HOT CURRENT 14 JULY 2024 |

  Рет қаралды 23,023

DZIWE TV

DZIWE TV

Ай бұрын

Пікірлер: 97
@patrickndojime1632
@patrickndojime1632 Ай бұрын
Go on Guy's we wait to see the changes in Malawi eeeee from Bakili muluzi up to know am in RSA because of politics of Malawi throwing as away not thinking of coming back to home eeeeeeeeesh
@Yungjoe786
@Yungjoe786 Ай бұрын
Chilima was assassinated that's the truth what more do u want to hear?
@user-lj8ug5lq8c
@user-lj8ug5lq8c Ай бұрын
Guys keep it like this ,this is Hot current we know from those days congratulations
@JamesIngeni-ku3qj
@JamesIngeni-ku3qj Ай бұрын
Manganya ndi mcp anapha chilima.
@Martha-m6e
@Martha-m6e Ай бұрын
Usi si wa UTM. Munamuwona muja amarandira udindo muja? UTM yachita bwino kuwaturuka.
@gracemkandawire8769
@gracemkandawire8769 Ай бұрын
Ngozi ija singozi ngozi ,,komanso yonse taona ndimafinso
@BambordKabambe
@BambordKabambe Ай бұрын
😂😂😂😂😂 chaka chino ndi CHONG'ALURA
@JohnNjerenga
@JohnNjerenga Ай бұрын
Kkkkk akut ipondeni fadha
@paulpaseli6310
@paulpaseli6310 Ай бұрын
Apa ndiye mwabwelatu chilungamo chimenecho
@EstherChimombo
@EstherChimombo Ай бұрын
🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥💯💯
@InnocentnMbale-zq8pk
@InnocentnMbale-zq8pk Ай бұрын
Times muziwe kuti chilima agwila bwanji ntchito ndi chakwela mu 4years
@henryphiri6100
@henryphiri6100 Ай бұрын
Masapota a UTM tonse tatuluka ku mgwirizano Chifukwa tinkasapota Chilima.Usi alibe masapota.
@user-oh9bh1cl3b
@user-oh9bh1cl3b Ай бұрын
Well spoken guy's adzimva akawalalawa
@clintonhodda9830
@clintonhodda9830 Ай бұрын
Walephera Chakwera kulamulira kuchedwa 4yrs ndipo akhala akungodandaula DPP mmalo mopanga ziganizo msanga
@OrtonKabbichi
@OrtonKabbichi Ай бұрын
Sizachilendo olo pa ngozi ya ndege ija anachedwanso kukafufuza ayambe kuchotsa ameneo onwe amaenera kukafufuza za ngozi ya ndege
@patricksinyala1345
@patricksinyala1345 Ай бұрын
Mtsukuluzi ukulankhula mopusa, kufooka kwa Ussi kunayamba Chilima alimoyo. Ndipo. Chilimma anali atamuzindikila Kale Ussi ukathyali wake.
@user-un6qv6sj3h
@user-un6qv6sj3h Ай бұрын
Inu ussi siwa UTM 😂😂😂😂ameneuja ngawa MCP
@chitanibenito1109
@chitanibenito1109 Ай бұрын
Chakwera so asamale zomwe wawona Nzake wa kwa merica zija zichitikanso kuno.
@symonmakata938
@symonmakata938 Ай бұрын
Changucho chiyambile pa kafukufuku wa ndege inapha chilima kenako the public ikhala ndi changu
@user-hl3st3cc4v
@user-hl3st3cc4v Ай бұрын
Dziko ndilathu osaonesa kutopa azibambo ipondeni thawi ino palibe kuopa ng,alulani basi ng,ambani
@user-jk8sh7fh2d
@user-jk8sh7fh2d Ай бұрын
Usi atha ngati nankhumwa sure, olo kuthesako akufuna kukhaulisa manganya coz anamuziwa kuti uyu sitili limozi ndi wa mcp.
@JohnmarkNazombe-hi9xd
@JohnmarkNazombe-hi9xd Ай бұрын
Dziko nkumasawukaaaaah!!!!!!!
@henryphiri6100
@henryphiri6100 Ай бұрын
Masapota ake ati omwe atsatire Usi ku MCP. Musanamizane palibe yemwe angavotere MCP true member wa UTM
@EfeloYovita
@EfeloYovita Ай бұрын
ngati bola Allience latha ndibwino kukhala opanda president cs chakwela polowa m boma unali mgwilizano maka utm inali ndimavoti ambiri kuposa mcp we must have emergency presidental election
@INNOCENTMOFOLO-io8tg
@INNOCENTMOFOLO-io8tg Ай бұрын
MCP yayambitsa nkhondo yoopsa yokha amalawi sangasangalale nazo izi Zotsatila results zangozi kuli ziiiii mpaka pano what do you do
@GraceZumazuma
@GraceZumazuma Ай бұрын
Keep it up Guy's ife ndalama tidya koma sitidzawavotela talira kokwana sife opusaso pano
@MPHATSOKALUWA-lm2uy
@MPHATSOKALUWA-lm2uy Ай бұрын
Akuchedwa Nd pule yomweyo😂😂😂😂😂
@imaculadaAndre-ns1py
@imaculadaAndre-ns1py Ай бұрын
Fiti ndifiti basi awa sangaulule chilingamo kwao ndikunama basi koma ife chilingamo tinachipeza kale
@zimmekapachika6784
@zimmekapachika6784 Ай бұрын
Akuti mbwexe😅😅😅😅😅😂😂😂
@catherineKalinga-m4c
@catherineKalinga-m4c Ай бұрын
🤩
@AishaChipande
@AishaChipande Ай бұрын
Chakwela azuzula bwanji pomwe iyeyo anaphaso muzake
@EsnartMbalale
@EsnartMbalale Ай бұрын
Ipitilile ndiyabwino coz ikulakhula mosatenga bali
@imaculadaAndre-ns1py
@imaculadaAndre-ns1py Ай бұрын
Tamusiyani maganya abakhala komweko adzatiuza zenizeni abawatola zifukwa adzapange sewelo mutu wake chakwera anapha zake chifukwa chaudindo
@OfwaMwambila
@OfwaMwambila Ай бұрын
Alot of people re in marriages that ended a long time ago but due to kids u re forced to still living together that's what I think was the case of SKC&usi.
@StiveKantiki
@StiveKantiki Ай бұрын
Akuyambisa kuchedwa ndi achakwela ndipo ife tinalakwisa kumuika munthu onamizila ubusa Ngati uyu pa mpando
@chitanibenito1109
@chitanibenito1109 Ай бұрын
Mbwelera zokha zokha za mcp kkkkkkk koma pankuku!!!!!!
@BestonStima
@BestonStima Ай бұрын
Mcp ivutika chifukwa isanalowe m'boma amalawi ankaopa nkhanza za mbiri yawo Lero in their 4yrs rule patuluka nkhanza. Do you think they can reign???????????
@robertnambazo9936
@robertnambazo9936 Ай бұрын
President osaziwachomwe akuchita he is so relaxing President President uyu ndi bubu shatapu zake
@SteveKanongwa
@SteveKanongwa Ай бұрын
Koma ma guys inuo hahaha munatopa nalo dzikoli simufunaso zachikape
@KennedyPhiri-h9h
@KennedyPhiri-h9h Ай бұрын
Manganya ndi wa mcp not utm
@johnmhango9405
@johnmhango9405 Ай бұрын
Briefcase parties end just like that.
@chitanibenito1109
@chitanibenito1109 Ай бұрын
Uyakhura za chidodoyo ndiye ili mbudzi yoyambisa chakwera samasata zinthu that’s y anyamata ake angomisewera basi.
@SteveChapola
@SteveChapola Ай бұрын
A mcp chipani chokupha
@gracemkandawire8769
@gracemkandawire8769 Ай бұрын
Sitizalola report. Wonder you are very Intelligent than pankukuyo
@GodfryMalishe
@GodfryMalishe Ай бұрын
Salute u guys 😂
@MPHATSOKALUWA-lm2uy
@MPHATSOKALUWA-lm2uy Ай бұрын
How many meetings manganya has been attending?? Can he allow to apart from the alliance coz it's obvious manganya it's won't allow
@peterchikwakwa8476
@peterchikwakwa8476 Ай бұрын
Eeeeeee yankhulani guys ❤
@lukedumbula2724
@lukedumbula2724 Ай бұрын
Very true wonder and jona, a PULE akuchedwaa
@user-pv9uk6sc3w
@user-pv9uk6sc3w Ай бұрын
Pa nkhani yochedwetsa chitukuko, tingomuchotsa next year basi, sali fit Chakwera to be a President.
@gracemkandawire8769
@gracemkandawire8769 Ай бұрын
A Usi si president wanthu,,munthu mkazi wake tamuziwa polumbilitsa mkumazitama kuti ine sindinayendepo ndi mkazi wanga,,muthuyu angayendese chipani
@RafiqueChibwana
@RafiqueChibwana Ай бұрын
You guys u don't share kamba here really keep it up guys kkkkkkkkk
@JaphetSakala-pq4fl
@JaphetSakala-pq4fl Ай бұрын
Kuchokela pa ifa ya VP chilima kufikila pasiku la mavoti UTM ILI PA TOP ONE. or Dpp ndi mcp ita phatikizana. UTM IKUTENGA BOMA TIZAIPEPESA NDI VOTE.
@SheenahMwalabu-iz3pr
@SheenahMwalabu-iz3pr Ай бұрын
Lero munabweratu a jonah kkk wonder akuti back to sender eee Chakwera dzimvere mumtolo
@JuuuKomba
@JuuuKomba Ай бұрын
Eni ake a UTM ndifeyo ovotafe Tatupu ndife awowo dyela Paolo asaleko tilibe nawo film
@PartsonKamkuzi
@PartsonKamkuzi Ай бұрын
Osawopa ayi a malawi ambiri tikuyang'anira inu kut muziyakhura mosawopa apa
@CosimassShyman
@CosimassShyman Ай бұрын
Wakulu andevu zamwayi amayankhura Chichewa cha boo
@YamikanChirwa
@YamikanChirwa Ай бұрын
Ng'alula iwe
@INNOCENTMOFOLO-io8tg
@INNOCENTMOFOLO-io8tg Ай бұрын
😂😂😂😂😂 anyamata inu mwandisangalatsatu chikufunika ndichimenechi osanyangerera kulankhula chilungamo kubandaluka basi sizoopaso ayi
@user-mj2te7vl6p
@user-mj2te7vl6p Ай бұрын
Kaya DPP kaya ilibe ndalama iwinabe 2025
@user-rd9pd9hr2l
@user-rd9pd9hr2l Ай бұрын
Inuyo munabwera ngati coming 🔥
@MisheckAselo
@MisheckAselo Ай бұрын
A pule ayamba kupemphera ku CCAP kamutu kataya
@joneskalitsilo6556
@joneskalitsilo6556 Ай бұрын
Exactly Wonder bambo wanzelu amakonza mavuto amu nyumba mwake not kutuluka nkumakadandaula panja or kubwalo kuti mnyumba mwanga sitikudya ana anga sakuvala bwino, sitikudya bwino! Nde ana Inu muzivala bwino, muzidya bwino, ukuganiza kuti anawo azitenga kuti?
@peternashyo9850
@peternashyo9850 Ай бұрын
Nkhaniyo ndiyoona, a President akugona kwambiri pachiongolero, dziko silingatukuke ai
@henryphiri6100
@henryphiri6100 Ай бұрын
Anaphedwa ku Mwanza aja ndiochepa.pano ayesetsetsa kupha ambiri.athakati sadzasintha.Malawi Congress of Perishers
@DarlingtonMaya
@DarlingtonMaya Ай бұрын
Gyz mmmatha
@user-nf3ik3ff6y
@user-nf3ik3ff6y Ай бұрын
MCP ndi Yakupha
@PartsonKamkuzi
@PartsonKamkuzi Ай бұрын
Iwe pankuku osamayakhura mowopa apa
@BENSONRANGWANI
@BENSONRANGWANI Ай бұрын
Chakwela wamupha chilima zasala zosatila Zach
@MuhamadYassin-ye4hn
@MuhamadYassin-ye4hn Ай бұрын
Mumakwana mabigi
@Amos-tr6ro
@Amos-tr6ro Ай бұрын
Koma makosana inu MMM mwanditha keen on on our behalf
@jackmambo2638
@jackmambo2638 Ай бұрын
Kod amaphang’ombe ali kut😂😂
@user-cf9yz3ei5o
@user-cf9yz3ei5o Ай бұрын
Did. Mcp ask Afford
@StiveKantiki
@StiveKantiki Ай бұрын
Aganizq bwanji mwakuya kuposa anthu zosatheka ubongo unatha chifukwa ankadya zopasidwa Za chaulele
@user-tg7ni7wh2c
@user-tg7ni7wh2c Ай бұрын
Eeh 😂
@johnmhango9405
@johnmhango9405 Ай бұрын
A kaliati ndi a njawala nzokonza izi, akufuna apange handpick Kabambe, can't you read between the lines? Typical of atsogoleri a dyela.
@user-fd1tu6ku1r
@user-fd1tu6ku1r Ай бұрын
Emusipi ofunika isale yokha. Anthu woipa awa
@frankdomingo1109
@frankdomingo1109 Ай бұрын
Decisiveness palibepo
@yusufjab786
@yusufjab786 Ай бұрын
Ndipo inuyo kumeneko mumaitha 😂😂😂 akuchedwesa ndi chakwera
@user-cf9yz3ei5o
@user-cf9yz3ei5o Ай бұрын
You. are. wrong. it. Is. People. at. the. grassroots. who matters not individuals
@PartsonMdeza
@PartsonMdeza Ай бұрын
🤣🤣🤣 iponden fadah kkk
@MosesShaibu-ee8hn
@MosesShaibu-ee8hn Ай бұрын
Ofufuza ngozi akuti, khoswe akakhala pakhate sapheka
@SteveChapola
@SteveChapola Ай бұрын
Asiyeni atuiuka chifukwa chake achakwera apha chirima ndipo ndizoona
@lastonmasoatenganji-bs5gf
@lastonmasoatenganji-bs5gf Ай бұрын
Osamayiwala ku mudzi kaamba kokomedwa ndi maidyaidya chifukwa tsiku Lina amadzakusandutsa mtsamiro wa mfumu ikadzamwalira.
@michealchaomba9761
@michealchaomba9761 Ай бұрын
😂😂😂 President wake utiyo mukudikira kuti azuzuleyo
@MarthaBanda-ye4pt
@MarthaBanda-ye4pt Ай бұрын
Koma Wonder Ati kukura mtima 😂😂😂😂🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥uyatseni basi ng'alulani basi
@user-ru4px8os2v
@user-ru4px8os2v Ай бұрын
Anthu ake ndi chimwendo banda,howeh mkaka,zikhaleng'oma ndiomwe akuyenela kuchoka
@ThandiMbewe
@ThandiMbewe Ай бұрын
Musamamuzile zochita president, yekha samawona???
@Extratremendouszeus
@Extratremendouszeus Ай бұрын
President wake uti Ma comments 100 wa MCP yekha .chita manyazi😅😅
@SteveChapola
@SteveChapola Ай бұрын
Chakwera ndiwofoka koma kumagaanthu chimenecho ndiye chitukuko.chake
@NdazionaKumcheza
@NdazionaKumcheza Ай бұрын
Ine dakalira malemu za chipani tizitaye uko aaa
@YusufuUsumani
@YusufuUsumani Ай бұрын
agaluwa alilimosi ndi chachera
@JudithMaida-ug4oi
@JudithMaida-ug4oi Ай бұрын
Mumatiimilira big hands for you
@PartsonKamkuzi
@PartsonKamkuzi Ай бұрын
Osamayakhura ngat akupatsani za lent kung'alura basi ukuva iwe ndevuzamwayi !!
@user-ql8nf2vb8s
@user-ql8nf2vb8s Ай бұрын
Inu a times muyang'ane mgwirizanou kuchokela mmbuyo inunomwe mumaunikira mgwirizanou mmene umayendela chilima asanamwalile asiyeni ausi ali ndigululawo odya zake alibe mulandu
@MuhamadYassin-ye4hn
@MuhamadYassin-ye4hn Ай бұрын
Mumakwana mabigi
ZOMWE ALANKHULA DR CHAPONDA  KWA ATOLANKHANI  |
20:53
DZIWE TV
Рет қаралды 713
Harley Quinn's plan for revenge!!!#Harley Quinn #joker
00:49
Harley Quinn with the Joker
Рет қаралды 28 МЛН
World’s Largest Jello Pool
01:00
Mark Rober
Рет қаралды 127 МЛН
BEAN PHIRI WAFOTOKOZA ZOMWE ADZACHITE |
20:13
DZIWE TV
Рет қаралды 672
Malodza Akuchikangawa A Poem by Sir Michael Benjala
5:00
Clement Thanda
Рет қаралды 7 М.
Shamim Mayanja(Zubeda) akooye aba Family
50:18
Kasuku Live
Рет қаралды 3,1 М.
MAYI PATRICIA KALIYATI  WANG'ALURA KU INTERVIEW | PART 1 |
30:47
TIMES SPECIAL - ENG. VITUMBIKO MUMBA  |  6 AUGUST 2024
58:46
Club Junta
Рет қаралды 1,3 М.
KULANKHULA MOSAOPA MAYI PATRICIA KALIYATI  | GAWO LOMALIZA |
29:37
AKUFUNA KUPANGA ALLIANCE NDI MCP ALI OLANDILIDWA |
21:18
Harley Quinn's plan for revenge!!!#Harley Quinn #joker
00:49
Harley Quinn with the Joker
Рет қаралды 28 МЛН