No video

ABITI WILLIAM DAWOOD kusosombetsa NEC ya UTM...zimvere mtolo kachilungamo kalimo umu👐👐👐

  Рет қаралды 15,892

LIKI-LIKI Ladies

LIKI-LIKI Ladies

Күн бұрын

Пікірлер: 82
@peterchikwakwa8476
@peterchikwakwa8476 Ай бұрын
Chilima was a threat, that's why panopa MCP yayamba kumasuka, u can even see kusankhidwa kwa Micheal Usi akusangalala kwambiri.
@matiasncalaila4003
@matiasncalaila4003 Ай бұрын
Watching from Mozambique, ln fact Our SADC countries are in chaotic. Presidentes and ministers in SADC are different in coulors but are the one pessonal. Hospitals and Schools in their own countries always become useless when they are on top they tataly forget their background. My dear Sister , You are speaking and talking about the things that also is happening in my country. We need prayers for SADC leadership.
@NthambiInvestment
@NthambiInvestment Ай бұрын
Amati nkhondo ndi anasi judas sikaliyoti anapeleka Yesu,, chilima anapelekedwa ndi omuzungulila koma ambuye salakwisa amalola zowawa zichitike kuti ukulu wake uonekele may his soul of skc Rsst in Peace
@williamdaka79
@williamdaka79 Ай бұрын
Thanks good message,watching from Jeneva Switzerland 🇨🇭
@paulpaseli6310
@paulpaseli6310 Ай бұрын
Ya mantha ndi yowona. Amalawi tapusadi kugoyakhula uva uli ndi roya. Aaaa zowona tiwope kufa Ngati alipo wamuyaya bwanji
@clintonhodda9830
@clintonhodda9830 Ай бұрын
Ine ndiye sindiopa waudindo aliyense Chakwera anapha CHILIMA
@henryphiri6100
@henryphiri6100 Ай бұрын
Chakwera.Zikhale Ng'oma ndi Kunkuyu anapha Chilima.
@vivianmkwate8536
@vivianmkwate8536 Ай бұрын
keep it up Abiti 👏🏾👏🏾👏🏾
@user-gd2kl1fx1q
@user-gd2kl1fx1q Ай бұрын
Aunt God be with you, with ur wise words I wish ku chipan chathuchi ku takhala anthu 10 ngat inu please let's accomplish what our president started for his soul to continue resting in peace though the pain still exist bt God is all over tsogolo lowala lija litheka in jesus name
@MilikaKilion-tn1bn
@MilikaKilion-tn1bn Ай бұрын
Ifa ya chilima usi alimomo asamatinamize kufupika ngati ntchimba wa nkhoswe
@nafejonga972
@nafejonga972 Ай бұрын
My fellow nurse wowww😂😂😂
@nafejonga972
@nafejonga972 Ай бұрын
I love you mama😢😢
@eliffagondewe8214
@eliffagondewe8214 Ай бұрын
Mwayankhula mama ambuye akudalitseni..
@nafejonga972
@nafejonga972 Ай бұрын
I have started loving you too, am a utm member too
@peterchikwakwa8476
@peterchikwakwa8476 Ай бұрын
It's so sad ndege kugwa mpaka the whole Day no results,
@HameedahMasambuka
@HameedahMasambuka Ай бұрын
Mukhalike mama l love you ❤
@coastersRob
@coastersRob Ай бұрын
Ayi muziti kudambwe airport
@AlbertDuke-of9nn
@AlbertDuke-of9nn Ай бұрын
kuyakhura kwabwanji uku😂😂😂😂😂😂
@sparkdymon3429
@sparkdymon3429 Ай бұрын
Ccta ulindizeru zoveka ❤
@jamesgama5489
@jamesgama5489 Ай бұрын
Powerful speech
@ManyambaInnocent-x8i
@ManyambaInnocent-x8i Ай бұрын
Chilungamo sichipotsa apa mkadzi wayankhula moveka
@user-ui4ux5kc8d
@user-ui4ux5kc8d Ай бұрын
Chilungamo mchoti amalawi. Tiri ndimantha ndipo mantha amenewa ali ngakhale ku tsogolo komweku mmalo modzimenyera mkhondo tokha timadzifinya tokha ndithu ndiye Mai viuseni kwambiri
@user-te7xx8jg3k
@user-te7xx8jg3k Ай бұрын
Tupikene awechete yakuona
@peterjoshua2595
@peterjoshua2595 Ай бұрын
What a emotional ending malawi sad
@wonganikaunda
@wonganikaunda Ай бұрын
More fire mum
@tarkuesamson8838
@tarkuesamson8838 Ай бұрын
Amayiwa ndiosokoneza zedi ndakhala ndikwapangako follow, inu ndiena mumanyoza kwambiri kunyoza Author Mutharika munapangitsa astray Amalawi kuvotela Mcp lero ndiizi!palibe chanzeru mungatiuze inu.
@user-je8jm5uy1q
@user-je8jm5uy1q Ай бұрын
Mama.uyu amadziwa kubeleka nkowawa ndithu akudziwa kumwalira koti amadwala ndi kwina koma kumwalira kwa Chilima kunawaw
@WanangwaTauzie
@WanangwaTauzie Ай бұрын
Ndakumvani mama
@Leonilde-wn4le
@Leonilde-wn4le Ай бұрын
Fazem a escolha certa,no dia das eleições
@MaeCuinhane-gq7ub
@MaeCuinhane-gq7ub Ай бұрын
mom ulemu wanu, mkazi olimba mtima komanso wachilungamo ambuye azikudalitsa komanso apitilize kukupatsani mzeru
@isaacchipatala1618
@isaacchipatala1618 Ай бұрын
Very truly sisi
@mwaiwaobanda2691
@mwaiwaobanda2691 Ай бұрын
Ine nde ndinalidi supporter wa skc ....osati wa utm...mama mwandigwira mtima ndi mau awa....ngati kuli kopuma pumani mwa Ambuye bwana skc..😭😭
@beinhardkausiwa7107
@beinhardkausiwa7107 Ай бұрын
Chilima kusamva ,nanunso mungobwerera ku dpp otherwise mutha ngati makatani
@user-ee8og2mb5r
@user-ee8og2mb5r Ай бұрын
Wacthing from zambia madam
@isabelmartin7567
@isabelmartin7567 Ай бұрын
Chakwela the killer 💔
@noliachelewani2208
@noliachelewani2208 Ай бұрын
Kodi mamawa Ali Kuti Apapa Ali NDI nzelu kwabasi yooh
@user-zp8hv7bq3o
@user-zp8hv7bq3o Ай бұрын
A chemwa muku bandula bwino, a Malawi ndife a Tulo, Mantha ndi uchitsiru. Pitirizani kutilankhulira, zikomo mayi athu.
@jameshuwanzulu
@jameshuwanzulu Ай бұрын
Akunene zoona ka
@BandaSpeak-bg3ev
@BandaSpeak-bg3ev Ай бұрын
Listening madam
@CorneliousKaliat-od3un
@CorneliousKaliat-od3un Ай бұрын
Khani ndiyoona mama
@lame8
@lame8 Ай бұрын
Komatu mavutowa anachokela iye mwini alimoyo. Ndikumatha kuona zinazake zimamjchiyikila amaopsezedwa munthu uja 😢 koma zambiri akuzidziwa miniwake. Kalindo anayesetsa kumuuza chokako chokako zinakanika. Anayankhula za mngwilizano anamuyankha popo popo a mcp kuti sakuzidziwa 😢 nanga manganya ndindani kuti asaopsezedwe muzitionela patali guys.
@clintonhodda9830
@clintonhodda9830 Ай бұрын
Nthawi yakwana yokha anthu a dyera muaone ku UTM omwe akufuna kugulitsa chipani chanu walira mwana mkazi kuchililira chipani chake cha UTM zili kwa aKaliat, Fredox a Jawala ndi ena kulandira ndalama kuchokera kwa YUDASI MANGANYA
@isaacchipatala1618
@isaacchipatala1618 Ай бұрын
MCP blood
@user-ky2fs3zr8y
@user-ky2fs3zr8y Ай бұрын
Manese chitedze mdala mwakongolako ku USA.ubwera liti kwaSafarao kkkkkk
@alexsumani6823
@alexsumani6823 Ай бұрын
Ulemu wanu mama
@tracybennie7783
@tracybennie7783 Ай бұрын
Yomweyo
@henryphiri6100
@henryphiri6100 Ай бұрын
Anapha Sadik Mia kunamira covid
@user-zm9nl8zn2b
@user-zm9nl8zn2b Ай бұрын
Komatu iwe nabanda iwe yaaaa
@henryphiri6100
@henryphiri6100 Ай бұрын
Anthu amvere interview ya Brian Banda ndi Manganya
@Martha-m6e
@Martha-m6e Ай бұрын
Zowonadi matha kutenga za chipani cha uku kupiti nazo uku. Mulungu awaranga onse.
@cynthiakananji1608
@cynthiakananji1608 Ай бұрын
Eeee koma or a Patricia kaliyati akanangoganiza or kulingalira ngat iweyo mama,mmm anthu ndiye anawakonda ndipo akanaima popanda opikisana nawo,koma akuoneka kut ayamba kale kudya bans.koma nzomvesa chison anthu anali ndi hope pa mai wa,now amalawi ndiamasiye pano.ngatbndikunama tamverani speach yao yapamaliro a Lucius Banda.nokha muziyankha popanda fuso.
@WellingtonKoko
@WellingtonKoko Ай бұрын
Iweyo ndi 1 😊 phasaphase
@user-mx7oj1vx3l
@user-mx7oj1vx3l Ай бұрын
Every face tells a story mukawawona anthu powapatsa ma udindo,ngati wothandiza pomwe bolanso mfiti nthawi Zina ingakuwuze Kuti ndikuloza koma yawa ankawoneka ngakhale interview yawo inali pa dziwe TV two weeks back ,lilime lawo lidawonetsa Kuti mhu! ngogulitsana yawa😢😞
@wonganimoyoh2535
@wonganimoyoh2535 Ай бұрын
wise saying sister
@user-rm2xv8ys1i
@user-rm2xv8ys1i Ай бұрын
❤❤❤❤❤
@RobertMvina
@RobertMvina Ай бұрын
Tiuzeni titani
@MakandeMpambalika
@MakandeMpambalika Ай бұрын
Ndikumasulani yes go deeper mum
@ElliottBelon
@ElliottBelon Ай бұрын
Mau amphamvu mama
@clocksigns9755
@clocksigns9755 Ай бұрын
Nambo niwakutakata
@anthonynkhoma4265
@anthonynkhoma4265 Ай бұрын
Wasowa chokamba uyu. Ngati anthu akufalitsa zabodza aziwaombera mmanja? Undunawo akanapatsa iwe ungakane?
@MakandeMpambalika
@MakandeMpambalika Ай бұрын
Mmm ndiwe mzimayi wochenjera ka bandle kanga kathela pompo
@user-yk5qd6sk8e
@user-yk5qd6sk8e Ай бұрын
usi akuymila kabula
@GraciamChopih
@GraciamChopih Ай бұрын
Chemwali mwalankhuladi zoona zeni zeni,zonse mwalankhulazo palibe chomwe mwalakwitsapo bt chilungamo basi😂😂😂
@ritchardchakuma5725
@ritchardchakuma5725 Ай бұрын
Mama Uyo gwenembe Uyu mumusiye timuwonela 2025 tasanduka zisilu Koma mufufuze kuafilika kose ndife zisilu uphawi njala kukwala kwazithu gwenembe chakwera maikousi mutayeni ndiwamisala bambo asikono mutunjasiugwila
@Leonilde-wn4le
@Leonilde-wn4le Ай бұрын
Amalawi mantha achuluka kwambili,chilima wafera dziko😢
@AndrewInnocent-he8gs
@AndrewInnocent-he8gs Ай бұрын
Fasefase yomweyo
@user-be1zt6xl3f
@user-be1zt6xl3f Ай бұрын
Mayakhura mau abwino kwambiri sister
@TonyOkoibedi
@TonyOkoibedi Ай бұрын
Mama ukukambazo ndizoona ndikukutsatila kuno Ku South Africa
@AmaliYahaya
@AmaliYahaya Ай бұрын
😢😢😢😢😢
@thulanimpphiri6873
@thulanimpphiri6873 Ай бұрын
A ccta inu muli ndi zeru kwabasi mwina pa akazi akumalawi azeru inu muli panambala yabwino. Ndege ija si imafunika anthu ena ochokera kunja kuzafufuza ayi. Even mwana wa standard one kuti afufuze za ndege ija atha kupeza kuti boma ndilolakwa vuto Malawi mantha komaso kutenga atsogoleri ngati ndi Mulungu. Pazina kumalawi tinakula molakwika. Manganya tinanena kale kuti si wa utm. Manganya ali mu cabinet ya president chilima bwana wake wasowa 10 o'clock analola bwanji kuti president awuze mutundu wa Malawi 11 o'clock usiku. Pali zimasache zina za utm zopanda zeru ife sitikufuna banja limozi kulemera ayi tikufuna Malawi aliyese aziva kukoma ccta inu mukufunika mukhale president wamalawi
@WeziKamanga
@WeziKamanga Ай бұрын
Talking
@ExcitedBreakingWaves-oh3zb
@ExcitedBreakingWaves-oh3zb Ай бұрын
Zonsezi nchifukwa chakusanva kwa kwanu tinakuuzani ku MCP mukafako anthu aja ndi afisi .
@user-gd7xm7xr9v
@user-gd7xm7xr9v Ай бұрын
Ungokhala president wa UTM ndiwe
@GeorgeLipengaphiri
@GeorgeLipengaphiri Ай бұрын
Your a strong woman mama in politics
@RobertMvina
@RobertMvina Ай бұрын
Too much examples
@user-un8yq1gg2i
@user-un8yq1gg2i Ай бұрын
Kamkazi kokongolatu, koma eti kakuyankhuranso chichawa eti akuti fasafase Kaya ndiyekuti chiyani? Kkkkkkkkk pachilungamo chake ukunena zoona mchemwari.
@user-lg2ws2ki3d
@user-lg2ws2ki3d Ай бұрын
Zaziii
@cynthiakananji1608
@cynthiakananji1608 Ай бұрын
Za ziii Za ufiti,nyau?dyera magazi mmanja???
@isaacchipatala1618
@isaacchipatala1618 Ай бұрын
MCP blood part
@lewisdicksonmlozi130
@lewisdicksonmlozi130 Ай бұрын
Powerful speech
@SteveTebulo
@SteveTebulo Ай бұрын
Tikufuna anthu olimba mtina choncho usi siwa utm limbikani mayi kulankhula tchaya tchaya
@immaculatechitsakamile252
@immaculatechitsakamile252 Ай бұрын
akut anali a Ussi😢😅😅
Times Exclusive with Fredo Penjani Kalua - 14 August 2021
58:13
Times 360 Malawi
Рет қаралды 52 М.
Parenting hacks and gadgets against mosquitoes 🦟👶
00:21
Let's GLOW!
Рет қаралды 13 МЛН
English or Spanish 🤣
00:16
GL Show
Рет қаралды 8 МЛН
طردت النملة من المنزل😡 ماذا فعل؟🥲
00:25
Cool Tool SHORTS Arabic
Рет қаралды 23 МЛН
Кто убил СССР: называем поименно
54:09
НО.Медиа из России
Рет қаралды 64 М.
TIKUDZIWENI - 13 AUGUST -  ABITI MANICE WILLIAM DAUDI
28:46
Times 360 Malawi
Рет қаралды 49 М.
NAYO ZAMBIA KULIRA IMFA YA CHILIMA..MHSCRIP  till we meet again dear SKC
10:15
WATSEKA (Tribute to SIR SOLDIER LUCIUS BANDA) video.Oneraniko zimenezi
4:19
kumalawi kuno ndani wandale angamake??
1:01:32
Malawian Cameras
Рет қаралды 104 М.
TAMVANI ZA IMFA YA CHILIMA IJA
10:10
FRANCIS MTAWAYA TV
Рет қаралды 240 М.
KHAAAAAAA! KUIKHAPILA KOSATHWA MCP....KWAIPA
1:23:16
LIKI-LIKI Ladies
Рет қаралды 10 М.
Parenting hacks and gadgets against mosquitoes 🦟👶
00:21
Let's GLOW!
Рет қаралды 13 МЛН