Dr Bakili Muluzi ndi president wakale wa dziko la Malawi🇲🇼
Пікірлер: 75
@bonjechaula85423 жыл бұрын
1981 bakili muluzi anaba ndalama za makad a MCP, mbava yeni yeni.
@fanizoabrahamchimbalanga65293 жыл бұрын
God bless bakili muluzi adathandiza amalawi kuwachotsa muumbuli waukulu
@amisichiphiri82272 жыл бұрын
Kwambiri anatisambisa kumanso
@ImeedFranckАй бұрын
😂😂😂😂😂😂
@FrancisNyayi15 күн бұрын
Better anatipangisa tinkhare ndi maphone pano tikunvera pa phone good man
@davidbulla9390 Жыл бұрын
Wonderful di
@Littlefair73 жыл бұрын
Kodi achair kuba anayambira patali eti? Mpaka kuba £6? Ndi kudzasololanso K1.9bn
@franciskaponda86083 жыл бұрын
Komanso kulemera pamaso pa kamuzu zizinali zocheza ayi ameneyu adzafotokoze bwino part 2 akunenayo akhatiuza kuti a Gadama ndi amzawo aja akhati mukutipheranji akuwakhoma ndi hamala iye anali kuti ????????
@lastlevel19993 жыл бұрын
We will waiting for part 2
@mosesharoldngolombe10 ай бұрын
Anyamata apa town❤
@charlesmuyaya88393 жыл бұрын
Thanks for the info. Keep it up
@EsnatSayiwala2 ай бұрын
Wow ❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤
@ibrahimyusufu39272 жыл бұрын
FDU... NICE
@fredrickkhebozy66833 жыл бұрын
Well done sir
@maongambonde10043 жыл бұрын
Kamuzu inali mbalame
@sharifsaidi67063 жыл бұрын
Please upload it, we are waiting
@alexjeremanuel2541 Жыл бұрын
I like this man chair
@richardnkosi19343 жыл бұрын
Anagwetsa dziko la Malawi koposa Mafia wakuba
@mouricesaidi53483 жыл бұрын
oky?????? zako zimenezo
@m00n_pInK3 жыл бұрын
kuti malawi ilowe pansi ndi bakili akuluwa amakondela zoika apa.
Bakili anali nduna ya Kamuzu zonse zoipa amapangira limodzi ndi Bakili sikuti Kamuzu amapha yekha anthuwa ayi
@uthmanalex3 ай бұрын
@@charlesmuyaya8839 chisiyeni amwene ndichitsiru they miss understanding amavera alipanjinga 🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣
@hopesonnsongolo1049 Жыл бұрын
Bakili ndi dolo
@chikondimwale75173 жыл бұрын
Ati "mfana upange resign"
@goldencitytowerent95543 жыл бұрын
Hahaha eyetu
@Ibrahimson-su5ks Жыл бұрын
Skype Skills
@olipamaseko2693 Жыл бұрын
Or pano ma school achisilamu Ali kuti? Awa akungoyankhula za mmutu mwao pano ndi ndani anaphunzirapo sukulu ya chisilamu ndipo zili kuti?
@user-cy5ko2qw5d4 ай бұрын
Masukulu achisilamu kumalawi sukuwaziwa😂😂😂
@goldencitytowerent95543 жыл бұрын
Mbiri ya Bakili ija mwalowaso za khaza za MCP kkk
@LouisjrSaka3 жыл бұрын
😂😂😂😂😂😂😂😂koma adha
@goldencitytowerent95543 жыл бұрын
@@LouisjrSaka kkk koma kamuzu anamulakwira chachiku mukulu ameneyu, ofcourse a MCP anali akhaza koma kumapolako
@LouisjrSaka3 жыл бұрын
@@goldencitytowerent9554 chomwe adalakwa kamuzu kwa mkulu ameneyo nchachikulu heve 🤣🤣🤣🤣
@alankasiya73293 жыл бұрын
Zabodza izi Bakili sanaphuzile ankagulitsa matumbi ku zomba. School anaphuzila atasankhidwa kale u president
@charlesmuyaya88393 жыл бұрын
So You mean Bakili Muluzi anapeza scholarship yokaphunzira ma college akunja mzaka za mma 1960 ali osaphunzira? I think mbuli ndi iweyo palibe chomwe ukudziwa chokhudza Bakili Muluzi.
@danielmaluwa78963 жыл бұрын
Bakili muluzi ankagwira ntchito ngati clerk wa Ku court poyambilira penipeni. Ndie ukati anali osaphunzira ukutanthauza chani. Moreover bakili muluzi anali principal wa Nansawa technical college, kamuzu banda anamusankha kukhala MP komanso nduna ya boma pa nthawi yomwe anali mphunzitsi wamkulu wa pa Nansawa technical. Ndie ukati anali mbuli ukutanthauza chani. He was even minister of education mnthawi ya kamuzu. Mwina unangomvera ma propaganda a anthu kuti bakili muluzi anali osaphunzira iwe
@alankasiya73293 жыл бұрын
U have been mis informed Bakili ankamphuzitsidwa school ndi Dr Ken lipenganga Ali kale president. Jce and msce anazipeza Ali kale president.
@charlesmuyaya88393 жыл бұрын
@@alankasiya7329 kutanthauza kuti ukutsutsa kuti Bakili Muluzi sanagwire ntchito Ku khothi ngati clerk? Sanagwire ntchito ngati principal pa nansawa college? Sanapite kunja mzaka za mma 1960 kukaphunzira ma college a ku Denmark ndi ku Britain? Sanakhalepo minister of education mnthawi ya Kamuzu? Ukamati we were mis informed what do you mean? Ife tikunena zoona zenizeni zooneka ndi maso pomwe iwe ukunena zongomvera anthu za mabodza. Bakili Muluzi was even minister of portfolio mnthawi ya Kamuzu, and you think munthu angakhale minister of portfolio ali mbuli?
@alankasiya73293 жыл бұрын
@@charlesmuyaya8839 maphunzilo amene anenedwa kuti anaphuzilawo that's what I'm against kale anthu ankamphuzila up to STD 5 nkumapeza ntchito ngakhale Aleke Banda anali minister nthawi ya kamuzu koma anali ndi jc . Ngakhale ma minister ambiri muthawi ya amuluzi anali osaphunzira. Kukhala minister sikuphunzira