No video

Zina mwa zifukwa zikubweretsa mavuto ku chipani cha DPP

  Рет қаралды 51,898

Bakili Muluzi TV

Bakili Muluzi TV

Күн бұрын

Пікірлер: 219
@rajabumustafa729
@rajabumustafa729 Жыл бұрын
Enanu ngati mukuona kuti zimene akukamba sizikukusangalatsani bas siyan kuvera zokamba zake mukasiya mmalo mwainu apezeka athu 10+ okonda chanel imeneyi
@abe9104
@abe9104 Жыл бұрын
nice answer man
@user-ix4yp5lp8m
@user-ix4yp5lp8m Жыл бұрын
Yes eti MUNTHU OKUTI sizimakusangalatsa koma osadiya kumangolankhulabe haaaaa umbuli CHANI???
@AshrafuBwanali-qi3my
@AshrafuBwanali-qi3my Жыл бұрын
Kod abwana bwanji osapanga press conference anthu tikuziwine you are like professor lumumba 'you talk 👄 reality without fear 😨 and favor your words are full of wisdom
@suprianomgalla5512
@suprianomgalla5512 Жыл бұрын
Ndipo we need to know him mweee😂😂 I can't stop liking this guy
@jamesnzokomera2775
@jamesnzokomera2775 Жыл бұрын
This guy always says only the truth keep it brother
@chrisboyce229
@chrisboyce229 Жыл бұрын
Dausi asapangetu zachibwana ife tili pa mbuyo pa APM ❤❤
@ayamijackson1443
@ayamijackson1443 Жыл бұрын
Exactly BG. On point you never disappointed us respect to you bro
@CelestinoSimaoFrancisco
@CelestinoSimaoFrancisco Жыл бұрын
y_
@user-nf3ik3ff6y
@user-nf3ik3ff6y 3 ай бұрын
Good message Bakili Tv ❤
@tech-portmalawi5676
@tech-portmalawi5676 Жыл бұрын
Great mind.May God bless you bro
@Apschap-re7ch
@Apschap-re7ch Жыл бұрын
Mmatisegula maso bro..keep it up
@user-ix4yp5lp8m
@user-ix4yp5lp8m Жыл бұрын
Apa zanveka bwino tsopano inuyo mumatithandizatu.. ndipo piter ndiwanzeru kwambili
@Patrick-br1fy
@Patrick-br1fy Жыл бұрын
Apapa tadziwa chilungamo chifukwa dausi amaoneka ngat ali pa chilungamo chifukwa chakudziwa kuyakhula
@franciscoduartie5762
@franciscoduartie5762 Жыл бұрын
Its the narrators voice for me mawu a ndiiiiii😅😅
@suprianomgalla5512
@suprianomgalla5512 Жыл бұрын
Chikamati "Eeeeeh! Mkudziwa inu"😂 ine kumtima myaa
@Dickiez99
@Dickiez99 Жыл бұрын
Good job and well articulated❤ Zomveka mvemvemve ndithu.
@vusoacquaron9084
@vusoacquaron9084 Жыл бұрын
APM akuyenera kuyima basi enawa apeze zochita Dausi Nd zizingu zake zija akakhale pansi anthu osafunira zabwino dziko anthu oyipa
@LotiBanda-uo5vy
@LotiBanda-uo5vy Жыл бұрын
Zoti mcp imadalira chuma cha Kamuzu wanama mkulu iwe
@WatsonShawa
@WatsonShawa Жыл бұрын
Akunamadi, nkuluyi ndi wa DPP
@alfredbanda886
@alfredbanda886 Жыл бұрын
Mwini Channel iyi amatha kutambasula nkhani please ndilankhuleni pa Email yangayo ndizikupanga Support uli Ndi Luso kwambiri kumayamika ndibwino
@user-zx1zs8el7q
@user-zx1zs8el7q Жыл бұрын
Ndipo live
@webstermbewe8395
@webstermbewe8395 Жыл бұрын
Thanks for the video a good one boss
@user-jm8ft5dt9n
@user-jm8ft5dt9n Жыл бұрын
Big man inuyo🎉🎉
@hopeskafumbiphiri6011
@hopeskafumbiphiri6011 Жыл бұрын
Mr. Ur number one, vuto anthu ena amangofuna kusokoneza zinthu so ngati akufuna kuti peter azigwilisa ndalama zake nanga mau oti sichipani chake akubwelera pati. chifukwa akudalira ndalama yake Dausi ndinamumva pa Times koma zomwe ankalankhulazo mmmmm zaudani basi
@UssenNjirinah
@UssenNjirinah Жыл бұрын
This guy is agreat guy i
@user-zk5nu5fh6l
@user-zk5nu5fh6l Жыл бұрын
Jealous nde vuto lalikulu mmalawi 😂😂😂
@user-bv3pm1qb7n
@user-bv3pm1qb7n Жыл бұрын
Daus ndiamzake akufuna kusokoneza chipani, adad omweo
@DickMdala-pn4pd
@DickMdala-pn4pd Жыл бұрын
Akumuwopa APM komaso achina nankhumwa alembedwa ganyu
@esaumwanza3524
@esaumwanza3524 5 ай бұрын
No fear no fever straight to point ❤
@josephinemisomali6840
@josephinemisomali6840 Жыл бұрын
Koma kunena zoona interview ya Dausi ndi Brian Dausi ananena kuti APM asayime komano ananena kuti dongosolo lake silinayende ngati mmene chipani chimayenela kuchita ndipo kumapeto ananena kuti alibe vuto ndi APM koma ngati ndi Democracy aperekenso mwayi kwathu ena kaya adzaina APM iye adza support kodi ku DPP kulibeko anthu ena ofuna kupikisana nawo sindikusapota ndausi koma ndimmene ndinamvela pa interview yake
@charlesmuyaya8839
@charlesmuyaya8839 Жыл бұрын
2010 bwanji sanapereke mwayi kwa Joyce Banda? 2018 sanapereke mwayi kwa Chilima. Lero chifukwa apanga endorse ndi anzake basi kuyamba kulira? Ngati unamvera interview ananena kuti membership card isakhalepo kusonyeza kuti anthu asamasonkhe chipani chizithandizidwabe ndi Mutharika
@davenchimadzi6529
@davenchimadzi6529 Жыл бұрын
Anankumwa nd Dausi ngati akuzimva ndalama angotuluka bas ayambise chipani chawo vuto palibe ife zatikwana☹️☹️☹️
@superiormoses4802
@superiormoses4802 Жыл бұрын
Kuswa kuswa bro
@anafieintuka8090
@anafieintuka8090 Жыл бұрын
I will never disappoint you sir
@alicemalika677
@alicemalika677 Жыл бұрын
Very interesting Namkhumwa is failing to stand firm in the Parliament as leader of Opposition but he wants to be reader of Opposition in his own party. Koma ndizidabwitsa bwanji he can win
@user-pt1fy3qg4u
@user-pt1fy3qg4u Жыл бұрын
Never give up ❤
@khalidwetchaua24
@khalidwetchaua24 Жыл бұрын
Apa mwayankhula zoona Bro ,,, Nankhumwa ndi Dausi kunena chilungamo akusokoneza chipani
@Marialongwe-nzlib
@Marialongwe-nzlib Жыл бұрын
Vuto lake Chilungamo Chinayandikana Ndi Mabi😮 Dausi Ayambitse Chake Basi
@luciascharles4345
@luciascharles4345 Жыл бұрын
Izidi zikudabwisa kuti HRDC ikulowa Pati agulu awa ndiyamene ationongela zikoli ,,,inu a HRDC mukapitiliza zomalimbana ndi DPP tikuochelani mmanyumba mwanu Momo
@JeofreyNamalima-yn4tj
@JeofreyNamalima-yn4tj Жыл бұрын
Ife tikufuna apm bas ❤❤❤
@lyiemax
@lyiemax 7 ай бұрын
Dausi ndi Nankhumwa ndi anthu osokoneza kwambiri, we are tired with them
@mkupabanda-nd2vb
@mkupabanda-nd2vb 3 ай бұрын
Best chanel pa dziko lapansi pano
@user-tw2zf7bj3e
@user-tw2zf7bj3e Жыл бұрын
Adad woyeeee
@user-et3il7pi7t
@user-et3il7pi7t 11 ай бұрын
Your are saying the truth brother we need to change the party should be for all 😢 member who are at nec to contribute and surpot The party because they are one of the benefits res okay
@rashidstamburi2705
@rashidstamburi2705 Жыл бұрын
Nkhani yabwino koma adad ayimeso basi nde zomwe tikufuna
@user-kh5ko3ee7h
@user-kh5ko3ee7h Жыл бұрын
Paja awa nga dpp
@alickziba6756
@alickziba6756 5 күн бұрын
Powerful as well
@johnman4619
@johnman4619 Жыл бұрын
Dausi ndi mbuli yazinthu sadziwa ntchito ndipongasanje safuna anzao kuti azimveka Ali .ngati Symon vuwa Kaunda komanso khumbo kachali Sanji twoo much
@user-ne9qn5nm9d
@user-ne9qn5nm9d Жыл бұрын
Let Peter Munthalika to stand l support him forever
@chitimbethegreat-pc1bp
@chitimbethegreat-pc1bp Жыл бұрын
Dausi wagulidwa ndi MCP uyu asatinyase azipita ku MCP ndipo DPP ikuyenera kuchosa mbava ngati zimenezo
@joemlelemba6572
@joemlelemba6572 Жыл бұрын
You are always right bro, dpp for life ndipo nankhumwa, botman ndi dausi ndi osokonedxa we know
@ChipililoWame-lc8ul
@ChipililoWame-lc8ul Жыл бұрын
Dausi ndiwozungulila mutu kumalawi kuno kuli zitsilu
@moffatnsolomba6082
@moffatnsolomba6082 Жыл бұрын
Analysis yanu ya nkhani za Ku Malawi kuno mumakhala ndi mbali....
@user-ix4yp5lp8m
@user-ix4yp5lp8m Жыл бұрын
Daus ndi Nankhumwa ndimbuzi zawanthu...ngati ayambitse chipani chawo Adad bas
@EmercianahKasiku-en6hl
@EmercianahKasiku-en6hl Жыл бұрын
Cadet kulira mokweza dpp sidzalowaso mboma brother
@mafukenimasangwi5487
@mafukenimasangwi5487 Жыл бұрын
Kodi inuyo mmene zinthu zililmu mukuti dziko likuyenda bwino? Anthu akuvutka mmizimutu
@LotiBanda-uo5vy
@LotiBanda-uo5vy Жыл бұрын
Iweyo uli kumbali ya peter mutharika mbuzi
@WatsonShawa
@WatsonShawa Жыл бұрын
Munthu onena chilungamo chothirako bodza ndi wowopsa kuposa yemwe amanena bodza lopanda chilungamo.
@michealchilemba3149
@michealchilemba3149 Жыл бұрын
Nankhumwa akulandira ndalama ku chokera ku Mcp kwa Simbi phiri ndi kwa Chilima kuti Asokoneze DPP
@princedetbozsmallboy1749
@princedetbozsmallboy1749 Жыл бұрын
100% agree with you man
@beatricegulani5602
@beatricegulani5602 Жыл бұрын
Dausi sakulakwisa
@saidichirwa5456
@saidichirwa5456 Жыл бұрын
Bola munthalikayo.Awo asatiputsitse ndimbava zosakhutitsika ayi.Kulibe zimenezo.Iwe tokota osawopa ife umatitokotela history mopeleka chidwi and umakhala ndi maumboni okwanila.
@frezarphiri3480
@frezarphiri3480 Жыл бұрын
Yes ndi zoona kuli gulu Lina likukakamiza APM kt ayime iwe ukumbukile APM 2021 anane yekha kt sazayimeso koma pano anthu awo akumusokoneza APM kt ayimeso ndi zoona izo ???
@petermasenti2084
@petermasenti2084 Жыл бұрын
Akuwopa chiyani amusiye peter azayime , dausi ndiwosokoneza malawi atapoa ndi ulamuliro wa chakwera
@LUCKYM4787
@LUCKYM4787 Жыл бұрын
Zoona bg mn respect ndawi zonse
@actuarialscience2283
@actuarialscience2283 Жыл бұрын
HRDC instead of fighting problems that are making Malawians poor you're busy with APM. This is stupid.
@promisemakawa1556
@promisemakawa1556 Жыл бұрын
U r my hero
@johnman4619
@johnman4619 Жыл бұрын
Komanso adausi akuziwa zambiri zakuphedwa kwamalubinho ndioo adausi ndi nankhumwa komanso Ben botolo anapha alubino uja waku nkhatabay Mr makwenda phiri ndioo adausi ndi tim ya apm yomweyo mulamulilo wao akuziwa adausi kuti zao zidada ku dpp alibe chance
@idrissaKGO
@idrissaKGO Жыл бұрын
Akulakwitsa kutero amusiye anytime piter yemweyo
@ThoccoBondo-mx7vt
@ThoccoBondo-mx7vt Жыл бұрын
Ife timaziwa kale kuti Dausi ndiwosokoneza
@suleimanrabson4367
@suleimanrabson4367 Жыл бұрын
Talking true bro
@user-mz4tk1pw3f
@user-mz4tk1pw3f Жыл бұрын
Dausi Ali ndichibwana kwambiri
@stanleykumwembe4719
@stanleykumwembe4719 Жыл бұрын
Sometimes mtolakhani uyu, amaometsa mbali, khani ija yasokomekeranso…
@jacksontembo1530
@jacksontembo1530 Жыл бұрын
Inenso ndimaona choncho awa azingonena ma history omwewa onsati za ndale
@charlesmuyaya8839
@charlesmuyaya8839 Жыл бұрын
Uyu amanena fact. HRDC inasapota MCP, ndi chifukwa chani akufuna kulowelera zochitika ku DPP amenenso ali adani awo? Ndimawerenga nyuzipepala ina yake HRDC chairperson kumpoto akufuna kupita ku khothi kuti akamuletse APM asayime. Mtolankhani uyu amanena chilungamo chokhachokha man. MCP yapanga endorse Chakwera palibe wanena kuti si democracy. Ena apanga endorse APM akuti si democracy. Mtolankhani uyu ndi 1
@user-ix4yp5lp8m
@user-ix4yp5lp8m Жыл бұрын
Amene mukumasutsana Nayenu NDI mbuziso zawanthu...uyu amalankhula zogwila mtima..zoona zokhazokha
@festongrido3192
@festongrido3192 Жыл бұрын
Zikomo Braz izizi ndinkhondo yomwe akuisaka satidzalora zimenezo
@phillipstamaley7901
@phillipstamaley7901 Жыл бұрын
Lumumba ndi patali abwana just appreciate him not compare with lumumba
@blandinabonaventure
@blandinabonaventure Жыл бұрын
Ayambitse chawo amenewa Dausi ndi nakhumwa yambani chanu please
@dhaoudhiabedinegomaseko2363
@dhaoudhiabedinegomaseko2363 Жыл бұрын
Zitsilu zitatu zimenezi zisokoneza DPP maka uyo wonenepa ngati nkhuku ya vertinary. Ngati akuti Muthalika family azipanga yekha ndiye ali ndi ufulu wambiri even wochotsa anthutu.DPP inaluza coz of Nankhumwa ndi Dausi dyera.HRDC pamsana pano nonse ndinu mwawononga zikoli ndipo ndinu zitsilu musamalowelele za zipani agalu inu
@issabrightsaidibright1274
@issabrightsaidibright1274 Жыл бұрын
Ngani ijaa ndayivesesa sopano APM YEMWEYO
@johnjameskapito5151
@johnjameskapito5151 Жыл бұрын
Dausi ndi mfiti
@quraishmusakatunga1754
@quraishmusakatunga1754 Жыл бұрын
HRDC ikuopa ndipo anyani ameneo azaziona
@cephasnkhoma2301
@cephasnkhoma2301 Жыл бұрын
Thanks: kusonka kwabwino chipani sichingagwe .
@Marialongwe-nzlib
@Marialongwe-nzlib Жыл бұрын
Ubwino wake ife Sitikufuna APM Atibekekere Mwana 😅 Tikufuna Ntchito Zake zibwelere, Osat Wakura Wakura Wakalamba Ngat Akapanga chinkhoswe Ndi Mwana wa 2000
@alexbanda9315
@alexbanda9315 Жыл бұрын
ntchito zake ziti zimenezo?
@user-pf8fh5fp5y
@user-pf8fh5fp5y 8 ай бұрын
Ai asapange zimenezo. Mesa MCP munkati ikulakwa ikamagulitsa member ship card. Ndie zioneke zabwino lero?
@user-gn1xn3js4l
@user-gn1xn3js4l Жыл бұрын
Kumenek ndiye kulangula tisangomenyana basi anthuwa akutenga machasi
@vincentharry-ct3sw
@vincentharry-ct3sw Жыл бұрын
DPP yonseyo ndi yakatangale not only Dausi
@usg435
@usg435 Жыл бұрын
Dausi bottman ndi nankhumwa ayabise chipani chawaoo
@symonyohane6989
@symonyohane6989 Жыл бұрын
APM emweyo
@mordecaikachale2497
@mordecaikachale2497 Жыл бұрын
Dausi ndi galu wadyera
@KelvinmolganMasamba-th9by
@KelvinmolganMasamba-th9by Жыл бұрын
Kungoti dausi ndiwamanyi ndipo akuyenera achoke akayambise chipani chake shatapuiiiii
@ziwani3682
@ziwani3682 Жыл бұрын
BIG 👍
@GeorgeGeorge-bu6cy
@GeorgeGeorge-bu6cy Жыл бұрын
Ulemu wanu brother
@antonychika15
@antonychika15 Жыл бұрын
Anafufuma Masaya kkkk iwetu iwe
@user-rn8tx3nr4z
@user-rn8tx3nr4z Жыл бұрын
Mumatiimilila Bg
@nyararaishumba9288
@nyararaishumba9288 Жыл бұрын
Dausi ndiopa kuyambira kale atuluke mchipan akayambise chake akapume waba zambiri galu amenei
@alicklongwe6375
@alicklongwe6375 Жыл бұрын
Adha awawa ulemu wanu
@ndugwamoses2467
@ndugwamoses2467 Жыл бұрын
HRDC very useless asowa zochita mmalo mopanga zachitukuko akulowelela za ndale. failed organisation!!!
@maskinmsungeni8763
@maskinmsungeni8763 Жыл бұрын
DPP is for the Mutharikas family, Why can't u, the Dausis form ur own Party? Go a head APM .
@user-qh5jo5qh3b
@user-qh5jo5qh3b Жыл бұрын
Dausi ndi kape ndipo achita manyadzi very soon
@johnsong7236
@johnsong7236 Жыл бұрын
kkkkkkkkkk i will never give up for this guy he is making my day always
@princedetbozsmallboy1749
@princedetbozsmallboy1749 Жыл бұрын
I don't like dausi his heartless person
@johnmasangano890
@johnmasangano890 Жыл бұрын
​@@princedetbozsmallboy1749that😮
@HamzahrichardSuman-pg5mf
@HamzahrichardSuman-pg5mf Жыл бұрын
osanyengerera chilungamo chiyende ngati madzi popanda inu sitingadziwe kanthu
@user-fz6jf4fo2h
@user-fz6jf4fo2h 10 ай бұрын
Muli bho
@MaxwellMustafa-ec8fc
@MaxwellMustafa-ec8fc Жыл бұрын
Angochoka muchipamo basi amusiye Apm
@lewisbonongwe8518
@lewisbonongwe8518 Жыл бұрын
Ayerekeze kusintha malamulo awone tizaliza mabomba central yonse
@emmanuelkenneth4768
@emmanuelkenneth4768 Жыл бұрын
Akulu inu zambiri zomwe mumalankhula mumaonetsera mbari, Tamalankhulani zoona anthu amakutsatilani.
@inessmsiyambiri8517
@inessmsiyambiri8517 Жыл бұрын
Dausi ngwa mcp tu akungosokonezako
@user-ps8vq5co8n
@user-ps8vq5co8n 6 ай бұрын
Bg mumatha kulongosola zinthu
@kassimjummah9489
@kassimjummah9489 Жыл бұрын
Abwana simunyengelera munthu
@user-jx4dg8tz1u
@user-jx4dg8tz1u Жыл бұрын
Zikuchita kuonela kuti anthu azipani zina akumuopa peter kuti akhoza kuzawabudura peter 2025
@AdamAhamad-k2i
@AdamAhamad-k2i 5 күн бұрын
Kumtumbo kwadausi ndi Nankhumwa
@humairamalombe295
@humairamalombe295 Жыл бұрын
Koma yah iweyo ulemu wako
managed to catch #tiktok
00:16
Анастасия Тарасова
Рет қаралды 48 МЛН
Kind Waiter's Gesture to Homeless Boy #shorts
00:32
I migliori trucchetti di Fabiosa
Рет қаралды 15 МЛН
Dad Makes Daughter Clean Up Spilled Chips #shorts
00:16
Fabiosa Stories
Рет қаралды 3,4 МЛН
هذه الحلوى قد تقتلني 😱🍬
00:22
Cool Tool SHORTS Arabic
Рет қаралды 59 МЛН
Wolfram Physics Project Launch
3:50:19
Wolfram
Рет қаралды 1,7 МЛН
Asilikali alanda boma ku Niger chifukwa chani?
15:10
Bakili Muluzi TV
Рет қаралды 54 М.
Ngongole za Malawi zachulukitsa. Abwana anapita kunja kopempha ndalama.
15:58
Kodi ufiti ulipodi? Amene anayambitsa ndani
10:08
Bakili Muluzi TV
Рет қаралды 82 М.
CRUISE 5  - CHIFUNO CHIFUNDO MLAMBE - CHIPEMBEDZO CHAMAKOLO ACHIKUDA
1:09:21
Joab Frank Chakhaza
Рет қаралды 13 М.
Nankhumwa NGC Meeting; Chipwirikiti ku chipani cha DPP.
12:14
Bakili Muluzi TV
Рет қаралды 86 М.
managed to catch #tiktok
00:16
Анастасия Тарасова
Рет қаралды 48 МЛН