Watondeka; Chitukuko kulibe ku Malawi; Fetereza wadura kwambiri

  Рет қаралды 42,087

Bakili Muluzi TV

Bakili Muluzi TV

Ай бұрын

Пікірлер: 243
@IshmealSaidi-kw6pd
@IshmealSaidi-kw6pd Ай бұрын
We miss you bakili muluzi tv, it's been two days without you😢
@jogechawa6192
@jogechawa6192 Ай бұрын
I hope he is okay asatipheleyi
@abisalomchunga6695
@abisalomchunga6695 Ай бұрын
Timuikize mumanja mwa ambuye
@Homeofpeace321
@Homeofpeace321 Ай бұрын
Amene simunva chitumbuka akuti, Chakwela ndi Chule, Chilima Ndijoka
@MacmillanMakombe-sz4iy
@MacmillanMakombe-sz4iy Ай бұрын
😂😂😂😂😂
@harrymicah6140
@harrymicah6140 Ай бұрын
Kakakakak mmmm
@raytavares2256
@raytavares2256 Ай бұрын
Bodza akuti iwowa abusa MM anali mkati mwakasupe wamadzi koma ukakamiza chule akuthawa mmadzi mom amakhala ataona njoka mmadzi mom, he means that he him escape the serpent. Tell people the truth.
@BrownMainje-sh7hj
@BrownMainje-sh7hj Ай бұрын
Kkkkk inbox me please
@user-yb1nt9te7f
@user-yb1nt9te7f Ай бұрын
We need back our guy 😭😭😭
@Yabwata
@Yabwata Ай бұрын
Please 2025 vote for pm plz kuzabayizika yayo plz kumupoto kwi2 uko plz ,Only pm can rescue us, and plz brother tell us about vote here in SA how didi it go ,I wish DA could win.
@user-ro9sh3vp6j
@user-ro9sh3vp6j Ай бұрын
Hi boss we miss you y are quite
@macbestermtonga3015
@macbestermtonga3015 Ай бұрын
Ku Malawi anthu amadalira nsima sopano ngati fetereza akudula anthu otsaukafe tipanga bwanji? Mumidzi muli azigogo okalamba angagule? Mulungu akulangani ndithu pulezidenti wakuba Chakwera mbuzi ya munthu
@princedetbozsmallboy1749
@princedetbozsmallboy1749 Ай бұрын
Kodi akulu anakumangani 😢😢 mwasowatu tikusowa nkhani zeni zeni chonde wonekani😢
@DONNEXKhama-bk1gy
@DONNEXKhama-bk1gy Ай бұрын
Dpp is only our hope especially APM the best man
@user-pn7cj9hb3t
@user-pn7cj9hb3t Ай бұрын
Palibeso wina
@hanifahmponda8711
@hanifahmponda8711 Ай бұрын
Big man B muludzi TV 💪💪💪
@HallimaMakwinja
@HallimaMakwinja Ай бұрын
Zoonadi ifetu tivotera Dpp kapena Udf basi
@davenchimadzi6529
@davenchimadzi6529 Ай бұрын
😂 tilipambuyopo
@user-ln3zx6wo4w
@user-ln3zx6wo4w Ай бұрын
Or kuno kumpoto ndi chihana ndi peter basi
@mphandeEmmanuel-re5rc
@mphandeEmmanuel-re5rc Ай бұрын
I already miss the nice voice
@user-ix7pb6hk2w
@user-ix7pb6hk2w Ай бұрын
Perfect one
@kubengovender6996
@kubengovender6996 Ай бұрын
Big up brother man!!
@user-xi4pi9qy4l
@user-xi4pi9qy4l Ай бұрын
Thank you brother kk
@John-to8gl
@John-to8gl Ай бұрын
Powerful message 🙏
@TimbaTv001
@TimbaTv001 Ай бұрын
Sinnabotepo ulendo uno ndi vote apm my vote
@user-ro9sh3vp6j
@user-ro9sh3vp6j Ай бұрын
I wish you a safe and happy and good life boss
@webstermbewe8395
@webstermbewe8395 Ай бұрын
Thanks for the update on the video
@MoffatLanjesi
@MoffatLanjesi Ай бұрын
Best ever tv dankie
@collennyadile8179
@collennyadile8179 Ай бұрын
zose zomwe akunena anthu awa ndi chilungamo ndipo chakwera wakhumudwitsa anthu ambiri koma ine chakwera ndinaziwa kuti ndi wankhaza
@MphatsoMphatso
@MphatsoMphatso Ай бұрын
Big up raster
@user-it5zv2nz7f
@user-it5zv2nz7f Ай бұрын
Ndiwe katundu br God's time is the best,all the best
@saidichirwa5456
@saidichirwa5456 Ай бұрын
Brother usasiye kuyika mavideo awa amve kuwawa pomwe tikupita ku mavote next year.
@eliaskhofielias8152
@eliaskhofielias8152 Ай бұрын
Apm awina posakaikanso ayi.anthu momwe mumkamuvotera chilima ndikumat mfana oganizo booh ogonaniza mopusa bas and ndichitsilu kwambili anapusitsa mbuli zinzake zomwe anamvoterayo zianyani zopanda wisdom from GOD.kukavotera anthu makape ngat amenewa bas.amalawi ndife opusa kwambili tinapusitsidwanso ndi azitsogoleri ampingo ndiomwe amati tikawavotele mbalamezi zitsilu zachabe chabezi mxiiiii.
@user-xm5cq1fb8g
@user-xm5cq1fb8g Ай бұрын
❤❤❤Ulemu wanu big
@user-is5dl7np9g
@user-is5dl7np9g Ай бұрын
Peter mutharika akatundu
@user-oc9vl9xz8e
@user-oc9vl9xz8e Ай бұрын
This good speech
@stanleykaludzu-bm4pm
@stanleykaludzu-bm4pm Ай бұрын
Apm My vote
@IsaacMusa-py2jm
@IsaacMusa-py2jm Ай бұрын
Powerful 👊 👊
@JerryChain-cz8ru
@JerryChain-cz8ru Ай бұрын
APM ❤
@user-nf3ik3ff6y
@user-nf3ik3ff6y Ай бұрын
Good message ❤Bakili Tv
@ishakatimbe7341
@ishakatimbe7341 Ай бұрын
Adad woyeeee
@InnocentAssan-st3hb
@InnocentAssan-st3hb Ай бұрын
Big man Peter
@SibwenzaLevisoni-gm6rv
@SibwenzaLevisoni-gm6rv Ай бұрын
More fire 🔥 asambiseni anthu oipa
@user-cz6sd6fh7n
@user-cz6sd6fh7n Ай бұрын
Bwana wathu kodi mulikuti imfe tiri wodandawula kwambiri sitikuwona video new one😢😢
@McfrankJackson
@McfrankJackson Ай бұрын
Voice ya bigy zkutibwaaaa
@AuffiPillo-cf9rn
@AuffiPillo-cf9rn Ай бұрын
Best TV ever
@HappyAbyssinianCat-xt2bm
@HappyAbyssinianCat-xt2bm Ай бұрын
Km ine ndili ku south Africa chaka cha mawa ndkubwera kuzavota kumalawi ndpo chakwera uyu sindkumufuna ndizavotera adad tikufuna nsima ife feterez ndamene timafuna❤
@LysonMtalika-tb6fk
@LysonMtalika-tb6fk Ай бұрын
Powerful!!! 💪
@juliochiwalo
@juliochiwalo Ай бұрын
Mmalawi wa nzeru uyu
@abrahammwekinda9605
@abrahammwekinda9605 Ай бұрын
Hie Mr new presenter. Mukanakwezako mawu kuti tizimva bwino. My phone is at maximum volume but still am struggling to hear clearly.
@kingsleyhopematchaya5184
@kingsleyhopematchaya5184 Ай бұрын
Ndiye ku Zambia Mozambique Tanzania anakweza ndi chakwera kod tiziti ndivhiyani mumanganiza athunu or apm akanakhalapo akanakwera anakwera dziko lapasi
@honourablemcgregorysc97tv
@honourablemcgregorysc97tv Ай бұрын
Best Ever TV
@Razarusmbavachakwera
@Razarusmbavachakwera Ай бұрын
Guys I miss bakili muluzi tv 📺 where is our best journalist it's been a while
@chigokhalid9420
@chigokhalid9420 Ай бұрын
Lero akulankhulayu nde uti?
@UNIMAMOMENTS123
@UNIMAMOMENTS123 Ай бұрын
amene akuyankhulayu sakukumesa aaaaa
@AustinChiyembekezo-cx4mz
@AustinChiyembekezo-cx4mz Ай бұрын
Dzika yokhuzidwa
@sebi2439
@sebi2439 Ай бұрын
Boss tapangani check in mukusowatu, muli kutiko
@Kay-racle_mw
@Kay-racle_mw Ай бұрын
Best TV
@jogechawa6192
@jogechawa6192 Ай бұрын
BM tv takusowani koma muli bwinobwino?
@isabelmartin7567
@isabelmartin7567 Ай бұрын
Bakili muluzi please come out we need you this time please 😭😭
@user-ud6qc9mw7b
@user-ud6qc9mw7b Ай бұрын
Where is our man bakili muluzi tv we miss you too much
@ChifundoNinje
@ChifundoNinje Ай бұрын
Apm my vote
@marryphili5419
@marryphili5419 Ай бұрын
Zoona ife tikufuna Peter munthalika fertilize wunali wosika mapassport anali osavuta makhwara amapezeka muzipatara amapezeka sugar wumapezeka tatopa nazo mbamva izi za MCP
@obledijy280
@obledijy280 Ай бұрын
We miss you bakili muluzi TV when you stay two days no any updates we are very worried..... You make us happy always Mr bakili tv
@robertchitsulo8006
@robertchitsulo8006 Ай бұрын
Best tv
@SinoliaEphraim
@SinoliaEphraim Ай бұрын
Ine ndiye Peter muthalika basi ndimanva naye kukoma muntima mwangamu
@NomsaMsibi-il7ck
@NomsaMsibi-il7ck Ай бұрын
Thakusowa abro
@ishakatimbe7341
@ishakatimbe7341 Ай бұрын
Kod wakulu mulipo?? We miss you
@salimmkumakumakitombi-yc7pw
@salimmkumakumakitombi-yc7pw Ай бұрын
Tonse Alliance iwona za ANC .Paulendo 2025
@evancenasoro922
@evancenasoro922 Ай бұрын
Where are you bakili muluzi😢
@limbiechisaka1027
@limbiechisaka1027 Ай бұрын
Koma adha inu sanakupheni?
@ishakatimbe7341
@ishakatimbe7341 Ай бұрын
Bwana
@TimbaTv001
@TimbaTv001 Ай бұрын
Mulimonsemo koma chakwela asazawinenso 🙏🙏🙏🙏
@MfipaKapwera
@MfipaKapwera Ай бұрын
Ku Northern Region please please kubayiza yayi paluvotelaso Chakwela or MP wa MCP.
@user-kg5lf6bd1g
@user-kg5lf6bd1g Ай бұрын
Peter my vot
@noelnyirenda1117
@noelnyirenda1117 Ай бұрын
Kodi munasiya boss kusakatula history takusowani
@moyo77777
@moyo77777 Ай бұрын
🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥💪💪
@actuarialscience2283
@actuarialscience2283 Ай бұрын
May the Lord bless DPP and curse MCP. In the name of the Lord MCP shall go down and their place shall never be there.
@user-pn7cj9hb3t
@user-pn7cj9hb3t Ай бұрын
Amen
@MuhammadBAKILI-kl2mj
@MuhammadBAKILI-kl2mj Ай бұрын
Koma Bakiri muluzi TV ndayisowa bwanji
@user-px9jd9co3v
@user-px9jd9co3v Ай бұрын
A space of 4days without hearing your voice seems like a decade What next our ears should hear of bro?
@hastingselia1060
@hastingselia1060 Ай бұрын
Aise tipatse update kapena naweso waphulitsidwa 😢
@MBOGEZMuhammad
@MBOGEZMuhammad Ай бұрын
❤❤❤❤
@takondwaakamunachilimba4478
@takondwaakamunachilimba4478 Ай бұрын
3 days now without a video. Bakili muluzi TV are you there?
@juliochiwalo
@juliochiwalo Ай бұрын
Mmalawi uyu amaona zinthu patali ngwamasomphenya zedi
@WhiteRichard-cw2fo
@WhiteRichard-cw2fo Ай бұрын
APM vote 🥰
@CharliePaulelic
@CharliePaulelic Ай бұрын
Bakili muluzi tv are you there????
@GraceLimani-zw7dx
@GraceLimani-zw7dx Ай бұрын
Saulosi zibambo wa sweat talk pano ati uza chani kaya pa campaign ya ulendo wuno
@HaroldBanda-lk2dx
@HaroldBanda-lk2dx Ай бұрын
Ozelezeka adzavotera winayo,pano ndakonza kale ndifika ndilime wambiri Chaka cha mawa ndigura galimoto Chaka cha mawa ndi 4$
@HenryLaidon-pl9ly
@HenryLaidon-pl9ly Ай бұрын
Koma president uyuyu, anayimbira mfiti mmanja. Dziko lili pheeee eeeee eee, andale aku Malawi
@MuniraCassim
@MuniraCassim Ай бұрын
But I miss your voice big man
@ceciliamastala6824
@ceciliamastala6824 Ай бұрын
Where are you it's been 3 days
@Elvin-dr8tv
@Elvin-dr8tv Ай бұрын
Chakwera Timuleke ngwakutangwanika uyo😅😅
@actuarialscience2283
@actuarialscience2283 Ай бұрын
Kodi bwana Bakili Muluzi TV mulikuti😥😥
@user-qq1uj7ct6n
@user-qq1uj7ct6n Ай бұрын
chakwera ndi nsogoleri weni weni wasatanic. ndipo amene akuyamikira utsogoleri uwu... ameneyoyo simunthu kut umunthu alinawo ameyo Mmmmm ndimfiti
@HassanMbalaka-gb5sv
@HassanMbalaka-gb5sv Ай бұрын
Thats it
@precioustauzi4777
@precioustauzi4777 Ай бұрын
Akulu mwasowatu mwina akumanganitu cz aaah sizoona
@samsonmtumbati4855
@samsonmtumbati4855 Ай бұрын
Chakwera ndi chilima mbava za anthu adabwera kudzaononga dziko la Malawi
@ApocheC.
@ApocheC. Ай бұрын
Bwana Koma mulipo ziii ameneyu? Plz yankhani
@esthergweje4038
@esthergweje4038 Ай бұрын
Zoona ndipo Atati tivote lero ayi ndithu ine ndingakondwetu
@FosterMoyo
@FosterMoyo Ай бұрын
We're is this guy baliki muluzi why quite big man
@josephndalama5494
@josephndalama5494 Ай бұрын
Rumours has it that it was being run by Ralph kasambala
@thomaszulu7099
@thomaszulu7099 Ай бұрын
Kodi bakili muluzi TV anamugwila sakukutulusa ma letest
@shadrecknyalugwe2368
@shadrecknyalugwe2368 Ай бұрын
Ineso ndikudabwatu kwangoti ziiiii
@user-fu3ew9lv5v
@user-fu3ew9lv5v Ай бұрын
Anthu onse amene anabatizidwa ndichakwera akabatizidwenso kawiri,chakwera simunthu wa Mulungu ayiiiii
@OZIELBLESSINGS
@OZIELBLESSINGS Ай бұрын
Let me enjoy today's update 🎉❤
@user-ro9sh3vp6j
@user-ro9sh3vp6j Ай бұрын
Maybe the dictator have taken you boss
@EmilyBanda-xx8gd
@EmilyBanda-xx8gd Ай бұрын
Ndipo even chilima asakunamizeninso amalawi anzanga tiyeni ku DPP
@user-pn7cj9hb3t
@user-pn7cj9hb3t Ай бұрын
Awuze
@hastingsmunthali4298
@hastingsmunthali4298 Ай бұрын
Even panopa ku Jon kukuwawa chifukwa chachibwana awa akutcha apuledetiwa e.g fertilizer in 3 ago 100 thousands amagula 4 bags koma pano just the period of 3 years zikufunika kutumiza 500 zowawa kwambiri.
@user-dk6nk7hx5q
@user-dk6nk7hx5q Ай бұрын
Koma akuluwa alipo sathatu 2days opanda video ananjatidwa kapena 😢😢😢
@christophergondwe6562
@christophergondwe6562 Ай бұрын
8 days bro mwatiyiwala2. daily. bundle timagula bcouse ov u bro
@peterjim6810
@peterjim6810 Ай бұрын
No any updates for 6 days now are you arrested?
@AffickChaona
@AffickChaona Ай бұрын
Ulendo uno anthu avota malingana ndi zimene aona osati kunva Best TV in Malawi bakiri Muluzi TV
@davenchimadzi6529
@davenchimadzi6529 Ай бұрын
Kodi mwini voice mulipo big? Kapena akupezani a MCP aja😢
WHO LAUGHS LAST LAUGHS BEST 😎 #comedy
00:18
HaHaWhat
Рет қаралды 21 МЛН
I Can't Believe We Did This...
00:38
Stokes Twins
Рет қаралды 109 МЛН
When You Get Ran Over By A Car...
00:15
Jojo Sim
Рет қаралды 29 МЛН
LIVE: President Biden delivers speech to Nato summit
1:16:46
The Times and The Sunday Times
Рет қаралды 7 М.
Nancy vs Che Nkope - Zikhale Ngoma Kapena Drums?
10:46
CHE NKOPE
Рет қаралды 33 М.
Zomwe Zinachitika Kut Ndege Isowe
5:19
Sam Malvitha
Рет қаралды 168 М.
Atikumbutsa Samora Machel wa ku Mozambique
10:23
Bakili Muluzi TV
Рет қаралды 30 М.
WHO LAUGHS LAST LAUGHS BEST 😎 #comedy
00:18
HaHaWhat
Рет қаралды 21 МЛН