UTHENGA OPITA KU TONSE ALLIANCE BON KALINDO 11 July 2024

  Рет қаралды 10,471

HOT 265

HOT 265

22 күн бұрын

Пікірлер: 64
@Nelsonmatenda
@Nelsonmatenda 19 күн бұрын
Bon kalindo akutiyankhulila anthu osawukafe we love you❤
@Nelsonmatenda
@Nelsonmatenda 19 күн бұрын
Our own president kalindo you stand with poor people
@DineMaku-p7e
@DineMaku-p7e 19 күн бұрын
Mmakwa boss
@Mphatsochibweya
@Mphatsochibweya 18 күн бұрын
Since democracy came in I have never heard anything good from the people about ours leaders leaders here in malawi and Africa as a continent. The main reasons are regionalism, tribalism and favoritism. Kalindo has one or two of these effects that is why noising much .
@user-hl3xi3ok9g
@user-hl3xi3ok9g 20 күн бұрын
Bon keep on fighting for the good of Malawians imagine ku Queens zoyezera malungo kulibe at 60years please
@HassanIzaya
@HassanIzaya 19 күн бұрын
Bon kalindo amakwanila kwambili ❤❤❤
@user-bq1mb4fk1b
@user-bq1mb4fk1b 20 күн бұрын
Thank you so much Mr Bon kalindo for your information ❤❤
@BenMasangano
@BenMasangano 20 күн бұрын
From njeza village T/A mabuka central Africa malawi mwana woopya kwambiri ndipo sindiopa
@PhillipLuhanga-e6t
@PhillipLuhanga-e6t 19 күн бұрын
Wisely spoken
@JafaliAjusa-zg2xi
@JafaliAjusa-zg2xi 20 күн бұрын
Big up Mr kalindo
@dontreybanda278
@dontreybanda278 20 күн бұрын
Powerful massage massage
@GloryLouis-x2l
@GloryLouis-x2l 19 күн бұрын
Apa president wa anthu osauka wayooya eeeee
@DepsyNkosi-r2d
@DepsyNkosi-r2d 19 күн бұрын
koma tu zinganizo znazitu president i hope sakuzwa ai
@FrancissKenneth
@FrancissKenneth 20 күн бұрын
Mumakwana bg 💪
@dorcasmwale6328
@dorcasmwale6328 20 күн бұрын
tikuyamikileni potitsegula mitu
@MapandoJoseph
@MapandoJoseph 19 күн бұрын
Pano ndifuna ndikuyamike Bone ungoyambisa chako ife tikisata
@Nelsonmatenda
@Nelsonmatenda 19 күн бұрын
Makolo ankatiuza kuti mcp ndiyoophya now pano tawonano
@Homeofpeace321
@Homeofpeace321 20 күн бұрын
Kell kay nanja lake lasokonekela
@chimwemwepitros5067
@chimwemwepitros5067 20 күн бұрын
Dc
@ClementKampaka
@ClementKampaka 20 күн бұрын
😂😂 komalizako eee sikusinja ndi gwenembe
@user-zk7jw9up6m
@user-zk7jw9up6m 20 күн бұрын
Kkkkk kkkk koma The DC
@GraceZumazuma
@GraceZumazuma 20 күн бұрын
Anapha m'bale wake chifukwa chofuna kulamula Malawi mpaka 2060 akuti hehehe yomweyo chikangawa
@PatrickNkumba
@PatrickNkumba 20 күн бұрын
Sure
@masterkaselema6396
@masterkaselema6396 19 күн бұрын
Opoila uyu
@frankchirwa2301
@frankchirwa2301 20 күн бұрын
Vuto ndife amalawi kupusa zinthu ziku onongeka wanthu ali mphee.
@TemboHaswell
@TemboHaswell 20 күн бұрын
Km ineyo bone kalindoyi ineyo ndimamuda km nkhani akukambayi ndiyoona tizichita kugula Kaye kuboma nchenga 😂😂😂 kenaka kwamavenda noo this is not fair
@BarnesMwase
@BarnesMwase 20 күн бұрын
Koma kalindo ndi 1 kkkkkkkk
@user-hl3st3cc4v
@user-hl3st3cc4v 20 күн бұрын
Agalu achabe chabe awa ndipo anthu atope naye chakwera
@samhussen708
@samhussen708 20 күн бұрын
Gwenembe😂
@anthonynkhoma4265
@anthonynkhoma4265 20 күн бұрын
Kalondo ndi mbuzi yamunthu. Amandinyasa. Ameneyu sakudziwa kuti akubzala mbewu yachabe.
@user-re7fo3be2z
@user-re7fo3be2z 20 күн бұрын
Iwe mutu uwumawo do you think zikutisangalasa ifeyo nkhope yonyasayo
@brightkaunda920
@brightkaunda920 20 күн бұрын
Ngat kalindo ali mbuzi yamunthu iweyo ukhala ndani?
@marryphili5419
@marryphili5419 19 күн бұрын
Boma ili ndilopenga misara pompano ananena Kuti tisiye kudya nsima yoyera panopa akuti anthu asiye kuvuwura chenga pokhapokha atenge chilolezo Kodi ndarama zamisokho zachepa panopa mukufuna zamuchenga shame on you MCP
@PemphorafaelBasilio
@PemphorafaelBasilio 20 күн бұрын
Ya komadi e
@MathewsBenard
@MathewsBenard 20 күн бұрын
Adapenga uyu kuchita kunenerela kut kufuna kumangidwa ndiye tinene kut akamatuluka kupolisi amalandila ndalama eti
@user-ty1vq9lq6w
@user-ty1vq9lq6w 20 күн бұрын
Ayamba kulimbana ndi anthu osauka ndipo ziwanda zimenezi zalitenga dziko ngati ndi lao, zikanthidwa ndi zanja la Mulungu pompano
@user-re7fo3be2z
@user-re7fo3be2z 20 күн бұрын
Mpaka ntchenga koma eish
@ChikumbutsoDzukwa
@ChikumbutsoDzukwa 20 күн бұрын
Akuonjeza tsopano
@JafaliAkimu-ll1bf
@JafaliAkimu-ll1bf 20 күн бұрын
chakwera ndi chigawenga boma la mbava ili boma la zitsiru zokha zokha chakwera pantumbo pa make chitsiru mbava
@JozzyNthinda
@JozzyNthinda 19 күн бұрын
Km aonjeza achoke mbomamo palibe akupanga km ukakwatila umadalila makolo kd
@ProsperBanda-ju2mq
@ProsperBanda-ju2mq 20 күн бұрын
Koma mumapitadi ku vep bwana
@user-ln3zx6wo4w
@user-ln3zx6wo4w 20 күн бұрын
Chifukwa chadyera 😂😂
@user-sk3ld2ss7s
@user-sk3ld2ss7s 20 күн бұрын
A Malawi, chomwe mumafuna sichidziwika, mumatangwanidwa ndi kuchitira m'sanje president ndi chipani cholamula, presidente akakwera udindo amakhala oyipa kwayinu, Kodi mumafuna president otani?
@dalitson3558
@dalitson3558 20 күн бұрын
Aside kuba ndalama zamalawi
@GabrielAdson-x6t
@GabrielAdson-x6t 20 күн бұрын
Inu dzimvereni chisoni inuyo.Mukamawona usi mukumamva bwanji.Inuyo akalindo ngati achibale anu ngati ali anzeru bwanji osakutengani akakuwoneni kaganizidwe sikalibwino
@user-hm9nc7lz6e
@user-hm9nc7lz6e 20 күн бұрын
Utsi watani munthu oipa mtima umapereka chilima mmanja mwa cakwera kuti amuphe ukuona ngati amalawi sitikudziwa bon kalindo sanaphapo munthu alibe magazi mmanja sanalowepo satanic ndipo usanalakhule udziganiza wamva anthu ambiri timamukonda kalindo ndi munthu yekhayo yemwe amatitothonza udzikamuudza
@brightkaunda920
@brightkaunda920 20 күн бұрын
Bon kalindo musamamufanizile ndi usi chifukwa kalindo alibe dyera koma awo mukuti awusiwo ndi adyera
@samhussen708
@samhussen708 20 күн бұрын
Mbuzi iwe usi Nd chigananga
@dalitson3558
@dalitson3558 20 күн бұрын
Galu iwe ungafanizile Bon Kalindo ndi utsi what kind of you human being are you?
@JohnConar-kq4hi
@JohnConar-kq4hi 20 күн бұрын
The DDDDDDDDDCCCCCCCCCCCC 🤔 🤔
@StainDandize
@StainDandize 20 күн бұрын
😂
@user-gj4li2gc8o
@user-gj4li2gc8o 20 күн бұрын
Kodi amwene simukutopa mene munayambira aanzako Ali phee kuyendesa ziko
@user-hm9nc7lz6e
@user-hm9nc7lz6e 20 күн бұрын
Adzatopa cakwera akadzacoka kapema kusitha maganizidwe ace onyasa chifukwa anthu ambiri itikuona ubwino wachakwera chimene tikuona mwacakwera ndi kupha kuononga ndi kusakadza mmm cakwera munthu oipa ukamuudze wamva ndi iweyo
@TemboHaswell
@TemboHaswell 20 күн бұрын
Sangatope ameneyi chifukwa dzikoli eliyense akusata chamba atsogoleli akasiya kusuta nayeso asiya
@brightkaunda920
@brightkaunda920 20 күн бұрын
Akulimbana ndi inuyo a mcp kut musiye kuzunza amasiyewo
@actuarialscience2283
@actuarialscience2283 20 күн бұрын
Pamene ndimapemphera kupempherera dziko la Malawi ndinaona thambo la ziwanda. Tsiku lililonse limene Chakwera akilamula zithu ziwanda zikulowa m'Malawi. Mupemphere kuti Chakwera asadzawine. Chakwera ndi wa satanic.
@LukiahShaime
@LukiahShaime 20 күн бұрын
Tingomenyana yamanja basi
@robsontyg3928
@robsontyg3928 20 күн бұрын
Shitombo shag'wako bon mathanyula
@reggieanthony7508
@reggieanthony7508 20 күн бұрын
Matlamela a ng'uako nawenawe Robson nyompfi wako
@robsontyg3928
@robsontyg3928 20 күн бұрын
@@reggieanthony7508 hunro nayar
@user-lk8kj9zv6x
@user-lk8kj9zv6x 20 күн бұрын
Dangerous Child
@Homeofpeace321
@Homeofpeace321 20 күн бұрын
Komatu chakwela wafika pauchitsilu
@juliussamson6212
@juliussamson6212 19 күн бұрын
NDIMAGANIZA KUTI MWINA INU A UTM KUTI MAGANIZA NGATI ANTHU INU CHAKWERA ANAPHA CHILIMA LERO MUPANGASO ZAMGWILIZANO NDI SATANA MUGANIZA KUTI ASIYA KUPHA NOSE AKUPHA INUYO A UTM MUTHA
@user-zk7jw9up6m
@user-zk7jw9up6m 20 күн бұрын
Mfundo za boma zikakhale za nchenga koma mcp mwasowa zokambilana
MANGANYA VS AKWENI - KWAPHULIKASO INA KU UTM
13:37
Makosana
Рет қаралды 9 М.
A teacher captured the cutest moment at the nursery #shorts
00:33
Fabiosa Stories
Рет қаралды 45 МЛН
DAD LEFT HIS OLD SOCKS ON THE COUCH…😱😂
00:24
JULI_PROETO
Рет қаралды 16 МЛН
Пранк пошел не по плану…🥲
00:59
Саша Квашеная
Рет қаралды 6 МЛН
A Michael Usi Inu Si A UTM - Lyton Mangochi
23:13
Nyasa VoiceBox
Рет қаралды 17 М.
BON KALINDO KUNG'ALULASO LERO PA 31 July 2024
14:25
HOT 265
Рет қаралды 12 М.
EXCLUSIVE INTERVIEW WITH BON KALINDO
59:52
Zodiak Malawi
Рет қаралды 49 М.
The Day Ronaldinho Became a Barcelona Legend
15:14
BR7 Football
Рет қаралды 3,6 МЛН
נאומו המלא של רה"מ נתניהו בקונגרס האמריקני
53:36
כאן | חדשות - תאגיד השידור הישראלי
Рет қаралды 250 М.
A teacher captured the cutest moment at the nursery #shorts
00:33
Fabiosa Stories
Рет қаралды 45 МЛН