Dziko La Malawi Ndilosauka Kwambili Kuti Tizikhlala Busy Ndi Cybercrime - Samuel Lwara

  Рет қаралды 15,255

Nyasa VoiceBox

Nyasa VoiceBox

Ай бұрын

On Nyasa VoiceBox, Samuel Lwara says, Malawi's level of Socio-econonic development is too low for people and government to be busy with cybercrime laws instead of focusing on development and economic growth.
Pankhani ya Nyasa VoiceBox, Samuel Lwara wati chitukuko cha dziko la Malawi pa chitukuko cha chikhalidwe cha anthu ndi chochepa kwambiri moti anthu komanso boma limakhala lotanganidwa ndi malamulo okhudza umbava wa pa intaneti m’malo moika maganizo awo pa chitukuko ndi kukweza chuma.
#malawi

Пікірлер: 95
@alexsumani6823
@alexsumani6823 28 күн бұрын
Malawi has intellectuals like Lwara ,we need people like Lwara the country can do better
@user-nf3ik3ff6y
@user-nf3ik3ff6y 28 күн бұрын
Good Messnge Chakwela you mast go watinyasa
@JamesMalango
@JamesMalango 28 күн бұрын
Chilungamo sir great speech
@harrisbanda5891
@harrisbanda5891 28 күн бұрын
Sam umalankhula ma points ogwira mtima, keep it up bro, keep on fighting for those whose got a say but they can't talk
@princedetbozsmallboy1749
@princedetbozsmallboy1749 28 күн бұрын
This is powerful speech i ever heard before from anyone who fighting against this useless government. Chakwera ndimbuzi pamozi ndi anthu ake wose galu yamunthu
@user-qp8kh2hj9o
@user-qp8kh2hj9o 24 күн бұрын
Powerful message chilima anapanga kale compaign akangolowa kupanda kuganiza zochosa moyo wake koma mau ndi oti chilima sanafe alipo mpaka 2025 MCP isova chipani cha mwazi😢
@YasinMusa-ym8lp
@YasinMusa-ym8lp 28 күн бұрын
Achakwera opusa kwambili wapasako ukuvuna kulimbana ndiandu kusiyakukosa dziko boma lopusa lilibeseluso
@AllanWyson
@AllanWyson 28 күн бұрын
This guys impresses me with his naked truth, may god continue keeping this guy for us so that he must continue speaking for those who cant speak.
@user-qg4it7my9n
@user-qg4it7my9n 28 күн бұрын
kachilungamo2 ulemu wanu ine pheee!!!! ❤❤
@user-iw6cz5ft2l
@user-iw6cz5ft2l 28 күн бұрын
Thank you sir
@user-fp5qn5ci2v
@user-fp5qn5ci2v 28 күн бұрын
😅😅😅😅 Lwara ai ndithu lero kulibe Bakili Muluzi TV ndipo sindikanagona bwino kupanda iwe anthu ngat inu mukufunika mMalawi muno kwambiri
@jacksonmaster2288
@jacksonmaster2288 28 күн бұрын
Samuel Lwara ndiwa nzeru.
@user-xd1cm7tm7t
@user-xd1cm7tm7t 28 күн бұрын
Very nice mr this goverment is felia
@meeksonmkhala
@meeksonmkhala 28 күн бұрын
Well facts presented. Well done Mr Samuel
@StevenAjusugama
@StevenAjusugama 28 күн бұрын
Good talking brother
@harrisbanda5891
@harrisbanda5891 28 күн бұрын
Tell dem bro, they don't know de definition of the word CIBER CRIME 😂😂😂😂😂😂
@chikublea8982
@chikublea8982 28 күн бұрын
From mangochi mumatha kwambiri
@user-wf2ii7zx5e
@user-wf2ii7zx5e 28 күн бұрын
Thank you brother, Chilima timulira mpaka tsiku lozavota. Mcp ichoke basi
@afritouch4660
@afritouch4660 28 күн бұрын
Powerful.!
@MaxwellMbesa
@MaxwellMbesa 28 күн бұрын
Zoona brother
@gizzykondwani865
@gizzykondwani865 28 күн бұрын
keep up the good work
@LumbaniNeba
@LumbaniNeba 28 күн бұрын
Congratulations brother
@SheenahMwalabu-iz3pr
@SheenahMwalabu-iz3pr 28 күн бұрын
Ndimamva Nanu kukoma abambo a Lwara ndipo izizi mmalankhulazi ziziikidwa ku times radio ku mibawa amalawi adzimva kuti atseguke mitu ndipo chilungamo chimawawa. Koma nde Chilima anali mbambande ndipo anali hope yathu RIP
@user-ve2ts3yr2n
@user-ve2ts3yr2n 28 күн бұрын
🙌 powerful achoke basi
@user-pl8kw3dc9d
@user-pl8kw3dc9d 28 күн бұрын
Zoona zoona brother kuputsa kwa chakwera
@user-xx3mg2gz5z
@user-xx3mg2gz5z 27 күн бұрын
Achape mutu my brother
@eliffagondewe8214
@eliffagondewe8214 28 күн бұрын
Kkkkkkk inu Mmayankhula bwino kwambiri🔥🔥🔥🔥reality..
@4ourcusworldwide426
@4ourcusworldwide426 28 күн бұрын
💪💪💪💪💪
@DavieMakwecha
@DavieMakwecha 26 күн бұрын
Ndipo pafunika kuotcha ma office onse plus magalimoto onse a mcp chitheretu chipani chimenechi mmalawi
@blessingsmaloya3570
@blessingsmaloya3570 28 күн бұрын
Shaaaa!!!!!
@SibwenzaLevisoni-gm6rv
@SibwenzaLevisoni-gm6rv 28 күн бұрын
Fire dem
@harrisbanda5891
@harrisbanda5891 28 күн бұрын
Muwawuzenso kuti social media ndiya azungu, Twitter, Instagram, WhatsApp, facebook, utube it's from European countries, and enu wake azunguwo akumaposita ma video and photos pa social media, ndeinu a mcp muzitilesa kuposita ma video pa social media, who are you?, peter kalaya , who are you? ,daud suleyman, who are you?, kumkuyu and chimwendo who are you?, zikhale ng'oma and yolamu who are you?. Stop intimidating malawians ok?, mxiem 😡
@user-tw2zf7bj3e
@user-tw2zf7bj3e 28 күн бұрын
I salute you sibweni
@user-ez8zs1iq9k
@user-ez8zs1iq9k 28 күн бұрын
inetu sindimakuteengerani a lwara pazoyankhula zanu koma ngati zoyankhaula zanu ndi izi nde kuyambira lero ndizikusatani chifukwa umu mwayankhula chilungamo komaso za nzeru kwambiri
@user-du9qs4tb6u
@user-du9qs4tb6u 28 күн бұрын
Amasuleni kuti boma likupita ili kkkkkkk koma Lwara kkkkk anthu osamva awa boma lililamulidwa ndi nduna president of ofoyila kkkk
@GraceLimani-zw7dx
@GraceLimani-zw7dx 28 күн бұрын
Kkkkk wawo wa mcp akuti uza yekha a tavala nsalu yawo amangetu
@user-ww2il4wb8o
@user-ww2il4wb8o 28 күн бұрын
😅😅😅😅koma chilungamo chitipha
@FrancoKaunga-rq2ki
@FrancoKaunga-rq2ki 28 күн бұрын
Mr lwara you are genuine comrade may God continue to bless you! Tell these idiots the truth.
@Mervic-vm8eo
@Mervic-vm8eo 28 күн бұрын
Cybercrime kunyumba kwako ndi family Yako chakwera,,not Kwa ife amalawi
@joyahmedjoma4615
@joyahmedjoma4615 28 күн бұрын
Ndipo live sukunama chakwera saziwa kanthu ndipo ndale saziziwa ata 😂😂😂😂
@JumaKachala
@JumaKachala 28 күн бұрын
Kkkkkkkk keep it up
@FelixBoss-yn9pe
@FelixBoss-yn9pe 28 күн бұрын
😮😮😮😮
@harrisbanda5891
@harrisbanda5891 28 күн бұрын
Why u were quiet for the whole last month bro?
@princedetbozsmallboy1749
@princedetbozsmallboy1749 28 күн бұрын
Wakumva wave koma agaluwa Chakwera ndi azinzake samba chifukwa ndi ana asatana
@user-gs7wc3nx3q
@user-gs7wc3nx3q 27 күн бұрын
Kkkkkk chakwera watikwana kwambiri nichifukwa ni lazar wa zironda
@HafizahHarack-bn3bf
@HafizahHarack-bn3bf 28 күн бұрын
Chakwela ngat uli wa mzelu unakangochoka wenkha pampandopo because watikwana ndikuti Nyasa kwambili.
@user-lb5gt4uv3s
@user-lb5gt4uv3s 28 күн бұрын
Chilungamo brother
@user-is5dl7np9g
@user-is5dl7np9g 28 күн бұрын
Uku ndiye kulankhula Kwa mzuru bwana Lwara
@ebenezerkamanga6016
@ebenezerkamanga6016 28 күн бұрын
Waying'alura momveka bwino aseh 😂😂😂
@remsychipani2896
@remsychipani2896 28 күн бұрын
Zamphavu kwabasi more fire big
@Trancy-xt4py
@Trancy-xt4py 27 күн бұрын
Inuyo comrade ndinu mafia Mutha kulowa Malo mwa chilimat inu chilungamo chomwe mukulakhula ZOMWE chilima amafuna zimu wawo SKC uziutsa mumtendere taluzat muthu UJA wapita wamala kwabasaaaaa mwatililisa mcp pachilima ndianthu 9 onse ujatalirat
@JohnKayinga
@JohnKayinga 26 күн бұрын
Ndipo izi nane ndinali wodabwa komaso chikudabwisa a police omanga anthuwo akuchokera ku LILONGWE Kodi ku BT ndi ku mzuzu a police kulibeko? MCP government is falling apart koma zomanganazo zikapitilira zitha kubwelesa kusamvana mziko
@harrisbanda5891
@harrisbanda5891 28 күн бұрын
Guyz!, sam rwala is here kkkkkk😂😂😂😂😂
@MilikaKilion-tn1bn
@MilikaKilion-tn1bn 28 күн бұрын
Sumapita kuchimbuzi ukadya question 😅😅😅😅
@alexsumani6823
@alexsumani6823 28 күн бұрын
Zoona zokhazokha mbambande
@tasmania527
@tasmania527 28 күн бұрын
Imwe muli wa chindele imwe, nzeru kuchuluka.
@EdwardSamuel-xj8qq
@EdwardSamuel-xj8qq 28 күн бұрын
Zowona
@fatshooter87
@fatshooter87 28 күн бұрын
S Tell them boss Lwara
@CharityMhone-uk9ym
@CharityMhone-uk9ym 28 күн бұрын
😂😂😂😂😂🎉🎉🎉 mtumbuka iyoo
@mayesojameskatete
@mayesojameskatete 28 күн бұрын
😂😂😂❤❤
@ClementKamwendo-ti4vi
@ClementKamwendo-ti4vi 28 күн бұрын
😢😂😂😂❤
@user-un6qv6sj3h
@user-un6qv6sj3h 28 күн бұрын
Samuel from the bible tiyeni nazo osamakhala ndimantha ngati ndinu obwela tell them truth mantha satithandiza
@NTHANDOHKHOROMANA
@NTHANDOHKHOROMANA 27 күн бұрын
25 mini zoyakhula za nzeru zokha zokha
@DONNEXKhama-bk1gy
@DONNEXKhama-bk1gy 28 күн бұрын
Ndipo live chilungamo kuwawa chakwera watiphera msogoleri wathu
@JerryChain-cz8ru
@JerryChain-cz8ru 28 күн бұрын
Awuze kuti onse ndamphawi tikuvutika
@HarryKandani
@HarryKandani 28 күн бұрын
😂😂😂 koma yeah
@harrisbanda5891
@harrisbanda5891 28 күн бұрын
Another freedom fighter is here guys 😂😂😂😂
@martinnyirongo2892
@martinnyirongo2892 28 күн бұрын
Aaaa kwathu kumzimba no chitukuko Kayama mps aliko ndkukaika, mzimba to eswazini, mzalangwe, kafukule upto ekwendeni mseu unayamba mnthawi ya bingu mpaka pano sunatheee ndikunena pano mcp government inachotsa contractor, mwachidule tinene kuti anasiya kumanga since chakwera anatenga boma mu 2020 ndiye ine ndikudabwa kuti mafumu amuboma lamuzimba akulephera bwanji kumuuza chakwera zamuseu imeneu chifukwa ena mwa mafumuwa ndikwawo kumeneku komaso akugwiritsa ntchito mseu omweu eeeeee abale kumzimba anthu akuvutika nthawi ya mvula mayendedwe,,
@margetjustin7170
@margetjustin7170 28 күн бұрын
Zoona apange resign onse felliar minister
@user-un4pm4yt5i
@user-un4pm4yt5i 14 күн бұрын
2030 akawavotela ndi ambuyawo ifetu mcp tinawavotera chifukwa cha Chilima adzidziwa zimenezo
@user-ky8eq5ek1p
@user-ky8eq5ek1p 28 күн бұрын
Zoonadi Big
@user-os7qt6lw2c
@user-os7qt6lw2c 28 күн бұрын
Iwe nde akumanga..
@Kamwachale
@Kamwachale 28 күн бұрын
Bingu came with helicopters from China, where are these helicopters ?
@ChimwemweHenry-uw1bq
@ChimwemweHenry-uw1bq 28 күн бұрын
Live talk ulemu wanu
@user-fq4kv8dj4t
@user-fq4kv8dj4t 28 күн бұрын
Presdent uyuyu nde ayi panja penipeni Chakwela lazalo
@YasinMusa-ym8lp
@YasinMusa-ym8lp 28 күн бұрын
Kapen asimti usachaniso agaluwa
@user-um6yo6nc3e
@user-um6yo6nc3e 28 күн бұрын
Cybèrspace 😢
@user-kj6qj1md5e
@user-kj6qj1md5e 28 күн бұрын
Amakambilana zaupandu afiti awa
@user-do2cs8nf4b
@user-do2cs8nf4b 28 күн бұрын
😂😂😂😂😂😂😂🙌🙌🙌🙌🙌🙌🙌🙌
@FelixBoss-yn9pe
@FelixBoss-yn9pe 28 күн бұрын
Nde mwati mwazi wachilima utani big
@MustafaAbdullah-pb5zv
@MustafaAbdullah-pb5zv 28 күн бұрын
Chilungamo biggy
@Philipmantchombe-bb5dx
@Philipmantchombe-bb5dx 28 күн бұрын
Komatu ndiemwayankhulabwino bolamusasinthekusogoloku pajatu kunali laitoni mangochi
@user-pl8kw3dc9d
@user-pl8kw3dc9d 28 күн бұрын
Mnthu kuchoka ku church kukankhara mutsogoleri wadziku kkkkkkk malawi ife kumbwambwana kukatsankha nkhumba
@Musa1828-l5d
@Musa1828-l5d 28 күн бұрын
MCP rest in peace
@hanifahmponda8711
@hanifahmponda8711 28 күн бұрын
Kkkk apatu apatu watokota dziedi lwala ti amva pena pake akuti a boma akupasini bazi ayiiii bodza anthu ngati inu ndimene mulungu adzikupatsani moyo wawutali anthu ankhadza mulungu adziwachepetsela moyo wawo chifukwa ngati a MCP akumanga anthu ndiboma lopaaidwa ndi malemu chilima mwalo mothokodza ndikumuphatso ufiti wanji abale nde awine 2025 malawi tafa basi chuma chiwakanika kukodza nsono akufuna amalawi adzatiiani kodi iiii mulungu simunthu achite nanu a MCP
@paulpaseli6310
@paulpaseli6310 28 күн бұрын
Lwala iwe ndi wazelu kobas ulemu wako
@harrisbanda5891
@harrisbanda5891 28 күн бұрын
Is dat true that you recieved the money from dis cruel and useless crocodile party?
@user-xx3mg2gz5z
@user-xx3mg2gz5z 27 күн бұрын
Kkkkkkkkkkk
@JackMvura-ik2td
@JackMvura-ik2td 28 күн бұрын
Olira sitimamutseka pakamwa chakwera bomaaa sanje akulu awa akalamba mwachangu kuipa mtima zedii utopa ndikulankhula chakwera sudzamuona kuyankhapo zopusa ngati izi very stupid massage to Malawians tikuuze tsono chakwera adzawina with landslide ukuonanso dikira
@HakeemJossam
@HakeemJossam 28 күн бұрын
kkkkkkk
@AmusedDimSum-hd5yp
@AmusedDimSum-hd5yp 28 күн бұрын
ipaseni moto fada empty head chakwera
@InnocentMlowoka-ew4lo
@InnocentMlowoka-ew4lo 28 күн бұрын
Ii
Эффект Карбонаро и нестандартная коробка
01:00
История одного вокалиста
Рет қаралды 9 МЛН
Stay on your way 🛤️✨
00:34
A4
Рет қаралды 2,5 МЛН
Donald Trump speaks for the 1st time on the assassination attempt
14:17
FOX 9 Minneapolis-St. Paul
Рет қаралды 9 МЛН
Watch Donald Trump's 2024 RNC speech in full
1:36:20
6abc Philadelphia
Рет қаралды 1,3 МЛН
Donald Trump speaks at the RNC: FULL SPEECH
1:32:24
FOX 4 Dallas-Fort Worth
Рет қаралды 3,4 МЛН
Wina Ndinamuthyola Khosi - Samuel Lwara
14:15
Nyasa VoiceBox
Рет қаралды 42 М.
Ruto, This is Courting Disaster
17:22
Herman Manyora
Рет қаралды 29 М.