No video

KULONDOLOZA ZA IMFA YA AGNESS KATENGEZA...

  Рет қаралды 45,185

LIKI-LIKI Ladies

LIKI-LIKI Ladies

Күн бұрын

Пікірлер: 49
@raytavares2256
@raytavares2256 8 ай бұрын
Why Are police exposing the details now while the other group is not arrested? You are still investigating the matter and revealing updates just gives a chance to the other criminals Amos committed all the crimes with. You have given the chance for other robbers and nurderes to escape justice.
@ChristianChimwaye-yg9ti
@ChristianChimwaye-yg9ti 8 ай бұрын
Koma MALAWI 🇲🇼 POLICE MWAYIGWIRA NTCHITO. ❤❤❤❤❤❤
@ChisomoMsiska-oi2vg
@ChisomoMsiska-oi2vg 8 ай бұрын
Uyu nayeso aphedwe chimunthu chopanda nzeru zoona kupha mubale wako yemwe amakudyesa😢
@mzeewandembonyirongo2972
@mzeewandembonyirongo2972 8 ай бұрын
Police you have been fast to talk to the public before arresting the others...you have made them run now.
@grayjames904
@grayjames904 8 ай бұрын
Zaboza inu ogwidwa agwidwabe though ayankhulapo and they’re not going in deep details zoyakhula zinalipo lkale how come they catch the dude? Mufuna Muzise ntchito a police 😅😅
@matheromichellenkhalamba
@matheromichellenkhalamba 8 ай бұрын
They know their job, if they have managed to find the lead they have already cracked the case.
@noshallsnesu9174
@noshallsnesu9174 7 ай бұрын
4:36
@user-hs5xv6bk2f
@user-hs5xv6bk2f 8 ай бұрын
Mapazianu apolisi mukulephela kumanga anthu amene akuphesa amalawi ambiri Pano zakubuchala zilipati zakufamase zilipati zawitika zilipati lelo mwabwela poyela chifukwa Choti ndimphawi uyu mukunena Kuti simumauzidwa inu apolisi zonse zakufamase kubuchala Moti simukuziwapo khanthu site ana tsiku likubwela muzanena nokha tisanakufunseni mafunso
@SinoliaEfelemu
@SinoliaEfelemu 8 ай бұрын
Good job keep it up
@raytavares2256
@raytavares2256 8 ай бұрын
This boy Amos Is dangerous, having a sister and living with his sister for free food and secured free
@MercyMwale-wc4lr
@MercyMwale-wc4lr 8 ай бұрын
Mmmh koma abale...your own blood
@user-gk6bf7xe9g
@user-gk6bf7xe9g 8 ай бұрын
Uyuso aphedwe bas palibe kuchitila mwina ai ⚔️🗡️⚒️🧷🔪🐯🐆🐅🪱🦂
@user-zr9uw5hd5f
@user-zr9uw5hd5f 8 ай бұрын
Good job
@user-uu3wy8vl1y
@user-uu3wy8vl1y 8 ай бұрын
Kodi za Njaunju zinathela pati?
@Martha1436
@Martha1436 8 ай бұрын
Ndipo Inenso ndikadakonda nditadziwa.
@user-vp5mg5qz9e
@user-vp5mg5qz9e 7 ай бұрын
Congratulation Lilongwe police
@ibrahimbamusi109
@ibrahimbamusi109 8 ай бұрын
Allan witika ndiye zili pat
@johnman4619
@johnman4619 8 ай бұрын
Apolice athu simumachedwa kumpeza munthu aka thawa .koma mulibe chilungamo mumamtayanso after mutadya mabanzi
@user-fg5iw1qy1k
@user-fg5iw1qy1k 8 ай бұрын
Kuthamangatu kumuonesa koma akapezeka wagulu la apolice azanu mubisa agalu inu mmmm
@EdythGloryNamponya
@EdythGloryNamponya 8 ай бұрын
Kenako tidzamva zoti wafera mu cell
@daniellchinjati2557
@daniellchinjati2557 8 ай бұрын
Ampanga xinthu kubisa zinaxi
@VictoriaWilliam-ms2ft
@VictoriaWilliam-ms2ft 8 ай бұрын
Nkuthekanso kuti mwina waulura kale Amosiyo Koma mwina ndiodziwika Akulephera kumubweretsa poyera
@masulasanudi7286
@masulasanudi7286 8 ай бұрын
Kod mulandu wa Witika uli pat? Pot uyo sali m'boma ndy kuthamangatu kumuyalutsa eee koma apolice mmmm chinyengo
@davidzgambo
@davidzgambo 7 ай бұрын
tikufuna detailed report ya Witika
@user-vh9uk1jy7w
@user-vh9uk1jy7w 8 ай бұрын
Mukamaliza mlandu umenewu mumtengenso Soulosi Chilima wa ku maulanso naye
@user-tz5jo3dd9t
@user-tz5jo3dd9t 5 ай бұрын
Mmmm koma anaganiza bwanji uyu
@user-mu2qw6br2f
@user-mu2qw6br2f 8 ай бұрын
Mtolakhani usamangoti "mlongo wawo" use also brother wa omwalirayo chichewa Cha mlongo wawo sichigwiritsidwa ntchito dziko lonse
@inessmsiyambiri8517
@inessmsiyambiri8517 8 ай бұрын
Iiiii chimunthu chikulukulucho kumasungidwa mmmmm ndekutidi chinali chigawega kwao anachilemphera mchobvuta iiiiii koma mpaka kupha mlongo wake eeeeee
@user-to4or4jw9g
@user-to4or4jw9g 8 ай бұрын
Koma ngakhale amupeza Amos'yo amufunse bwino bwino chifukwa nkutheka alipo anamutuma
@daniellchinjati2557
@daniellchinjati2557 8 ай бұрын
Andale anazela mwa iye
@tshepangmatebele7822
@tshepangmatebele7822 8 ай бұрын
Ndipo mukunena zoona
@user-qh3nb4vx9j
@user-qh3nb4vx9j 8 ай бұрын
We need cctv
@user-lg6ym4hz3w
@user-lg6ym4hz3w 8 ай бұрын
Ndipo tikudikila kuti timve watching from Lesotho
@azunguauskay4903
@azunguauskay4903 8 ай бұрын
Mnyamata oyipa
@user-zy8uy3fw5x
@user-zy8uy3fw5x 8 ай бұрын
Inu anatumidwa ndi andale ameneyo
@ChristianChimwaye-yg9ti
@ChristianChimwaye-yg9ti 8 ай бұрын
Palibeso zoti uyuyu ndi mlongo wawo ayi afunika akaphedwe
@user-in3sh8ru7o
@user-in3sh8ru7o 7 ай бұрын
Sikusinja uyu amphedwe
@BeautyKunje
@BeautyKunje 8 ай бұрын
Mu2 oipa kwambri olo umunthu osampeza
@inessmsiyambiri8517
@inessmsiyambiri8517 8 ай бұрын
Eeeeeeee 🙆🙆🙆🙆
@user-qj7ze8vh4l
@user-qj7ze8vh4l 8 ай бұрын
Eeeee
@user-rv2sr2gr5f
@user-rv2sr2gr5f 8 ай бұрын
Km galu iwe kupha mulongo wako food for free
@austinvincent773
@austinvincent773 8 ай бұрын
Anamuphelanji
@reziejamw4205
@reziejamw4205 8 ай бұрын
sad news😡
@user-ic1xl1tu3m
@user-ic1xl1tu3m 8 ай бұрын
Khondo ndanasi amakupha ndi wako
@EstherZintambira-sq3yy
@EstherZintambira-sq3yy 8 ай бұрын
Ndipo iih chibale chinaopsya
@ChrissyKazinga-jd8dx
@ChrissyKazinga-jd8dx 8 ай бұрын
Km zoti ndichibale ai ndithu muthu oipa uyu
@user-is9fk8uz9i
@user-is9fk8uz9i 8 ай бұрын
Good job
AKUTI BWANJI NZAKE WENI WENI WA THE LATE  DR SAULOS CHILIMA?
54:44
LIKI-LIKI Ladies
Рет қаралды 687
UFITI ULIPO NDITHU...zambiri mukanema uyu
51:32
LIKI-LIKI Ladies
Рет қаралды 54 М.
WILL IT BURST?
00:31
Natan por Aí
Рет қаралды 30 МЛН
Ik Heb Aardbeien Gemaakt Van Kip🍓🐔😋
00:41
Cool Tool SHORTS Netherlands
Рет қаралды 9 МЛН
Glow Stick Secret Pt.4 😱 #shorts
00:35
Mr DegrEE
Рет қаралды 11 МЛН
IMFA YA JANET ULENDO..kafuku-fuku oyamba..
43:15
LIKI-LIKI Ladies
Рет қаралды 45 М.
NDAKUCHINYENGWA MANJE KARANGANDA TV
38:30
Karanganda Tv (Waiyepo ere ?)
Рет қаралды 4 М.
WILL IT BURST?
00:31
Natan por Aí
Рет қаралды 30 МЛН