Times Exclusive’s Brian Banda engages Consumers Association of Malawi Executive Director Mr. John Kapito on the fuel situation and economic crisis in the country.
Пікірлер: 89
@TichezeChitukula-zn5xh9 ай бұрын
This is the best Exclusive interview so far in 2023 done by Brian Banda.
@Mphamdala9 ай бұрын
You haven't watched the one with Dalitso Kabambe
@ThomasCosmaskanjuchi9 ай бұрын
Your indeed a freedom fighter Mr Kapito❤
@user-mo7cj2yn6h9 ай бұрын
Kapito in Christ do what you want bwana mavuto ochuluka skubwela chifkwa chosowa usogoleri wabwno know mwauze aboma amvere kapito
@smartchitimbe24509 ай бұрын
The best 2023 interview on TTV
@user-un9eb5vn2r9 ай бұрын
I Like this man ndipo apuleo akuyenela azinvele zimenezi ziapweteke chifukwa chilungamo chimawawatu
@user-mi3fw1zg8b9 ай бұрын
Chakwera ndi Munthu omva zake zokha uja Izek adanena kale kuti ndiwe Galu kwabasi,,,,,,Brian Banda iwe ndi 1
@salimmkumakumakitombi-yc7pw9 ай бұрын
A Brian muzibweretsa nkuruyu nthawi ndi nthawi .Akapito always speach the truth since 2011
@juneprice58799 ай бұрын
0
@juneprice58799 ай бұрын
😢😂🎉😅😮❤😢
@SheenahMwalabu-iz3pr8 ай бұрын
Daily ndipo samandikwana a kapito ndi mbambande ❤❤😂😂
@rashidmtembo60459 ай бұрын
This guy deserves to come back I really like chilungamo chake
@elton7mponda3979 ай бұрын
Am here because of the DC
@user-bt3qi1gt8b9 ай бұрын
Kuyakhula mwa zeru Malawi munoso muli athu azeru chochi
@chriscollinschanza70829 ай бұрын
This interview is an eye opener 🔥🔥🔥
@user-eb6sb6ie2y9 ай бұрын
This is the best medicine Malawi needs inorder to cure the deadly disease we are suffering from
@user-ki4bl9mm1h9 ай бұрын
Kodi Mr chakwera amaonera Times TV?
@mphatsomhoney38769 ай бұрын
I like the guy for he can talk wisely and he seems to know more about running the government and lead him to link with born kalindo for they are talking the same thing lastly I like the way brian is paying attention
@AvellyMamvura-hu3vk9 ай бұрын
Hamayo!!!!!!!!!pali ngamot apa simasewela........mr mulungu akudalisen ndithu.....I LIKE U MR
I love the confidence this man portrays. This is amazing and wonderful.
@Almighty_Shaw9 ай бұрын
Very insightful Mr Kapito
@user-fy5lw8vk9k9 ай бұрын
Mbuzi ndi mbuzi zimzmva kathu.ndiye chakwera
@patrickdecember21119 ай бұрын
Now Mr Kapito is talking, but is he talking this. Out of love of Malawians, or he is not able to eat together with this government as he did with past government. I like that though.
@ririvilla14239 ай бұрын
Kapito and Kalindo our only freedim fighters
@edwardhau66849 ай бұрын
Akapito tayimirani inu tikuvoterani
@user-xz7mo8zy8f9 ай бұрын
Ngati uzingomvetsela.pano ndikumvetsela kachitatu
@Malawinews17 ай бұрын
This guy makes sense
@elizasiwakwe67089 ай бұрын
The best interview ever
@MarvinChilombo.flourish9 ай бұрын
adhawa akuoneka ngati ali serious'tu
@robertkalima34979 ай бұрын
The guy is genius ...he knows what is saying
@jaydee12369 ай бұрын
❤❤❤ brilliant 🎉
@ashadokhomzy57819 ай бұрын
Za nzeru bwana, kuyankhula Koma kumeneku
@chiletsommanga48589 ай бұрын
MR kapito one of best citizen
@leonardjika21009 ай бұрын
A WISE THINKER WILL GOVERN OUR LAND SO HELP ME GOD
@chifundokandani97958 ай бұрын
The best interview of 2023, insightful
@Johnybegood2609 ай бұрын
Kachilungamo kowawa
@BenMononga-en4cc8 ай бұрын
Powerful massage osayang'ana mbali
@jameskadete21969 ай бұрын
Tizayangana track record yomweyo john😊
@rashidmtembo60459 ай бұрын
Umakwanila Big Kapito
@phermade10009 ай бұрын
Hello Malawi
@masterkachingwe74489 ай бұрын
Kuyankhula zolungama zenizeni
@hopesato8 ай бұрын
Kapito is real freedom fighter
@princedavidmapiri28769 ай бұрын
I think chakwera agopanga rising watikwana zeedi
@zondanitzulumusicfly.52029 ай бұрын
We want people like this one in Malawi, even here in Zambia.❤❤❤❤❤
@juliuschiona94628 ай бұрын
Our prayer is that Kapito shud continue to unfold the stupidity that the Govt does😊
@MalawiMediaBaseАй бұрын
Machine 🙌🔥👏
@user-hb2hr5oc9l9 ай бұрын
chimene ndachiona ine palibe chingachitike chifukwa ndalama okuyika nthumba mwawo ife basi khani ndi iyi basi😢😢😢😢
@user-nf3ik3ff6y9 ай бұрын
Zoona big man ❤
@user-ki4bl9mm1h9 ай бұрын
Apo mkuyooya chilungamo
@LuckyChucky-vd8vg9 ай бұрын
John kapito ndi kumtunda amwene!!
@SheenahMwalabu-iz3pr8 ай бұрын
Komatu uncle a Kapito ndimbambande eee the way amalankhuliratu zachilungamo zokhazokha osaona mbal, dzina olo chipani. ❤❤😂😂
@amoschisisi20708 ай бұрын
This man is great
@user-sp8nt2zk1d9 ай бұрын
I like kapito
@christophermatemba22419 ай бұрын
❤
@user-mo7cj2yn6h9 ай бұрын
Boma la akhutukumve ndlimeneli ndipo palibe chomwe akusonyeza kut amvere malangizo ayi boma la zitsilu
Osati kuwona koma nakhumwa ndi wa mcp galu ujaa , bola peter basi ..osati mcp
@razackadan71209 ай бұрын
Mr. Kapito is a brave man. He never side with any government. He offered constructive criticism on UDF, DPP and now MCP regimes. Unfortunately they don't listen instead they brand him as merely an opposer.
@mcdonaldchakwira31459 ай бұрын
Kapito the boy, he is ready 😅
@angelicajoseph30809 ай бұрын
😭😭😭
@LoydBanda-tt3zp9 ай бұрын
Dziko likufunika anthu a economics osat aliyese
@phillipkapata37909 ай бұрын
Kapito 2025 vice President of Malawi😅😅😅
@MasroorJafar-hg3wv9 ай бұрын
Tag Mr president
@leonardwadi91489 ай бұрын
Aa achapondawa kwapasa mpando onona awa sangayankhure zimenezi, analipo anzao
@user-hd5id5mh4o9 ай бұрын
Big man
@anthonyjimu83549 ай бұрын
Kulankhulankoma uku Kothandiza kusintha dziko apo biii aaaaa mavuto okhaokha ndiatsogoleri osadziwa zochita zachuma sazidziwa dziko Liye da bwanji?
@user-my5jj5we5j4 ай бұрын
Inu kapito lowani mutenge usogolel ine vot yanu
@godfreymopiwa-yj5zv8 ай бұрын
panakambidwa zinthu
@frightonemataka90209 ай бұрын
Koloviko
@suzgongwira7919 ай бұрын
Kapito kapito kulongola too much. Tazayesaniko u president please
@user-rk3gq7gd8f7 ай бұрын
Chakwera ndi bulutu
@charlessakwata73199 ай бұрын
Ok kunena zoona dziko likufunika chilima ili
@welcempira29109 ай бұрын
Ndipo serious. Vice wake Kapito 😂😂
@charlessakwata73199 ай бұрын
Chifukwa tawonani since chilima ananena zama reform anthu amadana naye
@oneprophetMathewschisale9 ай бұрын
vuto achakwera sakudziwa kuti alikuti akuwona ngati anakalibe ku church akumbutsen ndikupemphela kuti mulungu alange achakwera pamodzi ndi igwira nawo ntchito atuluke mabala kusana lalikulu