Bon kalindo akutiyankhulila anthu osawukafe we love you❤
@Nelsonmatenda19 күн бұрын
Our own president kalindo you stand with poor people
@DineMaku-p7e19 күн бұрын
Mmakwa boss
@Mphatsochibweya18 күн бұрын
Since democracy came in I have never heard anything good from the people about ours leaders leaders here in malawi and Africa as a continent. The main reasons are regionalism, tribalism and favoritism. Kalindo has one or two of these effects that is why noising much .
@user-hl3xi3ok9g20 күн бұрын
Bon keep on fighting for the good of Malawians imagine ku Queens zoyezera malungo kulibe at 60years please
@HassanIzaya19 күн бұрын
Bon kalindo amakwanila kwambili ❤❤❤
@user-bq1mb4fk1b20 күн бұрын
Thank you so much Mr Bon kalindo for your information ❤❤
@BenMasangano20 күн бұрын
From njeza village T/A mabuka central Africa malawi mwana woopya kwambiri ndipo sindiopa
@PhillipLuhanga-e6t19 күн бұрын
Wisely spoken
@JafaliAjusa-zg2xi20 күн бұрын
Big up Mr kalindo
@dontreybanda27820 күн бұрын
Powerful massage massage
@GloryLouis-x2l19 күн бұрын
Apa president wa anthu osauka wayooya eeeee
@DepsyNkosi-r2d19 күн бұрын
koma tu zinganizo znazitu president i hope sakuzwa ai
@FrancissKenneth20 күн бұрын
Mumakwana bg 💪
@dorcasmwale632820 күн бұрын
tikuyamikileni potitsegula mitu
@MapandoJoseph19 күн бұрын
Pano ndifuna ndikuyamike Bone ungoyambisa chako ife tikisata
@Nelsonmatenda19 күн бұрын
Makolo ankatiuza kuti mcp ndiyoophya now pano tawonano
@Homeofpeace32120 күн бұрын
Kell kay nanja lake lasokonekela
@chimwemwepitros506720 күн бұрын
Dc
@ClementKampaka20 күн бұрын
😂😂 komalizako eee sikusinja ndi gwenembe
@user-zk7jw9up6m20 күн бұрын
Kkkkk kkkk koma The DC
@GraceZumazuma20 күн бұрын
Anapha m'bale wake chifukwa chofuna kulamula Malawi mpaka 2060 akuti hehehe yomweyo chikangawa
@PatrickNkumba20 күн бұрын
Sure
@masterkaselema639619 күн бұрын
Opoila uyu
@frankchirwa230120 күн бұрын
Vuto ndife amalawi kupusa zinthu ziku onongeka wanthu ali mphee.
@TemboHaswell20 күн бұрын
Km ineyo bone kalindoyi ineyo ndimamuda km nkhani akukambayi ndiyoona tizichita kugula Kaye kuboma nchenga 😂😂😂 kenaka kwamavenda noo this is not fair
Ayamba kulimbana ndi anthu osauka ndipo ziwanda zimenezi zalitenga dziko ngati ndi lao, zikanthidwa ndi zanja la Mulungu pompano
@user-re7fo3be2z20 күн бұрын
Mpaka ntchenga koma eish
@ChikumbutsoDzukwa20 күн бұрын
Akuonjeza tsopano
@JafaliAkimu-ll1bf20 күн бұрын
chakwera ndi chigawenga boma la mbava ili boma la zitsiru zokha zokha chakwera pantumbo pa make chitsiru mbava
@JozzyNthinda19 күн бұрын
Km aonjeza achoke mbomamo palibe akupanga km ukakwatila umadalila makolo kd
@ProsperBanda-ju2mq20 күн бұрын
Koma mumapitadi ku vep bwana
@user-ln3zx6wo4w20 күн бұрын
Chifukwa chadyera 😂😂
@user-sk3ld2ss7s20 күн бұрын
A Malawi, chomwe mumafuna sichidziwika, mumatangwanidwa ndi kuchitira m'sanje president ndi chipani cholamula, presidente akakwera udindo amakhala oyipa kwayinu, Kodi mumafuna president otani?
@dalitson355820 күн бұрын
Aside kuba ndalama zamalawi
@GabrielAdson-x6t20 күн бұрын
Inu dzimvereni chisoni inuyo.Mukamawona usi mukumamva bwanji.Inuyo akalindo ngati achibale anu ngati ali anzeru bwanji osakutengani akakuwoneni kaganizidwe sikalibwino