kenako aziyankha . Ndichinduna cha mwano komanso Makati kwambiri. Changoseza mimba uko phwiiii kumapanga makani apa ngati ndi munthu ozindikira power ndi mbuzi ya munthu. Musazachiitanenso pa hot current kawiri , chizikhala ndi chakwera wakeyo kudikira kuchoka 2025. AIP ikuyenda bwino pakhomo pakwawo osati kwa amalawi anthu okuba Mulungu awalanga pompano anthu amenewa
@eliffagondewe8214
@eliffagondewe8214 Жыл бұрын
Kkkkkkk
@gavinpillay1253
@gavinpillay1253 7 ай бұрын
Galu wammpha dzikodi silingalongosoke ili nduna yaza chitetezo ikuyikiraso kumbuyo mbwererazi
@Extratremendouszeus
@Extratremendouszeus 14 күн бұрын
Chilbe nzeru chunkhumba chimenechi He uses his udindo wrongly
@zechariah265
@zechariah265 11 ай бұрын
This shows how hot current bases on issues with no tract evidence. Please Brian learn to be prepared for the program
@moseskavalo3304
@moseskavalo3304 Жыл бұрын
The nduna himself doesn't know how to argue,,too much emotions ķkkkkkkkkkk hahaha MCP is dangerous party indeed
@salimmkumakumakitombi-yc7pw
@salimmkumakumakitombi-yc7pw Жыл бұрын
Kodi mlendo anali ndani pa Hot current imeneyi.... nduna yoonjedxera nkwiyo kwa A malawi
@user-eh1gn1nj9d
@user-eh1gn1nj9d 3 ай бұрын
2025 ndi Chaka chamawa Why panic with this thing Let's go and work for our better
@MotivatedI
@MotivatedI Жыл бұрын
This is exactly how government lives in denial. Very interesting. All this time there is nothing you can point that the minister was able to answer. Like nothing
@Littlefair7
@Littlefair7 Жыл бұрын
He forgot we're in a democracy with his dictatorship mentality.
@rasulrayman4517
@rasulrayman4517 Жыл бұрын
Increasing the AIP beneficiaries will mean increase in poverty on household. This initiative is pathetic n we can't do better. Smallholder farmers are failing to extend their farm sizes due to high level of dependence on AIP same way as we depend much on foreign Aid. Teach more farmers on how they can manufacture mbeya fertilizer and do some extensions to their farms..
@thondoyaenterprise3795
@thondoyaenterprise3795 11 ай бұрын
Big up minister for taking these kids to school.
@Mbesa09
@Mbesa09 Жыл бұрын
I love The Hot Current and I always look forward to it. However, for so long, I have had issues with the show to where the hosts don't usually "think" of how important this show is to the students in colleges and universities world over. It is very difficult for a student to use what is said on this program as real evidence because the hosts take it as a discussion would have with someone at a bar. The hosts are barely ready for it and do not cite their outside sources, something that, maybe, morden universities do not accept. Much as I was not in agreement with The Minister, he seemed to challenge the hosts to produce evidence of what they wanted to ask him. I know the hosts, more specifically, Brian Banda, is educated enough, he should take this as a learning process and always cite his sources when asking the people 'he' invites to the show. This program has been a wonderful addition to Malawian programs but if it was done the right way, it could do much better than it has already done. Let members of parliament use it as a source of evidence in parliament. Let people sue one another using this program to change the face of Malawi. That cannot happen if the discussion is only done as a casual discussion. I was impressed seeing the minister showing his notes on things because he is an educated fellow who knows not to say something on a national television without evidence. Fox News in America paid big money for spreading false news without proper evidence. Please, Times Television, let your producers cite their stories or use the word "hypothetical" so some of us can really know if it's worth it or not.
@user-ux8bc6wy1i
@user-ux8bc6wy1i Жыл бұрын
😂
@tadalarhostinchiphwanya7891
@tadalarhostinchiphwanya7891 Жыл бұрын
Hundred percent I agree with u. I think it's high time Times find some guys well-informed on today's current affairs and issues to do so socials economics and governance.
@ezekielchihana2927
@ezekielchihana2927 11 ай бұрын
@@tadalarhostinchiphwanya7891true
@BenissoneErnesto-kn9bd
@BenissoneErnesto-kn9bd Жыл бұрын
Nduna imeneyi ndichisiru chamuthu ndposo ndisatana ndikufunisisa kt mulungu amulange panse pompa aziwe chimo lake akuphesa A2 osalakwa Aku ruwanda ndimuthu oipa kwambir ameneyi osamusekerera chisiru chamuthu ndiwadyera kwambir
@christopherbokosi514
@christopherbokosi514 7 ай бұрын
Nduna imeneyi ndimanyi
@kamuchirwa8940
@kamuchirwa8940 Жыл бұрын
The worst hot current, zikhale is too much into politics.
@geee7672
@geee7672 Жыл бұрын
...I really wonder why the anchor seems to be touting this guy a if he has some extra-ordinary skills and talent. What does nyama zikulu-zikulu mean? Lets not get excited and worship the same people who are promoting poverty amongst us. And I think we are micro-managed by Rwanda and collecting kickbacks by hunting refugees that he still seeks to kill. Well, I look at it as the most stupid thing for us to be proud of having more AIP beneficiaries. Instead of graduating these subsistent costly farmers into viable and productive citizens….on the US ambassador, I have never seen an ambassador who enjoys strange diplomatic protocol. He even finds himself in locations eating mandasi with locals, now, if he enjoys that freedom, then it is not a problem if he decides to walk into a media house as a news source. After all, the Malawi economy is surviving on debts, loans and credits that he approves every week, perhaps every day…The problem in Malawi is lack of ambitious leadership. We, currently do not have anyone fit for the position he holds in this government apart from the female ministers.
@KinziwindassoniKinzi
@KinziwindassoniKinzi 4 күн бұрын
Nzeru ilibe ndunayo ubwino wake 2025 mbava zikuchoka
@user-qs2tx7wt6g
@user-qs2tx7wt6g 5 күн бұрын
Mwakumana ndi nyama zikuluzikulu ndichochenjelaaa ichiii
@user-uz6tr2db6g
@user-uz6tr2db6g 8 күн бұрын
Nzeru ilibe ndunayi
@stanleymatolabanda5460
@stanleymatolabanda5460 Жыл бұрын
Useless cabinet minister who could not explain 🚮
@g_deonm5793
@g_deonm5793 11 ай бұрын
I like this . The minister is a very interesting political figure., He was able to spin out of questions and provide alternative view and he slipped out of Brian's popular "monkey wrench" questions.
@moseskavalo3304
@moseskavalo3304 Жыл бұрын
Now tell the minister about Quantitative and qualitative data, qualitative part of AIP is negative osamatinamiza apa
@languitoneelias9972
@languitoneelias9972 Жыл бұрын
Wakumana nawo anzako akhambi iwe Brian umaziona ngati ozindikila ukamafunsa mafunso amzako apa taziyankha osati zibwibwi its true pamafunika kumakamba zinthu uli ndi umboni osati kumangopeka nkhani or ena akangoyim a foni basi mwakhulupilira One day adzakutenga sukudziwa Kuti akukuuza zimenezoyo ndiwamalamulo becareful Brian de
@patricklimiton1023
@patricklimiton1023 11 ай бұрын
Inuyo kuzitenga kuzindikila ??
@leonardjika2100
@leonardjika2100 Жыл бұрын
A NEW VERSION WISE GOOD THINKER WILL GOVERN OUR LAND SO HELP ME GOD
@PeterThawi-jc7zl
@PeterThawi-jc7zl Жыл бұрын
This zikhale ng' oma has shown he is an intellectual....he can cite his sources...Brian Banda didn't come prepared...this time.i hope u do better next time around.this minister has killed the interview.
@lumbizayigadama-wd9ox
@lumbizayigadama-wd9ox 11 ай бұрын
No ndiwopoira
@louisbonongwe8537
@louisbonongwe8537 11 ай бұрын
Aaaaaa awanso
@lewisbonongwe8518
@lewisbonongwe8518 Жыл бұрын
Azikhale muziopa kumwamba uliposo moyo wina oposa umene mukubela anthuwu kudziko kuno, Musamale
@rashidsaid2232
@rashidsaid2232 3 ай бұрын
Mr Zikhale Ng'oma udindo wakulilila sakudziwa chimene akunena
@user-hy4ty2ig1t
@user-hy4ty2ig1t 11 ай бұрын
I do understand a minister wants everything wth a prove coz amalawi timangoyankhula zongomva,,,is really nyama zikuluzikulu wth more intelligent I enjoy this kkk
@TrizaMaluwa-by9jw
@TrizaMaluwa-by9jw 3 күн бұрын
Andunawo nzeru alibe sakutha kuyankha funso
@vukanifracksonchinkonde7324
@vukanifracksonchinkonde7324 11 ай бұрын
The minister is intelligent,has really handled the hosts,he is really based on facts from my observation.A china Brian and pamkuku accept a defeat,the guy has really outweighed you.
@lloydchinyenye7704
@lloydchinyenye7704 11 ай бұрын
Exactly
@AustinChingoma-el4wo
@AustinChingoma-el4wo 11 ай бұрын
Exactly the host defeated
@moseskavalo3304
@moseskavalo3304 Жыл бұрын
We are sad Nation
@keithmlenga4657
@keithmlenga4657 11 ай бұрын
You, not we😅, I am not
@PeterThawi-jc7zl
@PeterThawi-jc7zl Жыл бұрын
Guys let's gather here for comments😂🤣🤣🤣
@dellingsmunthali2669
@dellingsmunthali2669 11 ай бұрын
Nyama zikulu-zimulu dada zikhare munthu murara chomeneeee ntchindii zikumwenererani chomene pa yankho rakut president azakhara chakwera motoooo💥💥💥💥💥💥
@augustinechibbalazi8897
@augustinechibbalazi8897 7 күн бұрын
Zinkhali Ng"oma is skilful at his work.Hon.Minister please,keep watch on illegal influx of immigrants here Malawi.
@SautsoBandah-lf4so
@SautsoBandah-lf4so Жыл бұрын
Guys u r losing control of your interview
@giftmakoyo1441
@giftmakoyo1441 2 күн бұрын
Mpaka ali ndi nyolo ndani aaaaa ife tiwope unyolo za ziiiiiiiiii
@BenissoneErnesto-kn9bd
@BenissoneErnesto-kn9bd Жыл бұрын
Watching from mozambique
@innocentissah2636
@innocentissah2636 Жыл бұрын
Nduna yoononga dziko kwambiri, katangale ali thoooo
@jacquesnsabiyaremye3166
@jacquesnsabiyaremye3166 Жыл бұрын
Akuti zinthu zitsika😢! Koma Chimunthu chi ndi cha Pokoso bwanji!!
@user-kr8bn1bb8c
@user-kr8bn1bb8c 6 күн бұрын
Nduna iyi ikhadzangolowatsa mboma it means dera lakero ladzaza zitsiru zokha zokha
@mercythom5868
@mercythom5868 7 ай бұрын
Poyamba ndimaona ngat Times imadana ndi DPP koma now ,,,,,ndazindikira kut it's only times yomwe tingaipange trust❤❤❤❤❤
@chrispinechirwa2655
@chrispinechirwa2655 3 күн бұрын
Uyu si nduna koma chigawenga😢😢😢 wofunsa mesa ndi mtola nkhani?
@joaquegerman2250
@joaquegerman2250 Жыл бұрын
Wadya 2.5 biliyoni ameneyo
@fedson2050
@fedson2050 11 ай бұрын
Ameneyo mumamuitaniranji wamakani ngat ameyo
@user-qs2tx7wt6g
@user-qs2tx7wt6g 5 күн бұрын
Koma akunena zoonaaa
@wakisawinga2744
@wakisawinga2744 7 күн бұрын
Now I know what he meant by being the strategist 😢😢😢😢
@Sabina-hw4js
@Sabina-hw4js 9 күн бұрын
People are sleeping for days without food yet them are having big stomachs
@dalisoulphiri3094
@dalisoulphiri3094 Жыл бұрын
Za trend zo munthu wakumudzi azidziwa bwanji abale?
@leonardmussah7902
@leonardmussah7902 Жыл бұрын
This has been one of the poorest interview so far, the minister has failed to take all the questions & frankly speaking he has acted as a football commentator
@user-hb1ff2wd8c
@user-hb1ff2wd8c 6 күн бұрын
Zikhale ndi mbuzi kma adzinga azake bas akukanika kuyakha mafutso ake amakani bas born kalindo must release 😮
@jeuzywandasigner4908
@jeuzywandasigner4908 7 күн бұрын
This is why you can't choose your family partner kukhala okuthandizila cz pakakhala vuto saangayankhule olo kusamala zaena apadela kuposa m'bale wake olo m'bale akulakwisa Malawi ali pa moto i hope wi know what to do next year to save our lovely country mayi Malawi 🇲🇼🙏🏾
@charlespaulbanda8136
@charlespaulbanda8136 11 ай бұрын
I like how nduna imeneyi pays attention when someone is on the flow
@ancientnkhata1137
@ancientnkhata1137 3 ай бұрын
He pays attention to details Eish
@madalitsoonale5338
@madalitsoonale5338 11 ай бұрын
My Malawi 😭😭😭😭 y having useless minister like this one, useless government too😭😭😭😭😭
@mbumbajilowele6511
@mbumbajilowele6511 Ай бұрын
Akuluwa angonenepa ndi achisilu kobasi😊
@chawackchinthenga6696
@chawackchinthenga6696 Жыл бұрын
Just remind you Chilima will never stand for 2025 presidential candidate 😢
@aronluka8086
@aronluka8086 Жыл бұрын
Duna imeneyi kodi imakhalira kuti zoti anthu adalandidwa ma 30 pn iyeyo sakuzidziwa koma ameneyi
@nickmumba2131
@nickmumba2131 Жыл бұрын
Kkkkkkkkk Nduna he doesn't know what's talking about
@user-nz1tf2ie6n
@user-nz1tf2ie6n 6 ай бұрын
Wotching from South Africa
@ephraimkadamika
@ephraimkadamika Жыл бұрын
Minster uyu ngozikonda
@DavieJames
@DavieJames Жыл бұрын
Let the minister answer questions not asking questions
@thomasbodo4099
@thomasbodo4099 11 ай бұрын
The Minister is not serious on what he is saying he cant say all is well with Malawians just becoz his familly and relatives are well
@user-eb2gi5dt6o
@user-eb2gi5dt6o 2 ай бұрын
Koma ndunazi zikamana manyazi zilibe eish
@chikoko-uj2tt
@chikoko-uj2tt Жыл бұрын
Tell him mr Nanyon is a human being also
@user-pt8wb4vw6r
@user-pt8wb4vw6r Жыл бұрын
Azikhale akukwana pa udfend
@precioussauli2887
@precioussauli2887 Жыл бұрын
Honorable Minister is not able to take questions as asked. It is normal for AIP beneficiaries to increase as the population of the country is also growing extremely. And regardless of the increase of the beneficiaries, only a few out of the ones that were supposed to benefit this year benefited.
@James-uq6hv
@James-uq6hv 11 ай бұрын
Kkkkk kids are taken into a class, the kids have their sponsor, bravo to the minister Zikhale for the response trying to educate a bulutiwa
@wezzieneba9238
@wezzieneba9238 2 ай бұрын
As for Brian and your colleague, I think you lost direction on the main theme of the program. Next time try to stick to what has been prepared, not flowing by the emotions of the visitor. You were taken up ending in no concrete and tangible issue at the end. Wishing you all the best. All in all, YOU ROCK GUYS!!!
@livemonkaposka3714
@livemonkaposka3714 Жыл бұрын
Ali busy kuba ndalama zobwerekazo
@alfredmankhwali-ku3ef
@alfredmankhwali-ku3ef 4 күн бұрын
Nkhani si nambalayo ayi , koma kodi ikumafikira onseo .
@francistonysanena5349
@francistonysanena5349 7 ай бұрын
Mr Based on facts😊...
@MphatsoSimiliwadi
@MphatsoSimiliwadi Күн бұрын
Very wise minister
@farmupmalawi
@farmupmalawi Жыл бұрын
Chisilu chimenecho chikundisekesa heavy
@MathewsLiwonde
@MathewsLiwonde 7 күн бұрын
Alibe nzerhu nduna yoipa iyi amapemphera mpingo wanji zonse chauta akuwona mulibe nthawi musamuka.
@loveborn1085
@loveborn1085 2 ай бұрын
Two term ya president iri mu constitution ya Malawi Koma ngati president sanachite bwino ndipo anthu sakufuna kuti aimenso kachiwiri, anthu amasapota presidential candidate amene akumufuna nkuwina. Sindiye kuti president amene sanamalize 10 years yakeyo ndiye kuti apita ku khotitu ai.
@user-xz6uf8uk8t
@user-xz6uf8uk8t 4 ай бұрын
Koma ngati a Brayan Banda ngati atolankhani amaimila athu chifukwa chifukwa chiyani amaka mba mokhalira mbali imodzi
@omarajibu860
@omarajibu860 Жыл бұрын
Economy ikhala bwino bwanji utanena kuti zinthu zilibwino?
@kestinmacheso-zc7cz
@kestinmacheso-zc7cz Жыл бұрын
Akugwilisa ntchito mphavu sakuyankha mafuso bwanji mbudz yanduna iyo
@vusoacquaron9084
@vusoacquaron9084 Жыл бұрын
2.5 billion dollars ya Kagame
@Sabina-hw4js
@Sabina-hw4js 9 күн бұрын
Whether kukwera or not people are suffering.
@MphatsoMgaiwa-sr7vn
@MphatsoMgaiwa-sr7vn 11 ай бұрын
Abrian mumacheza ndi chitsilu kwambili
@joshbosh6157
@joshbosh6157 10 ай бұрын
Brian, mkulu uyu ndiwachabechabe. Mayankhidwe ake ndi achabechabe, ndipo ndangotaya nthawi yanga pa program imeneyi
@awesomechannel7752
@awesomechannel7752 10 күн бұрын
This guy need an evidenve from you guys but was he producing the the documentantion ya constitution yo?
@raytavares2256
@raytavares2256 11 ай бұрын
Today Brine wanyachuka and exposed pa mtunda chibwibwi when did Brian start stammering? I realised how deflated he was. He was hiding what Brian has been doing and after seeing that he is being exposed he was like a flat tyre.
@MsosakaisiAdamson-pg6uv
@MsosakaisiAdamson-pg6uv 11 ай бұрын
Iyi ndi mbuzi yamunthu ,, brian muzititengera anthu azeru iwowo anadya ma 30pin afeteredxa mpaka pano sitikupindula nd boma limenero
@user-xd9fp2bw8j
@user-xd9fp2bw8j Жыл бұрын
mukungovutikatu a brian ndigaluyi dzikoli akuona ngati ndilamayi awo tikakumana komweko
@preciouskasusu1271
@preciouskasusu1271 Жыл бұрын
Kuyakhula kwa anduna kosapatsa chiyembekezo aaaa
@phillipstamaley7901
@phillipstamaley7901 10 ай бұрын
Brain wawoneka m'sana after kubisala m'mbatata
@user-wd7lk7nx7m
@user-wd7lk7nx7m 10 ай бұрын
Ku Malawi kulibe nduna yopanda zeru Ngati imeneyo galu weniweni
@dinganinedsontchongwe610
@dinganinedsontchongwe610 5 ай бұрын
The minister is using his position to defend himself but he is not true from what he is saying.
@user-jr9oh3ye9u
@user-jr9oh3ye9u 11 ай бұрын
Mximm zautsiru anduna anuwo akuyankhula zichani😊
@user-th4dg9bn9i
@user-th4dg9bn9i 11 ай бұрын
Thanks zikhale
@user-ix7pb6hk2w
@user-ix7pb6hk2w 5 ай бұрын
Nduna ya manya mavote mwana kale ndi a make koma sizitheka ife tikuziwa mulimonse
@FelixChimsNyirenda
@FelixChimsNyirenda 10 күн бұрын
Malawian politics is a dirty game and Malawian politicians ndiankhuluku kwambiri
@GiftMakowa-k9f
@GiftMakowa-k9f 23 сағат бұрын
Uyu panyapa xikhale Ng,oma kaye kutopa mawonekedwe
@TimbaTv001
@TimbaTv001 8 күн бұрын
Thise brains are just old brain yomwe ilibe vision pa Malawi akudzatsaka pension ya executive. Aaa basi tikufunilani kufa konvetsa chison
@JamesChimera-hw1nv
@JamesChimera-hw1nv 2 ай бұрын
Atola nkhani ahot current amakhala ndi mbali koma Chilungamo chimafunika osati kusokoneza anthu
@user-cn2mg2ee2p
@user-cn2mg2ee2p 8 ай бұрын
Mpakana 18 minutes musanayambe kumufunsa mafunso uyu ndigalu kwambili nduna yopusa kwambiri
@daviegunde5287
@daviegunde5287 Жыл бұрын
A nduna sakukwanira kukhala kuyimira boma pa program yi coz akukana kuyankha mafunso. Next time ndi bwino kukana kukhala pa program
@dellingsmunthali2669
@dellingsmunthali2669 11 ай бұрын
Mmm ayizikomo MOTi nthawi yomwe anthu akudandaura kut president akuyenda kwambiri osaziwa kut ondevu zamwai anali mugulu😃😃
@FranciscoMandawala
@FranciscoMandawala 16 сағат бұрын
brian tawasiyan awa ndiopepela saziwa kut munthu amayankha with explanation.
@bugadada5752
@bugadada5752 4 күн бұрын
Zikhale Ngoma zinazo ayi 😂😂😂😌
@user-lr7ix1tm5b
@user-lr7ix1tm5b 7 ай бұрын
Anduna atuluka mimba itaphya ndimafunso eish Brian ndiwe wamwano😢
@WinerdJombo
@WinerdJombo 9 ай бұрын
Uyu akuti ife sitikuvutika aaaaa😢 pokhapo wandikwiyitsa kwabasi ndipo mapwa.... ake ndithu
@christopherbokosi514
@christopherbokosi514 7 ай бұрын
😂😂😂😂😂😂😂😂
@abubakrmustafa6105
@abubakrmustafa6105 Жыл бұрын
Zisikarit mwarephera bwana😜😜😜😜
@molicieeosama8877
@molicieeosama8877 Жыл бұрын
Duna yachibwana kwambili
@princedavidmapiri2876
@princedavidmapiri2876 Жыл бұрын
Nkulu ameneyu ngopusa zeedi musazamuitaneso akuzitenga ngati ngochenjera musiyeni azawona 2025
hot Current..Kumkuyu Vs Namalomba
1:14:23
Malawi Lovers 🇲🇼
Рет қаралды 39 М.
The Plan featuring Sheikh Dinala Chabulika - 26 June 2024
59:55
Times 360 Malawi
Рет қаралды 9 М.
World’s Deadliest Obstacle Course!
28:25
MrBeast
Рет қаралды 144 МЛН
когда повзрослела // EVA mash
00:40
EVA mash
Рет қаралды 2,9 МЛН
Was ist im Eis versteckt? 🧊 Coole Winter-Gadgets von Amazon
00:37
SMOL German
Рет қаралды 11 МЛН
CRUISE 5 WITH PATRICIA KALIATI
59:03
Joab Frank Chakhaza
Рет қаралды 155 М.
Wer war Rudolf Heß? - Hitlers Stellvertreter | SPIEGEL TV
33:46
DER SPIEGEL
Рет қаралды 104 М.
Hat die AfD Sonneberg nach einem Jahr verändert? | Länderspiegel
13:28
ZDFheute Nachrichten
Рет қаралды 159 М.
Times Exclusive featuring Atupele Muluzi - 15 July 2023
1:06:57
Times 360 Malawi
Рет қаралды 53 М.
Die Radikale (4/5) | Podcast Sahra Wagenknecht | MDR
19:15
MDR Mitteldeutscher Rundfunk
Рет қаралды 3,4 М.
Interview ndi Norman Chisale
1:05:22
Malawi Lovers 🇲🇼
Рет қаралды 211 М.
Times Exclusive featuring Thomson Mpinganjira - 3 February 2024
1:07:40
Times 360 Malawi
Рет қаралды 150 М.