No video

Kachikenaso Born Kalindo 😂🙌😂😂🙌 pa Chi Sunday 14 July 2024

  Рет қаралды 25,668

Malawian Cameras

Malawian Cameras

Ай бұрын

Пікірлер: 85
@user-do2cs8nf4b
@user-do2cs8nf4b Ай бұрын
Ndalama zingowonongedwa anthu angofa mdzipatalamu mankhwala kulibe anthu angofa sisawawa Mulungu akuwoneni mwapaderadera
@user-nz7bd7lm4i
@user-nz7bd7lm4i Ай бұрын
Born mulungu azikudalitsa kwambiliiiiiiiiiiii ndipo azikuteteza🙏🙏🙏
@MustaphaCassim
@MustaphaCassim Ай бұрын
Chakwera akuwalipira azungu pa ntchito yomwe adagwila pakupha chilima
@ExcitedBreakingWaves-oh3zb
@ExcitedBreakingWaves-oh3zb Ай бұрын
Achakwera akuwononga dziko lathu kwambiri.
@user-wd9yd1bg9n
@user-wd9yd1bg9n Ай бұрын
Dziko lochitisa manyanzi, nkumati achakwera akugwira ntchito ngati president.
@user-fh7sd6gp3f
@user-fh7sd6gp3f Ай бұрын
Tiyamike kubwera kwa tonse Alliance anthu mukung'alula kuti anthu tiziwe zenizeni more 🔥 🔥
@officemoyenda-rj2hz
@officemoyenda-rj2hz Ай бұрын
Koma this very very shameful 😢😢😢😢😢
@cjaymw496
@cjaymw496 Ай бұрын
Ya balance I think so too😂😂😂
@fredsemu7136
@fredsemu7136 Ай бұрын
KOMA CHIKANGAWA ATIPWETEKA NDITHU
@MisheckAselo
@MisheckAselo Ай бұрын
Chakwera mchifukwa chake anakapemphera ku CCAP kamutu kataya mission yapheduka, umkaona ngati wapha chilima zako ziziyenda, chilima sanafe akanalipo muona zakuda inu😂
@ThokozaniMunkhondia
@ThokozaniMunkhondia Ай бұрын
A born kalindo,inu ndi mbambande😢😢
@edsonnyasulu5394
@edsonnyasulu5394 Ай бұрын
Koma bon mulungu akuteteze
@ClearKondowe-m3j
@ClearKondowe-m3j 28 күн бұрын
Very sorry a Malawi kaya dziko lathu likonzedwa. Yoooo
@HappyAbyssinianCat-xt2bm
@HappyAbyssinianCat-xt2bm Ай бұрын
Mulungu wakiya nawe chakwera waona mulungu wakwiya ndpo mulungu achita nawe iweyo
@user-qn2nu4xs9i
@user-qn2nu4xs9i Ай бұрын
Ati akukonza zinthu!....😅😅😅😅😅😅😅...koma kukonza kunasintha..
@ZettaImuranYunusu
@ZettaImuranYunusu Ай бұрын
Osati Ifeyo Amalawi ai.... But all opposition party's we are with you Trap
@user-ik5sz8hc6f
@user-ik5sz8hc6f Ай бұрын
Ima poyela ndipo aliyense azimva ndithu.Tinasankha satana
@crosbeygondwe5403
@crosbeygondwe5403 Ай бұрын
Kung'alulaaaa😂😂😂😂
@robertkamtimaleka4394
@robertkamtimaleka4394 Ай бұрын
a Born Kalindo 42 million yommweyi basi
@wonganichakakanyirenda3299
@wonganichakakanyirenda3299 Ай бұрын
Chakwera iweyooo
@user-hh4wn4vf9e
@user-hh4wn4vf9e Ай бұрын
Auze DC ❤ agaru amenewo
@SumanJames
@SumanJames Ай бұрын
Akalindo sakunama
@stevenbanda6665
@stevenbanda6665 Ай бұрын
Tiuzeni zambiri bwana .kma dziko lathu lomwe kuzunzika
@DineoKotjomela
@DineoKotjomela Ай бұрын
Ma mafia ati😂😂😂
@user-oy6dl1pv9e
@user-oy6dl1pv9e Ай бұрын
The DiiiiiiiiiiiiiiiiiiiiiiiiiCiiiiiiiiiiiiiiiiiiiii
@JamesTeacher-b3o
@JamesTeacher-b3o Ай бұрын
Bwana inuyo mmatha kuyankhula ulemu wanu
@AufiThera
@AufiThera Ай бұрын
Wathu wathu born kalindo ✌️🔥 Kung,alula💯💪
@HalisonSolomon
@HalisonSolomon Ай бұрын
KKKKKKKKKK BALANCE KUWAMALIZIRA PANTCHITO YOMWE ANAGWIRA PAKUPHA CHIRIMA NDI ANZAKE SHAME CHAKWERA
@user-ck7eb7tb7v
@user-ck7eb7tb7v Ай бұрын
Munyengo yakung'alula
@Mikekajawo-pq9nr
@Mikekajawo-pq9nr Ай бұрын
At we are building Malawi yet ndalama zikutuluka
@Musa1828-l5d
@Musa1828-l5d Ай бұрын
Ndalamq zathu misokho yutha ukupeleka kwazigawenga azipha azibale anthu osalakwa Chakwera sukuwina ase ndakuuza
@peternashyo9850
@peternashyo9850 Ай бұрын
Malawi akulowera kuti abale? Long live the DC
@SolomonNjolomole
@SolomonNjolomole Ай бұрын
The DC ❤❤❤
@DineoKotjomela
@DineoKotjomela Ай бұрын
Ma mafia 😂
@Pangolinimw
@Pangolinimw Ай бұрын
The DC 😅😅😅
@user-xx4mt8ox8e
@user-xx4mt8ox8e Ай бұрын
Mwati ndi Balance?
@RitaKainga
@RitaKainga Ай бұрын
Ulemu wanu the DC
@GeoffreyMaulana-rh5rx
@GeoffreyMaulana-rh5rx Ай бұрын
Ng'ona zalusa kufuna kusaulisa Malawi
@patrickmacheso5062
@patrickmacheso5062 Ай бұрын
Mr Bon Kalindo ndinu oyankhuliradi a Malawi tonse, keep it up the DC.
@WilliamKawaza
@WilliamKawaza Ай бұрын
Tell them DC
@jamesgama5489
@jamesgama5489 Ай бұрын
Ayi zikomo
@BlessingsMikeyasi
@BlessingsMikeyasi Ай бұрын
Nazoooo
@adzonzicomedy
@adzonzicomedy Ай бұрын
😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂
@user-do2cs8nf4b
@user-do2cs8nf4b Ай бұрын
Chili chonse chingowululika kumwamba kulandire ulemu
@AnnastasiaChakwiya
@AnnastasiaChakwiya Ай бұрын
Ai zikomo achakwera
@Leo-fj6gz
@Leo-fj6gz Ай бұрын
😢😢😢😢😢
@user-rs7vx6hc1k
@user-rs7vx6hc1k Ай бұрын
Koma what is the use of our currency in Zambia? I don't understand this.
@BornfiyesignalSignalmtema
@BornfiyesignalSignalmtema Ай бұрын
The dc
@pempheroraynnoxmpesi8713
@pempheroraynnoxmpesi8713 Ай бұрын
Ya balance 😢 RIP SKC
@user-bd5kw8oq1r
@user-bd5kw8oq1r Ай бұрын
Choka iwe mbuli zokhazokha zomwe ziimakunvera iwe gawanani ndlmazo paja ndiyo ntchito yanu 😂😂😂mwayi ndi MCP ukudya bwino kamba ka mabodza akowo azipani akumakulipila 😅😅😅uziyamklika wamva
@tingamasi106
@tingamasi106 Ай бұрын
Mbuli ndiwe mavuzi okhwimawo
@Dysonkhofi
@Dysonkhofi Ай бұрын
Iwenso ndiwe galu,chitsiru
@user-bd5kw8oq1r
@user-bd5kw8oq1r Ай бұрын
@@Dysonkhofi fisi,chule,mbuzi,,bulu munayiwala zimenezo zikomo God bless you 😊😊❤️❤️❤️ work up time is almost finished Jesus Christ is coming soon get ready before we die
@ednakaluwa5414
@ednakaluwa5414 Ай бұрын
​@@user-bd5kw8oq1rutukwana anzako..opanda chifukwa ena akubwexera utchula dzina la Mulungu shame on you.
@ednakaluwa5414
@ednakaluwa5414 Ай бұрын
Vuto u need attention
@JamesAlinafe
@JamesAlinafe Ай бұрын
Tha DDDDD ccccccccc
@katalamajames4947
@katalamajames4947 Ай бұрын
Koma keni nsonda amadya mutu nkhope the same sekeleton ma R. V.sakugwira nchito
@zimmekapachika6784
@zimmekapachika6784 Ай бұрын
😅😅😅😅😂😂😂mankwala anapima sakugwila 😅😅😅😅😅😂😂😂yomweyo galu iwe
@GanieAlidih-gu7no
@GanieAlidih-gu7no Ай бұрын
Kukuyu nyamayake
@user-wd9yd1bg9n
@user-wd9yd1bg9n Ай бұрын
Komanso chibadwireni ine ntchito ya asilikali athu muno mu malawi sindikuiziwa, chifukwa ngati nkuteteza dziko .bwezi atalipanga boma ili held responsible pa nkhani iyi infact predent akadamuchosa.
@user-lc3sw8iz2g
@user-lc3sw8iz2g Ай бұрын
Balance
@AndersonChimwala-hz4so
@AndersonChimwala-hz4so Ай бұрын
koma amalawi
@LiamTennessee
@LiamTennessee Ай бұрын
Amazalandila malipilo a ntchito yomwe adagwila
@RobertLuka-wy9cl
@RobertLuka-wy9cl Ай бұрын
Born kalindo 🙏🙏🙏🙏🙏
@user-jn7bt1uy5s
@user-jn7bt1uy5s Ай бұрын
Zovetsa chisoni 😢
@JohnConar-kq4hi
@JohnConar-kq4hi Ай бұрын
The DDDDDDDDDCCCCCCCCCCCC 🤔
@kelvinsibande8779
@kelvinsibande8779 Ай бұрын
The DDDDDCCCCCCC
@WilliamBandaWili
@WilliamBandaWili Ай бұрын
Mmmmm haa?
@CharityChikomo-hl1gz
@CharityChikomo-hl1gz Ай бұрын
Ma 20kwachawooo??
@MinhoMasanza
@MinhoMasanza Ай бұрын
Yah ndima mk20 koma each carton contains more than a million
@hudycorex1893
@hudycorex1893 Ай бұрын
Mk20 Sindalama????? Iwe ndendiopepera bwanji!!!
@rhodricksalima5387
@rhodricksalima5387 Ай бұрын
Paliso ma 5 pin tu
@CharityChikomo-hl1gz
@CharityChikomo-hl1gz Ай бұрын
Opepela ndi amako
@chadreckchibwithala1493
@chadreckchibwithala1493 Ай бұрын
ANTHU PANO MMANGO PANGA MA COMMENT KOPANDA KUSATILA ZINTHU . NDALAMA ZOMWE ZAPEZEKA KU ZAMBIA NDI ZAMAYIKO ANGAPO KUPHATIKIZA MALAWI ANTHU OMWE APEZEKA NAZO NDIZINKA ZA KU RUSSIA OMWE AKUPANGA MA BUSSINES A MA DRUGS OSATI ZOTI BOMA AYI MMM KALINDO ECHI BOZA LENILENI ZINAMIZA ACHILOMWE AKOWO
@TysonMwenye
@TysonMwenye Ай бұрын
Ndiye anthu aku Russia wo angapeze ndi ndalama zathu chifukwa choti akugulitsa ma Drugs? Ifeyo tikamapita ku mayiko akunja timasintha ndalama zadziko lomwe tikupitako.Ndipo tikamaliza business yathuyo tisanatuluke mudzikolo timasinthilatu zamalawi.Ndiye awowo apezeka bwanji ndi ndalama zathu (Mwk) koma kudziko lina chinawakanikitsa kusintha kumalawi konko ndichani ngati ndizachilungamo ndalamazo
@tingamasi106
@tingamasi106 Ай бұрын
Ndalama zama drug mpaka sealed? Iwe ndichimbutumwa wamva
@munashemoyo4190
@munashemoyo4190 Ай бұрын
Kusonyeza kt zomwe zikuchitika dziko muno iwe zikukusangalasa et i uzaziwona ukazakwatila ukasiya kudyesedwako mbudzi yamunthu iwe kape
@AmosScott-z9x
@AmosScott-z9x Ай бұрын
Kape iwe
@chadreckchibwithala1493
@chadreckchibwithala1493 Ай бұрын
mbutuma ndinu osaziwa zinthu alomwe matama basi tiyeni uko . mleke kutivuska mngalamuliraso yai chalo ichi jiiiiiiiii peter wanuyo no
@user-si8vm5vj8s
@user-si8vm5vj8s Ай бұрын
Shame on you chakwera
@warrenmwambazi8342
@warrenmwambazi8342 Ай бұрын
Very bad 😊😊😊
@FrancoKaunga-rq2ki
@FrancoKaunga-rq2ki Ай бұрын
Kalindo ndi nyatwa auze zitsiru izi.
@DineoKotjomela
@DineoKotjomela Ай бұрын
Ma mafia 😂
EVOLUTION OF ICE CREAM 😱 #shorts
00:11
Savage Vlogs
Рет қаралды 14 МЛН
CHOCKY MILK.. 🤣 #shorts
00:20
Savage Vlogs
Рет қаралды 27 МЛН
Викторина от МАМЫ 🆘 | WICSUR #shorts
00:58
Бискас
Рет қаралды 6 МЛН
Get 10 Mega Boxes OR 60 Starr Drops!!
01:39
Brawl Stars
Рет қаралды 13 МЛН
Tamale Mirundi Afudde Munyivu!! Muganda we Abotodde Ebyama ne Tapes
38:56
MALAWI COURT.... TAMVANI IZI ABALE 🤔
20:45
Jimmy
Рет қаралды 151 М.
BON KALINDO  LERO PA 17 JULY 2024 |
18:32
DZIWE TV
Рет қаралды 25 М.
Zomwe Zinachitika Kut Ndege Isowe
5:19
Sam Malvitha
Рет қаралды 226 М.
JOHN KAPITO WATOPA NAYE CHAKWERA. Ityoke ityoke Osabisa mau // PART 1
33:23
kumalawi Chinyengo Chaonjeza mopyola muyeso Iyaa
3:45
Malawian Cameras
Рет қаралды 6 М.
EVOLUTION OF ICE CREAM 😱 #shorts
00:11
Savage Vlogs
Рет қаралды 14 МЛН