Akuti MCP iwinaso 2025 Zifukwa Zake Nazi

  Рет қаралды 2,769

Hanifa Mw

Hanifa Mw

3 ай бұрын

Akuti MCP iwina 2025 opanda thandizo la Tonse

Пікірлер: 37
@MustafaLikaomba
@MustafaLikaomba 2 ай бұрын
Awa ndiye manyiiiiii onunkha
@omarajibu860
@omarajibu860 2 ай бұрын
Ndiganiza kuti pansi pa mtimapo mukuziwa kuti mukunama zomwe mukulankhulazo
@user-do2cs8nf4b
@user-do2cs8nf4b 2 ай бұрын
Chonsecho agona ndi njala anthu anthu osawona patali😩
@MustafaLikaomba
@MustafaLikaomba 2 ай бұрын
Chala imapele ka usilu
@user-eh1mg3ww6d
@user-eh1mg3ww6d 2 ай бұрын
Athu ovetsa chisoni kwambili
@PeterPhiri-nd6op
@PeterPhiri-nd6op 2 ай бұрын
Kumalawi kwene umo wathu tikugonela nanjala thena bwenu tikukhumba ku votelaso chakwela mmmmm sata nadi malawi wazingizga nadi eshìii koma
@AleksaWilliams-qc6cn
@AleksaWilliams-qc6cn 2 ай бұрын
Awa asandichimwise odi mgone
@user-ub9on7oj7l
@user-ub9on7oj7l 2 ай бұрын
Sakuziwa chomwe akuchita
@giftblack7690
@giftblack7690 2 ай бұрын
Kkkkkkkk koma munthu anakonza alibe kalikose akuvutika ndikumatamililabe ng'ona party mbava yachabe chabe chakwela kwamtele
@stanleymollen7273
@stanleymollen7273 2 ай бұрын
Azibambo ena mzeru zero...sad
@user-uv7yq1fx4r
@user-uv7yq1fx4r 2 ай бұрын
Thawi yanu koma sangalalani komaliza malizitsani thawiyanu yatsala pang.ono
@user-xw6rr9gm1z
@user-xw6rr9gm1z 2 ай бұрын
Zomvesa chison ndithu mmh
@AdamAPhiri
@AdamAPhiri 2 ай бұрын
Pa mtsonkhano wa mcp angayinyoze ndani kuti akadyedwe ndi ng'ona
@omarajibu860
@omarajibu860 2 ай бұрын
Iwe ukunena kuti anthu akonzekere, ife tinakonzeka kale zochotsa masanjewa 2025.
@omarajibu860
@omarajibu860 2 ай бұрын
Komadi anthu opanda nzeru mulipo, zoona munthu wanzeru mpaka kumasiya kupuma kwawo kupita kunsonkhano wa izizi?
@user-wi9pe2hz7e
@user-wi9pe2hz7e 2 ай бұрын
Mdalayu akudwala chakwela wapanga chan😅
@binalidjeyshabahzombamalawi
@binalidjeyshabahzombamalawi 2 ай бұрын
Mbuli za anthu
@MariaRajabu
@MariaRajabu 2 ай бұрын
Munthu Ali PA Laine yokalandila zithu za mcp anganene kuti mcp iluza 2025 mukufuna asalandile kkkkkkkkkk
@UseniMailosi
@UseniMailosi 2 ай бұрын
Anthu enawa ndi agalu awanthu
@LukaAron-el5qh
@LukaAron-el5qh 2 ай бұрын
Azimai ovesa chisoni kwambiri pomwe kunyumba kwako kulibe chakudya
@ImraanJafali-dk7rg
@ImraanJafali-dk7rg 2 ай бұрын
Ndiposo inu mwina adyesedwa ma2 pin
@user-hm9nc7lz6e
@user-hm9nc7lz6e 2 ай бұрын
Zoopsatu anthu amabgidwa papango komaso asekedwA maso sakuona
@user-cy7gd1go6y
@user-cy7gd1go6y 2 ай бұрын
Iwe ukuyendela chigoba chimoz chachimanga komaso chigobacho chokakamisa nde kumati chakwera awina chamba eti chifukwa akupasani chitenje panyo panu anyapapi inu nanuso inu adala magalasiwo ndi mutucho pakolo pako
@user-qp8kh2hj9o
@user-qp8kh2hj9o 2 ай бұрын
Kodi inu mumamufuna azinena kuti DPP izawina kodi tonse ingakhale ana agogo????
@user-pt8wb4vw6r
@user-pt8wb4vw6r 2 ай бұрын
Dziwani kuti tonsefe sitingakhale ndimaganizo amozi malawi ndi dziko zalazipani zambiri tosefe sitingakonde dpp aliyese ali ndi chisakho chake ndiye adpp mkuchedwa
@user-gx8or3yz9u
@user-gx8or3yz9u 2 ай бұрын
Ndalamazotu tilandila mudzipereka ndithu ife tidzilandila komasikuti tidzakuvoteraninso ai zimenezo muiwale amalawi tatopa Nanu kkkkk mudzalila chaka Cha mawa muli ku mastand tikufuna tione zina
@user-vh9uk1jy7w
@user-vh9uk1jy7w 2 ай бұрын
Mukunama chemwali
@alexsumani6823
@alexsumani6823 2 ай бұрын
Izi izi ,muchepese ndithu ,kufuna kuutsa mkwiyo wa anthu uku mxeuii
@user-vl8uw8mc3u
@user-vl8uw8mc3u 2 ай бұрын
Anthu akufa awa komanso osapenyanso awa sorry kwabasi
@FefieTenisha-du7ge
@FefieTenisha-du7ge 2 ай бұрын
This is very pathetic With this kind of thinking how can we move forward as a country? I can now see clearly why this country will never develop... People are commenting on things they don't really understand.. Democracy will never work in Malawi... The masses are so idiotic that they can't even know how to elect a good leader for them
@spargomw
@spargomw 2 ай бұрын
Nthaw mkachitsiru. Tionana 2025. Zidzakuvoteran nd Ndondocha osat anthu
@mamulemathekga
@mamulemathekga 2 ай бұрын
Ndarama sosi kwapusisa 2000 munduwamay kumanena simeneso mundu wobeleka sovesa chison asimay atu 😭🤔🤔
@NgomaRaheem
@NgomaRaheem 2 ай бұрын
Kuyakhula kopusa ndithu tikumana 2025 ino
@LukaAron-el5qh
@LukaAron-el5qh 2 ай бұрын
Bambo vumbe mukunena zoona inu
@user-uf4db7im7d
@user-uf4db7im7d 2 ай бұрын
Manyi anu
@user-pt8wb4vw6r
@user-pt8wb4vw6r 2 ай бұрын
Mcp bomaaaaaa❤❤
Mlaka Maliro - Yasowa (Official Music Video) Dir VJ Ken
6:53
Mlaka Maliro
Рет қаралды 234 М.
Chegutu : Ruvimbo wekuurairwa $100 onzi opfuka asati avigwa
1:03:06
President Chakwera walemba ntchito anthu 1.3 million; Source SONA 2024
9:02
ZINA UKAMVA: NZANGA WANDIDYERA MKAZI WANGA
18:58
Hanifa Mw
Рет қаралды 46 М.
ZOMWE ZIDALI KU BALAKA 🙌🙌🙌🙌25 July 2024
27:52
HOT 265
Рет қаралды 13 М.
GEFFREY KAPUSA WALOWA MMANDA PA 25/04/2024...Mzimu wake uuse mu mtendere
58:27
Misomali Ya Six Inches Yothana Ndi Zipani Zotsutsa - Bon Kalindo
17:18
Mutharika Ndi DPP Anaimitsa Dziko | Umu ndi m'mene zinalili
10:37