No video

Bon Kalindo Ndi Guru lake la Malawi first ayankhura izi pamene anapangitsa press conference lero

  Рет қаралды 38,771

Makosana

Makosana

Күн бұрын

Пікірлер: 172
@user-mg5yy5hk9t
@user-mg5yy5hk9t Ай бұрын
Anganga Alula malawi fist member all the way from mangochi mamatiyimilira mr big man keept up mangochi yosaopayo
@Moses51
@Moses51 Ай бұрын
The Dc bon kalindo keep up update 💪💪🇲🇼🇲🇼💯 osawopa
@VungaQueen
@VungaQueen Ай бұрын
Boni Kalindo munthu wotiyimilira 🔥🔥🔥
@user-ez8uk7py8n
@user-ez8uk7py8n Ай бұрын
That is true it needs all Malawian to vote as long as he/ she is Malawian Mr president keep continue loving your poor people abd our country Malawi proud of you thanks
@user-eh1mg3ww6d
@user-eh1mg3ww6d Ай бұрын
Ndipo athu inuyo tchito mukuigwila mulungu azikusungani ndi moyo maka Mr boni kalindo simutopa mwamangidwa kambili mbili mukanakhala wina bwezi mutatisiya ife athu osauka sikuti ndinu Muthu ovutika ayi koma mumasiya pogona pabwino zakudya zabwino kukagona Malo onyasa chifukwa Cha ife aphawi kuzipeleka m,sembe pokhapo mulungu adzikudalitsani ❤❤
@RiyemaDomybusiness
@RiyemaDomybusiness Ай бұрын
Exactly 💯💯 bon amatiyimirila ampwawi
@user-eh1mg3ww6d
@user-eh1mg3ww6d Ай бұрын
@@RiyemaDomybusiness sure tidziwapephelela ndithu athu amenewa
@esaMoha-dm4kj
@esaMoha-dm4kj Ай бұрын
I respect your Mr nkalindo together with Malawian fest and the cautrry everyone DC is so powerful as well and you are always welcome to our team of Malawi wholld my Allah bless you always about the what happened with Malawian
@esaMoha-dm4kj
@esaMoha-dm4kj Ай бұрын
I am a Malawi but now I'm in the sauth Africa estan about working on
@WysonJalamu
@WysonJalamu Ай бұрын
Big up the DC osatopa, osafowoka, osawopa malawi ndi wathu uyu, tili limodzi pa nsewu basi.
@user-ml4bl2ll2g
@user-ml4bl2ll2g Ай бұрын
Please please ife TIKUFUNA ufulu wathu wovota a MCP asauchotse ponamizira ma id, aliyense akuyenera kukavota popanda id
@Franklifo2217
@Franklifo2217 Ай бұрын
Nzelu mulibe enanu! Anthu omwe mumalephelesa malawi kutukuka🙌
@hudycorex1893
@hudycorex1893 Ай бұрын
Inu amzeru kwambiri?​@@Franklifo2217
@SamKaposa-i5c
@SamKaposa-i5c Ай бұрын
Anzeru ndinuyo? ​@@Franklifo2217
@MussaHassani-zg1hm
@MussaHassani-zg1hm Ай бұрын
This is our president kalindo thanks so much for your help Malawias
@DavieBinzih
@DavieBinzih Ай бұрын
More fire mr kalindo we proudly of you keept up we love you
@WezzieChimuzi-ek7bk
@WezzieChimuzi-ek7bk Ай бұрын
Good job my people Ambuye azikutetezelani ndi mwanzi wawo nthawi zonse ..
@chippakaribafox2865
@chippakaribafox2865 Ай бұрын
Lets presure dem evo!....aluta continua!
@YousufMpunga
@YousufMpunga Ай бұрын
Ndine Yusuf wakumangochi kmnso amalawi amene Ali kumaiko akunja apasidwe mwai wovota kuchokera kunja konko kumene ali
@patrickmacheso5062
@patrickmacheso5062 Ай бұрын
That's true, we need to vote and choose the President that we want not this Manyaka Government, but the problem is Akazembe athu sathandiza or kuwapempha kuti atipatse mwayi ovota.
@FrankSpison-o7o
@FrankSpison-o7o Ай бұрын
The Dccccccc Booooooooon kalindo inu nde anthu oti mzika zamalawi tizikupemphererani kwambili 🙏
@AnussaAlli
@AnussaAlli Ай бұрын
Big up the DC Bon kalindo continue timakunyadlan❤❤❤❤❤❤🎉🎉
@ChristopherMadulira
@ChristopherMadulira Ай бұрын
Congugulations Mr DC ntchito mukugwila anthu inu only God bless you ❤❤❤❤❤
@user-uf4db7im7d
@user-uf4db7im7d Ай бұрын
Every malawian should be in a possession of ID, If the NRB is failing to reach all malawians for ID registration, you should expect Malawi to be on fire, because voting results will not be accepted, People have rights to vote for who they want not rigging.
@jogechawa6192
@jogechawa6192 Ай бұрын
Bon Kalindo and malawi first our hope basi
@esaMoha-dm4kj
@esaMoha-dm4kj Ай бұрын
I respect your nkalindo bisid ashankwela and everyone else has been in the path of mcp I don't respect anyone anymore because the people who keep and keeling Malawian people 2025 mashall Allah bless you nkalindo 😮😮😮
@harrisonlowheat6569
@harrisonlowheat6569 Ай бұрын
My president
@user-uf4db7im7d
@user-uf4db7im7d Ай бұрын
This government must go
@user-wi9pe2hz7e
@user-wi9pe2hz7e Ай бұрын
Good move Malawi First ❤
@NellieKabvina
@NellieKabvina Ай бұрын
Pa ziphatsopo ndie zikudabwitsa zikupezeka kuti anthu ambiri akumadziwa tsiku lokuti akumaliza kupanga ma ID,,,sakulengeza tsiku loyamba anthu ambiri akudandaula
@user-gs7wc3nx3q
@user-gs7wc3nx3q Ай бұрын
yaa wa mcp ngati akunyasidwa ni boni karindo asavere khani zake ayi chonde ife anthu osauka tiyeni tizimuvera boni koma uzayime iwe boni tizakuvotere
@RemaniNkhoma
@RemaniNkhoma Ай бұрын
boni karindo tingopita mawa bwanji pa sewu kuti agaru awa tiwakhawurise
@SamKaposa-i5c
@SamKaposa-i5c Ай бұрын
Viva malawi first Richard mphepo umadziwa kuyankhula more fire dc
@FatimanickisJaffer
@FatimanickisJaffer Ай бұрын
Wa mcp ngt born kalindo amakunyasa usamaver nkhan Zak iwey ndy opanda zelu ife tikufuna dziko libwerer ngt kal osat mukumakambo shem on you 😢😢😢😢
@KhalidwePentani-c6q
@KhalidwePentani-c6q Ай бұрын
Iwe ndamene ukava ngat ine mbuz izi za duuu
@OdettaLowrence
@OdettaLowrence Ай бұрын
Ulemu wanu Mr Born 🙏🙏🙏🙏
@amoschataika7440
@amoschataika7440 Ай бұрын
Well done guys kpt up
@user-uv5rf4zt5q
@user-uv5rf4zt5q Ай бұрын
Malawi first all the best u are representing poor people. To be honest Malawi is the poorest country in the world our leaders are selfish we are going backwards.
@BacklinebwanaliBwanali
@BacklinebwanaliBwanali Ай бұрын
Akupatsen moyo was utali
@dawsonwaya4722
@dawsonwaya4722 Ай бұрын
Za ziiiiiiiii munthu unalephera kuimirira constituency ndiye ukati amalawi osauka aaaa zangokuvutani Moya, .
@robenallie6985
@robenallie6985 Ай бұрын
Ndizako zimenezo dc number 1
@FatimaAyami
@FatimaAyami Ай бұрын
Vuto ndi bomalo iyeyo amangopanga imprement
@Samu-q3z
@Samu-q3z Ай бұрын
Boni karido ndikatundu
@YohaneChitapini
@YohaneChitapini Ай бұрын
Mumakwana ndipo ndinu nokha boss ndagwada ndikumvesela
@user-dq9oe8sp8k
@user-dq9oe8sp8k Ай бұрын
Ifetu though tilibe ma ID kma tikazavota Angoona kuzinamidza agwapewa Fireeee the DC❤
@AndrewNyondo-ut3gk
@AndrewNyondo-ut3gk Ай бұрын
King David bon kalindo the DC❤
@AlidWidon
@AlidWidon Ай бұрын
Wosawopa bon kalindo tili limodxi 💪💪💪🔥🔥🔥👆👆
@Okalekale
@Okalekale 26 күн бұрын
Tikufuna tidziwe kuti ndi ndani amapanga sponsor gulu lanuli Mr.Kalindo?.The nation should know if you claim to advocate for transparence.
@MercyJohnsonkanchure
@MercyJohnsonkanchure Ай бұрын
Mr Kalindo Mulungu azikupansani zeru zakuya ngati Solomon ❤
@MikeKoloko
@MikeKoloko Ай бұрын
Mumatiimilira, big up
@ShariffAbdul-m9t
@ShariffAbdul-m9t Ай бұрын
I salute you
@RanaQari-py4bd
@RanaQari-py4bd Ай бұрын
Mumakwana guys we love you all the time 🙏🙏🙏🔥🔥🔥🔥
@usherjamson174
@usherjamson174 Ай бұрын
Mulungu azikhala namu guy's 💪💪
@HusseinAdamLidezo
@HusseinAdamLidezo Ай бұрын
Never give up guys let's see what happens
@lastonkandiyado4526
@lastonkandiyado4526 Ай бұрын
Respect 🎉🎉🎉
@isabelmartin7567
@isabelmartin7567 Ай бұрын
The DC ❤
@MuhammedNtaba
@MuhammedNtaba Ай бұрын
❤❤❤ The DC
@ImanRashidi-so4oo
@ImanRashidi-so4oo Ай бұрын
Congratulations mr DC
@KeftonChimaliro
@KeftonChimaliro Ай бұрын
Iyayi zonsezitu akupangazi akufuna ndalama mtambo samachitaso chocho anango kuwapatsa zochita ndikungokhala duuu osayakhulaso amalawi anthuwo ndi amodzi Lucia's. Anayimba kale
@Lazarus-qo1sl
@Lazarus-qo1sl Ай бұрын
Pick up guys chilungamo ndimwano
@patrickmacheso5062
@patrickmacheso5062 Ай бұрын
Ndimayesa ngati mukhala kumbuyo kwa a name anu kkkkkkkk let's fight together, this country is belongs to all Malawians not MCP only.
@RanaQari-py4bd
@RanaQari-py4bd Ай бұрын
🙏🙏🙏🙏🙏 Thnx good work
@GodisoneNoel
@GodisoneNoel Ай бұрын
Asirikali achirendo muzikorathu zichepe mr DC
@user-bd5kw8oq1r
@user-bd5kw8oq1r Ай бұрын
Akumangeni ngati mwaphwanya malamulo dala mbuli
@kenmasta
@kenmasta Ай бұрын
Ndiye mmene akumamumangamo ndiye akumamupeza ndi milandu yanji,,,,..ndaletu zisakusokonezeni mchimwene andale amabwera amapita koma Malawi adzakhala yemweyu ndiye let's love Malawi.
@user-bd5kw8oq1r
@user-bd5kw8oq1r Ай бұрын
@@kenmasta mwanena nokha awa asiyeni koma akanalankhula zinthu zambili ndi za against popeza ine ndinapanga nawo compain ndiye sanandipatse udindo awona, zimenezo ndi zabodza,chikuwawe sichimanga dziko amwe awa ndi a ndale musokonekera sayamika ndi ankhwidzi amafuna zawo ziwayendere kalindo akudya makobidi inu mukudya nawo 🤗🤗 ayi so bola yesu
@user-dy5bj9ck5e
@user-dy5bj9ck5e Ай бұрын
The DCCC
@CostanceLalli
@CostanceLalli Ай бұрын
Good move bafethu salute you
@GetrudeBanda-sd1yf
@GetrudeBanda-sd1yf Ай бұрын
Only GOd Bless you DC
@SueWahna
@SueWahna Ай бұрын
Big up Malawi first 💪💪
@TiyamikeMakande
@TiyamikeMakande 29 күн бұрын
Mumatiuankhulira ndinu bwana ,mutiyankhulireso za ndrama za masiye ku Capital hill Chaka chino nchachitatu ndrama sakutipatsa tikuvutika ndi ana
@HarrisonMangani
@HarrisonMangani Ай бұрын
They need to address those issues other wise Mmmmm panunkha mphira
@PempheroMoleni
@PempheroMoleni Ай бұрын
Firr the DC
@EliasMcray
@EliasMcray Ай бұрын
Go go ahead
@frankiechasokoneza5802
@frankiechasokoneza5802 Ай бұрын
Point of correction not guru lake koma Born kalindo ndi guru la Malawi 🇲🇼 first
@nelsonmhango7515
@nelsonmhango7515 Ай бұрын
Inu ndi king
@gracetjomane-jj3ib
@gracetjomane-jj3ib Ай бұрын
Kutundu uyu the DC❤❤❤❤❤❤
@YohaneChitapini
@YohaneChitapini Ай бұрын
Guys inu musazafe mulungu azikudalisani
@user-tw2zf7bj3e
@user-tw2zf7bj3e Ай бұрын
❤❤❤❤ guys
@AnockyDavidd
@AnockyDavidd Ай бұрын
Congratulations to all
@Malambia
@Malambia Ай бұрын
Mr kalindo ulemu wanu
@KhalidwePentani-c6q
@KhalidwePentani-c6q Ай бұрын
Zopanda ntchito izo akalindo mumangofuna udindo ngat mungakwanitse kutumikila dziko aaaa zawumbuli
@Mervic-vm8eo
@Mervic-vm8eo Ай бұрын
Wa MCP pamtu...
@InnocentKavalo
@InnocentKavalo Ай бұрын
Zoona big umakwana dc
@ambeweburton
@ambeweburton Ай бұрын
Timenyeleni nkhondo please mulungu imvani kulira kwathu
@PetroMatias
@PetroMatias Ай бұрын
Amarawig fct muri nbi mfunbo zabwini timakuyamikirani
@Fridayasani
@Fridayasani Ай бұрын
Osawopha Bon kalindo tikukupembela kwamulungu Kuti anzikala nawe kwina kulikonse komwe udziyenda
@ntandokazindzwana3083
@ntandokazindzwana3083 Ай бұрын
Fire fire tili pa mbuso pa malawi oyambirira
@ritchardchakuma5725
@ritchardchakuma5725 Ай бұрын
Apomwayikwanisa maiko enasaziwa Chichewa pakufunika ayaluke mbavazi 💯🔥🔥🔥🔥🔥
@Samu-q3z
@Samu-q3z Ай бұрын
Zikomo boni karindo umatiyimilila big Kom amalawi sitimayamika
@chikoko-uj2tt
@chikoko-uj2tt Ай бұрын
Salute 🫡 The DC
@user-dy4gc2hr5e
@user-dy4gc2hr5e Ай бұрын
Good move
@HajaSande
@HajaSande Ай бұрын
Zikomo kwambiri umawona patali
@AgnessChiwalo
@AgnessChiwalo Ай бұрын
Your good man bon
@DavidJackson-ox4xm
@DavidJackson-ox4xm Ай бұрын
The DC'S mwana woooopsa kwambiri chilungamo chiyende ngat madzi.
@AgnessChiwalo
@AgnessChiwalo Ай бұрын
❤❤❤ good news
@JafaliAjusa-zg2xi
@JafaliAjusa-zg2xi Ай бұрын
Respect Mr
@user-mh7cc8up4i
@user-mh7cc8up4i Ай бұрын
❤❤❤💯💯🔥🔥🔥
@LukaJaulanchirwa
@LukaJaulanchirwa Ай бұрын
You people you thinking harder that is good Diction thank chakwera is not thinking
@SolokingChimzy-yt7dj
@SolokingChimzy-yt7dj Ай бұрын
Following with all my chidwi
@shephardlonex3371
@shephardlonex3371 Ай бұрын
Booooooooni kalindo
@Mervic-vm8eo
@Mervic-vm8eo Ай бұрын
Go konko bwana DC❤
@kurhikhoza8298
@kurhikhoza8298 Ай бұрын
Tipiya pa sewu akapanda kuyakha
@sarahmphande6108
@sarahmphande6108 Ай бұрын
I'm sure, the government you will grant our request
@PreciousKARINGANIZA
@PreciousKARINGANIZA Ай бұрын
Tilikomweko
@shephardlonex3371
@shephardlonex3371 Ай бұрын
Munene kuti ife ngati A Dpp
@MaryNgola
@MaryNgola Ай бұрын
Mmene wafikira Malawi alipodi amene akumamuona uyu kt akupanga zolakwika? Iweyotu wa MCP nkana akukubowa
@JoshuaNyirongo
@JoshuaNyirongo Ай бұрын
Go konko..
@PiusMpando
@PiusMpando Ай бұрын
Tikukunyadilani kuno
@DaglasUseni
@DaglasUseni Ай бұрын
Well
@kashmirmohakashmirmoha8659
@kashmirmohakashmirmoha8659 Ай бұрын
Ulemu wanu DC😊😊
@dondamissonchdziwe3958
@dondamissonchdziwe3958 Ай бұрын
Wina Aliyense amavota kumene adabwadwira Ndipo amfumu amadziwa Wanthu wao,apapa wina Ali yense azavota amene ali mbadwa ya Malawi zama I'D za chani?zopusa
@ShadreckChimaimba-l9y
@ShadreckChimaimba-l9y Ай бұрын
Osatopa big
@user-ru6fc3qy5n
@user-ru6fc3qy5n Ай бұрын
Zilibwino kwambili osaopa
Blue Food VS Red Food Emoji Mukbang
00:33
MOOMOO STUDIO [무무 스튜디오]
Рет қаралды 17 МЛН
This Dumbbell Is Impossible To Lift!
01:00
Stokes Twins
Рет қаралды 36 МЛН
Prank vs Prank #shorts
00:28
Mr DegrEE
Рет қаралды 10 МЛН
Magic trick 🪄😁
00:13
Andrey Grechka
Рет қаралды 55 МЛН
Venâncio Mondlane Retorna a Moçambique: Jovens Celebram com Euforia
14:35
Malema addresses Gauteng EFF members
1:25:51
SABC News
Рет қаралды 268 М.
WATSEKA (Tribute to SIR SOLDIER LUCIUS BANDA) video.Oneraniko zimenezi
4:19
Blue Food VS Red Food Emoji Mukbang
00:33
MOOMOO STUDIO [무무 스튜디오]
Рет қаралды 17 МЛН