KWAGWANJI - KUSANTHULA ZOMWE ZACHITIKA KU UTM 12 July 2024

  Рет қаралды 59,064

HOT 265

HOT 265

26 күн бұрын

Пікірлер: 252
@cassimyusuf6683
@cassimyusuf6683 24 күн бұрын
UTM have made a brilliant decision, simungakhale limodzi ndi anthu ankhaza, okhesa mwazi
@augustMag
@augustMag 24 күн бұрын
Kuganiza mwanzeru UTM palibe chokhalira mu gwirizano pamene mwini wake amene anasayinira kulibe ❤❤❤
@user-ty1vq9lq6w
@user-ty1vq9lq6w 24 күн бұрын
Achita bwino kutulukamo ngati ankaonetsa nkhanza chilima alipompo
@DinesiKafukiza
@DinesiKafukiza 19 күн бұрын
Mbambande zakhalabwinokwambili
@CathrineBizza
@CathrineBizza 24 күн бұрын
Zandikomela izi till pambuyo panu a utm osafooka
@user-im7sc2my4w
@user-im7sc2my4w 24 күн бұрын
Tingopempha kuti amene atenge mpando wa chilima akhale munthu wokhwima nzeru ,kuti ma members asabalalike. Mr Usi ,ndi munthu wanzeru ,mumuwone zomwe apange ,musiyeni amalize term yoyambaonga mwa Mr malemu Chilima Mr Usi akhalabe wa UTM ,mudzandikhulupilila
@GeraldMandindi-ll1zq
@GeraldMandindi-ll1zq 24 күн бұрын
Mwina??
@mkhulukinyata5198
@mkhulukinyata5198 23 күн бұрын
Well done UTM..You have made the good decision for being separate it yourself from the Killer's .. I'm from Zimbabwe but my fore-fathers are Malawian's.. So they've been telling us about how Harsh MCP was on that past years ago ..Mapanga bino kuchokha ku muwanthu wakuyipa yawa ..
@juliusnjerengo2610
@juliusnjerengo2610 23 күн бұрын
The combination of Brian, Jona and Wonder it is same as Aki, Paw Paw and Sam Loko. Very Entertaining.
@user-tf7yi9fp2u
@user-tf7yi9fp2u 24 күн бұрын
UTM is intact and is more united after the death and infact many people have joined UTM but don't just see the NEC only. We are set with votes in 2025. Whatever will come out as UTM we will cling to the principles no matter what come may. Viva UTM. If agreement was respected there would have been cordial working relationship. Why out of the full support, campaigning for you and you choose to ill treat him the whole of four years mmmmm not true of being a true Malawian and a Christian. So what is your conscious telling you today? Remember there is always tmrw. Be good to people as you will soon need them. Viva UTM
@JohnTchirati
@JohnTchirati 24 күн бұрын
MCP imapha kuyamba kare historically, komabe Chakwela is not involved but people around him.
@JohnTchirati
@JohnTchirati 24 күн бұрын
Just the remarks oti ndizaimanso? Pa alliance??????
@StiveKantiki
@StiveKantiki 24 күн бұрын
Banja linali la amayi amagonesedwa nyumba yo dontha lelo amai amwalila mukagulile anawo nyumba adabwa anawo ndi ulemu ukubwelawo amai awo samaziona achitabwino kutuluka l ❤ utm more 🔥
@jacobstvn7995
@jacobstvn7995 24 күн бұрын
Malawi lost a visionary leader because MCP greedy behavior....UTM has moved out, let them enjoy the seats!! As Malawi we have not benefited from this alliance....we have been hurt even more!! So disappointing!!
@AustinChiyembekezo-cx4mz
@AustinChiyembekezo-cx4mz 24 күн бұрын
Very disappointed broz .
@user-fd6oh2vc1c
@user-fd6oh2vc1c 22 күн бұрын
You guys so massive.Wonder u r so wise dear brother….we are proud of you three Big boys.
@JohnChiwaya-ym5me
@JohnChiwaya-ym5me 24 күн бұрын
Ma guys , you have scrutinised the politics well. Ndakunyadilani zeedi
@ThaboMoffia-j7p
@ThaboMoffia-j7p 23 күн бұрын
Big up UTM ndipo zamanganyazo ndizosagwiladi mtima zatha zatha osabwelela mbuyo
@user-zh9kb2sj2i
@user-zh9kb2sj2i 24 күн бұрын
Akanatuluka kalekale chilima sanakamwalila 😢
@user-pv9uk6sc3w
@user-pv9uk6sc3w 24 күн бұрын
Jona pankuku ukunena zoon, Usi si wa UTM, bwanji amakaimila u mp as independent pamene ali mu UTM. Manganya ndi wa MCP basi.
@AlexKaunda-ny2eg
@AlexKaunda-ny2eg 24 күн бұрын
Achita bwino a UTM kusiyana nadzo dzigawenga dza MCP dzamagazi mmanja 😢😢
@ChimwemweBottomani-hc5ju
@ChimwemweBottomani-hc5ju 24 күн бұрын
This is brilliant Utm u made a right decision my advice is...dont let USI to join you hes evil like chakwera...congrats team
@Christophermalema-o8t
@Christophermalema-o8t 24 күн бұрын
Thanks for your constructive decision UTM.You have made a right channel which will attract some people even to join you & vote for you in 2025 elections.May the almighty God paveway for you.
@ahmedwyson4865
@ahmedwyson4865 24 күн бұрын
Apapa nde ma team akumana Ndikamamvera nganizi chaaa ndimachita kumva kukhoma
@VincentKatimba
@VincentKatimba 24 күн бұрын
That's a good distion wamkulu akakhala kuyipa sachita kumuuza amaonera mphepo tiripambuyo panu utm oyeee am I ❤🎉tikulira chilima ife timamukonda kwambiri 😂😂😂😂
@user-lz4kc5ob1t
@user-lz4kc5ob1t 24 күн бұрын
Ndevu zamwayi munthu wanzeru kwambiri
@FrankKambwani
@FrankKambwani 24 күн бұрын
Mtsikana wamzeru amati akafunsilidwa ndi mamuna panjira asanalore amapita kukawafotokozera abale ndi makolo ake cholinga onse adziyendera limodzi ndi mtsikanayo mumaganizo...Apapa vuto ndidaliwona ine pa Usi atasankhidwa kuti akhale vp sadapite kwamakolo(utm)kukakhala nao pansi adangoti ndatola banja dzotsatila dzake makolo akudzamuzimudziwa mamuna uja kuti ndi chimbalangondo it's too late ana akwatilana kale.Usi adzikhweza ndithu.😅😅
@user-ru5xg9qw4x
@user-ru5xg9qw4x 24 күн бұрын
😂😂😂😂
@user-wi8xw9qh7n
@user-wi8xw9qh7n 24 күн бұрын
Sitikuwaopa sitifooka mcp must goooo
@stanleymatolabanda5460
@stanleymatolabanda5460 24 күн бұрын
Ndangwirizana nazo zomwe chipani changa cha UTM chachita ndipo MCP iyiwale zotenga boma ndipo Chewa Muziwona kwanu kwatha akupha inu
@MayorMagombo
@MayorMagombo 24 күн бұрын
You are a liar , mcp is there to stay , you are just waste your time. DPP HAS MANIPULATED YOU SICK PEOPLE.
@lillynhlema9656
@lillynhlema9656 24 күн бұрын
Ndipo achita bwino kwabasi
@batsong.chitseko5903
@batsong.chitseko5903 24 күн бұрын
Usi ngwa MCP. kuchoka mu mgwilizano a UTM achita bwino.
@JohnConar-kq4hi
@JohnConar-kq4hi 24 күн бұрын
That's what I was waiting utm be strong 💪
@Lunnah-b1t
@Lunnah-b1t 24 күн бұрын
Mwayakhula bwino zedi ,wakumva wamva,mumatiyimilira guys love from cp,more fire
@YOMALO.
@YOMALO. 24 күн бұрын
😂guys, you're making the show enjoyable
@ChifundoNinje
@ChifundoNinje 24 күн бұрын
Mwaganiza mwa mzelu a utm km mubwerere kumeneko munachokela
@GospelSoldiers-sr7np
@GospelSoldiers-sr7np 24 күн бұрын
Ndipo chilungamo
@RobertGoliat-gt2qh
@RobertGoliat-gt2qh 24 күн бұрын
Usi ndi wamzeru zakuya and tsiku lina azalankhulanso zamzeru kma UTM yachita bwino kutuluka mumgwirizano
@BittonRashid
@BittonRashid 23 күн бұрын
Koma azibambo tikuyamikileni siyamika mukulowa mmanda mumatilankhulila odana nanu ndiodana ndichilungamo.ndakamba izi chifukwa mbalizonse mumagundako osanva asanve zikomo azibambo ❤
@SandforeKadzamira
@SandforeKadzamira 24 күн бұрын
Brian Banda,sitidzampezanso presenter ngati iwe
@MercyMwale-wc4lr
@MercyMwale-wc4lr 24 күн бұрын
Ndipo live....mmmhamatha owez on point
@JohnConar-kq4hi
@JohnConar-kq4hi 24 күн бұрын
Brian ndimachini
@user-ru5xg9qw4x
@user-ru5xg9qw4x 24 күн бұрын
Ndipo zoona
@user-oj2fy7vx1z
@user-oj2fy7vx1z 22 күн бұрын
Best analysis
@mphatsosadiki4983
@mphatsosadiki4983 24 күн бұрын
Its not too late for UTM kubwelera Kwa make komwe anachokera.......🎉🎉🎉.I would love ma alliance akamachitika azinena zomwe agwilizana .
@TonnyDyton
@TonnyDyton 24 күн бұрын
Likamatha banja or palafini wamunyali amapopedwamo
@user-ml2vw1dc9c
@user-ml2vw1dc9c 24 күн бұрын
Lef nthawi coach adachoka 😢😢😢
@BlessigsChabzola
@BlessigsChabzola 24 күн бұрын
Achita bwino kutuluka chakwera angakhale oyamba kupereka kalata ya upulezidenti kuchipani chawo, osakumbukira zosawakhuza zomwe anasayinira ndi malemu.
@leonardgondwe1470
@leonardgondwe1470 24 күн бұрын
Zoonadi kuti Mr usi wabalalika chifukwa chakuti masapota a utm sakufuna mgwirizano pomwe a usi ndi a vice a boma😊😊😊
@WilsonMagongwa
@WilsonMagongwa 23 күн бұрын
Ngati pali kugawikana ku utm koma ochokawo apanga chiganizo chabwino ndale za a Michael Usi zitipwetekesa akufuna iwo okha ziziwayendela bwino kusiya 20 million people omwe akuvutika.
@Aqiec09
@Aqiec09 19 күн бұрын
Can you pliz build your own better Malawi than criticizing others , I mean all those with meaningless coments , because I see no one Will ever be perfect on this
@user-du9qs4tb6u
@user-du9qs4tb6u 24 күн бұрын
I'm coming to malawi I want to meet you guys well done
@user-zh9kb2sj2i
@user-zh9kb2sj2i 24 күн бұрын
Inu musapusisike mcp ndiyomweinanenakuti zagwilizano sakuzidziwa
@AndersonChiponola
@AndersonChiponola 24 күн бұрын
Koma to be honest utm Ikuyenera kukhala pasi kusankha munthu wa nzeru otherwise chipani chawo chitha kudzakhala chopanda tsogoro because to be honest wisdom ya Chilima simugafanizira Anthu amene angoyankhulawa chifukwa foundation ya utm akudziwa bwino ndi Chilima koma vuto anafa Anthu asanawauze zithu. UDF ngati inatha tsogoreri alipo kuli bwanji UTM leader anamwalira kwa ine is no future ku UTM
@user-oc8nj3or6y
@user-oc8nj3or6y 24 күн бұрын
We're not afraid anymore ndipo we're going to register with the aim of goin to vote ❤on a serious note,,,we cannot fail to survive that's because of Michel Utsi,,,nono let him do what he can
@Cathy-oc7vd
@Cathy-oc7vd 24 күн бұрын
Gwirizano sunathe pano ayi.. unatha 2 years ago, this is just formal panopo
@grantnantchito2919
@grantnantchito2919 24 күн бұрын
To us🎉we had no questions on the Statement made 😢 Don't put us words in our mouths. Decision well made on our behalf
@LeviChakwira
@LeviChakwira 24 күн бұрын
This is a great move❤❤❤❤
@HappyKanyangala-oq1kk
@HappyKanyangala-oq1kk 24 күн бұрын
Amabodxa inu
@SlindileAyanda-sz4zw
@SlindileAyanda-sz4zw 23 күн бұрын
That's great idea utm
@RemaniBanda-u2n
@RemaniBanda-u2n 24 күн бұрын
achita bwino awonezina
@lillynhlema9656
@lillynhlema9656 24 күн бұрын
Koma decision ndaikondq That's part of kumulemekezq chilima after all the torture he went through with mcp
@InnocentEdasi
@InnocentEdasi 24 күн бұрын
UTM osafooka🔥🔥🔥. , mzimu wa Chilima wuse mumtendele
@MadaKanene
@MadaKanene 24 күн бұрын
Komatu band yagawana zida vinyo atantha kale 😮,,, I think is too late 🕐,,,, when justice delays become injustice
@user-un6qv6sj3h
@user-un6qv6sj3h 24 күн бұрын
Achita bwino ndithu ❤❤❤
@ManninLongwe
@ManninLongwe 24 күн бұрын
Ngati mwatelemu mwathesa mugwilizano amene azayimila usogoleri kumbali yanu ya utm yomwe azakhala pa baluti ndindani?
@user-nj5vu8cd5l
@user-nj5vu8cd5l 24 күн бұрын
Usi is good guy, he is not far behavior like Chilima. UTM members don't destroy party because of losing Chilima. Once you will start pointing figure someone in a party you will realize tomorrow when party is going to an end
@user-tl9xg4fg9x
@user-tl9xg4fg9x 24 күн бұрын
Zachitabwino mubwelele kumene munachoka kuti tichose chigawengachi
@SamuelAntone-mz6nq
@SamuelAntone-mz6nq 23 күн бұрын
Zakhala bwino tidakalila ife malilo wanthu panopa
@user-vm7iz6oz6r
@user-vm7iz6oz6r 24 күн бұрын
Zilibwino kwambilili mmm sha,,,wakwiya ndi fit😂😂
@samalanimacdonald9373
@samalanimacdonald9373 23 күн бұрын
Ndenvu zamwayi koma abanda akulakwila chiyan
@VanaKhama
@VanaKhama 24 күн бұрын
Amene anathawqpo a yufi ngati ine sangadabwe
@user-dg5pc6rz1b
@user-dg5pc6rz1b 24 күн бұрын
Mcp yatha koma vuto ndilakuti libela mavoti mfunso nkumati inu azipani mukukonzekela chani kuti nchitidwe obela mavoti usadzachitike?
@ProsperBanda-ju2mq
@ProsperBanda-ju2mq 24 күн бұрын
Mcp singathe Koma chipani chathuchi ndichimene chingathe
@brainsmkumbwa6267
@brainsmkumbwa6267 24 күн бұрын
Iam over the moon for the decision made by U.T.M,zaunetsa kuti Chilima wasiya anthu oganiza moyenelera
@HarrisMathew-ve5ib
@HarrisMathew-ve5ib 24 күн бұрын
Bravo 👍
@allahslave7177
@allahslave7177 24 күн бұрын
Usi ali ngati munthu wa banja amene ali ndi chibwenzi panja ndipo nachipanga value chibwenzi pamaso pa banja ndiye ankhoswe abanjawo they come to know , thats alibe intereste mwa Usi a Utm
@omarmkwanda2184
@omarmkwanda2184 23 күн бұрын
Micheal usi ndi njoka mu udzu, alibe mtsogolo
@user-co3wr3rn4h
@user-co3wr3rn4h 24 күн бұрын
Ife tilinganga pambuyo pa utm phee
@NosiphoMazwai
@NosiphoMazwai 24 күн бұрын
Live from capetown
@ziggympandakwaya3054
@ziggympandakwaya3054 24 күн бұрын
Keep the fire burning UTM
@madalitsochiumia755
@madalitsochiumia755 24 күн бұрын
That's great decision UTM
@FrancisDominic-w1s
@FrancisDominic-w1s 24 күн бұрын
Ausi ngati sasamara azafera kusata
@dondamissonchdziwe3958
@dondamissonchdziwe3958 24 күн бұрын
Achoka mochedwa atawaphera Kale Chilima,kuimba chiminingo Njobvu zaononga zapita Kale
@PatrickMulangala-os4by
@PatrickMulangala-os4by 24 күн бұрын
Ndevu za mwayi wadya mbali yake
@GeraldMandindi-ll1zq
@GeraldMandindi-ll1zq 24 күн бұрын
Mr usi akusamala ntchito, osati zachipani
@BlessingMkonda
@BlessingMkonda 22 күн бұрын
Sats true words
@user-vm7iz6oz6r
@user-vm7iz6oz6r 24 күн бұрын
Muziyagana kuno guys mukuopa?
@PeterDandaula-ci5un
@PeterDandaula-ci5un 24 күн бұрын
Komabe atuluka nkhwangwa ili mmutu kale
@fumumdolo7341
@fumumdolo7341 24 күн бұрын
UTM has made the right political decision. Deputy President was supposed to lead to put the house in order. The guy lacks stamina to judge Malawians mind. USI can't afford to unite UTM it's lost opportunity, he could have demonstrated in presence of his boss. Very tricky situation to USI and MCP.
@ChimwemweBottomani-hc5ju
@ChimwemweBottomani-hc5ju 24 күн бұрын
Exactly
@user-du9qs4tb6u
@user-du9qs4tb6u 24 күн бұрын
A mcp ndi akupha Chakwela ndiwe munthu oipa machende ako
@gracemkandawire8769
@gracemkandawire8769 24 күн бұрын
Usi ndi Tambwali,,nanji wakhalila Mpando wonona
@user-du9qs4tb6u
@user-du9qs4tb6u 24 күн бұрын
Ausi si wa utm ndi anthu usana
@GreyMtungama
@GreyMtungama 24 күн бұрын
Umakwana wonder kikikik ma usher omweo
@LawrentNyasulu
@LawrentNyasulu 24 күн бұрын
Koma apamkuku banja latsopabo anthu amagona 4pm akuti usiku umafupika
@user-cf9yz3ei5o
@user-cf9yz3ei5o 24 күн бұрын
Bravo Kalitta asiyeni
@LinlyNakombe
@LinlyNakombe 23 күн бұрын
Good decision
@GodfreyWhayo-hh1dm
@GodfreyWhayo-hh1dm 24 күн бұрын
A MCP adakwera pachulu ndikulengeza kuti wina afune Kaya asafune iwowo adzapambana chisankho ndi 70% . Kodi kapena anaconda kale mwala ?
@sylviamsonthe
@sylviamsonthe 24 күн бұрын
Good move❤UTM
@gracemkandawire8769
@gracemkandawire8769 24 күн бұрын
It's too early for questions
@user-un6qv6sj3h
@user-un6qv6sj3h 24 күн бұрын
Usi sadakapange consult anzake a UTM kuti andisankha udindo ndiye titani? Koma adangoti mutu gwaaa kukalumbira uyu ngwa MCP basi
@user-zh9kb2sj2i
@user-zh9kb2sj2i 24 күн бұрын
Gyz mwayankhulamawu amphamvu kwambili kumapetoku mcp ikudzimva kuti inafikapo anthuose atulukawa anagwilantchitoqambili maka chilima
@user-xx4jb9se3z
@user-xx4jb9se3z 24 күн бұрын
Utm my vote
@lukepeter8290
@lukepeter8290 22 күн бұрын
A banda mwati anatani 😅
@francisvisage2705
@francisvisage2705 24 күн бұрын
Body language ya Ndevu Zamwayi can tell Kuti anadyako Chibanzi from MCP
@beinhardkausiwa7107
@beinhardkausiwa7107 24 күн бұрын
Wonder amaonetsera kuti iyeyo ndiwa mcp
@princekaponda
@princekaponda 24 күн бұрын
Panja amati azayakhula zambiri pa 19 ... Nde mafutso tizafuse zimenezo , azatiyakhaa
@onester4946
@onester4946 24 күн бұрын
It's so sad to hear that in 2024 mcp is doing what it did during kamuzu era
@user-uv5rf4zt5q
@user-uv5rf4zt5q 24 күн бұрын
It's a right decision if they moved out early chilima could be alive today.
@user-rp9wy6rd1q
@user-rp9wy6rd1q 24 күн бұрын
Achita bwino 🎉
@Aqiec09
@Aqiec09 18 күн бұрын
Chilima was the only perfect leader to utm party enanu ndiye worse wat makes you better than the other political leaders, the problem is that you guys simukufuna usi kudzakhala acting president because of your stiggy minds trust God on this he might guide you better than akhungu okhaokha kutsongorerana njila , that's means your don't love Malawi but being proud to your self intrest
@AndersonNason
@AndersonNason 24 күн бұрын
Aiaiaia kodi et
@gracemkandawire8769
@gracemkandawire8769 24 күн бұрын
Palibe chokanila ,,iwe wonder,,,chipanichi chikulondoledwa ndi anthu ,,anachita bwino kukana mafuso
@IssaJohn-cb8vn
@IssaJohn-cb8vn 24 күн бұрын
Amwene awa ali pakatiwa sindimawavesesa zokamba zawo serious
@SheenahMwalabu-iz3pr
@SheenahMwalabu-iz3pr 24 күн бұрын
Ndipo ngati ndinu nokha kkk amamuikilanji kaya. Apapa ikanabeba akanakhalapo a Chunga not Jonayo aaa. Amangodziwa kusokosa ndipo muli fundolesi 😂 mudzitimverako plz a times we love you but uyoyo wavala blueyo apume mu programyi. Ndinakupemphaninso to bring Mr Kapito John, Asowa and muli mutu mmenemuja 😂
Pleased the disabled person! #shorts
00:43
Dimon Markov
Рет қаралды 31 МЛН
Как бесплатно замутить iphone 15 pro max
00:59
ЖЕЛЕЗНЫЙ КОРОЛЬ
Рет қаралды 8 МЛН
لااا! هذه البرتقالة مزعجة جدًا #قصير
00:15
One More Arabic
Рет қаралды 13 МЛН
MISS CIRCLE STUDENTS BULLY ME!
00:12
Andreas Eskander
Рет қаралды 20 МЛН
THE  MALAWI  COURT....TAMVERANI IZI ..
24:40
Jimmy
Рет қаралды 20 М.
#SABCNews AM Headlines | 12 July 2024
1:28
SABC News
Рет қаралды 4,9 М.
MWAMBO OYATSA MA KENDULO KU CHILIMBA.🙌🙌🔥🔥🔥
19:58
MZIKA ZOKHUZIDWA NDI ATOLANKHANI 🔥🔥🔥🙌🙌
22:50
JOHN KAPITO WATOPA NAYE CHAKWERA. Ityoke ityoke Osabisa mau // PART 1
33:23
Chikonzero chakaita kuti Baba Harare vatendeuke
45:03
STAR FM LIVE
Рет қаралды 85 М.
EXCLUSIVE INTERVIEW WITH BON KALINDO
59:52
Zodiak Malawi
Рет қаралды 62 М.
Pleased the disabled person! #shorts
00:43
Dimon Markov
Рет қаралды 31 МЛН