Amen amen a bishop mulungu wathu salephera, Achilima anati mudima or ukule bwanji koma kuzacha ndithu ❤❤
@EvelynLungu-lj8tpАй бұрын
Mwaputa nkhondo. Akatorika si anthu wamba. Wina atengapo thembelero
@user-ir1lj8ir5t17 күн бұрын
Amen and amen inenso ndipemphelo langa ambuye afute ma vote abale anga zoona zomwe timaziyembekezela sizimenezi ayi
@user-wr1km2gh4g29 күн бұрын
Kuyankhula kwa mphavu,kopanda mantha,osaopa munthu,tiziopa mulungu
@user-ek6wf7bt7f29 күн бұрын
Father mupitilize kumuthira fire chakwera,watikwana
@user-pv9uk6sc3wАй бұрын
A Bishop mwalitha bomali, ndipo kumene ali Chakwera sakugona ndi m'mene mwatulukila ma Bishop. Chakwera ndi boma lake la MCP lalephera tatopanalo.
@MeckMdoma28 күн бұрын
Dpp nayo tinatopa nayo nkuona tinayithamangitsa. Mavuto ali mdziko muno solution si dpp. Awa adzawonjezera kusawuka kwa a Malawi kupsola apa. Malawi is going througheconomic problems because dpp mismanaged this country's economy.
Palibe zofuna kutchuka chilungamo chinenedwe achulewa a mcp anapha anthu pangoz ya ndege( chilima) ndi ena onse
@user-oc9vl9xz8eАй бұрын
Azisogoleli ameneqa onse alandile ma thembelelo kuyambila ana awo komanso zizukulu zawo za ana awo onse amene azadye ndalama zomwe akubasi za anath osauka alandile thembelelo ndibkhate mu zina la yesu....
@TiyanjaneMkwate-we8guАй бұрын
Amen
@CathreenKadwala28 күн бұрын
Amen Amen
@marthansaliwa7732Ай бұрын
Amen! Father Ambuye azikutetezani.
@user-uf4db7im7d16 күн бұрын
Mwaputa a katolika ndipo simunati muziona, campaign ali mmatchalichi
Zowona ndithu, malawi akufunika ma demo kuti akozeke
@CharlesChagudubuka-rm6bhАй бұрын
Akuti apule chasanduka choseketsa 😂😂😂for
@WisikiBlack-gj4guАй бұрын
Ameen ameen abusa. Apa boma palibe koma chizuzo basi kuononga dziko uku. Koma apa pakufunika nkhondo ambuye atithandize.chifukwa ngati afika pomupha chilima ife ationa ngati ndani.koma nkhondo ndimeneyatsala basi
@AndersonChimwala-hz4soАй бұрын
Mau ogwila mtima zoona .
@user-vx5kv8dz3d5 күн бұрын
Allah amutibule Farawo wathuyu
@AndersonChimwala-hz4soАй бұрын
Anthu amulungu kugwa kwa munthu openphela amalandila nazo Themberelo.
@user-wi8xw9qh7n20 күн бұрын
Yes father God will help us
@thatgirrroskrr357024 күн бұрын
Powerful message
@elizasinganoАй бұрын
Amen and amen mulungu atithandiza kumeneya nkhondo imeneyu
@MasausoMsiska-rz3id25 күн бұрын
Amen man of God
@JamayakoJamayako-rv2he24 күн бұрын
Powerful massage Pipo shud listen carefully
@LingsonMaidaАй бұрын
Ifeso talanda bwana😂😂😂😂😂😂
@JosterNgalawaАй бұрын
Amen bishop, ndipo pitilizani
@user-hs4bm2yj8r26 күн бұрын
Amen 🙏 father, Mulungu kutetezeni
@TiyanjaneMkwate-we8guАй бұрын
Mulungu alemekezeke, amalawi tikuzunzika kwambili, atithandize potiteteza kwa anthu a nkhanza ngati awa.Ft Mulungu akudaliseni pobwera ndi chilungamo.mwina liwu lanu linveka kwa MULUNGU.
Amen mau awa agwile ntchito kwa woipayo kuti Malawi apulumuke
@1kumilala1Ай бұрын
Mawu amalenga. Amen Father
@user-do2cs8nf4bАй бұрын
God is speaking to the government of Malawi anayiwala kuti kunja kuno kuli Mulungu, akupembedza ndalama. Mulungu dzukani pa mpando wanu wachifumu mutimenyere nkhondoyi
@WilliamBandaWiliАй бұрын
Munthu wamulungu walankhula apa
@MalawianCameraАй бұрын
@@WilliamBandaWili Kung'alula
@user-nf3ik3ff6y28 күн бұрын
Amen Chakwela you mast go watikwana
@DafterKhungwa27 күн бұрын
Amen,nanenso ndayitengako
@FazilahKazembe27 күн бұрын
Amen wathu sameneyo ..
@allansili-rc9gcАй бұрын
Wow this is charming
@Allan-bk1Ай бұрын
😂😂😂😂eeesh pastor
@user-ve4zn2ne1kАй бұрын
Alleluia Abosa naneso ndi banja Langa ndaitengako mulungu afufute ndithu!!!!
@JamayakoJamayako-rv2he24 күн бұрын
Mateyu 18 vs 18 Yomweyoo ikhake nyimbo ndi chitsogodzo kwa ife
@MacreaChilingulo-ob9gbАй бұрын
You are the Greatest , Amen !
@MestreMaday-fv7qo25 күн бұрын
Chipan ali nacho ndi mulungu wathu
@MarthaMbewe-uk5nnАй бұрын
Pharaoh watsala pang'ono kuonetsedwa ukulu wa Mulumgu pompano aziona iyeyo kodi sakuona kuti ulemu wake unachoka Kale kale? President wanji omangotukwanidwa mgati chitsiru?
@PeterChuma-yf1ps25 күн бұрын
Vote yanga naneso itengedwe
@MestreMaday-fv7qo25 күн бұрын
IWE loya wachani IWE ndi m.malawi ukunva bwanji siya zimenezo
@RachealHarawa-xc9gsАй бұрын
Chilichonse chili ndinthawi koma na apapa zafikapa Ambuye chitaponi kanthu mwasanga
@PaxKinley27 күн бұрын
Ndatenganso nane VOTE yanga
@doreenkaliati3166Ай бұрын
Ulemu wanu Abusa ❤❤❤❤❤❤
@sthoramexjrsa902Ай бұрын
Amen father 🙌🙌🙌
@MarthaMbewe-uk5nnАй бұрын
Tathokoza abusa ameneyu musasiye kumudzudzula pali mau amanena kuti :ONDIUZA ANALIPO KOMA KUSAMVELA KWANGA KWANDIPWETEKETSA
@user-uy8uk7so9d14 күн бұрын
God be with you
@isabelmartin756726 күн бұрын
Analowa mu Zina la ubusa 😢😢😢osaziwa satana watola joker eeeeee ai chakwela wapweteka Malawian 😭😭
@munashemoyo4190Ай бұрын
Amen father Amen mau mau
@ChilangoNdalamaАй бұрын
Amen abshop
@alexmkolongo3089Ай бұрын
Chakwela azindikile kuti akadzangotuluka boma akutengedwa komaso manganya ndi wa MCP asamatinamizepo apa
@HassanJameskananjieАй бұрын
Kod amalaw mupepela mpaka liti lawyer nde kuti chan
@gracekamzatiАй бұрын
Ameni abusa ine nde sinavotereko ndipoyamba pomwe ili siboma ayi koma kupha anthu