Akatundu awa!!!!! He is so courageous!!! speaking with no Fear,, he sounds like Chilima in his Bond of courageous.
@lloydjeremiah2250Ай бұрын
eeee kma this man is so courageous
@MasausoMsiska-rz3idАй бұрын
Munthu koma uyu speaking without fear....Big up Mr chihana
@user-fz3gu2ez1o29 күн бұрын
Eeeeee Koma SKC 😭😭😭😭 Ine imfa iyiyi.. Imandiwawa.. eeeeee
@JesusChristFollowers-ez9zuАй бұрын
Mr. Chihana is man of his word, ndipo zikupanga prove that he is the son of his father. Amenewa ndi amene anathema ndi kamuzu, apa chakwera akuchoka, ndavomereza anthufe sitimafa koma maonekedwe athu ndi amene amasintha
@arnoldkaikenkayangeАй бұрын
Afford my vote
@iconiclife681125 күн бұрын
So powerful bwana We need this Energy in our country honestly achinyamata ambiri akufuna ngati iziiii
@kusekejereАй бұрын
SKC has gone leaving a message that malawi is the land with possibilities but the problem are the leaders. What a humble guy. Rest well sir
@jonasmunthali848Ай бұрын
I didn't know dis guy can talk lyk dis🙌🙌🙌🙌🙌🔥🔥🔥🔥🔥
@hopesatoАй бұрын
Anthu akwiya mkoz
@jonasmunthali848Ай бұрын
@@hopesato ndaonaso🙌
@magex88721 күн бұрын
Koma ndiye.big up chihana❤
@luciatembo-e4fАй бұрын
Straight wise proud of you chihana🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥
@AgnessMzengoАй бұрын
Wise leader...... Tell them
@amandamoyo7156Ай бұрын
God protect Mr Chihana....we love u
@HopeJaffariАй бұрын
Ramaphosa wanthu waku Malawi 💪💪
@NoluvuyoMatutuАй бұрын
😂😂😂😂even me I thought like that ndtaona pic yake poyamba
@memoryziyaya2593Ай бұрын
true ..they are resembling very 😅
@fostersimbi8820Ай бұрын
Didn't know this guy amayankhula mwamphamvu chonchi ❤🔥
@lyiemaxАй бұрын
Powerful, proud of you Honourable Chihana
@FelixChimsNyirendaАй бұрын
Tell them the truth don't be afraid 😨 GOD will guide and protect you, we relay behind your your back.
@HappyAbyssinianCat-xt2bmАй бұрын
Km ndi zoona chakwera popanda chilima sukanawina galu iwe chakwera unapanga ndiwolotse ndikakutafune galu iwe chakwera dzimaso dzako unatiphera ngoni wathu
Ndiye chilima popanda chakwera adakhala vp tisamalakhule mbali imodzi chilima tu adali vp from 2014 up to 2024 ineyo ndimafuna nditadziwa zomwe adapanga kapena ankadikila adzakhale President kuti inuyo mudzayamve kusangalala to me i don't know thanks God ineyo ndimadziyimila from nyumba ya maudzu to mansion bra inuyo dikuilani chiloma wina kuti moyo wanu udzasithe
Zomvetsatu chisoni kwambiri. Ndikanakonda a ku Banja akanaketsa Zopusa zimenezo. Chidziwika ndi chakuti SKC ndi CHIHANA were not Friends. Ngati zomwe akunenazo ndi zoona tione umboni wake. Atiuze nthawi, tsiku komanso Audio or ma message olemba. Musaiwale kuti ndi yomweyinso anabweretsa nkhani yonama ku Nyumba ya Malamulo atafunsidwa za umboni anakanika kupereka. SKC awuza bwanji iyeyo kusiya kuuza utm members?. CHIHANA ndi ONAMA kwambiri
RIP CHILIMA....😢😢. Auzeni live live..akapukuu ..nduna zokuda mbuuuuuuu
@MirriamKambaleАй бұрын
Chakwerayutu si m'busa anthunu mangosokoneza munthu uja ndi nthakati. Mfwiti ya tyala iliye na mzeru ingaphepese yai after those words pray hard angakusowetse
@WilliamNyirenda-xq4kmАй бұрын
Viphalileni bwana viwanthu voina mitu ivi you are my vote
@MadalitsoTamayenda-ez5pjАй бұрын
Powerful voice
@user-dh8ho2qt4h24 күн бұрын
❤❤❤ love you dad. We all cry our vice president chilima.😢😢😢
@ClaraMkandawire-d2k29 күн бұрын
Kuyankhula koma ukuuu aaaaseeeee👊😂
@tumpalechihana5073Ай бұрын
Our own leader
@louisbonongwe8537Ай бұрын
Whoever has a hand on SKC will never have peace and enjoy his days of life.
@Issahkabichi7.Ай бұрын
Ana achibwanaa
@williamchimpesaАй бұрын
For sure
@KennedyChitundaАй бұрын
In Jesus name Amen
@wilkeyskapanga751026 күн бұрын
True
@wymankamanga-xd5pv29 күн бұрын
achihana uko muli uko Pala pangawa mwayi mwizeko ku nkhatabay mkondezi area I beg
@ruthkundwe7448Ай бұрын
No rest for the wicked
@user-jm8kw9gw2dАй бұрын
Aford the mother of all political parties in Malawi, it's your time Big Man, mcp is afraid of you in Jesus name
@OsimanIbnAkimАй бұрын
Your the best speach 💪💪
@WAZAKILIBANDAАй бұрын
Kumeneko nde kulankhula dad🥰🥰🥰🥰🥰
@EmmanuelGasiten-fo5drАй бұрын
No SKC, indeed no MCP
@unstorice4045Ай бұрын
Appreciate you chihana🎉🔥🔥🔥🐐
@MaloneBanda26 күн бұрын
Big up 💥💥💥
@user-oc9vl9xz8eАй бұрын
Kumeneku ndiye kuyankhula Kwa Mtsogoleli wadziko kuyankhula mosaipa wina aliyense
@shonmike-su7qkАй бұрын
Mcp inalakwitsa kwambiri kuphwanya lonjez ndipo izizi zimenez amalawi zatikwiitsa kwambiri from molongolo Tanzania
@isaaczuze6 күн бұрын
Enock chihana akunena zoona ...amasuleni agaluwa ..chimwendo ndiye akuzimva kwambili ndipo ndi munthu amane amakonza ziwembu zonse za chakwera
@WilsonMillion-p2u14 күн бұрын
Ndiye cadet wachabechabe uzithupsya amalawi kuya nkhula chilungamo.apa ngakhale wina azinama koma imfa ya chilima ipase phunziro
@RespectMbeweАй бұрын
Speak out Mr Chihana
@RoseTaika9 күн бұрын
So courageous
@user-ko1lk3br4r26 күн бұрын
Km Inu simudzalowapo mboma truth
@clearbooks355Ай бұрын
Well spoken
@PemphelaniTchezaАй бұрын
We have lost a great leader SkS because useless party mcp😢😢
@NeemaMatewereАй бұрын
Thanks for the information
@GraceZumazumaАй бұрын
Chilungamo osamaopa chakwera aziziwa
@PiliraniMalemia4 күн бұрын
God is watching from a distance
@CharlesChilinde28 күн бұрын
Kuulula nzinsinsi za chulungamo timauula miniwake ali ndimoyo osatizi izi menenezo ayi ulekeni Mzimu wa chilma uuse mu mtendere osati zonena mbweeeee pezani zina zonena osati kutukwana anzanu .😅😅😅