KWAGWANJI / U KUSANKHIDWA KWA MICHAEL USI

  Рет қаралды 48,217

HOT 265

HOT 265

8 күн бұрын

Пікірлер: 89
@blessiousphiri3109
@blessiousphiri3109 6 күн бұрын
Kumakhala bwino ndi anthu muma office mu a Malawi chonde. Big up Banda, Chunga and Msiska
@PaulChaleka-lb4vx
@PaulChaleka-lb4vx 6 күн бұрын
Koma mcp mene yachitira treat chilima according to agreement manganya asamale mcp ndi yakupha and dishonest
@KennedyChitunda
@KennedyChitunda 6 күн бұрын
Dziko lalowa chibwana mpaka manganya kukhala vp,,,,ur not serious
@AlfredNazombe-me2ly
@AlfredNazombe-me2ly 6 күн бұрын
Komtu azibambo inu musamakonde kumutchula Mulungu munkhani zandale bashop usatchule dzina la Yehova Mulungu lako pachapabe bashop bashop
@blessingsmunthali9202
@blessingsmunthali9202 6 күн бұрын
Mwadziwa bwanj kut akumtchula pachabe??
@AlfredNazombe-me2ly
@AlfredNazombe-me2ly 6 күн бұрын
Munthu amene akumuchemelelayo is good at dramer but ....... Something is wrong
@clintonhodda9830
@clintonhodda9830 6 күн бұрын
Zibwana zenizeni ndi dziko maliro sanathe koma asankha munthu
@wisdom20mkango49
@wisdom20mkango49 5 күн бұрын
😂😂😂 Boy this is the country not family thing..... There is a constitution that runs not people feelings... Show maturity before you utter nonsense
@AminaPhiri-pp9tw
@AminaPhiri-pp9tw 6 күн бұрын
Muzikagona azimayi a eni autsi muli ndi mbili yonyasa kwambili inu
@emmammatsa1284
@emmammatsa1284 2 күн бұрын
Mr Ndevu zamwai timati, ❤Mdyanyemba amaiwala koma mtaya makoko saiwala chifukwa amazaloza pomwe anataya osati Mdyamakoko chitukwa makoko a nyemba sitidya ayi
@SahijidNgwindima-qd3dk
@SahijidNgwindima-qd3dk 6 күн бұрын
Koma mummuuze manganya akumbuke .mama sikono........chibwana. ......
@IssacMateyo
@IssacMateyo 6 күн бұрын
Palibe ndipo ine ndiye ndakodwa kwambili ausi vice 🔥🔥
@AlfredNazombe-me2ly
@AlfredNazombe-me2ly 6 күн бұрын
Kod awa atatu ndiamene ali oziwa kwambiri amangokhala pamenepa bwanji
@IssacMateyo
@IssacMateyo 6 күн бұрын
Koma palakwika pangono chifukwa thawi yachepa kwambili sikale lija aikidwa malilo lija ngati panafunika kudikila kaye
@user-er2jv3nn4g
@user-er2jv3nn4g 6 күн бұрын
Malamulo amati asankhe kwa 7 day's
@user-vu4cz1mt4f
@user-vu4cz1mt4f 6 күн бұрын
Tili nchisoni chanji,anagawana zovala zanga yesu anatero
@user-xx4jb9se3z
@user-xx4jb9se3z 6 күн бұрын
Wakupha uyu chilima adali amfanaoganiza bho .akutha Mau sakudziwa ZA mawa a usi mau awawa adzakutembenukilani soon.ife tli ku ma stand
@user-ve2ts3yr2n
@user-ve2ts3yr2n 6 күн бұрын
Ndipo mukhalisepo atumwi inu.....aaaa ma compassion aanthu mpaka zaka peletu ati sanasayinile.....
@AlfredNazombe-me2ly
@AlfredNazombe-me2ly 6 күн бұрын
They think that this TTV it's belong to them kom kumakhala bwn ndi anzanu zatsogolo lamunth amaziwa ndi Mulungu
@corretabanda7685
@corretabanda7685 6 күн бұрын
Ine sanandipeze speech yawo nsaname
@user-xc2zm9bu1i
@user-xc2zm9bu1i 6 күн бұрын
We are waiting incompetent inquiry Poor leadership Not following the democratic values Remember next year is just around the corner Things are not working on the ground Guys we need a servant leader
@EsnartMartin
@EsnartMartin 6 күн бұрын
Ma guy inuyo simuli serious ndale zakulowani
@user-wx1jt5fd2j
@user-wx1jt5fd2j 6 күн бұрын
Ndi andale ochepa amavomereza kuti chiweluzo chiliko ndi chifukwa chake samasamala za anthu Ena ngakhale akubvutika bora iwo zawo zikuyenda koma mulungu ndi oweluza olungama
@user-co3wr3rn4h
@user-co3wr3rn4h 6 күн бұрын
Manganya ndi ka yudasi kakafupi kwambili fiti kapha, zake chilima
@yusufbakali
@yusufbakali 5 күн бұрын
❤ Manganya ndiyekhayo maso a malawi
@josephhchimpepa8753
@josephhchimpepa8753 6 күн бұрын
That's a good discussion! Those who have ears have heard something!
@chitanibenito1109
@chitanibenito1109 5 күн бұрын
Yaaa aghothiiii akhutukunve malo moti azitengera mphunziro pa zinzawo.
@clintonhodda9830
@clintonhodda9830 6 күн бұрын
Kodi malamulo adziko amachokera kuti ndipo amapangidwa ndi anthu akuti?
@ykzt
@ykzt 5 күн бұрын
Walowa dziko litavunda kale palibe chingasithe apa😢😢
@blessingkamanga1781
@blessingkamanga1781 6 күн бұрын
Very educative discussion
@blessiousphiri3109
@blessiousphiri3109 6 күн бұрын
Suziwa zamawa yes. Fact to the point ❤
@MustafaAbdullah-pb5zv
@MustafaAbdullah-pb5zv 5 күн бұрын
Powerful message
@user-nw6ie3xx8b
@user-nw6ie3xx8b 6 күн бұрын
Wishing you the best , help chakwera he is the man of God
@MichaelWilliamsNyirenda
@MichaelWilliamsNyirenda 6 күн бұрын
😅 killing man
@AlfredNazombe-me2ly
@AlfredNazombe-me2ly 6 күн бұрын
Zomwe lankhula sizingatheke muone azangoti pasakhale owasokoneza nduna zina zidangowelamila pansi muona when it comes to action let's wait
@user-oj2jr6kf9c
@user-oj2jr6kf9c 6 күн бұрын
Unawomaso eti!!?
@user-bl6km6kx7n
@user-bl6km6kx7n 5 күн бұрын
Mabwana chonde kuyamikila tiyamikile koma kod chikalidwe chathu monga amalawi chimati chani munthu akafa plz timakukulupililani
@ChrissySasenga
@ChrissySasenga 5 күн бұрын
Nice kma
@Geraldmkwewu
@Geraldmkwewu 6 күн бұрын
Chisiru manganya yudasi atiphera chilima ndichakwera achina nkunkuyu zikhare ngoma osatchura mulungu zautsiru zimenezo manganya Mesa amafuna udindo kuyiwara kt ose ndichakwera kt awupeze udindowo ndichilima tikulira chilima wanthu lfe 😢
@80kiloputodaboacena9
@80kiloputodaboacena9 6 күн бұрын
Mphaka Manganya kula vice president
@ClementJacob-sd8lf
@ClementJacob-sd8lf 3 күн бұрын
Malawians group of discussion without solutions doy you think you will change Malawi for the situations just wait and see
@ClementJacob-sd8lf
@ClementJacob-sd8lf 3 күн бұрын
Wina president akachoka mtengo kumakwela liti zizasitha mpake tife tose zopusa
@ClementJacob-sd8lf
@ClementJacob-sd8lf 3 күн бұрын
Sugar k200 Lifeboy soap k50 nthochi 20 t, zibwelele kwa d.r banda ngati sizitelo nde kutinamizako ife sitifuna ndale
@FortuneNkhoma-bc9hh
@FortuneNkhoma-bc9hh Күн бұрын
Kharedwe ndichuma
@AllanSanena
@AllanSanena 5 күн бұрын
Zosakoma dzikoli😢😢
@blessiousphiri3109
@blessiousphiri3109 6 күн бұрын
Mudya nyemba amayiwala, koma mudya makoko sayiwala
@PaulChaleka-lb4vx
@PaulChaleka-lb4vx 6 күн бұрын
Mulungu mutimenyele nkhondo taluza chilima munthu yemwe anthu adamukhulupilira
@rabeccamasebo6261
@rabeccamasebo6261 5 күн бұрын
Life is in stages
@dymonleven7571
@dymonleven7571 6 күн бұрын
Abambo asikono kumeneko zalowa chibwana ndithu 😊
@wypatrickdakankhoma9655
@wypatrickdakankhoma9655 6 күн бұрын
Mwakwera m c p😢
@homeremedys3748
@homeremedys3748 6 күн бұрын
Akufuna Aphe Born Kalindo then APM, chenjerani nayoni boma ili zinali kokambilana dzulo
@PaulChaleka-lb4vx
@PaulChaleka-lb4vx 6 күн бұрын
Chilima anali munthu osunga nthawi ndipo tidzamusowa
@MaggieCement
@MaggieCement 5 күн бұрын
Kwathu kosauka ine olo wagalimoto kulibe
@CalvinThabang
@CalvinThabang 5 күн бұрын
Tikuferanji amaLawi pomwe Manganya ali m'bwaLo??!!
@LovemoreTaulo-yj3pj
@LovemoreTaulo-yj3pj 6 күн бұрын
Times mcp tv mbuyomu inali times ya bwino km pano anawadyesa Baz awa
@wonganichakakanyirenda3299
@wonganichakakanyirenda3299 6 күн бұрын
Inu inu abrayan musazafee
@RobertNyaude
@RobertNyaude 6 күн бұрын
Tizikhala bwino ndi anthu🤣🤣
@SamukLungu-zg7fl
@SamukLungu-zg7fl 6 күн бұрын
Ausi kaya ndi usi wamutengo utiwo koma mumbari yopha chirima arimomo koma nawo apitabe basi
@maulanaallie6194
@maulanaallie6194 5 күн бұрын
Umbuli
@ZungeniBanet
@ZungeniBanet 6 күн бұрын
Inu chupiti
@AlexKaunda-ny2eg
@AlexKaunda-ny2eg 6 күн бұрын
Agalu atatuwaso atinyasa machende anu
@adibwekumz3085
@adibwekumz3085 4 күн бұрын
That's illegal. Kupusa
@Yungjoe786
@Yungjoe786 6 күн бұрын
Pachoka nzako palidi Malo...
@PaulChaleka-lb4vx
@PaulChaleka-lb4vx 6 күн бұрын
Koma mcp tikuchotsa 2025 yatililitsa koopsa
@user-gs7wc3nx3q
@user-gs7wc3nx3q 6 күн бұрын
Iya mapazi anu
@RABSONSIKELO
@RABSONSIKELO 6 күн бұрын
Moyodi ndi pelete
@polesanamakwenda6932
@polesanamakwenda6932 6 күн бұрын
Kkkkkk
@user-nf3ik3ff6y
@user-nf3ik3ff6y 6 күн бұрын
Dziko latha
@ChrissySasenga
@ChrissySasenga 5 күн бұрын
Chilima anali dolo simukunama
@ykzt
@ykzt 5 күн бұрын
Kod pali chodyadira pamenepo anthu inu
@MAYGOSPELALBUMSChawawa
@MAYGOSPELALBUMSChawawa 6 күн бұрын
Don't take malawian as stupid because the president has got powers to make decisions like on this situation to change the decision because you can see when did we did the barial for Chilima and today you're busy enjoying with the post of vice president shamm on you mr. President and your vice president
@user-mv4us2yx1o
@user-mv4us2yx1o 6 күн бұрын
Zopusa zeni- zeni,manganya mzomwe amafuna amamuyenda mmapazi chilima,mmmmmm ,dziko lamalawi larowa chibwana ,mpana Usi?mzimu wachilima komwe uliko ukunva chisoni
@PatrickMailos
@PatrickMailos 6 күн бұрын
I disappointed MCP
@user-nj5vu8cd5l
@user-nj5vu8cd5l 6 күн бұрын
Vote for USI ❤❤❤
@AlfredNazombe-me2ly
@AlfredNazombe-me2ly 6 күн бұрын
I hate nyana these guys bcoz even they isolate Jona Pankuku every program they put Jona at last sit why and they use to cat him word on the mouth when ever he is speaking just wash 5 kwagwanji and hot current u will agree with me
@IssaJohn-cb8vn
@IssaJohn-cb8vn 6 күн бұрын
This stupid radio this days we must stop listening and trust
@FrankKambwani
@FrankKambwani 6 күн бұрын
MCP yamagazi yanuyo ngakhale itachita zabwino komabe mbiri yake ndiyamagazi basi
@SaidiMbawa-st6bj
@SaidiMbawa-st6bj 6 күн бұрын
Dpp so ndi yamagazi ndiye musathe mawu boma ndi Boma
@tasmania527
@tasmania527 6 күн бұрын
Ndipo DPP yinathiphela abale athu 20 ku Mzuzu mu 2011. Yinapha Chasowa, Njaunju, ndi ma membala a UTM ku Lilongwe; kodi amenewo si magazi a anthu? Kodi anthu onsewa ophedwa ndi DPP anali nkhumba? Nde musamalankhule kuti MCP yamagazi ngati muli ndi umboni- DPP umboni ulipo.
@MaryNyirenda-nq3mh
@MaryNyirenda-nq3mh 6 күн бұрын
Kod anthu mulimbalibe ya MCP yomweyo uhuuuu bola zipani zina osat MCP yakupha
@tasmania527
@tasmania527 6 күн бұрын
Za zii. I would rather support MCP than family parties of killers like DPP or UDF
@kingsleyhopematchaya5184
@kingsleyhopematchaya5184 6 күн бұрын
Nanga popeza yakhala mcp yokha chipani cha phavu nanga muthu wa zaka 92 angaganize zulu zinatha tiyenazoni bola mukavote katatu aliyese koma kamodzi aaa mcp ikudutsa
@AlexAlick-bx9by
@AlexAlick-bx9by 6 күн бұрын
Times it's mcp TV
@MOOSANOWAH184
@MOOSANOWAH184 6 күн бұрын
Kuyambila liti?
@JafaliAkimu-ll1bf
@JafaliAkimu-ll1bf 6 күн бұрын
boma lolamula ndi chigawenga
@IssacMateyo
@IssacMateyo 6 күн бұрын
Palibe ndipo ine ndiye ndakodwa kwambili ausi vice 🔥🔥
@IssacMateyo
@IssacMateyo 6 күн бұрын
Palibe ndipo ine ndiye ndakodwa kwambili ausi vice 🔥🔥
DRIEMO  - TRAILER (Official Music Video)
3:03
Driemo
Рет қаралды 5 МЛН
Khóa ly biệt
01:00
Đào Nguyễn Ánh - Hữu Hưng
Рет қаралды 20 МЛН
Always be more smart #shorts
00:32
Jin and Hattie
Рет қаралды 34 МЛН
Alat Seru Penolong untuk Mimpi Indah Bayi!
00:31
Let's GLOW! Indonesian
Рет қаралды 8 МЛН
Khó thế mà cũng làm được || How did the police do that? #shorts
01:00
Maloto A Bon Kalindo (Part 2) - Bon Kalindo
14:17
Nyasa VoiceBox
Рет қаралды 71 М.
KUCHIPANI CHA UTM CHADABWITSA ANTHU🤔🤔
49:16
HOT 265
Рет қаралды 69 М.
KAFUKUFUKU PA IMFA YA ACHILIMA
30:18
Jimmy
Рет қаралды 80 М.
GWEDE-GWEDE PA 27 June 2024🙌🙌🙌
25:27
HOT 265
Рет қаралды 16 М.
Bingu from Perth & Asia Part 8 - Press Questions 1
13:21
Nkhani Digest
Рет қаралды 219 М.
Khóa ly biệt
01:00
Đào Nguyễn Ánh - Hữu Hưng
Рет қаралды 20 МЛН