No video

Kamlepo Kalua wayankhura mosaopa ndipo iye Wati wamvaso kuti they’re planning to kill his son

  Рет қаралды 64,753

Makosana

Makosana

Күн бұрын

Пікірлер: 165
@AlbertEngelbercht
@AlbertEngelbercht Ай бұрын
Mwachitamakola kuwaphalila unenesyo, chiuta wamusungeni dada kamulepo,we are In democracy time!!!!.
@user-dp9uy6qt7x
@user-dp9uy6qt7x Ай бұрын
Makolawaka 😊kwalinamwe manda 6 jjjjjoo9ooj .0pll0 V
@petermanMitambo
@petermanMitambo Ай бұрын
Very powerful speech.long live Mr KALUA. may God protect you from these heartless swines
@Shelifibraheem
@Shelifibraheem Ай бұрын
Good massage Mr u are the strongest man
@georgemsowoya6525
@georgemsowoya6525 Ай бұрын
Mcp pamoz ndi achakwera achepa there days are numbered....live long dad kaluwa and much love to fredo kiss ,,, I speak divinely protection in that family ,God be with you
@user-uv5rf4zt5q
@user-uv5rf4zt5q Ай бұрын
Mr kamlepo kaluwa one of the greatest politician in Malawi u fought for democracy MCP is getting us backwards to dictatorship arresting and killing innocent people this is not what the voters wanted.
@MosesKalenge
@MosesKalenge Ай бұрын
Powerful massage bwana Mr KALUA ❤🎉🎉🎉
@normantondole2669
@normantondole2669 Ай бұрын
Why not taking them (police) to court Mr Kalua?
@PrinceernestBorniface-x1m
@PrinceernestBorniface-x1m Ай бұрын
Apolisiwo ndi chakwela onse machende awo fotsek...
@mathewskhamula3212
@mathewskhamula3212 Ай бұрын
😂😂😂😂😂
@CliftonMaseya
@CliftonMaseya Ай бұрын
Mvamvekatu ma words umu 🔥🔥🔥🔥🔥
@JailosGazahBoica
@JailosGazahBoica Ай бұрын
My Land 😢😢😢our warm heart of Africa 😢😢😢😢our peace,joy and harmony county has turned into Sodom and Gomorrah 😢😢😢😢
@DavidJackson-ox4xm
@DavidJackson-ox4xm Ай бұрын
I support kamlepo munthu wa mkulu kwambiri mumakwanila.
@user-ky4ce9gb6j
@user-ky4ce9gb6j Ай бұрын
Ndipo ari mu history
@FrancisMbewe-xn2pl
@FrancisMbewe-xn2pl Ай бұрын
Powerful Papa ❤ palibe wamuyaya tonse tizafa bas
@brightsonsaidi
@brightsonsaidi Ай бұрын
Pls bring out the CCTV footage here, ASAP. It will have a heavy impact on people's minds
@MadalitsoMalamba
@MadalitsoMalamba Ай бұрын
MCP makolo amkatiuza kuti ndi chipani chakupha ndiye tikutha kuonadi and I don't think wachinyamata ozindikira bwino mkumakaponyera vote MCP....
@MikeMerecah
@MikeMerecah Ай бұрын
Konwani kamponje ndiwe opusa kwabasi ukuona ngati kamlepo kalua ndi size yako, Bwana my God protect your family,,,,,,,,
@unitelectronicmedia4581
@unitelectronicmedia4581 Ай бұрын
This man is loaded! Wati ndigenda waponda MWALA
@StevenTembo-mb7rm
@StevenTembo-mb7rm Ай бұрын
Well said I hope pala ni wanthu wa umunthu wawo wapulika and if they may attempt to kill Fredo this country will go beyond what happened in Kenya. We are ready
@tamandaninampinga
@tamandaninampinga Ай бұрын
Thanks dada for the message
@samchibenene4458
@samchibenene4458 Ай бұрын
God is great be safe and your family Mr kamulepo
@user-wf8xm3km3s
@user-wf8xm3km3s Ай бұрын
What a powerful message
@shaffiejumah6385
@shaffiejumah6385 Ай бұрын
We respect you mr kalua we leant alot and we still learning much love...
@MuhammadBAKILI-kl2mj
@MuhammadBAKILI-kl2mj Ай бұрын
🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏 Father kamulepo kaluwa tili pambuyo panu
@PrinceThom-pe6ie
@PrinceThom-pe6ie Ай бұрын
Don't worry dad 2025 mcp police tizayikhaulisa
@JuliusChamwanje
@JuliusChamwanje Ай бұрын
History we learn alot
@amadichembe4068
@amadichembe4068 Ай бұрын
100%
@chirwaellace1093
@chirwaellace1093 Ай бұрын
Ayiwala zoti achoka pampando, shame on you. May God be with you Kamlepo
@PrinceKachimanga
@PrinceKachimanga Ай бұрын
WE LOVE U KAMLEPO...MCP YIKUTULUKA M'BOMA CHAKA CHA MAWA...
@PrinceernestBorniface-x1m
@PrinceernestBorniface-x1m Ай бұрын
This is very stupid insane 😠... Chakwela should resign galu wachabechabe
@user-nf3ik3ff6y
@user-nf3ik3ff6y Ай бұрын
Good Messnge Mr Kamulepo kaluwa ❤ Chakwela you mast go watikwana
@alicegama8138
@alicegama8138 Ай бұрын
Apo ndipo wamanya kuti watumbuka wokhumba yay kuwaseweleska
@WillamChihana
@WillamChihana Ай бұрын
Mwayowoya bwana ndipo nakondwa nazo fundo zino zose chiuta wakuona vose
@TopoTopo-bm4vw
@TopoTopo-bm4vw Ай бұрын
Good massage kalua
@user-vf2fo1mb2c
@user-vf2fo1mb2c Ай бұрын
Yebo mwawanthu, don't touch Tumbuka people, we believe in Jesus
@lumbaninyirenda8223
@lumbaninyirenda8223 Ай бұрын
kumpoto MCP kulibe vote
@johnmponda9070
@johnmponda9070 Ай бұрын
Oh my God Malawi police and Malawi defence force are just used they don't even know what they responsibility is really shame on them
@user-ex7jn2fh1g
@user-ex7jn2fh1g Ай бұрын
I love the the guy
@ElemiahKavute
@ElemiahKavute Ай бұрын
Mupheni kkkkkkk andale amwene 🤣🤣🤣🙌 atitu enawo anyumwe kkkk muphenitu akamlepo akusendeno muone
@augustMag
@augustMag Ай бұрын
Mmmmm koma abale mpaka kukuonongerani zinthu mnyumba abweze katundu ameneyo
@FrancisMbewe-xn2pl
@FrancisMbewe-xn2pl Ай бұрын
We fear God not person 💪🔥
@user-so7wg6ii5m
@user-so7wg6ii5m Ай бұрын
Message ya mphamvu ❤
@HendrixGrem
@HendrixGrem Ай бұрын
Wise speech Honourable
@user-ro1pl7rv7z
@user-ro1pl7rv7z Ай бұрын
*Amtumile mwenye* kwabasi nambo ngadandaula Mcp chipani changalumbana Ata panondi.
@JailosGazahBoica
@JailosGazahBoica Ай бұрын
May God protect you and your family
@SolokingChimzy-yt7dj
@SolokingChimzy-yt7dj Ай бұрын
Ndikukaika ngt anthu afike nthaw yovota bwinobwino ..zikundionekela ngat mavote azizizi akhoza kuchitika mu Mziko muno...
@simonsteven7577
@simonsteven7577 Ай бұрын
Kwabasi
@stevenchimombo9815
@stevenchimombo9815 Ай бұрын
Kkkkk😂
@KateRose-sh8zl
@KateRose-sh8zl Ай бұрын
Pathu sipadziko zoona but the voters are suffering bwana
@user-cx5hh8yf5h
@user-cx5hh8yf5h Ай бұрын
😂 koma kwachema osapanga mantha aonese
@natashamathala8715
@natashamathala8715 Ай бұрын
Koma nde mwangoti 3stars apa pali nkhani apa tiuzeni zambili bwanaaa
@giftstima2613
@giftstima2613 Ай бұрын
What does it mean?
@PrinceBlessings-bv5bs
@PrinceBlessings-bv5bs Ай бұрын
Mmmm nde afika posausano... Kupha bas!!!!! Eeee why Malawi now
@glynbulambo
@glynbulambo Ай бұрын
Mwana wamupoka wayoghoya wa chewa mfela za Eni 😅
@wonganikaunda
@wonganikaunda Ай бұрын
Mukapha uyu nde muyalukatu poyerayera
@user-ky4ce9gb6j
@user-ky4ce9gb6j Ай бұрын
Ndipo kwambiri tu mmm
@AbdulSelemen-q5j
@AbdulSelemen-q5j Ай бұрын
Osaopa osaopa palibe wambewu padziko pano, ndipo kalikonso kazalawa imfa.
@zayedmitawa8345
@zayedmitawa8345 Ай бұрын
Andale amafuna kukhala pa mpando forever yet amapanga zoononga mu nthawi yochepa I don't understand then at all. Being good will not make you lose anything at all but being bad eeeh ndi izi za cheucheuzi
@MustaphaCassim
@MustaphaCassim Ай бұрын
Chitukuko chA razalo ndikupha basi
@user-tk6qh9zs7h
@user-tk6qh9zs7h Ай бұрын
Ngati muja Chinalilinso Chitukuko Cha Peter Mutharika pakupha Issah Twaib Njaujyu, Buleya, Masambuka, Tambala Family kutchulapo chabe ochepa
@isaacpelani
@isaacpelani Ай бұрын
​@@user-tk6qh9zs7hmuli m'bomatu. Tengerani umboniwu kukhoti tidziwe zoona zenizeni. Mwina munkapha ndinu kuti muipise mbiri yaamnzanu
@LukaThawe
@LukaThawe Ай бұрын
Yah ndimakape
@VincentTembenu-ip5ii
@VincentTembenu-ip5ii Ай бұрын
Mmm mpaka I know akumidima omwe mumadalila 2025 Kuli ntchito
@RABSONChisambi
@RABSONChisambi Ай бұрын
30:24 my God protect you kamulepo and your family ilike what you saying
@kidneyblessingschilinguloj7292
@kidneyblessingschilinguloj7292 Ай бұрын
Rise up Kamlepo we want peace
@zaitwazaitwa941
@zaitwazaitwa941 Ай бұрын
Koma ndiye Kwachema
@chifundochimenya6368
@chifundochimenya6368 Ай бұрын
😢 indeed this world it's not our home am crying Malawi
@IsaacTsinde
@IsaacTsinde Ай бұрын
Mwayankhula abwana
@FiskaniTonymahone-vl3og
@FiskaniTonymahone-vl3og Ай бұрын
Chakwera, don't know,do good, be good, live good, he's no good..
@BenjaminMoffat
@BenjaminMoffat Ай бұрын
big boy ting set
@MagretMvula
@MagretMvula Ай бұрын
Dadi apa mwafikapo muuzeni zoonaasiye chibwanamooto uyake asazolowele
@AustinBornface
@AustinBornface Ай бұрын
Tili mukati mweni mweni
@JoyMpinga
@JoyMpinga Ай бұрын
Ntchana asamuyese ghetto azaimva
@KunyengaMoyo
@KunyengaMoyo Ай бұрын
Kuyankhula kwabwino uku, nawo apolice alibe nzeru angowagwiritsa ntchito malipiro ochepa km kumangozunza anthu
@AlexKaunda-ny2eg
@AlexKaunda-ny2eg Ай бұрын
Tavuka na mcp onse wa mcp mavi yao (komaso inu akamulepo mukufoila kwambili mr kalua u sleep too much
@MirajLaja
@MirajLaja Ай бұрын
Za phone iwalani asiyileni ikhale yawoo...
@mathewskhamula3212
@mathewskhamula3212 Ай бұрын
Leader
@mathewskhamula3212
@mathewskhamula3212 Ай бұрын
Ing'aluleni bwana Kaluwa,,,,,,,,,,,,
@emanuelnziza1193
@emanuelnziza1193 Ай бұрын
Awawa ngat ali mau awodi. Aah the Man must be suspected sure
@MuhammadBAKILI-kl2mj
@MuhammadBAKILI-kl2mj Ай бұрын
Kamulepo kaluwa mumatiyomilira munatsala nokha (RIP chakufwa chihana)
@GibsonLackson
@GibsonLackson Ай бұрын
Ayelekeze 😳😳😳😳
@MuhammadBAKILI-kl2mj
@MuhammadBAKILI-kl2mj Ай бұрын
We love you Kamulepo Kaluwa
@MacdonaldMisomali-lt4wu
@MacdonaldMisomali-lt4wu Ай бұрын
Aphe fredo awone
@ShakiraOsman-e8g
@ShakiraOsman-e8g Ай бұрын
Komanso katundu anaonongayo abweze
@DavidMtambo-zm8ne
@DavidMtambo-zm8ne Ай бұрын
Nabo bafwenge bachakwera kulije wamuyaya
@chirwaellace1093
@chirwaellace1093 Ай бұрын
Achilundi samalani, msaone ngati mwafika. Lindani madzi achilundi apite nde mziti mwadala, nzosiilanatu izi osasimbwa.
@user-bm1sf4sk1p
@user-bm1sf4sk1p Ай бұрын
Powerful
@HawaiijeminieHawaii
@HawaiijeminieHawaii Ай бұрын
Fact
@user-lc3sw8iz2g
@user-lc3sw8iz2g Ай бұрын
Akapha mwana inunso tiyeni tikaphe awo. Ofunika kuyamba kubwenzera. Zatopetsa. Athuwa akufuta chifukwa amalawi sabwenzera.
@TadalaMaumbo
@TadalaMaumbo Ай бұрын
I support you
@BrightNkhoma-xz4bg
@BrightNkhoma-xz4bg Ай бұрын
With heavy heart
@SydneyChiphaka
@SydneyChiphaka Ай бұрын
Why Mr Kamulepo want to kill his own son? Sad
@josephnkungunthah4472
@josephnkungunthah4472 Ай бұрын
Nonsense did you here him kut akufna kumupha mwana wawo
@GiftJulius-gx2kb
@GiftJulius-gx2kb Ай бұрын
Afa okha
@user-un4pm4yt5i
@user-un4pm4yt5i Ай бұрын
Koma ndiye ndinthawiso yakamuzutu aaa
@FRANKCHIFUNIRO-c6h
@FRANKCHIFUNIRO-c6h Ай бұрын
28:52
@ellenchipula9809
@ellenchipula9809 Ай бұрын
Chakwera pa m’tongo pa mako
@GospelSoldiers-sr7np
@GospelSoldiers-sr7np Ай бұрын
Ndipo ndizoonadi zamawa siziziwika
@prettytambala5687
@prettytambala5687 Ай бұрын
Muzazisumire zimbava izi zidzakulipireni hiyaaaaa
@MussahWilliam-py1ff
@MussahWilliam-py1ff Ай бұрын
Koma ndalama mani mmmmmh ay ndinthu mmmh anthuwa guyz samagona muja tigonera enafe
@KhumboZimba-x1z
@KhumboZimba-x1z Ай бұрын
Mawu amphamvu kwambiri chakwerayo ngati kulikumva wamva dziko ndilizungulira
@kelvinedson685
@kelvinedson685 Ай бұрын
That's fact's indeed
@bridgetmajor3646
@bridgetmajor3646 Ай бұрын
Koma z..ikoli ...Amwene
@JaxyKumwenda
@JaxyKumwenda Ай бұрын
Munthu wamkulu wayankhura❤
@OwenMajoni-qv3eg
@OwenMajoni-qv3eg Ай бұрын
Osapita ku khothi bwanji a Kalua? Komanso ndalama zanga simunabwenze kuchoka 2019 paka lero mumaganiza bwanji bwana Kalua? Koma umunthu mulinawo?
@maxwellmsonkho9112
@maxwellmsonkho9112 Ай бұрын
Panyopanu inu achitsilu
@giftwisdom-km7yh
@giftwisdom-km7yh Ай бұрын
Mwachita makola mwawa phalila unenesho. Chiuta wakudangirileni.
@user-vj6jt2df3e
@user-vj6jt2df3e Ай бұрын
Mwamuyambapo kaluwa amayabwatu chwe mwana chwe
@edakweni
@edakweni Ай бұрын
Voice sinali yanu kkkkkk. Apaso mukanaso kuti siyanu
@kondwanimandala4575
@kondwanimandala4575 Ай бұрын
Mawu a mphavu ,ana achepa
@sjrecordschannel7687
@sjrecordschannel7687 Ай бұрын
Chakwera is coword. ..is a worsiest fool ....he stepped into power by grace he was supposed to be a great leader but chitsiru nchitsiru olo kuchipatsa Mwai amauononga...now kupha anthu mopanda chisoni....who do u think u r chakwera?...u think u r immortal?
@zwdydigonia8730
@zwdydigonia8730 Ай бұрын
Ng'aluuulaaaa iwe
Little brothers couldn't stay calm when they noticed a bin lorry #shorts
00:32
Fabiosa Best Lifehacks
Рет қаралды 21 МЛН
❌Разве такое возможно? #story
01:00
Кэри Найс
Рет қаралды 4 МЛН
ISSEI & yellow girl 💛
00:33
ISSEI / いっせい
Рет қаралды 25 МЛН
Schoolboy Runaway в реальной жизни🤣@onLI_gAmeS
00:31
МишАня
Рет қаралды 4,1 МЛН
A Michael Usi Inu Si A UTM - Lyton Mangochi
23:13
Nyasa VoiceBox
Рет қаралды 34 М.
Little brothers couldn't stay calm when they noticed a bin lorry #shorts
00:32
Fabiosa Best Lifehacks
Рет қаралды 21 МЛН