Mukaona munthu akuti MCP my vote ameneyo ndi wa family ya chakwera mwina ndi ankolo ake kapena chakwera anakwatira pakwawo which means phindu la chakwera akuliwona ameneyo wachita zolozeka kwawoko
@macdonaldmunthali9895Ай бұрын
Very wrong decision,the end of utm.chilima was the only leader with great vision and calmness, you can't make decision out of anger.
Njawala number one, kaluati number two be careful ndi anthu awiriwa ndi anthu oyipa mutima kwambiri We love utm kwambiri koma isakhale ya munthu
@doreenkaliati3166Ай бұрын
Zoona zake anganidze mofasa sure ❤❤❤❤❤
@JaphetSakala-pq4flАй бұрын
UTM motomoto osadandaula
@MosesNanchingaАй бұрын
Ma comment onsewa bwanji simukukamba za ndalama ai kma UTM sinalakwitse kuchoka ku alliance coz sanalandire ulemu uku ku MCP atizuza ndlmazo mukukanika kugulira mankhwala zipatala bwnj
@TonykalicheloKalicheloАй бұрын
Inu ngat mwin wake amafuna kusazika ndiye mukufuna omusatila atan
@lyiemaxАй бұрын
Proper narration, big up guys ❤❤❤
@RegistermoseskashonKashonАй бұрын
Inu nde munabwela kudzauza amalawi tchutchutchu osat akapilikon enawa ongokamba zinthu zopanda kumutu
@user-rf4br1fv2zАй бұрын
Mwawathandiza ulemu
@DalitsoPhiri-sq5nlАй бұрын
Skc ankafuna kutchoka after kusalemekdza mgwirizano omwe unalipo ndiyeno kutchoka it's a good move komano to agree with ndikutenga mnthu kunja that's wrong indeed
@EdsonNjonjoАй бұрын
Munthu uyu akunena zoona
@AlliSaitiАй бұрын
Athu akuda ndife opanda nzeru
@MervinKandojeАй бұрын
You to be specific
@OsmanMasamba-ck4moАй бұрын
Manganya iwetu wagulidwa ndichisilu chinzako
@FloraBanda-w7tАй бұрын
Koma selina 😂😂😂akut kod akabambe akulowela kut 😂😂😂😂
@user-ux9ik4zr5xАй бұрын
Probably the best program
@InnocentEdasiАй бұрын
Ndibwino kt atengane okhaokah
@StevieTaiza-r9jАй бұрын
Mulungu azikutete bro
@user-vm7iz6oz6rАй бұрын
Akumatibera zathu zomwezi zamisokho
@EstherManda-ex3bcАй бұрын
🤣🤣🤣🤣 nkhani zake
@Aqiec09Ай бұрын
Yea that's very true and I see it ku utm utsogoleri unali wa chilima ena onsewa mavuto bola ku MCP komweko mudziwa bwanji mwina the death of chilima was planned with those who are on top blaming MCP for the death yets amafuna mpando wachilimawo why so early kutuluka mugwilizana without solid proof that is MCP guilty , ine unless pa social media muzabwerese real proof how you saw the killing happen that's when I will find them guilty
@ChiyembekezoPhiri-sv8nwАй бұрын
Njawala ndi kaliati mutiwonongera chipani chathu ndakwiya Nanu heavy kuno kuntheu mutisamale awirinu
@Ishriss1999Ай бұрын
Ma prophet watu koma atilankhilitsa pambali mxiiiiew
@mzeewandembonyirongo2972Ай бұрын
Gwende u have fairly advised
@user-lg6ym4hz3wАй бұрын
Kkk😂😂😂😂😂😂😂😂 anzanga afumu owuka
@SabinaNkhoma-sf7kzАй бұрын
Mmmmm km mcp yaonjeza,zot amalawi akuvutika sakuganizako
Nduna zomwe zikugawa ndalamazo akumatibera misonkho yathu yomweyi...ifetu maso athu tikuona ndipo tilankhula chaka cha m'ma chino....40million plus just for one meeting business yanji imene akupanga? Apapa zaonekeratu kuti andale amatibera pomwe anthu akufa ndi njala. Ambuye akukuonani ndithu
@innocentissah2636Ай бұрын
Pamaliro wandale athamangitsidwe
@JasonMailosАй бұрын
😢😢😢😂 ozuka kumandao Eeeeee kusokonezatu kkkkkkk
@cynthiakananji1608Ай бұрын
First to comment
@MasaukoNyirongoАй бұрын
😂😂😂😂😂😂😂 koma zinaz abale kkkkkkk kuthamangitsa masiket mudzi kkkk
@SamKaposa-i5cАй бұрын
😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂Koma abale
@AdenaGuest-g4bАй бұрын
Kuwechetamwangajimbilambali
@AdenaGuest-g4bАй бұрын
Aaaaa Malawi
@ZioneMkangadzulaАй бұрын
utm igawana zida zafikapa angonamizana
@chrisgremu740Ай бұрын
MCP 🔥🔥🔥🔥
@IshmaelIbrahim-s8cАй бұрын
Pathako pako 😂
@ThomasShugaАй бұрын
Wabaya ase kkkkkk@@IshmaelIbrahim-s8c
@ThomasShugaАй бұрын
Iwe fisi eti 😢😮
@user-he4jv1sb1mАй бұрын
Mapazi ako nd mcp yomweyo
@MaryNyirenda-nq3mhАй бұрын
Njoka iwe fiti
@AdenaGuest-g4bАй бұрын
Umakwana
@PociahMackАй бұрын
Kma nkhani ya a pro andiseketsa bwanj😂😂
@PhiriChitaniАй бұрын
Ndinu a Mcp chokani apa mukuyiwala kuti UTM idayamba yokha without mcp
@user-nj5vu8cd5lАй бұрын
Usi ndi munthu yimodzi yomwe mwini wa UTM
@SprianoJekeАй бұрын
Kugawa ndalama Koma ma servants ndee ka salary ka mmanja
@SprianoJekeАй бұрын
As government I think abalalika ndithu
@ChristopherKabangaАй бұрын
vuto amalawi timasapota vitsilu kali ndi ........
@user-gk4nu4xr8rАй бұрын
Of course
@GeorgePhiri-ub2ofАй бұрын
akuononga chipani cha utm ndi mai kaliati ndi azao filex njawala anthu awawa ndithu amaliza chipani cha utm samalani
@RhodaBandah-sh1irАй бұрын
Tafotokozani mmene akuwonongela ....
@MsondaBandaАй бұрын
Ntchindi mulije mu utm
@user-kj7hr2jf1lАй бұрын
Zowona utm yisatenge munthu wakunja
@atupelemposa4786Ай бұрын
😂😂😂
@MayesoKulea-sh8xdАй бұрын
MCP ☑️
@YohaneMotisonАй бұрын
😂😂😂😂😂😂
@PulayaKalakaАй бұрын
Mcp mooootooooooooo
@user-cb5gh9md4iАй бұрын
Kodi ntchentche zikutanipo pamibawapo
@officemoyenda-rj2hzАй бұрын
Si ntchentche
@SamKaposa-i5cАй бұрын
😂😂😂😂😂
@FloraBanda-w7tАй бұрын
😂😂😂😂esh I think ndi lens
@YamikanAbubakary-my4ieАй бұрын
Ambuye mulungu daritsani chipani cha mcp 🇲🇼❤️ 🙏🙏
@ExtratremendouszeusАй бұрын
Ndiwe opembedza mafano Mulungu wa Abraham sangadalitse MCP...siwachisokonezo ngat Chakwera wakoyo...usamutchule Mulungu pachabe...ungaone tsoka
@user-px6kt8rx2pАй бұрын
Ukunama ukadakhumudwa mcp chiyembekezo cha Malawi ambiri
@robertkalima874Ай бұрын
@@user-px6kt8rx2p MCP chipani chafuko
@SamKaposa-i5cАй бұрын
Usatchule dzina lamulungu wako pachabe chome iwe
@MosesNanchingaАй бұрын
Ma comment onsewa bwanji simukukamba za ndalama ai kma UTM sinalakwitse kuchoka ku alliance coz sanalandire ulemu uku ku MCP atizuza ndlmazo mukukanika kugulira mankhwala zipatala bwnj
@ExtratremendouszeusАй бұрын
Abwenza ndalamazi...eni ake akutuwa kusowa sopo...akuoneka a fumbi lokha lokha km ena akuononga mosaopa Mulungu...ayi tiona posachedwapa....nafe tikudikira