Enock Chihana kuulura poyela zinsisi zomwe chilima anamuuza asanamwalire zokhunza Tonse Alliance

  Рет қаралды 235,130

Makosana

Makosana

Ай бұрын

Пікірлер: 411
@StanleyMkulama
@StanleyMkulama 25 күн бұрын
Akatundu awa!!!!! He is so courageous!!! speaking with no Fear,, he sounds like Chilima in his Bond of courageous.
@lloydjeremiah2250
@lloydjeremiah2250 Ай бұрын
eeee kma this man is so courageous
@MasausoMsiska-rz3id
@MasausoMsiska-rz3id Ай бұрын
Munthu koma uyu speaking without fear....Big up Mr chihana
@user-fz3gu2ez1o
@user-fz3gu2ez1o 29 күн бұрын
Eeeeee Koma SKC 😭😭😭😭 Ine imfa iyiyi.. Imandiwawa.. eeeeee
@JesusChristFollowers-ez9zu
@JesusChristFollowers-ez9zu Ай бұрын
Mr. Chihana is man of his word, ndipo zikupanga prove that he is the son of his father. Amenewa ndi amene anathema ndi kamuzu, apa chakwera akuchoka, ndavomereza anthufe sitimafa koma maonekedwe athu ndi amene amasintha
@arnoldkaikenkayange
@arnoldkaikenkayange Ай бұрын
Afford my vote
@iconiclife6811
@iconiclife6811 25 күн бұрын
So powerful bwana We need this Energy in our country honestly achinyamata ambiri akufuna ngati iziiii
@kusekejere
@kusekejere Ай бұрын
SKC has gone leaving a message that malawi is the land with possibilities but the problem are the leaders. What a humble guy. Rest well sir
@jonasmunthali848
@jonasmunthali848 Ай бұрын
I didn't know dis guy can talk lyk dis🙌🙌🙌🙌🙌🔥🔥🔥🔥🔥
@hopesato
@hopesato Ай бұрын
Anthu akwiya mkoz
@jonasmunthali848
@jonasmunthali848 Ай бұрын
@@hopesato ndaonaso🙌
@magex887
@magex887 21 күн бұрын
Koma ndiye.big up chihana❤
@luciatembo-e4f
@luciatembo-e4f Ай бұрын
Straight wise proud of you chihana🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥
@AgnessMzengo
@AgnessMzengo Ай бұрын
Wise leader...... Tell them
@amandamoyo7156
@amandamoyo7156 Ай бұрын
God protect Mr Chihana....we love u
@HopeJaffari
@HopeJaffari Ай бұрын
Ramaphosa wanthu waku Malawi 💪💪
@NoluvuyoMatutu
@NoluvuyoMatutu Ай бұрын
😂😂😂😂even me I thought like that ndtaona pic yake poyamba
@memoryziyaya2593
@memoryziyaya2593 Ай бұрын
true ..they are resembling very 😅
@fostersimbi8820
@fostersimbi8820 Ай бұрын
Didn't know this guy amayankhula mwamphamvu chonchi ❤🔥
@lyiemax
@lyiemax Ай бұрын
Powerful, proud of you Honourable Chihana
@FelixChimsNyirenda
@FelixChimsNyirenda Ай бұрын
Tell them the truth don't be afraid 😨 GOD will guide and protect you, we relay behind your your back.
@HappyAbyssinianCat-xt2bm
@HappyAbyssinianCat-xt2bm Ай бұрын
Km ndi zoona chakwera popanda chilima sukanawina galu iwe chakwera unapanga ndiwolotse ndikakutafune galu iwe chakwera dzimaso dzako unatiphera ngoni wathu
@catherinesilverio-d5w
@catherinesilverio-d5w Ай бұрын
Pankongo pake ameneyu ndipo mabala awawa sazapola taaaa
@user-ky4ce9gb6j
@user-ky4ce9gb6j Ай бұрын
Ndipo dziko lino analitembenuza dziko lino
@user-rf4br1fv2z
@user-rf4br1fv2z Ай бұрын
Ndiye chilima popanda chakwera adakhala vp tisamalakhule mbali imodzi chilima tu adali vp from 2014 up to 2024 ineyo ndimafuna nditadziwa zomwe adapanga kapena ankadikila adzakhale President kuti inuyo mudzayamve kusangalala to me i don't know thanks God ineyo ndimadziyimila from nyumba ya maudzu to mansion bra inuyo dikuilani chiloma wina kuti moyo wanu udzasithe
@DJBless1506
@DJBless1506 21 күн бұрын
@@user-rf4br1fv2z chilima anakhala vice president chakwera kulibe kapena wadya chamba eti?
@MikeMerecah
@MikeMerecah Ай бұрын
Kuno kwa msundwe keep it up chihana we need truith,
@kennedybanda
@kennedybanda Ай бұрын
Even the bible itself says do not touch my anointed ones.
@papelariareis.e.
@papelariareis.e. 8 күн бұрын
This guy is very strong 💪 🎉🎉🎉
@user-cn3gi2vf5n
@user-cn3gi2vf5n Ай бұрын
You are the great man thanks for the truth
@DN-mp8pp
@DN-mp8pp Ай бұрын
We need fearless leaders like you! Ndipo ma leaders ena atengelepo phunzilo, learn to be fearless like Chihana osamangokhala phwiiii osalankhula
@WilliamNhlane-fd9hi
@WilliamNhlane-fd9hi Ай бұрын
Good leader
@chrisneySwanepoel-yu5vd
@chrisneySwanepoel-yu5vd Ай бұрын
Voice iyiyi itha kundipangisa kuyamba kusapota afford 💪💪💪💪
@WilliamNyirenda-xq4km
@WilliamNyirenda-xq4km Ай бұрын
Koma ajoinane ndi utm ndili mumbuyo mwao
@tsanzomwanya
@tsanzomwanya 25 күн бұрын
Akut Chisilu chilichonse Chitha kukhala nduna
@dalsonkaluwa6575
@dalsonkaluwa6575 29 күн бұрын
Mwana wa Simbi ya Moto 🔥🔥🔥💪
@josephphiri7481
@josephphiri7481 Ай бұрын
Great leader 🎉mr chihana keep up
@ritanjolomole2076
@ritanjolomole2076 Ай бұрын
All the best Aford
@JoelMphoka
@JoelMphoka 28 күн бұрын
Watching from Soweto Johannesburg. Powerful.
@user-nf3ik3ff6y
@user-nf3ik3ff6y Ай бұрын
Good Messnge Mr Enock Chihana❤
@tawongamhango7335
@tawongamhango7335 25 күн бұрын
Chihana we dont want hate speech be like you father who never preach hate speech
@YohaneMuonja
@YohaneMuonja 29 күн бұрын
Am not a politician and am from kumwera but ilove ana achihana personally.Courage ya nyoo
@EmmanuelMlinganiza-bm7li
@EmmanuelMlinganiza-bm7li Ай бұрын
Enock Chihana (Akatundu aboma) 🎉🎉🎉🎉 Thawi yakwana 🎉🎉🎉🎉
@sylvesteralfred8355
@sylvesteralfred8355 Ай бұрын
Lero ndiye kuli kung'aluladitu sizinaoneke
@EstherDebwe
@EstherDebwe 27 күн бұрын
Kuli zinthutu👐
@yvescadet8524
@yvescadet8524 Ай бұрын
Congratulations honorable chiana
@karenn2969
@karenn2969 15 күн бұрын
True voice of a leader, thus why he was the first to demand enquiries into the death of Chilima
@PemphelaniTcheza
@PemphelaniTcheza Ай бұрын
Chilungamo sanong'onotu 😢😢with heart broken
@smashingogden4236
@smashingogden4236 Ай бұрын
We soldier on!... very brave mr chihana junior 💪🏼🇲🇼... speak it like it is....
@RamzyMsukwa
@RamzyMsukwa Ай бұрын
The guy fearless and speak energetic
@augustMag
@augustMag Ай бұрын
Haaaa mwatipha basi tonse Amalawi mukanamuuza zoona mwanao kuti fisi ndi fisi sangasithe mawaanga 😭😭😭😭
@DaveChirwa-s4j
@DaveChirwa-s4j Ай бұрын
I lv it.
@PatrickKabudula
@PatrickKabudula Ай бұрын
You are not alone mr
@NysonStandy
@NysonStandy Ай бұрын
Go ahead mr Cihana
@user-jv7xw1fo6c
@user-jv7xw1fo6c 27 күн бұрын
Sadzagona tulo wopha chilima
@SigoMw
@SigoMw Ай бұрын
Ndipo simunati akanantchulidwabetu chilima mpaka mpaka muphulikeee amfiti inu
@user-nv3rf7bl7r
@user-nv3rf7bl7r Ай бұрын
A chilima asanduka kamupeni pano 😢😢😢 ambuye nkhondo ndiyanu chilichose mukudziwa ndinu
@user-tk6qh9zs7h
@user-tk6qh9zs7h Ай бұрын
Zomvetsatu chisoni kwambiri. Ndikanakonda a ku Banja akanaketsa Zopusa zimenezo. Chidziwika ndi chakuti SKC ndi CHIHANA were not Friends. Ngati zomwe akunenazo ndi zoona tione umboni wake. Atiuze nthawi, tsiku komanso Audio or ma message olemba. Musaiwale kuti ndi yomweyinso anabweretsa nkhani yonama ku Nyumba ya Malamulo atafunsidwa za umboni anakanika kupereka. SKC awuza bwanji iyeyo kusiya kuuza utm members?. CHIHANA ndi ONAMA kwambiri
@user-nv3rf7bl7r
@user-nv3rf7bl7r Ай бұрын
@@user-tk6qh9zs7h ndipo inu koma ambuye akuwona zomwe akupangazi ziwabwelela wokha kapeni ngati yavuta kungosiya mbanji elsh
@mishecksipolo7153
@mishecksipolo7153 Ай бұрын
Palibe wasanduka campaign apa ,akungokamba chilungamo period
@viennasamuel2976
@viennasamuel2976 Ай бұрын
Ndipo live akunenazo ndizoona ikakhala campaignyopangila munthu nawonso apanga ya kamuzu iyaaaa
@user-nv3rf7bl7r
@user-nv3rf7bl7r Ай бұрын
@@mishecksipolo7153 musalowetse ndale pa imfa yamunthu muziganiza mofatsa musanayankhule nyasi zanuzo inu simulungu
@user-ty4pq5ub3q
@user-ty4pq5ub3q Ай бұрын
RIP CHILIMA....😢😢. Auzeni live live..akapukuu ..nduna zokuda mbuuuuuuu
@MirriamKambale
@MirriamKambale Ай бұрын
Chakwerayutu si m'busa anthunu mangosokoneza munthu uja ndi nthakati. Mfwiti ya tyala iliye na mzeru ingaphepese yai after those words pray hard angakusowetse
@WilliamNyirenda-xq4km
@WilliamNyirenda-xq4km Ай бұрын
Viphalileni bwana viwanthu voina mitu ivi you are my vote
@MadalitsoTamayenda-ez5pj
@MadalitsoTamayenda-ez5pj Ай бұрын
Powerful voice
@user-dh8ho2qt4h
@user-dh8ho2qt4h 24 күн бұрын
❤❤❤ love you dad. We all cry our vice president chilima.😢😢😢
@ClaraMkandawire-d2k
@ClaraMkandawire-d2k 29 күн бұрын
Kuyankhula koma ukuuu aaaaseeeee👊😂
@tumpalechihana5073
@tumpalechihana5073 Ай бұрын
Our own leader
@louisbonongwe8537
@louisbonongwe8537 Ай бұрын
Whoever has a hand on SKC will never have peace and enjoy his days of life.
@Issahkabichi7.
@Issahkabichi7. Ай бұрын
Ana achibwanaa
@williamchimpesa
@williamchimpesa Ай бұрын
For sure
@KennedyChitunda
@KennedyChitunda Ай бұрын
In Jesus name Amen
@wilkeyskapanga7510
@wilkeyskapanga7510 26 күн бұрын
True
@wymankamanga-xd5pv
@wymankamanga-xd5pv 29 күн бұрын
achihana uko muli uko Pala pangawa mwayi mwizeko ku nkhatabay mkondezi area I beg
@ruthkundwe7448
@ruthkundwe7448 Ай бұрын
No rest for the wicked
@user-jm8kw9gw2d
@user-jm8kw9gw2d Ай бұрын
Aford the mother of all political parties in Malawi, it's your time Big Man, mcp is afraid of you in Jesus name
@OsimanIbnAkim
@OsimanIbnAkim Ай бұрын
Your the best speach 💪💪
@WAZAKILIBANDA
@WAZAKILIBANDA Ай бұрын
Kumeneko nde kulankhula dad🥰🥰🥰🥰🥰
@EmmanuelGasiten-fo5dr
@EmmanuelGasiten-fo5dr Ай бұрын
No SKC, indeed no MCP
@unstorice4045
@unstorice4045 Ай бұрын
Appreciate you chihana🎉🔥🔥🔥🐐
@MaloneBanda
@MaloneBanda 26 күн бұрын
Big up 💥💥💥
@user-oc9vl9xz8e
@user-oc9vl9xz8e Ай бұрын
Kumeneku ndiye kuyankhula Kwa Mtsogoleli wadziko kuyankhula mosaipa wina aliyense
@shonmike-su7qk
@shonmike-su7qk Ай бұрын
Mcp inalakwitsa kwambiri kuphwanya lonjez ndipo izizi zimenez amalawi zatikwiitsa kwambiri from molongolo Tanzania
@isaaczuze
@isaaczuze 6 күн бұрын
Enock chihana akunena zoona ...amasuleni agaluwa ..chimwendo ndiye akuzimva kwambili ndipo ndi munthu amane amakonza ziwembu zonse za chakwera
@WilsonMillion-p2u
@WilsonMillion-p2u 14 күн бұрын
Ndiye cadet wachabechabe uzithupsya amalawi kuya nkhula chilungamo.apa ngakhale wina azinama koma imfa ya chilima ipase phunziro
@RespectMbewe
@RespectMbewe Ай бұрын
Speak out Mr Chihana
@RoseTaika
@RoseTaika 9 күн бұрын
So courageous
@user-ko1lk3br4r
@user-ko1lk3br4r 26 күн бұрын
Km Inu simudzalowapo mboma truth
@clearbooks355
@clearbooks355 Ай бұрын
Well spoken
@PemphelaniTcheza
@PemphelaniTcheza Ай бұрын
We have lost a great leader SkS because useless party mcp😢😢
@NeemaMatewere
@NeemaMatewere Ай бұрын
Thanks for the information
@GraceZumazuma
@GraceZumazuma Ай бұрын
Chilungamo osamaopa chakwera aziziwa
@PiliraniMalemia
@PiliraniMalemia 4 күн бұрын
God is watching from a distance
@CharlesChilinde
@CharlesChilinde 28 күн бұрын
Kuulula nzinsinsi za chulungamo timauula miniwake ali ndimoyo osatizi izi menenezo ayi ulekeni Mzimu wa chilma uuse mu mtendere osati zonena mbweeeee pezani zina zonena osati kutukwana anzanu .😅😅😅
@ChisomoKalimba
@ChisomoKalimba 12 күн бұрын
Mudzamwalira osalamulirako dziko inu! Chifukwa chachimtima chasanje
@ConnexMtika
@ConnexMtika 18 күн бұрын
Ilov AFORD leader fearless
@TakalaneManizo
@TakalaneManizo Ай бұрын
Interesting
@sweedenBanda
@sweedenBanda 24 күн бұрын
Nice ndzaknda
@user-cx8gk5en6h
@user-cx8gk5en6h Ай бұрын
I respect this guy
@JusticeDamalekani
@JusticeDamalekani 16 күн бұрын
Akamuna awa❤ osati akapamba enawa😢
@lonelychakhala8449
@lonelychakhala8449 23 күн бұрын
Maliro aja trapeze zolankhula pa campaign popanda maliro aja fundo tinalibe fundo zake zimenezi zingatukule Malawi?
@CatherineChalema
@CatherineChalema 22 күн бұрын
Umbuli wazika mizu pa Malawi! Kwawo safa agalu awa komanso ngozi saidziwa. School ija ndiyabwino umbuli chihana chonsecho akudziwa kuti munthu anafa pa ngozi🚮
@McbeaulzJere-g7u
@McbeaulzJere-g7u Ай бұрын
Ndifera ndembera no2
@LouisNgowera
@LouisNgowera Ай бұрын
Ndayamba afford basi😂😂😂
@cynthiakamunga8045
@cynthiakamunga8045 Ай бұрын
😂😂😂
@user-dh8ho2qt4h
@user-dh8ho2qt4h 24 күн бұрын
😂😂😂
@FannyKumwenda-u4h
@FannyKumwenda-u4h 12 күн бұрын
My vote
@adonvingison4331
@adonvingison4331 18 күн бұрын
Vuto ndiloti some time the voice depending on the language that person use but in really this voice is for him
@chcmzuzudiocese5916
@chcmzuzudiocese5916 21 күн бұрын
Chakufwa Chihana weniweni
@ZahnoorMilan
@ZahnoorMilan 20 күн бұрын
Powerful talk
@martinBPhiri
@martinBPhiri Ай бұрын
Nanga zoona tizingomva zoti a Chilima adandiuza 😅😅😅 usiyeni Mzimu wa Vice President wathu uwuse mumtendere
@johnkatapeh7182
@johnkatapeh7182 Ай бұрын
Kkkkkk chitsiru chinachake ndi nduna,,,,moto buuuuuuu
@MosesKalenge
@MosesKalenge Ай бұрын
Assaaaaaaa 😂😂😂😂😂 good news 🙏🙏🙏🙏 chehana❤🎉🎉🎉🎉🎉🎉🎉
@chippakaribafox2865
@chippakaribafox2865 Ай бұрын
It was a very tricky deal to sign such deal.....zopepela without solid constitutional grounds I brame those who advised skc to take that deal
@faidaceciliaYekha
@faidaceciliaYekha Ай бұрын
Kumakhala munthu wolimba mtima ngati chihana💪
@GiftmvulaZimba
@GiftmvulaZimba Ай бұрын
I salute you
@SHENCOHNSOLOMBA
@SHENCOHNSOLOMBA 16 күн бұрын
Dolo 🎉
@FabianMhango-zk6nv
@FabianMhango-zk6nv Ай бұрын
No secret under the sun
@tanishadias
@tanishadias Ай бұрын
Go deeper Enock chihana
@Jacjilinesawu
@Jacjilinesawu 9 күн бұрын
Koma yaaaa❤
@janetbyson
@janetbyson 24 күн бұрын
Chakwela mfiti kobasi waiwala kuti anakupangila campaign Chilima analakwa chani
@HastingsMnyenyembe
@HastingsMnyenyembe Ай бұрын
Tiona ma vote .
CHOCKY MILK.. 🤣 #shorts
00:20
Savage Vlogs
Рет қаралды 27 МЛН
The Joker saves Harley Quinn from drowning!#joker  #shorts
00:34
Untitled Joker
Рет қаралды 56 МЛН
Идеально повторил? Хотите вторую часть?
00:13
⚡️КАН АНДРЕЙ⚡️
Рет қаралды 17 МЛН
KAMLEPO KALUA WATI SAKUOPA KUFA MPAKA CHILUNGAMO CHIDZIWIKE
23:30
KAFUKUFUKU PA IMFA YA ACHILIMA
30:18
Jimmy
Рет қаралды 146 М.
MALAWI COURT.... TAMVANI IZI ABALE 🤔
20:45
Jimmy
Рет қаралды 153 М.
EXCLUSIVE INTERVIEW WITH ENOCK CHIHANA
56:27
Zodiak Malawi
Рет қаралды 56 М.
JOHN KAPITO WATOPA NAYE CHAKWERA. Ityoke ityoke Osabisa mau // PART 1
33:23