Mr Chikangawa Chakwera Bp yakwera kale kuti muulura chani 😅😅😅😂😂😂😂yomweyo galu iwe
@MikeKanyaza-bm5tp16 күн бұрын
Osamasowa antanyiwa please 😊
@GanizaniKamvazaana16 күн бұрын
Koma ndaseka ngati zabwino 😂😂😂 athu onsewo akaphedwa nde iwo adzawina zisakho Kom hahahaaaaa chakwera akunama kwambiri kumwamba kukanena kuti kwatha ndi kwatha basi paribeso zoti apha muthu wina a ntanyiwa dzikoli silachakwera ndalama sizingamupindulire komaso paribe zoti anga gure chipani paribe yemwe afuna achoke komaso akaliyati sangalore mudzina layesu ndikuti patibe zoti muthu anga gure chipani awo akalandira ndalama ndizawo za kunyumba kwao and olo apatse ndalama kakiyati olo adzalandira koma chilungamo chisitha chimakhalabe chilungamo ndinaonera esau ndi abere choipa chitsata mwini MLUNGU WATHU SALEPHERA
@DavidJackson-ox4xm16 күн бұрын
I support Limpopo FM with Comrade Mtanyiwa God bless you all the time.
@esaMoha-dm4kj16 күн бұрын
ose amene ankufunna kuphedwa mulungu salolla mashall Allah bless you always
@JosephHill-fy1bb16 күн бұрын
We are here already comrade ✌️
@MaxwellumbiriLumbiri16 күн бұрын
Zakwanitsa tate akuona zonse
@MaxwellumbiriLumbiri16 күн бұрын
Yehova akuona chilichonse afa yekha
@meganabigail-ye7fw16 күн бұрын
Sitiopa wokupha thupi koma timaopa mulungu amene amapha thupi ndi mzimu. Ondikumbila dzenje agwelamo yekha. Mulungu wa Daniel, shadreck, mishel and abdenego will protect onse amene mayina awo Ali pa list.
@VaseleMsiska16 күн бұрын
Koma kukhala anthu Ku Malawi. Koma chakwelà azatha ngati ma curtain.
@zimmekapachika678416 күн бұрын
Good morning, welcome back tinakusowani tinayamba kudandaura
long live Mtanyiwa here in capetown i support you❤
@sparkdymon342916 күн бұрын
Atchela kumawa nkhangazaona anyanayo
@MebleNgulinga-hi6rg16 күн бұрын
Oh Lord have mercy on us Malawians Tipulumutseni ambuyeeeee ............Mbuzi ikakondwa kwambiriiii amalonda alipafupi la 40 likudzaaaaaaaa list mwayikayo ikhala yanuuuuu anthu akupha amagazi m'manja inu
@SydneySibande-z6k16 күн бұрын
Long liveNtanyiwa
@JamesDaud-jz7uq16 күн бұрын
You are our head lamp Mr Mntanyinya tipempha mayiko ena atithandize kuchotsa president okuphayu
@louismagongwa16 күн бұрын
😂😂😂😂😂 nde mcp itsala yokhatu nanga anthu osewo akawapha ku opposition kudzakhala ndan mcp muzitenge bwino zithuzi vuto mwakhalitsa padzuwa muli kotsutsa😅😅😅😅😅😅😅😅
@sulleahmnyimbili136216 күн бұрын
Lord have Mercy
@user-iv4dj1pi3b16 күн бұрын
Comrade ntanyiwa ..great man ft kalindooooo
@PetroMatias16 күн бұрын
Antanyiwa nlipo abale osamasowa chonchi
@CharlesmakveliNyirenda16 күн бұрын
Iwe chakwela Mano kuyipa ngati nyemba ya pa nyini ya Monica wako uyo usatibowe ife
Am just a Malawian but my president is Traore..on my DP😅😅😅
@originalblack10016 күн бұрын
aziwombere yekha lazalo wa ku kasiya ndi a zinzake onse, kuyambila zikhale, chimwendo kukunyu ndi agututu a thakati onse a congress. BRR brrrrr pha pha pha, comarde mumakwana boss.🤣🤣🤣🤣🤣🤣
@mathewsmdzanja327616 күн бұрын
I salute you comrade!
@MerryWayson16 күн бұрын
Timakunyadilani Mr Mtanyiwa koma za anthu ogwidwa pa Bedbrig Ili pat naosotu akanapita Maliro kwao kumalawi iya
@GraceZumazuma13 күн бұрын
Koma mulipo a Ntanyiwa, mulibwanji kumeneko
@HusseinMoffatt-mi1fl16 күн бұрын
Amtanyiwa bwanji Kodi odio sikumveka bwinotu
@kondwaniwhite287116 күн бұрын
Nice 👍 nndinakusowani
@CharlesPhiri-ds1rk16 күн бұрын
Mmmmmmm ayi zagawana ku mitunduzo ayi....usatinamize ingonena zoooyenera kunenazo....timakutsat Ra mwachidwi...km zotigawanisazo sitilora...tonse nda Malawi ndipo palibe adzatigawanisa
@Musa1828-l5d16 күн бұрын
Mr Chakwera pamtumbo panu ndinthu
@AminahMussah16 күн бұрын
anthu onsewo awakwanitsa koma Mulungu wake waliyenseyu aaaa
@ZionekaMember16 күн бұрын
Mukamachedwa kupanga post timakhala ndi nkhawa Kut chachitika chan
@LeonardMhone-cg1tk16 күн бұрын
Apa bet bridge aja awafinye especially waku MALAWI athane naye ndi opusa
@kamwazabonomali82516 күн бұрын
Komatu kulimbana ndi aNtanyiwa kuzipusisa ndithu. Awa ndi akatundu omangidwa ndizitsulo. Mbambande.
Muwamve Mai kaliyati mmene anayankhulira kumaliro a LUCIUS BANDA kumuyamikira president kut ankamuthandiza Lucius,pomwe Lucius wavutika kwambiri mmoyowu.i will never trust politicians.kulira konsekuja,lero akufuna alemerere pa imfa ya chilima.Amai awawa apapa ndiye azionongera mbiri .Akufuna awanamize aMalawi.
@AnaffSayamika-uh6vg16 күн бұрын
💥💥💥💥
@edmorswalley666316 күн бұрын
Mulungu sichejemu auzeni
@PatrickMtira16 күн бұрын
Tinakusowani Boss
@user-bw2cv9sd7x16 күн бұрын
a comrade yobu 13;13 yakhulani mosaopa
@VanessaGwangwa16 күн бұрын
❤❤
@AminAbbass-xc4qk16 күн бұрын
🎉🎉🎉🎉🎉🎉
@PetroMatias16 күн бұрын
👍👍👍👍🤝🤝🤝🤝👍
@user-hj5oq5jm9v16 күн бұрын
Ing'alureni fadah
@user-oq5rg5mz7q16 күн бұрын
Zosatheka osewo kafu olo atalimbikila bwanji
@ArnoldBinali16 күн бұрын
Koma chakwela eeee
@ChiefJustin-cl8jl16 күн бұрын
Nthatha za njaladi
@LouisKanje16 күн бұрын
Chilango
@ZionekaMember16 күн бұрын
Koma Chakwera zoti kuli Court la ICC lomwe limathana ndi ma President aku Africa akuziziwa Mr President becareful kunali ma President a mphavu kunjaku koma anaphedwa enaso anali okondedwa ndi anthu awo osati inu
@Uncle_B26516 күн бұрын
Komatuu tili pa ululu eeeeee
@hanifahmponda871116 күн бұрын
MCP or chakwela si mulungu agalu amenewa atikwana dzene 2025 kwatalika dzedi asanephe anthu ofunika MOTI PAKANGOFA MUNTHU WINATSO CHILIMA NDI ANTHU 8 AJA AKWANA chifukwa ife amalawi sitimakhulupila kuti MCP yokupha timati yakele yija iyi ya wong"ono ung'onu KOMA PANO ALIYETSE WAWONA YEKHA KUTI MCP YAMAGADZI NDINTHU