Who was the real Kamuzu Banda? Kodi Kamuzu Banda kwawo kunali kuti?

  Рет қаралды 199,012

Bakili Muluzi TV

Bakili Muluzi TV

3 жыл бұрын

What was Kamuzu Banda nationality, tribe and parents?

Пікірлер: 292
@manfredjamesbrown4051
@manfredjamesbrown4051 2 жыл бұрын
I have been following this channel for a long time now...To be honest with, i like your channel ....Anthufe takhala mu mdima kwa nthawi yayitali..... Nkhani zambiri zimene mumafotokoza ndizoona zokhazokha.. Ambiri wa akumatsutsa ndi ana ama 80s ndi 90s..Nkhani zambiri zi enafe tinkazimva pa nthawi yo mwama mememene without real facts.... Mwachitsanzo Pa History yomwe tinkaphunzila mu STD 8 yakale B4 MANEB , tinkaphunzila kuti chipani cha MCP adayambitsa ndi Kamuzu Banda...But i do remember my class History teacher (adatiuza poyela kuti MCP adayambitsa ndi Orton Chiwa ndipo ananenanso kuti in case pamayeso funso litabwera tizingoti adayambitsa ndi Kamuzu Banda....Honestly i salute you.. Nkhani yama Card ndi msonkho..Ndizoona ndipo ine ndinawona ndithu azimai amimba akudulitsidwa ma Card awiri yake ndi ya mimba yake .. Makolo athu ankachita kuthawa akangomva kuti kwabwera amsonkho...Ndipo atonga ankauzani mwachiningá mu Chitonga kuti KWAZA CHIMKWAWU CHAMBULA MAZILA ADA " monga mmene timanenela mwambi omuchenjeza mnzako kuti anthu ena asamve KUTI 'PANSI NTEDZA...Ndimmene zinalili ndithu pa nthawiyo ndipo anthu angathamanga kuthawa osati zocheza....
@fatimachidima4260
@fatimachidima4260 2 жыл бұрын
Iam with you on dis one...
@FOSTERLUPIYA-zc1xv
@FOSTERLUPIYA-zc1xv Ай бұрын
Ndinu ana ndipo simdziwa kanthu uyu ngwa bodza.Angofuna kudzitchukitsa
@anniekhonje7853
@anniekhonje7853 3 жыл бұрын
Ine I left Malawi and live in Zambia koma ndima yankhula chiwewa bwino bwino,even this article am very much able kumva
@mwai72
@mwai72 3 жыл бұрын
Not the same thing...Zambia ndi Malawi they all speak a similar language.
@isaacmussa2942
@isaacmussa2942 3 жыл бұрын
Ndizoona mkulu uja sadali m'malawi ndi chifukwa dziko lathuli lili losaukitsitsa foreigner presdent sangakhare ndi chidwi chotukula dziko zidakanika pa chiyambi basi ngakhale ma plan akamangidwe kuti malawi adzioneka bwino kudavuta dziko loyamba kulamulira foreigner silingatukuke
@takondwabanda1922
@takondwabanda1922 3 жыл бұрын
Munthuyi simmalawi inu osadabwa kut amakanika ngakhale kuyankhula chichewa munthuyu anali waku Ghana nde pot kutsutsa galu mkukumba kaya wakufa sayankhula😜😜😜😜😜😜
@HellenKanyemba
@HellenKanyemba Күн бұрын
Kamuzu anali mmalawi I was a born free back then used to dance for him tsiku lomwe ankatsekulira kamuzu International Airport ineyo ndinaona ndikumva kamuzu akulankhura chichewa ndipo chomveka bwino kwambiri koma vuto lomwe ndimaona ndimaona ine ndilokuti kale muja athu olo omwe ankakhala ndi radio sanali athu wamba Maputo ake kumangokhala ma reported speech anthu tinkangovomereza zomwe wina wanena koma kwaamene nthawi zina amatha kukhala pafupi naye mmmm kamuzu was a true malawian
@thomluciouss7360
@thomluciouss7360 3 ай бұрын
This is what I was heard about the real story of our kamuzu Banda thanx for updating us always
@hamdanmasuku4800
@hamdanmasuku4800 Жыл бұрын
Thanks for this story
@richardwelliala2925
@richardwelliala2925 2 жыл бұрын
I like when you say eeeee! 😀😀😀 Keep it up. I.like your channel..watching from California USA 🇺🇸
@angelabulongo88
@angelabulongo88 3 жыл бұрын
Ngati Kenneth Kaunda anali mtonga ndiekuti sanali mtonga waku Zambia ayi course Ku Zambia kulibe mto nga yemwe mfundawake ndi Kaunda ayi kumalawi konko nkomwe kuli atonga otchedwa Kaunda osati kuzambiya ayi
@g_forcemusician4242
@g_forcemusician4242 9 күн бұрын
Kaunda bambo ake anali busa from nkhatabay full stop
@duncanchizizi6543
@duncanchizizi6543 Жыл бұрын
Very informative
@user-iv3do9vk3u
@user-iv3do9vk3u 9 ай бұрын
The truth serves us right that he was the first president of Malawi and he comes from kasungu ! Dr Banda, the son of the soil may he rest well... Anyone against that, that's your problem fotsek
@GiftBanda-jb1js
@GiftBanda-jb1js 9 күн бұрын
I agree with you
@bkelly3053
@bkelly3053 3 жыл бұрын
thanks lots nkhani yomwe tinapepha ndimenei mbuzi kamuzu anali aoukila😆
@listonnantapo1670
@listonnantapo1670 3 жыл бұрын
MChifukwachake ankangopha anthu ngati nkhumba. Amadziwa kuti ku Malawi sikunalikwawo.
@enockchipinga7668
@enockchipinga7668 3 жыл бұрын
Interesting
@abdulrafiquekalembo469
@abdulrafiquekalembo469 3 жыл бұрын
This is what we call investigative journalism.and if understood very well it can cover the truth.my advice to some of u is that don't ignore everything
@mwai72
@mwai72 3 жыл бұрын
Actually this is the TOTAL opposite of JOURNALISM, investigative or otherwise. This is total rubbish.
@abdulrafiquekalembo469
@abdulrafiquekalembo469 3 жыл бұрын
@@mwai72 you just can't digest the truth.wa Youth iwe.
@mwai72
@mwai72 3 жыл бұрын
@@abdulrafiquekalembo469 hahahaha!! No..."boni fili" weni weni ine. I think when you do JOURNALISM, if this is journalism, you need more air tight solid facts to back up what you are saying....may be that just me.
@abdulrafiquekalembo469
@abdulrafiquekalembo469 3 жыл бұрын
@@mwai72 sikukhoti,only by making comparison of things, statements,events and movements etc it can lead investigators to something and u can convict someone in court.!!!
@mwai72
@mwai72 3 жыл бұрын
@@abdulrafiquekalembo469 but courts just like journalists, deal with FACTS, right?
@nareshjatwa1643
@nareshjatwa1643 3 жыл бұрын
Thanks for the good story
@danielmaluwa7896
@danielmaluwa7896 3 жыл бұрын
@@thatlchiponda3368 iweyo ndie wabodza.This history is true koma vuto munaphunzira history ya mcp
@ellenrahman9959
@ellenrahman9959 3 жыл бұрын
This history is very interesting informative but, I wish you also had the English Chanel or English subtitles.
@brucewarchild2156
@brucewarchild2156 2 жыл бұрын
Ndi za a Malawi izi, chizungu chachani??
@pililani_blessings
@pililani_blessings 2 жыл бұрын
Yes...he shud put subtitles
@kingmanda9393
@kingmanda9393 Жыл бұрын
And Kamuzu also he had his school mate like my Grandfather Mr John Rafael leza Nkhoma who left Malawi 1914 after completing higher education at Livingstone and black Manda who died in UK my grandfather was part of the family of the loya family of Sathe kasungu but Mr Nkhoma died 2000 when he was 109 year he always told that Kamuzu was light and short man they also schooled to at old Bandawe his name Ackim kamkhwala
@thokokabanda5227
@thokokabanda5227 3 жыл бұрын
Thanks so much. Kamuzu banda analidi Ibarra kuchokera ku Ghana
@user-nf3ik3ff6y
@user-nf3ik3ff6y 9 ай бұрын
Nice story
@user-pl1tw2gn4u
@user-pl1tw2gn4u 5 ай бұрын
Well done Mr Bakili Muluzi tv
@kingmanda9393
@kingmanda9393 Жыл бұрын
The real name of Kamuzu was Ackim kamukhwala Banda his teacher Phillimon kamukhwala gogo Chirwa is the one who changed his name to Kamuzu because we're sharing the name and Kamuzu was a Malawian check The photo of Jenala Chatikha Banda ( Chatikha) means mwndida pa chitonga on the picture of the sister you will find similarities and his nephew he was residing in Soweto chawelo they looked like his nephew Nkhata
@alickwilsonthom7007
@alickwilsonthom7007 3 жыл бұрын
Program yabwino kwambiri ndithu, ndithokoze potibwezeretsa ku Sukulu mzaka za 1993, ndiri Standard 5, koma zomvetsa chisoni kwambiri kuti m'maphunziro a tsopanowa palibe History yokhudza kwambiri za dziko lathu ndi maiko ena akunja, Ndipo funso nkumati: kodi ndi chifukkwa chiyani kunabera maphunziro atsopanowa; Oti mwana mpakana Standard 3-4 osadziwabe kulemba ndi kuwerenga?
@robertkhoza
@robertkhoza 3 ай бұрын
This channel is a masterclass
@zeckbmalawi8017
@zeckbmalawi8017 9 ай бұрын
We love you boss🎉
@MayesoChingoma-zq8fg
@MayesoChingoma-zq8fg 12 сағат бұрын
Nice❤
@evertonbanda6091
@evertonbanda6091 3 жыл бұрын
This is nice story and good narration
@kcrecordsw
@kcrecordsw 3 жыл бұрын
My name is Stain Phiri. I was original member of Makasu Band with Bright Nkhata who was one of the real family members of Kamusu Banda who was actualy from Nkhotakota as his fathers home. This man must research properly. I was blessed when i met one very old man in Broadhurdt, Botswana who worked with Kamuzu in South Africa. That was in 1996 when I worked at Botswana Police. This man though he could not see properly, would talk of Hastings Banda, who was their leader as the distributed medicine around South Africa. Who would always say I remember this voice. Am sorry this man passed away, but research has be done in good faith that these lies. Am sorry
@Gundasonic
@Gundasonic 3 жыл бұрын
Even his south african storyvis dodgy... What southafrican languages did he speak ss a black man?
@mrmustdeDj
@mrmustdeDj 2 жыл бұрын
Kamuzu was a scambag dude..he was never a Malawian..13 years u can’t forget Chichewa..my niece 9 years old went straight to England not even a stopover in a Bantu country 22 years old now with perfect Nyasa language
@brucewarchild2156
@brucewarchild2156 2 жыл бұрын
Iwenso talemba chichewa tikumve asaaa, usatibhowe ndi kamuzu wakoyo
@arthursungitsa2708
@arthursungitsa2708 Жыл бұрын
This is a fake and shallow narrative. If this is a research then what a joke. In the researchers wisdom, he wants to tell us that Richard Armstrong people were all dead and didn't want to do anything with their Richard. When he died none not even one claimed their son. You want to tell us that the Ashanti and Zongo people sacrificed their Richard or they were bribed by their son to keep quiet. Do you want to tell us that at the college where the so called Armstrong and Kamuzu met they were the only ones in the classroom without other students who could easily identify Richard as Richard not as Kamuzu. Kamuzu must have bribed all.the people at University of Chicago, Scotland and Meharry medical college so that none would know him.Its not easy to fake someone's identity especially at such an International platform holding the title of a President, by now we would have been seeing claims and counterclaim from friends, relatives and peers. Kamuzu was out of power for over 5 years that was the time when all the truth would have come out from those who feared him. People can reject you when you are alive not when you are dead. This is a very fake narrative. The attempt to link Glyn Jones and Kamuzu is another failure. He claims that there is a biography do your research make it available but for this one my dear friend is CHILDISH attempt
@shashamilookofficial1951
@shashamilookofficial1951 9 күн бұрын
you're a great historian 📣
@chisomotaika4479
@chisomotaika4479 3 жыл бұрын
Maybe he was a secret agent. Who knows! Mama Kadzamira maybe will tell us this one day maybe yes maybe not. Malawian untold history.
@jamesmwakisulu8975
@jamesmwakisulu8975 2 жыл бұрын
Keep on plz
@_mindview_7707
@_mindview_7707 2 жыл бұрын
Ineyo mbiri ya kamuzu ndinaimva ndi mkulu wina wa mdziko la South Africa 🇿🇦 ndipo anandiuza chimodzimodzi kuti kamuzu sanali mmalawi,anali black American.Anachoka ku America kupita ku Ghana ngati ku exile,after atagwilira odwala mchipatala coz iyeyo anali doctor by profession.
@Byayerayera
@Byayerayera Жыл бұрын
Kamuzu remains a mystery even in death
@haroldmatemba3298
@haroldmatemba3298 9 ай бұрын
Who is that man next to kamuzu face in that picture c
@chifundozintambira52
@chifundozintambira52 2 жыл бұрын
Kodi bwana nkhani zabwinozi mumazitenga kuti keep it up
@StanlyMakulun
@StanlyMakulun 18 күн бұрын
2:49
@marcotchauya8342
@marcotchauya8342 3 жыл бұрын
Mutiuzenso za Bingu wa Mnthalika yemwe adadziwana ndi Bakili Muluzi atakumana mubungwe la COMESA
@wallacenguluwe728
@wallacenguluwe728 Жыл бұрын
the photo next to HK Banda is that of a zambian man called dingiswayo banda
@FOSTERLUPIYA-zc1xv
@FOSTERLUPIYA-zc1xv Ай бұрын
Kamuzu was a a real Malawian but was a genius that most Malawians could not believe him to be an African . That's why this is confusing to very few Malawians like you.
@xinalungu9616
@xinalungu9616 2 күн бұрын
If Kamuzu was Richsrd Armstrong WHY IS IT THAT HE USED TO SPEAK BETTER TUMBUKA than English? What I know is that even Mtambo was alleged to be a Burundi becsuse he cant speak good chewa. Kasungu is part Tumbuka n part chewa. Mphonongo, father of Kamuzu (not mentioned in Kamuzus story) was a mixed race man and son of Arab slave traders who used to manage sugar plantations at MARAVI VILLAGE in Nkhotakota. Mphonongo, before marrying naPhiri of chiwengu, Kasungu used to write from right to left, and was not a Banda. He had Swahiri Arabic blood. The name Banda was chosen as an advice warning from chiwengu to evade slave trade stories. He had his cousin called Msimuko. Msimuko went to live east of Jenda in Mzimba. Kamuzu was a SAROGATE son of a cousin of Mphongolo called MSIMUKO of Mzimba conceived around Hoho in Mzimba. Msimuko was the true father of Kamuzu coz mphonongo could not give child.
@oktagonmw3340
@oktagonmw3340 3 жыл бұрын
I like your channel.....it is very informative and educational. Keep it up
@McNeverNjanji
@McNeverNjanji 4 ай бұрын
I like your shannel
@medsonkamala9020
@medsonkamala9020 8 ай бұрын
Nkhani iyi ndi yabodza. Kamuzu anali m'Malawi weni weni. Kodi a Malawi tidakhala bwanji? Pali nthawi ina mafumu a ku Machinga ankamukana Muluzi kuti anali wa ku Mozambique chifukwa dzina lake lokanakhala Mulusi osati Muluzi akanakhala wa ku Malawi kuno. Zikomo kwambiri kumpando. A Malawi ndife anthu osakondana ndipo abodza. Mulungu azitikhululukira.
@asidialuweni5637
@asidialuweni5637 Жыл бұрын
That can happen and it is happening people do forget and that its happening even here in south Africa
@najereeliya7761
@najereeliya7761 3 жыл бұрын
Sanali mmalawi uyu
@Gundasonic
@Gundasonic 3 жыл бұрын
Clearly, he wasn't
@sulemanbhattay9618
@sulemanbhattay9618 2 жыл бұрын
Zikomo Kwambiri. Ine ndina badwa ku Mulanje and left Malawi chaka cha 1975. I live in England Koma mpaka lero, sindina iwala ku lankhula chinyanja. So how did Kamuzu forget speaking chichewa. Doesn't make sense. Makes me wonder whether he was really a Malawian or a Ghanaian
@aubreywallo1987
@aubreywallo1987 3 жыл бұрын
Ok tamva nawo
@DOMINICSELETA
@DOMINICSELETA 2 ай бұрын
Real Malawian
@user-ti4yu6ob1e
@user-ti4yu6ob1e 3 ай бұрын
KK anali mtonga from Nkhata Bay makola ace anapita ku Zambia ko cifukwa can nchito cabe😮
@lucianosamuelsergio1735
@lucianosamuelsergio1735 3 жыл бұрын
Kamuzu sanali malawi
@user-ve7rx7vj1g
@user-ve7rx7vj1g 9 күн бұрын
What about sir Geofrey colby, who was also the governor of Nyasaland by the same time.
@jacomw5797
@jacomw5797 2 жыл бұрын
The title of this story was about who was Kamuzu Banda but i didn't get it because You didn't describe it briefly
@pencilrussell4711
@pencilrussell4711 2 жыл бұрын
Something about kamuzu was not normal, imagine he had official hostess who it is very much questionable if she was not a wife. Kamuzu is very mysterious. I doubt if he was Malawian blood
@Thewarrior7093
@Thewarrior7093 10 ай бұрын
He was not a Malawian
@frankcholimbirapo262
@frankcholimbirapo262 3 жыл бұрын
Koma ndie tiziwa zambir ndith even panopa ndikatenga history k xul kamba ka inu
@salomegondwe1322
@salomegondwe1322 Жыл бұрын
Kenneth kaunda was a tonga from Malawi not tonga from Zambia
@NdhlaminieNkosi
@NdhlaminieNkosi 5 ай бұрын
Nde tiziti pa 14 paja ndi Richard Armstrong day😂
@ObedyMakhenjera
@ObedyMakhenjera 8 ай бұрын
There is no sense saying something evil against a fellow Malawian like our first President the late Dr. H.Kamuzu Banda when the truth is very clear before us.
@ranalucky6628
@ranalucky6628 3 жыл бұрын
Koma analamulirabe mkuluyu ngankhale mnene kuti sanali mmalawi
@happyrandall7783
@happyrandall7783 3 жыл бұрын
Hastings Banda was an extraordinary man who lived an extraordinary life. He was fluent in Chichewa we saw him in several occasions correcting his interpreters. Fake channel, fake news
@user-wd9yd1bg9n
@user-wd9yd1bg9n 9 ай бұрын
Ehich occasion, the guy wasn't amalawi. The only word in chichewa he new was Kwacha
@user-wd9yd1bg9n
@user-wd9yd1bg9n 9 ай бұрын
Which occasion?
@user-zp8ph8hv2b
@user-zp8ph8hv2b 3 ай бұрын
There is a grain of truth in this conspiracy.. l stayed in Mlw during his reign... Kamuzu couldn't speak Chichewa in his rallies.. He could only say the slogan .. "Kwacha"..
@geee7672
@geee7672 Жыл бұрын
Kamuzu was a true Malawian. His challenge in Chewa should not confuse people. You horn the language by consistently interacting with people. In RSA he did not live with Malawians, he lived in a Tswana household, no one has every questioned if ever he spoke Tswana, and yet we all like to question his Chewa skills. However, I agree that much of his other avatars remain a mystery. But he was a true Malawian. That Richarm Armstrong claim should be investigated with Ghana DNA rather than just rhetoric.
@mbizi4573
@mbizi4573 Жыл бұрын
That's BS. I grow up in Zimbabwe for 10 years of my life. Went to an all white school. Educated by whites. Family relocated to Canada since my mother is a white Canadian and came back in 2018 after 25 years and yet I still speak fluent Shona. That he could convince Malawians that he couldn't speak the language anymore goes on to show how gullible and stupid some of us can be
@geee7672
@geee7672 Жыл бұрын
@@mbizi4573 what is your point? What is BS?
@aubs4321
@aubs4321 3 жыл бұрын
Uyudi sanali m,Malawi. You can even see he was half cast
@ellenrahman9959
@ellenrahman9959 3 жыл бұрын
What is half cast, I find this ironic and derogatory. Even if one of his parents was not a black African he was still black because one of his parents was black. There is no such thing as coloured. This how the colonialists separated children born from African parents to look better than their own parents. The system of apartheid thrived on such divisions. This is my experience. Learn from the Australian Aboriginal how the pride themselves. Any woman, man and, child born from an Australian Aborigine, is an Aborigine regardless of whether his father or mother is an Anglo-Saxon.
@mariagoba2494
@mariagoba2494 3 жыл бұрын
Munthu obwera kapolo wa Ku Ghana kamuzu
@Gundasonic
@Gundasonic 3 жыл бұрын
🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣@kapolo
@GeraldChisokeza-er5cf
@GeraldChisokeza-er5cf 2 күн бұрын
Ooh ndimkamva koma ndikasutsa
@FrightonKandodo
@FrightonKandodo 15 сағат бұрын
He was not a true Malawian that's why he was brutally morderd the people of malawi
@jumbradoone4164
@jumbradoone4164 2 жыл бұрын
Zitha kukhala zowona kuti Kamuzu sadali m'Malawi 1): M'malawi sakadapanga chitukuko mmene adapangila Kamuzuyi,m'malawi amafuna zabwino zikhale zake. 2: Munthu ungatchonebwanji sungayiwaliletu chilankhulo chakwanu.
@sydneysimbi9821
@sydneysimbi9821 8 ай бұрын
😂😂😂
@adamkaisi6954
@adamkaisi6954 3 жыл бұрын
Thanks a lot keep on doing such reports & research
@patricklichapa761
@patricklichapa761 Жыл бұрын
I knew alot of history because of you please keep going report and research other history
@user-tw9vq6to3b
@user-tw9vq6to3b 8 ай бұрын
Kmatu anthu a ku kasungu makani pambiri ya kamuzu😊
@AbdulChamanyi-sf7gc
@AbdulChamanyi-sf7gc 7 ай бұрын
Umakwana brother
@peterarvaszulu5069
@peterarvaszulu5069 2 жыл бұрын
If the MCP committed a lot of atrocities why can't they be brought before the courts of law?it's like Malawi has not yet healed from its past political wounds. Don't you think there's need for a truth and reconciliation commission to take place now in Malawi ?
@actuarialscience2283
@actuarialscience2283 2 жыл бұрын
Izi zinakanika kalekale bwana
@mcandrewsmaunda7921
@mcandrewsmaunda7921 Жыл бұрын
It was not MCP; it was individuals within MCP who committed a lot of atrocities
@alanomanguissa3160
@alanomanguissa3160 3 жыл бұрын
ine ndinachoka ku Malawi ndi zaka 8 (1974) ndimakhala ku Mozambique /Maputo koma , mpaka lelo ndimakamba , ndimalemba chichewa. Kamudzu 13 years anawila chichewa?
@wanangwachunga9071
@wanangwachunga9071 3 жыл бұрын
Kamuzu amalankhula chichewa ndipo alipo ma videos amene amalankhula chichewa
@wanangwachunga9071
@wanangwachunga9071 3 жыл бұрын
Ndipo musiyanitse munthu okhala dziko la azungu okhaokha ndi inu amene mumatha kumakumanatso ndi a Malawi Nthawi zonse
@mwai72
@mwai72 3 жыл бұрын
Kamuzu was away for 13yrs?? Ndithu??? Try over 30yrs!!
@Gundasonic
@Gundasonic 3 жыл бұрын
And howcome his accent didnt reflect the time he spent in western world? Kamuzu history dont add up
@tisuhmakhwah7085
@tisuhmakhwah7085 Жыл бұрын
Ine ndinachoka ku Malawi ndili ndi zaka 9 ndpo ndakhala ku Britain kwa zaka 17 bwanj ndimayankhula ndi kulemba chinyanja?
@paurosi123
@paurosi123 2 жыл бұрын
Zikomo, please can you also imvestigate the history of Richard so that this can be linked and closed
@alickrebirth-sj3ci
@alickrebirth-sj3ci 3 ай бұрын
komaso amene anapanga realese Banda from gwero snali Ian mcloud pa 1 april 1960 osat glyn Johns zabodza zinazo
@jesselongwe7424
@jesselongwe7424 3 жыл бұрын
Kenneth kaunda is mtonga from nkhata bay, his father went to Zambia by missionaries , Kenneth anapita ku Zambia ali kanyamata ndi makolo akewo moti even family yachina Kenneth kaunda ilipobe ku nkhata bay .
@alickrebirth-sj3ci
@alickrebirth-sj3ci 3 ай бұрын
Kusaziwa ndi kufs komwe, wakafukufuwe komanso womverafe osaziwa sakuziwika chalowa nkhutu chalowa
@dausonmariha2195
@dausonmariha2195 Жыл бұрын
Now I know
@popboybobo4123
@popboybobo4123 2 жыл бұрын
Kamuzu mfiti ya munthu
@EDSONMAKIYI-mu8ye
@EDSONMAKIYI-mu8ye 16 күн бұрын
Sanali mmalawi
@richardwelliala2925
@richardwelliala2925 2 жыл бұрын
Tifuse nawo apa.. Mwati Kamuzu anamwalira ali ku school. Komano family inapanga kalondo londo ku school komwe anali kuti apeze zowona zeni zeni?? Story yanu nanu is confusing us.😀😀
@patlamb355
@patlamb355 2 жыл бұрын
Strange
@aleluyabanda2759
@aleluyabanda2759 3 жыл бұрын
Kamuzu was an imposter
@simbiphiri1425
@simbiphiri1425 3 жыл бұрын
Kaunda is not a Zambia Tonga but Malawian Tonga, the two Tongas from these countries are not the same , research better.
@isaacbanda2973
@isaacbanda2973 3 жыл бұрын
Which is which?
@isaacbanda2973
@isaacbanda2973 3 жыл бұрын
Mwana wa zaka 13 sanhayende ulendo wa pasi mpaka ku South Africa
@eunicemoyo5808
@eunicemoyo5808 3 жыл бұрын
yaa zambia malawi paja kale akut adali dziko limodzi ndye ndizosadabwisa kaunda kupezeka ku zambia or malawi
@yamikanimwenda1800
@yamikanimwenda1800 3 жыл бұрын
Am a fully Zambian what I know is that Kaunda was a Malawian
@MasaukoPhiri-rp2oe
@MasaukoPhiri-rp2oe 2 ай бұрын
Mkuluyu ngwabodza
@andrewbanda9661
@andrewbanda9661 Жыл бұрын
Kenneth Kaunda was not Tonga but bemba from chinsali and parents came from malawi
@MaggieYassin-tv7sf
@MaggieYassin-tv7sf 11 ай бұрын
Achilungamo ndi inu Ndekuti?
@jesselongwe7424
@jesselongwe7424 3 жыл бұрын
Manowah chirwa was mtonga from nkhata bay not mtumbuka
@goodwellchanunkha1971
@goodwellchanunkha1971 10 ай бұрын
Ine ndimakaikila kuti Kamuzu anali mmalawi nzathu anali wamwano udyo no wonder minyama simatithela mmalawi muno
@stanleydamalekani2398
@stanleydamalekani2398 3 жыл бұрын
I'm very sad with my country:(
@omegasheibamussa3900
@omegasheibamussa3900 3 жыл бұрын
AMalawi anali zisilu kwambili murola bwanji mutu wakut sakuta kuyakula shishewa ndikumuika phuresiethet mbola Ndi shifukwa shake kumalawi ndikovutika simunaganize bwino inuyo amene munali akulu akulu tawi imeneyo 1966 mbola kamuzu siwakumalawi siwakumalawi siwakumalawi 🏁🏁🏁🏁🏁🏁🏁😭😭😭😭😭😭😭🔒🔑🔧🔫🐑🦍🦍🦍🦍🦍🦍🦍
@miryamkatundulu
@miryamkatundulu Жыл бұрын
Osamawanamiza anthu
@patrickmatiki4778
@patrickmatiki4778 Жыл бұрын
Mr AW
@benimbewe1811
@benimbewe1811 Жыл бұрын
Yes,we had leakages about this man playing a big coverup in human history when we were in school around 1986....
@alickwilsonthom7007
@alickwilsonthom7007 3 жыл бұрын
Pitirizani kuti patsa zambiri
@rainfordisaacs6789
@rainfordisaacs6789 Жыл бұрын
Kenneth Kaunda sanali mutonga
@bongomafia4409
@bongomafia4409 3 жыл бұрын
Timakunyadirani. Pitilizani ndithu tikudziwa zambiri zobisika pano
@user-zp8ph8hv2b
@user-zp8ph8hv2b 3 ай бұрын
This conspiracy can be true... The Life president of Malawi ..
@user-dm3bb4of9d
@user-dm3bb4of9d 9 ай бұрын
Kamuzu anali khuluku mbava chigawengaaa.munthu ameneyuu ehee
@nellietchuwa9913
@nellietchuwa9913 3 жыл бұрын
Why dobu mean by saying "keneth Kaunda anali mtonga"? U mean now he is not tonga or he passed away 😂
@alepelemgwamgwa8006
@alepelemgwamgwa8006 3 жыл бұрын
He was an imposter
@omegasheibamussa3900
@omegasheibamussa3900 3 жыл бұрын
Sizinaveke baba ndeno mwanenakut munena shisisi shakamuz????????
@henrynyirendahk-f5k
@henrynyirendahk-f5k 2 күн бұрын
Was chewa by tribe
@StoreNkhoma-ii2lo
@StoreNkhoma-ii2lo 6 ай бұрын
Akuluakulu aMCP a nthawiyo anali GAWANDA,AMULUZI,ATEMBO,ANTABA ndi ena ndiye kuti inuyo mukutanthawuza kuti ndiwo ankanamiza aMalawi.
@StoreNkhoma-ii2lo
@StoreNkhoma-ii2lo 6 ай бұрын
NDATITU MR.GWANDA CHAKUWAMBA
@danielchulu1933
@danielchulu1933 2 жыл бұрын
Mambala iwe Kenneth Kaunda was a chewa born to Malawian parents not a Tonga
@politicalspider8175
@politicalspider8175 2 жыл бұрын
The foreigner ruled Malawi. He was very evil.
@fatimachidima4260
@fatimachidima4260 2 жыл бұрын
😅 😅 😅 😅 Yeah
Kamuzu Academy - Malawi - "The Eton of Africa" (1987)
49:37
kasiyamaliro
Рет қаралды 45 М.
FOOLED THE GUARD🤢
00:54
INO
Рет қаралды 63 МЛН
МАМА И STANDOFF 2 😳 !FAKE GUN! #shorts
00:34
INNA SERG
Рет қаралды 4,3 МЛН
My little bro is funny😁  @artur-boy
00:18
Andrey Grechka
Рет қаралды 13 МЛН
6 - Albert Muwalo Nqumayo, Focus Gwede and  Kamuzu - Documentary
14:06
Zifukwa zomwe Brian Banda anachoseredwa ntchito
9:55
Sam Malvitha
Рет қаралды 112 М.
Samora Machel visits Malawi (Complete)
18:26
Samora Machel
Рет қаралды 1 МЛН
Manganya in Munthu 22
11:17
Edson Gunsalu
Рет қаралды 92 М.
Once upon a time in Ghana
23:50
Bakili Muluzi TV
Рет қаралды 34 М.
LUCIUS BANDA EXCLUSIVEINTERVIEW - 20 MAY 2021
56:54
Joab Frank Chakhaza
Рет қаралды 108 М.
FOOLED THE GUARD🤢
00:54
INO
Рет қаралды 63 МЛН