LIMPOPO FM WITH COMRADE NTANYIWA USIKU wathawu

  Рет қаралды 15,565

Club Junta

Club Junta

18 күн бұрын

Пікірлер: 83
@zimmekapachika6784
@zimmekapachika6784 16 күн бұрын
Mr Chikangawa Chakwera Bp yakwera kale kuti muulura chani 😅😅😅😂😂😂😂yomweyo galu iwe
@MikeKanyaza-bm5tp
@MikeKanyaza-bm5tp 16 күн бұрын
Osamasowa antanyiwa please 😊
@GanizaniKamvazaana
@GanizaniKamvazaana 16 күн бұрын
Koma ndaseka ngati zabwino 😂😂😂 athu onsewo akaphedwa nde iwo adzawina zisakho Kom hahahaaaaa chakwera akunama kwambiri kumwamba kukanena kuti kwatha ndi kwatha basi paribeso zoti apha muthu wina a ntanyiwa dzikoli silachakwera ndalama sizingamupindulire komaso paribe zoti anga gure chipani paribe yemwe afuna achoke komaso akaliyati sangalore mudzina layesu ndikuti patibe zoti muthu anga gure chipani awo akalandira ndalama ndizawo za kunyumba kwao and olo apatse ndalama kakiyati olo adzalandira koma chilungamo chisitha chimakhalabe chilungamo ndinaonera esau ndi abere choipa chitsata mwini MLUNGU WATHU SALEPHERA
@DavidJackson-ox4xm
@DavidJackson-ox4xm 16 күн бұрын
I support Limpopo FM with Comrade Mtanyiwa God bless you all the time.
@esaMoha-dm4kj
@esaMoha-dm4kj 16 күн бұрын
ose amene ankufunna kuphedwa mulungu salolla mashall Allah bless you always
@JosephHill-fy1bb
@JosephHill-fy1bb 16 күн бұрын
We are here already comrade ✌️
@MaxwellumbiriLumbiri
@MaxwellumbiriLumbiri 16 күн бұрын
Zakwanitsa tate akuona zonse
@MaxwellumbiriLumbiri
@MaxwellumbiriLumbiri 16 күн бұрын
Yehova akuona chilichonse afa yekha
@meganabigail-ye7fw
@meganabigail-ye7fw 16 күн бұрын
Sitiopa wokupha thupi koma timaopa mulungu amene amapha thupi ndi mzimu. Ondikumbila dzenje agwelamo yekha. Mulungu wa Daniel, shadreck, mishel and abdenego will protect onse amene mayina awo Ali pa list.
@VaseleMsiska
@VaseleMsiska 16 күн бұрын
Koma kukhala anthu Ku Malawi. Koma chakwelà azatha ngati ma curtain.
@zimmekapachika6784
@zimmekapachika6784 16 күн бұрын
Good morning, welcome back tinakusowani tinayamba kudandaura
@SamukLungu-zg7fl
@SamukLungu-zg7fl 16 күн бұрын
Ndikamava kanyimboko ndiye ndimasangarara ndimazdziwa kuti chirungamo chirimunjira
@amoschataika7440
@amoschataika7440 16 күн бұрын
The best Radio station in the world. Big up Comrade
@simonpaul6567
@simonpaul6567 16 күн бұрын
I ❤ this program
@user-ul1fb4yn5o
@user-ul1fb4yn5o 16 күн бұрын
I salute Comrade ntanyiwa,, ndiye titani Comrade amalawi tiyen titengen gawo tipemphere kwambiri
@CostanceLalli
@CostanceLalli 13 күн бұрын
Loud n clear from Johannesburg
@user-pl2lj6mh1z
@user-pl2lj6mh1z 16 күн бұрын
Koma dziko lathu tinalozedwa bas zoona kumuopa chakwela kamuthu kamodzi tiyen tipange ngat ku Kenya please zausilu zikuchitikazi
@user-ht7vs3dp2u
@user-ht7vs3dp2u 16 күн бұрын
Pemphelo rathu ndichida chomwe timangonjesera adani zenje akuwakumbira athu onseo agweramo onse akupereka mayina awathu osarakwa imfa akunenayo atamwalire ndiwo 2025 isanafike mulungu akuona
@AnusaNkhoma
@AnusaNkhoma 16 күн бұрын
Waying'alura kuno mtanyiwa
@INNOCENTMOFOLO-io8tg
@INNOCENTMOFOLO-io8tg 16 күн бұрын
Ntanyiwa wadzuka bwanji kumeneko ifetu tilibwino ndithu tiye nazoni
@DaitonKabila
@DaitonKabila 16 күн бұрын
Comrade am 100% support u always ing'alure fadah
@modestamhango7737
@modestamhango7737 16 күн бұрын
Angozinamiza anthu onsewa Mulungu sangalore kuti aphedwe.
@user-ul1fb4yn5o
@user-ul1fb4yn5o 16 күн бұрын
Muzina la yesu christu achakwera kungopha modzi muziona ndithuuu😭😭😭😭
@MustafaAbdullah-pb5zv
@MustafaAbdullah-pb5zv 16 күн бұрын
Amalawi kumudziko tadzukani mumchotse chakwelayo......dziko silake
@AbdullahBnp-l8m
@AbdullahBnp-l8m 16 күн бұрын
long live Mtanyiwa here in capetown i support you❤
@sparkdymon3429
@sparkdymon3429 16 күн бұрын
Atchela kumawa nkhangazaona anyanayo
@MebleNgulinga-hi6rg
@MebleNgulinga-hi6rg 16 күн бұрын
Oh Lord have mercy on us Malawians Tipulumutseni ambuyeeeee ............Mbuzi ikakondwa kwambiriiii amalonda alipafupi la 40 likudzaaaaaaaa list mwayikayo ikhala yanuuuuu anthu akupha amagazi m'manja inu
@SydneySibande-z6k
@SydneySibande-z6k 16 күн бұрын
Long liveNtanyiwa
@JamesDaud-jz7uq
@JamesDaud-jz7uq 16 күн бұрын
You are our head lamp Mr Mntanyinya tipempha mayiko ena atithandize kuchotsa president okuphayu
@louismagongwa
@louismagongwa 16 күн бұрын
😂😂😂😂😂 nde mcp itsala yokhatu nanga anthu osewo akawapha ku opposition kudzakhala ndan mcp muzitenge bwino zithuzi vuto mwakhalitsa padzuwa muli kotsutsa😅😅😅😅😅😅😅😅
@sulleahmnyimbili1362
@sulleahmnyimbili1362 16 күн бұрын
Lord have Mercy
@user-iv4dj1pi3b
@user-iv4dj1pi3b 16 күн бұрын
Comrade ntanyiwa ..great man ft kalindooooo
@PetroMatias
@PetroMatias 16 күн бұрын
Antanyiwa nlipo abale osamasowa chonchi
@CharlesmakveliNyirenda
@CharlesmakveliNyirenda 16 күн бұрын
Iwe chakwela Mano kuyipa ngati nyemba ya pa nyini ya Monica wako uyo usatibowe ife
@Nelsonmatenda
@Nelsonmatenda 16 күн бұрын
We love you comrade ..tell us more
@user-wl4nd7ic1s
@user-wl4nd7ic1s 16 күн бұрын
GOD bress u Mr mtanyiwahhh!!
@LouisKanje
@LouisKanje 16 күн бұрын
Okhesa mwazi yehova sakondwera naye olo nyama ikatero Mulungu amapereka Chicano paizo
@augustinechibbalazi8897
@augustinechibbalazi8897 16 күн бұрын
My gracious heavenly Father have mercy on Malawians
@user-zr7wk4oq2x
@user-zr7wk4oq2x 16 күн бұрын
We're always with you buddy Ntanyiwa.♥️🔥🔥
@user-hg5oj3ko1o
@user-hg5oj3ko1o 16 күн бұрын
Iiiii ndiye atipha tonsetu
@esaMoha-dm4kj
@esaMoha-dm4kj 16 күн бұрын
Mtanyiwwa ulemu wanuw mulungu adalise wina aliyese astaguffllal yha Allah thallah brother
@HallimaMakwinja
@HallimaMakwinja 16 күн бұрын
Achakwera ku state house atawako posachedwapa
@MariamJaffali
@MariamJaffali 16 күн бұрын
Ndipo galu ameneyo siomuchula kuti mr iyayi chakwera akufuna amalawi atani 😂😂😂
@Extratremendouszeus
@Extratremendouszeus 16 күн бұрын
Am just a Malawian but my president is Traore..on my DP😅😅😅
@originalblack100
@originalblack100 16 күн бұрын
aziwombere yekha lazalo wa ku kasiya ndi a zinzake onse, kuyambila zikhale, chimwendo kukunyu ndi agututu a thakati onse a congress. BRR brrrrr pha pha pha, comarde mumakwana boss.🤣🤣🤣🤣🤣🤣
@mathewsmdzanja3276
@mathewsmdzanja3276 16 күн бұрын
I salute you comrade!
@MerryWayson
@MerryWayson 16 күн бұрын
Timakunyadilani Mr Mtanyiwa koma za anthu ogwidwa pa Bedbrig Ili pat naosotu akanapita Maliro kwao kumalawi iya
@GraceZumazuma
@GraceZumazuma 13 күн бұрын
Koma mulipo a Ntanyiwa, mulibwanji kumeneko
@HusseinMoffatt-mi1fl
@HusseinMoffatt-mi1fl 16 күн бұрын
Amtanyiwa bwanji Kodi odio sikumveka bwinotu
@kondwaniwhite2871
@kondwaniwhite2871 16 күн бұрын
Nice 👍 nndinakusowani
@CharlesPhiri-ds1rk
@CharlesPhiri-ds1rk 16 күн бұрын
Mmmmmmm ayi zagawana ku mitunduzo ayi....usatinamize ingonena zoooyenera kunenazo....timakutsat Ra mwachidwi...km zotigawanisazo sitilora...tonse nda Malawi ndipo palibe adzatigawanisa
@Musa1828-l5d
@Musa1828-l5d 16 күн бұрын
Mr Chakwera pamtumbo panu ndinthu
@AminahMussah
@AminahMussah 16 күн бұрын
anthu onsewo awakwanitsa koma Mulungu wake waliyenseyu aaaa
@ZionekaMember
@ZionekaMember 16 күн бұрын
Mukamachedwa kupanga post timakhala ndi nkhawa Kut chachitika chan
@LeonardMhone-cg1tk
@LeonardMhone-cg1tk 16 күн бұрын
Apa bet bridge aja awafinye especially waku MALAWI athane naye ndi opusa
@kamwazabonomali825
@kamwazabonomali825 16 күн бұрын
Komatu kulimbana ndi aNtanyiwa kuzipusisa ndithu. Awa ndi akatundu omangidwa ndizitsulo. Mbambande.
@DONNEXKhama-bk1gy
@DONNEXKhama-bk1gy 16 күн бұрын
Nsembe yomwe inapelekedwa zaka zapitazo ya ufulu chakwera waipangisa expire akufuna mwazi wina otchuluka
@leonardjika2100
@leonardjika2100 16 күн бұрын
WHEN YOU ARE PLAYING THE MUSIC OR OTHER VOICES WE CAN NOT HEAR CLEAR PLS TELL YOUR TEACHINIAN
@user-mv8vy3ht3n
@user-mv8vy3ht3n 16 күн бұрын
God is able
@user-wo2kh4xe8q
@user-wo2kh4xe8q 16 күн бұрын
futi yomwe akufuna aphere azawo apita ndi iwoo mulungu simunthu
@user-lj7lm6ly7z
@user-lj7lm6ly7z 16 күн бұрын
Palibe so kuphedwa apa Inu ambuye akukutetezerani a ntanyiwa ndi azinzanu onse timakuikizani mmapephero
16 күн бұрын
Okupha nayeso azafa... palibe kuopa mcp ndi azitsogoreli ikagwere
@user-yu4np2wq4s
@user-yu4np2wq4s 16 күн бұрын
Zosatheka athu APHA Aja sanakwane BaiBulo Linati okumba zenje agwelemo yekha ndiiiiiiithu amene watenga gawo lokupha athu amenewa agweramo okhaaaaa ambuye invani simunawalenge athu Kuti azuzike paziko pano inu mukule Ife tichepe
@user-ny3it3jp9l
@user-ny3it3jp9l 16 күн бұрын
Lipopo support ❤ 💙
@user-ny3it3jp9l
@user-ny3it3jp9l 16 күн бұрын
Lipopo ❤ ❤ ❤ ❤ ❤ ❤ ❤ ❤ ❤ ❤ ❤ ❤ ❤ ❤❤❤❤
@cynthiakananji1608
@cynthiakananji1608 16 күн бұрын
Muwamve Mai kaliyati mmene anayankhulira kumaliro a LUCIUS BANDA kumuyamikira president kut ankamuthandiza Lucius,pomwe Lucius wavutika kwambiri mmoyowu.i will never trust politicians.kulira konsekuja,lero akufuna alemerere pa imfa ya chilima.Amai awawa apapa ndiye azionongera mbiri .Akufuna awanamize aMalawi.
@AnaffSayamika-uh6vg
@AnaffSayamika-uh6vg 16 күн бұрын
💥💥💥💥
@edmorswalley6663
@edmorswalley6663 16 күн бұрын
Mulungu sichejemu auzeni
@PatrickMtira
@PatrickMtira 16 күн бұрын
Tinakusowani Boss
@user-bw2cv9sd7x
@user-bw2cv9sd7x 16 күн бұрын
a comrade yobu 13;13 yakhulani mosaopa
@VanessaGwangwa
@VanessaGwangwa 16 күн бұрын
❤❤
@AminAbbass-xc4qk
@AminAbbass-xc4qk 16 күн бұрын
🎉🎉🎉🎉🎉🎉
@PetroMatias
@PetroMatias 16 күн бұрын
👍👍👍👍🤝🤝🤝🤝👍
@user-hj5oq5jm9v
@user-hj5oq5jm9v 16 күн бұрын
Ing'alureni fadah
@user-oq5rg5mz7q
@user-oq5rg5mz7q 16 күн бұрын
Zosatheka osewo kafu olo atalimbikila bwanji
@ArnoldBinali
@ArnoldBinali 16 күн бұрын
Koma chakwela eeee
@ChiefJustin-cl8jl
@ChiefJustin-cl8jl 16 күн бұрын
Nthatha za njaladi
@LouisKanje
@LouisKanje 16 күн бұрын
Chilango
@ZionekaMember
@ZionekaMember 16 күн бұрын
Koma Chakwera zoti kuli Court la ICC lomwe limathana ndi ma President aku Africa akuziziwa Mr President becareful kunali ma President a mphavu kunjaku koma anaphedwa enaso anali okondedwa ndi anthu awo osati inu
@Uncle_B265
@Uncle_B265 16 күн бұрын
Komatuu tili pa ululu eeeeee
@hanifahmponda8711
@hanifahmponda8711 16 күн бұрын
MCP or chakwela si mulungu agalu amenewa atikwana dzene 2025 kwatalika dzedi asanephe anthu ofunika MOTI PAKANGOFA MUNTHU WINATSO CHILIMA NDI ANTHU 8 AJA AKWANA chifukwa ife amalawi sitimakhulupila kuti MCP yokupha timati yakele yija iyi ya wong"ono ung'onu KOMA PANO ALIYETSE WAWONA YEKHA KUTI MCP YAMAGADZI NDINTHU
@mipeacemakermw9501
@mipeacemakermw9501 16 күн бұрын
Wina watukwana chakwera uku 😂😂kzfaq.info/get/bejne/jbh0nrRp2MWXZJ8.htmlsi=r_3Qm9tNpQwXfR0D
Happy 4th of July 😂
00:12
Alyssa's Ways
Рет қаралды 66 МЛН
I Can't Believe We Did This...
00:38
Stokes Twins
Рет қаралды 129 МЛН
Cat Corn?! 🙀 #cat #cute #catlover
00:54
Stocat
Рет қаралды 16 МЛН
마시멜로우로 체감되는 요즘 물가
00:20
진영민yeongmin
Рет қаралды 32 МЛН
He doesn’t like illusions
0:17
V.A. show / Магика
Рет қаралды 12 МЛН
When an RV meets a zombie outside #rv
0:21
campingWorld
Рет қаралды 24 МЛН
Задержи дыхание дольше всех!
0:42
Аришнев
Рет қаралды 1,7 МЛН
Waka Waka 😁 #funnyshorts #rianashow
0:14
RianaShow
Рет қаралды 3,7 МЛН