Abusa akuti vote yao atengapo anapanga mistake❎ 😂😂😂

  Рет қаралды 30,531

Malawian Cameras

Malawian Cameras

Ай бұрын

Пікірлер: 177
@augustMag
@augustMag 28 күн бұрын
Powerful words may God continue bless you Fr Mnthalika 🔥
@MorrisMapiri-d6z
@MorrisMapiri-d6z 27 күн бұрын
Mlungu anamufunsa KAINI nati: alikuti m'bale wako Abele? Nde anati, taona mwazi wake ukundililira ine kunthaka. Zotsatira anali matembelero pa KAINI. Kukhetsa mwazi kumadzetsa tsoka.
@user-sv2vc7ie2m
@user-sv2vc7ie2m 29 күн бұрын
Anthu atengapotu phunzilo ndizovuta zomwe tikuziona chifukwa anthu amati akufuna kuona kusintha ndiye aonatu nyekhweeeeee
@GiftPhiri-tt7nn
@GiftPhiri-tt7nn Ай бұрын
Umenewu ndiye utsogoleri munthu wa Mulungu asamaope kuyankhula chilungamo , osati azibusa enawa kungowapatsa ndalama basi kusekelera zopusa , ana anjoka Inu Mulungu akulangani
@marryphili5419
@marryphili5419 28 күн бұрын
Amen abishop ndipo talira mokwana koma mulungu simunthu safulumira ndipo sachedwa one day is one day mulungu ayakha
@user-oc8nj3or6y
@user-oc8nj3or6y 28 күн бұрын
What a teaching ❤❤❤ impressed me so much waooooo❤❤❤
@CathreenKadwala
@CathreenKadwala 28 күн бұрын
Father Inu Ambuye azikupasani moyo wautali simuwopa kuyankhula chilungamo
@PrinceBlessings-bv5bs
@PrinceBlessings-bv5bs 4 күн бұрын
Eeee eeee Bon Kalindo siwamisalatu... Adanena kuti anthu akadzatopa adzalankhura m'modzi modz.... God be with you ❤
@ReginaKasambiza-ie2rp
@ReginaKasambiza-ie2rp 29 күн бұрын
Kumwamba kulande vote yanga Tsiku lina Mulungu wamva Pemphero lathu
@user-cf9yz3ei5o
@user-cf9yz3ei5o Ай бұрын
you have spoken man of. God we. are listing God is God. does not. fail
@bysongeorge3243
@bysongeorge3243 Ай бұрын
Chilungamo chokhachoka. Zokhumudwitsa wina tinamusankha anali M'busa..koma lero anasanduka ..
@patrickndojime1632
@patrickndojime1632 Ай бұрын
Father mumakwanisa ulaliki wanu wabwino kwambiri
@JustinChinombo-dy6tp
@JustinChinombo-dy6tp Ай бұрын
Amen amen a bishop mulungu wathu salephera, Achilima anati mudima or ukule bwanji koma kuzacha ndithu ❤❤
@EvelynLungu-lj8tp
@EvelynLungu-lj8tp Ай бұрын
Mwaputa nkhondo. Akatorika si anthu wamba. Wina atengapo thembelero
@user-ir1lj8ir5t
@user-ir1lj8ir5t 17 күн бұрын
Amen and amen inenso ndipemphelo langa ambuye afute ma vote abale anga zoona zomwe timaziyembekezela sizimenezi ayi
@user-wr1km2gh4g
@user-wr1km2gh4g 29 күн бұрын
Kuyankhula kwa mphavu,kopanda mantha,osaopa munthu,tiziopa mulungu
@user-ek6wf7bt7f
@user-ek6wf7bt7f 29 күн бұрын
Father mupitilize kumuthira fire chakwera,watikwana
@user-pv9uk6sc3w
@user-pv9uk6sc3w Ай бұрын
A Bishop mwalitha bomali, ndipo kumene ali Chakwera sakugona ndi m'mene mwatulukila ma Bishop. Chakwera ndi boma lake la MCP lalephera tatopanalo.
@MeckMdoma
@MeckMdoma 28 күн бұрын
Dpp nayo tinatopa nayo nkuona tinayithamangitsa. Mavuto ali mdziko muno solution si dpp. Awa adzawonjezera kusawuka kwa a Malawi kupsola apa. Malawi is going througheconomic problems because dpp mismanaged this country's economy.
@marryphili5419
@marryphili5419 28 күн бұрын
Borani DPP inali bwino fertilize wunali bwino anthu tinali ndi chakudya mapassport amapezeka palipose kuchoka ku mzuzu mupaka kumangochi ndalama sinali yotha mphamvu panopa wesi
@PrinceBlessings-bv5bs
@PrinceBlessings-bv5bs 4 күн бұрын
Kodi Dpp idalakwanji????
@user-xx4jb9se3z
@user-xx4jb9se3z Ай бұрын
Abusa awawa MULUNGU awapatse moyo wautali.imfa ya chilima akatolika sakugona ndipo akati apemphere amakhala serious mcp bro apule samalani
@MarkManyowa
@MarkManyowa 25 күн бұрын
🤣🤣🤣🤣 Malawi ikakhala Nyekhwe nde taithamatu🤣🤣🤣🤣🇹🇿
@lawrencemakina2882
@lawrencemakina2882 Ай бұрын
Amen. Mulungu ndiye omenyera nkhondo ana ake
@user-dm2fs6hf1b
@user-dm2fs6hf1b Ай бұрын
Palibe zofuna kutchuka chilungamo chinenedwe achulewa a mcp anapha anthu pangoz ya ndege( chilima) ndi ena onse
@user-oc9vl9xz8e
@user-oc9vl9xz8e Ай бұрын
Azisogoleli ameneqa onse alandile ma thembelelo kuyambila ana awo komanso zizukulu zawo za ana awo onse amene azadye ndalama zomwe akubasi za anath osauka alandile thembelelo ndibkhate mu zina la yesu....
@TiyanjaneMkwate-we8gu
@TiyanjaneMkwate-we8gu Ай бұрын
Amen
@CathreenKadwala
@CathreenKadwala 28 күн бұрын
Amen Amen
@marthansaliwa7732
@marthansaliwa7732 Ай бұрын
Amen! Father Ambuye azikutetezani.
@user-uf4db7im7d
@user-uf4db7im7d 16 күн бұрын
Mwaputa a katolika ndipo simunati muziona, campaign ali mmatchalichi
@user-mj2te7vl6p
@user-mj2te7vl6p Ай бұрын
True talking man of God
@MalawianCamera
@MalawianCamera Ай бұрын
@@user-mj2te7vl6p Kung'alula
@SueWahna
@SueWahna 4 күн бұрын
Amen ine ndagwirizana nanu atsogoleri
@user-te3ps3kf2t
@user-te3ps3kf2t Ай бұрын
Ali ndi khutu amve,powerful Massage.
@user-gv2uu3cs3g
@user-gv2uu3cs3g Ай бұрын
Amen a Bishop.Amenewa Ndiye mau
@user-dy4gc2hr5e
@user-dy4gc2hr5e 22 күн бұрын
Powerful message Ambuye akutetezereni ntumiki
@WilliamNhlane-fd9hi
@WilliamNhlane-fd9hi 19 күн бұрын
Amen , tangovomerezani bwana president tulani pansi udindo nokha mukuona kuti zakukanikani .
@innocentissah2636
@innocentissah2636 Ай бұрын
Tiwemphelere atisiye anthu oipawa afe ndithu, mkhwiyo wa ambuye uwakwapule anthu akubawa
@user-il8cn7ko9m
@user-il8cn7ko9m 27 күн бұрын
😂😂 eshi amen
@ThokozaniKaluluma-rj6rp
@ThokozaniKaluluma-rj6rp 27 күн бұрын
Koma muli ndi lawyer? Kkkk
@user-vm7iz6oz6r
@user-vm7iz6oz6r 29 күн бұрын
Pano agula mifut malo mogula makhwala zipatalam
@NatashaBema
@NatashaBema Ай бұрын
Amen abusa inuyo mumatha
@user-qg4it7my9n
@user-qg4it7my9n 29 күн бұрын
Amen ambuye akudaliseni coz mwaonse azitumiki asakha kukhara cete ngati dziko likuyenda bwino koma mulungu azapeleka cilango coopsa kwa anthu amenewa
@AdamSteven-ne9hg
@AdamSteven-ne9hg 21 күн бұрын
Ulaliki ugwira mtima ndithu🔥
@user-xv3nr5kj2u
@user-xv3nr5kj2u 19 күн бұрын
Amen father
@MosesShaibu-ee8hn
@MosesShaibu-ee8hn 26 күн бұрын
Amen jone chilebwe
@ThokohPrescotKalonga
@ThokohPrescotKalonga Ай бұрын
Zowona ndithu, malawi akufunika ma demo kuti akozeke
@CharlesChagudubuka-rm6bh
@CharlesChagudubuka-rm6bh Ай бұрын
Akuti apule chasanduka choseketsa 😂😂😂for
@WisikiBlack-gj4gu
@WisikiBlack-gj4gu Ай бұрын
Ameen ameen abusa. Apa boma palibe koma chizuzo basi kuononga dziko uku. Koma apa pakufunika nkhondo ambuye atithandize.chifukwa ngati afika pomupha chilima ife ationa ngati ndani.koma nkhondo ndimeneyatsala basi
@AndersonChimwala-hz4so
@AndersonChimwala-hz4so Ай бұрын
Mau ogwila mtima zoona .
@user-vx5kv8dz3d
@user-vx5kv8dz3d 5 күн бұрын
Allah amutibule Farawo wathuyu
@AndersonChimwala-hz4so
@AndersonChimwala-hz4so Ай бұрын
Anthu amulungu kugwa kwa munthu openphela amalandila nazo Themberelo.
@user-wi8xw9qh7n
@user-wi8xw9qh7n 20 күн бұрын
Yes father God will help us
@thatgirrroskrr3570
@thatgirrroskrr3570 24 күн бұрын
Powerful message
@elizasingano
@elizasingano Ай бұрын
Amen and amen mulungu atithandiza kumeneya nkhondo imeneyu
@MasausoMsiska-rz3id
@MasausoMsiska-rz3id 25 күн бұрын
Amen man of God
@JamayakoJamayako-rv2he
@JamayakoJamayako-rv2he 24 күн бұрын
Powerful massage Pipo shud listen carefully
@LingsonMaida
@LingsonMaida Ай бұрын
Ifeso talanda bwana😂😂😂😂😂😂
@JosterNgalawa
@JosterNgalawa Ай бұрын
Amen bishop, ndipo pitilizani
@user-hs4bm2yj8r
@user-hs4bm2yj8r 26 күн бұрын
Amen 🙏 father, Mulungu kutetezeni
@TiyanjaneMkwate-we8gu
@TiyanjaneMkwate-we8gu Ай бұрын
Mulungu alemekezeke, amalawi tikuzunzika kwambili, atithandize potiteteza kwa anthu a nkhanza ngati awa.Ft Mulungu akudaliseni pobwera ndi chilungamo.mwina liwu lanu linveka kwa MULUNGU.
@BestonMakochera-qk4sz
@BestonMakochera-qk4sz 28 күн бұрын
Sibas katolika waziwa chomwe chinachitik game yathapo yambani kulongeza 😢😢 anthu amene ziululika lero zayambik
@user-oc9vl9xz8e
@user-oc9vl9xz8e Ай бұрын
Amen mau awa agwile ntchito kwa woipayo kuti Malawi apulumuke
@1kumilala1
@1kumilala1 Ай бұрын
Mawu amalenga. Amen Father
@user-do2cs8nf4b
@user-do2cs8nf4b Ай бұрын
God is speaking to the government of Malawi anayiwala kuti kunja kuno kuli Mulungu, akupembedza ndalama. Mulungu dzukani pa mpando wanu wachifumu mutimenyere nkhondoyi
@WilliamBandaWili
@WilliamBandaWili Ай бұрын
Munthu wamulungu walankhula apa
@MalawianCamera
@MalawianCamera Ай бұрын
@@WilliamBandaWili Kung'alula
@user-nf3ik3ff6y
@user-nf3ik3ff6y 28 күн бұрын
Amen Chakwela you mast go watikwana
@DafterKhungwa
@DafterKhungwa 27 күн бұрын
Amen,nanenso ndayitengako
@FazilahKazembe
@FazilahKazembe 27 күн бұрын
Amen wathu sameneyo ..
@allansili-rc9gc
@allansili-rc9gc Ай бұрын
Wow this is charming
@Allan-bk1
@Allan-bk1 Ай бұрын
😂😂😂😂eeesh pastor
@user-ve4zn2ne1k
@user-ve4zn2ne1k Ай бұрын
Alleluia Abosa naneso ndi banja Langa ndaitengako mulungu afufute ndithu!!!!
@JamayakoJamayako-rv2he
@JamayakoJamayako-rv2he 24 күн бұрын
Mateyu 18 vs 18 Yomweyoo ikhake nyimbo ndi chitsogodzo kwa ife
@MacreaChilingulo-ob9gb
@MacreaChilingulo-ob9gb Ай бұрын
You are the Greatest , Amen !
@MestreMaday-fv7qo
@MestreMaday-fv7qo 25 күн бұрын
Chipan ali nacho ndi mulungu wathu
@MarthaMbewe-uk5nn
@MarthaMbewe-uk5nn Ай бұрын
Pharaoh watsala pang'ono kuonetsedwa ukulu wa Mulumgu pompano aziona iyeyo kodi sakuona kuti ulemu wake unachoka Kale kale? President wanji omangotukwanidwa mgati chitsiru?
@PeterChuma-yf1ps
@PeterChuma-yf1ps 25 күн бұрын
Vote yanga naneso itengedwe
@MestreMaday-fv7qo
@MestreMaday-fv7qo 25 күн бұрын
IWE loya wachani IWE ndi m.malawi ukunva bwanji siya zimenezo
@RachealHarawa-xc9gs
@RachealHarawa-xc9gs Ай бұрын
Chilichonse chili ndinthawi koma na apapa zafikapa Ambuye chitaponi kanthu mwasanga
@PaxKinley
@PaxKinley 27 күн бұрын
Ndatenganso nane VOTE yanga
@doreenkaliati3166
@doreenkaliati3166 Ай бұрын
Ulemu wanu Abusa ❤❤❤❤❤❤
@sthoramexjrsa902
@sthoramexjrsa902 Ай бұрын
Amen father 🙌🙌🙌
@MarthaMbewe-uk5nn
@MarthaMbewe-uk5nn Ай бұрын
Tathokoza abusa ameneyu musasiye kumudzudzula pali mau amanena kuti :ONDIUZA ANALIPO KOMA KUSAMVELA KWANGA KWANDIPWETEKETSA
@user-uy8uk7so9d
@user-uy8uk7so9d 14 күн бұрын
God be with you
@isabelmartin7567
@isabelmartin7567 26 күн бұрын
Analowa mu Zina la ubusa 😢😢😢osaziwa satana watola joker eeeeee ai chakwela wapweteka Malawian 😭😭
@munashemoyo4190
@munashemoyo4190 Ай бұрын
Amen father Amen mau mau
@ChilangoNdalama
@ChilangoNdalama Ай бұрын
Amen abshop
@alexmkolongo3089
@alexmkolongo3089 Ай бұрын
Chakwela azindikile kuti akadzangotuluka boma akutengedwa komaso manganya ndi wa MCP asamatinamizepo apa
@HassanJameskananjie
@HassanJameskananjie Ай бұрын
Kod amalaw mupepela mpaka liti lawyer nde kuti chan
@gracekamzati
@gracekamzati Ай бұрын
Ameni abusa ine nde sinavotereko ndipoyamba pomwe ili siboma ayi koma kupha anthu
@harrisbanda5891
@harrisbanda5891 Ай бұрын
Tikufuna anthu olimba mtima kumalawi kuno ngati fazzala awaa
@MzikaPhiri
@MzikaPhiri 27 күн бұрын
Yangaso ndatenga
@KennethMchenga-j9c
@KennethMchenga-j9c 27 күн бұрын
Uthenga uwo siwamasewela mulungu akutetezelen ameni
@user-wd5tw1mz8h
@user-wd5tw1mz8h Ай бұрын
Wakutumani ndimulungu lankhulan mosaopa chifukwa malawi waonongeka ndi chakwela
@AlexKaunda-ny2eg
@AlexKaunda-ny2eg Ай бұрын
Mukatenge chinzukwa uko Kuti chilamulire Amalawi mwandilidza😢
@FredKanyerere
@FredKanyerere 27 күн бұрын
Bishop Amen
@AchinaKellz
@AchinaKellz Ай бұрын
Ine aroma ndimayiziwa ndiyimeneyi kafuseni malemu kamuzu aroma sia mcp
@deborahngwira724
@deborahngwira724 27 күн бұрын
Mkwiyowutu ukuchedwa. Ine nde ndikuufuna nsanga nsaname
@user-oc9vl9xz8e
@user-oc9vl9xz8e Ай бұрын
Uthenga uwuwu ukamufika woipa chikumbu mtima chimugwile
@tresawillicky
@tresawillicky Ай бұрын
Mau amphamvu zedi
@GeorgeKambwiri-xr9ri
@GeorgeKambwiri-xr9ri 24 күн бұрын
Koma yaa🤝 9:58
@gladysbonongwe1038
@gladysbonongwe1038 Ай бұрын
Amen
@user-uy8uk7so9d
@user-uy8uk7so9d 14 күн бұрын
Munavotela zisilu kodi nanu
@user-gg9hw4oj2v
@user-gg9hw4oj2v Ай бұрын
Amen 🙏
@WilliamNhlane-fd9hi
@WilliamNhlane-fd9hi Ай бұрын
Amen God hear our prayers , rescue Malawi
@WesleyKalimwayi
@WesleyKalimwayi Күн бұрын
Mau Mau amen
MALAWI COURT.... TAMVANI IZI ABALE 🤔
20:45
Jimmy
Рет қаралды 25 М.
Mom's Unique Approach to Teaching Kids Hygiene #shorts
00:16
Fabiosa Stories
Рет қаралды 38 МЛН
Они так быстро убрались!
01:00
Аришнев
Рет қаралды 2,3 МЛН
Olo Anthu A Ku Kasiya MCP Sakuyifuna - Comrade Ntanyiwa
21:24
Nyasa VoiceBox
Рет қаралды 24 М.
FULL SPEECH: Donald Trump speaks before the NABJ in Chicago
36:28
FOX 32 Chicago
Рет қаралды 368 М.
Rev. Alexander Kambiri preaching at the funeral service at Area 18 cemetery
19:59
Rev. Alexander Kambiri
Рет қаралды 146 М.
Mom's Unique Approach to Teaching Kids Hygiene #shorts
00:16
Fabiosa Stories
Рет қаралды 38 МЛН