Once upon a time in Ghana

  Рет қаралды 34,963

Bakili Muluzi TV

Bakili Muluzi TV

3 жыл бұрын

Kamuzu Banda mdziko la Ghana

Пікірлер: 99
@mapatayusu4371
@mapatayusu4371 3 жыл бұрын
George chaponda anakhalanso kunja zaka 30 koma amatha kuyankhula chilomwe ndi chichewa chomwe meke ntewa nayanso anakhala zaka zambiri koma amatha kuyankhula chiyawo
@johaneskampila9915
@johaneskampila9915 3 жыл бұрын
Izi zimandivetsa chison ,ena mpakapano akunthandizabe azungu Ku Afrika kuno ,kuwapatsa malo mwachinyengo,kulola kuzunza antundu wawo +........
@Africasfinest11
@Africasfinest11 3 жыл бұрын
Nanga mutani. Kamuzu kulibe. Zikanakhala bwino akadakhala alipo tikadaganiza mwamtundu wina.
@Justman34_dislike
@Justman34_dislike 3 жыл бұрын
This is investigative journalism
@alexanderkaunda9554
@alexanderkaunda9554 3 жыл бұрын
Malawi unagona kale tulo monga awemba ndi kaunda
@kassimjuma8822
@kassimjuma8822 3 жыл бұрын
Kkkkkkkkkkkk
@macmillanmakombe7142
@macmillanmakombe7142 Жыл бұрын
Kkkkkkkk
@dalitson3558
@dalitson3558 3 жыл бұрын
We love you brother
@allanbanda4388
@allanbanda4388 Жыл бұрын
Km pls muziyesetsa kutiuza zoonad coz ndakwiyat kwambili kulakalaka nditadyela msima thupilake mfiti imeneyooo
@homeremedys3748
@homeremedys3748 Жыл бұрын
Kamuzu ankayankhuranso chichewa, Ankawakoza chichewa ma interpreters nthawi zina pa nsokhano
@medsonboti1984
@medsonboti1984 3 жыл бұрын
Mutipatse mbiri ya Kamuzu wathu weniweniyo tiyidziwe.
@johndulla7705
@johndulla7705 3 жыл бұрын
This is good story bro. Keep it up the good work
@majiyabanda4510
@majiyabanda4510 3 жыл бұрын
You're the best bigman
@kasaukephiri635
@kasaukephiri635 3 жыл бұрын
Kkkkkkkk chipumi ndende anthu Aku Ghana
@allanmakwiti5145
@allanmakwiti5145 3 жыл бұрын
This is good history worth listening to 🙏🏼
@memoryfrancisco6558
@memoryfrancisco6558 3 жыл бұрын
Anali obwera uyu.
@kalimawandale7161
@kalimawandale7161 Жыл бұрын
Those that know Kamuzu's Tumbuka and Chewa ascent know that he was a real Malawian, if you talk about him killing people you will find that in those days politics was about killing opponents all over the world
@user-ie5pc4ox8i
@user-ie5pc4ox8i 5 ай бұрын
Nde a wat chakwera amubera carpet😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂
@temwachi9992
@temwachi9992 3 жыл бұрын
Nkona amapha anthu ozindikira????zoopsa And how come mpaka kumakanika kuyankhula language yakwawo.hmmmm
@twisimwaighogha1822
@twisimwaighogha1822 Жыл бұрын
The British Government should now declassify Kamuzu's file.
@isaacbanda2973
@isaacbanda2973 3 жыл бұрын
Kamuzu Banda was real devil in a human form
@jeromeuriah7235
@jeromeuriah7235 3 жыл бұрын
you prolly dont give a shit but if you guys are bored like me during the covid times then you can watch all the new series on instaflixxer. Have been watching with my gf recently =)
@harrylouie7955
@harrylouie7955 3 жыл бұрын
@Jerome Uriah Yup, have been watching on InstaFlixxer for years myself :)
@alexanderkaunda9554
@alexanderkaunda9554 3 жыл бұрын
Nanga asilikali ndi apolice anagonabwanji
@bobkenneth2947
@bobkenneth2947 9 ай бұрын
This's real history,ulemu wanu Bigman pitilizani kupanga expose anthu amenewa
@abudardachilangwe6791
@abudardachilangwe6791 3 жыл бұрын
Ine chomwe ndisakumvesa ndichoti why mama kadzamila sakufuna kulemba book la life ya kamuzu banda ngati iye munthu mmodzi yemwe akumudziwa dr banda kuposa wina aliyense
@g_deonm5793
@g_deonm5793 3 жыл бұрын
Chifukwa ntchito anthu akhoza kukuukila mama pothandiza kubetsa dziko...ichi ndi chinsisi chomwe adzalowe nacho mmanda pofuna mtendele. Koma boma litafuna kuti anthu adziwe izi akhoza kufufuza ndikulemba mwatsanetsatane chilungamo chomwe..but they choose the easier path: " pretending not to know".
@shabbanusuf5096
@shabbanusuf5096 3 жыл бұрын
We love you brother keep it up
@frankcholimbirapo262
@frankcholimbirapo262 3 жыл бұрын
Tikuziwa zambr via pa phone
@wycrefkambalah4753
@wycrefkambalah4753 Жыл бұрын
Inuyo ndiye mulendo apa. If timalankhula nate chichewa ndichitumbuka bwino bwino.
@martinnyirenda3096
@martinnyirenda3096 2 жыл бұрын
So lovely and very true story
@lamecknyadani1905
@lamecknyadani1905 10 ай бұрын
Tisazamve kamuzu Banda stadium.... Sanamangepo stadium mkulu wa ku Ghanayi
@lamecklipenga855
@lamecklipenga855 Жыл бұрын
At least Kamuzu helped those who may say they are real Malawians yet stealing and stealing.
@giftmingo9293
@giftmingo9293 Жыл бұрын
You're a genius Comrade
@frasernamaona6526
@frasernamaona6526 3 жыл бұрын
Sanali mmalawi uyu ada Kamuzu
@leonardmchiela6533
@leonardmchiela6533 Жыл бұрын
That is his original home country
@EBBOY-nl7gr
@EBBOY-nl7gr Жыл бұрын
Ine munthu uyu sindimawonanso chifukwa chake chomwe amamuyikira pa pepala la ndalama
@chelseajackson3200
@chelseajackson3200 3 жыл бұрын
He could easily be Kwame's cousin even brother.
@shabbanusuf5096
@shabbanusuf5096 3 жыл бұрын
This is really Ghanaian we don't have these faces in Malawi
@osamabinraden9391
@osamabinraden9391 3 жыл бұрын
Adali wa Ku Ghana sadali m'malawi
@yaissah4518
@yaissah4518 3 жыл бұрын
Za chipumi is true
@georgeamosi9931
@georgeamosi9931 Жыл бұрын
Very good!
@jkfodya9997
@jkfodya9997 Жыл бұрын
Ndavula kachisoti bwana
@osamabinraden9391
@osamabinraden9391 3 жыл бұрын
😁😁😁😁Dzaka 31 lokomwana Ku Malawian adali chumba m'dalawu😁😁😁😁😁😁😁😁😕😕
@giftmingo9293
@giftmingo9293 Жыл бұрын
Kojo Botsio
@williammaseko8542
@williammaseko8542 3 жыл бұрын
This guy knows how to dig deep with investigations based on facts. I enjoy watching and listening to your videos. Keep the fire burning for us to see the flames. You rock.
@charlesmuyaya8839
@charlesmuyaya8839 3 жыл бұрын
@@ishmaelchiponda5471 iweyo ukuchita kudziwa kuti a MCP ankaletsa wina aliyense kulemba history ya Kamuzu. Mabukhu ambiri anachitidwa ban Ku Malawi kuno. Iweyo ukunena zopusa zakozo potengera history yabodza imene ankakuphunzitsa a MCP. But the truth is that there are many books that said Kamuzu Banda's real name was Richard Armstrong. Go and read the book titled post colonials in Africa.
@johndulla7705
@johndulla7705 3 жыл бұрын
@@ishmaelchiponda5471 ndie tiuze iweyo kuti ndi chifukwa chani mnthawi ya ulamuliro wa kamuzu tinkaphunzira Ashanti kingdom ya ku Ghana mu syllabus ya Malawi? What great was Ashanti kingdom to be in our syllabus instead of other tribes near us?
@johndulla7705
@johndulla7705 3 жыл бұрын
@@ishmaelchiponda5471 of course it is true kuti mnthawi ya kamuzu kunalibe chilungamo and Ana sankadziwa zoona zenizeni zokhudza history chifukwa zambiri ankangonyepula, komanso mabukhu ambiri amene ankalemba chilungamo ankaletsedwa kuwerengedwa ndi Ana mmasukulu. Ndikupatse chitsanzo cha bukhu la Norman Lowe limene linaletsedwa kuwerengedwa ndi Ana mmasukulu mnthawi ya kamuzu. If you know history of the world you can understand that Norman Lowe books are one of the best history books in the world. And mcp govt banned those books, do you think Ana akanadziwa bwanji history yabwino without reading those books? .
@charlesmuyaya8839
@charlesmuyaya8839 3 жыл бұрын
@@ishmaelchiponda5471 iwe anthu anachangamuka nthawi ya Muluzi. Ana ozindikira anayamba kupezeka nthawi ya Muluzi. Nthawi ya Kamuzu Banda kunali mbuzi zokhazokha zodziwa ma types of grasshopper. Nthawi ya Bakili Muluzi ana ankawerenga mabukhu enieni okhudza mbiri za dziko lapansi. Even syllabus ya Malawi anayisintha tinkaphunzira world history 1 and 2. Mnthawi ya Kamuzu Banda kunalibe zimenezo.
@charlesmuyaya8839
@charlesmuyaya8839 3 жыл бұрын
@@ishmaelchiponda5471 iwetu ukuonekeratu kuti ndiwe mbuli. Mnthawi ya Kamuzu Banda mu syllabus kunalibe cold war, world war 1, world war 2, Vietnam war, even Cabinet crisis 1964 sanayikemo. Ma history akuluakulu okhudza dziko lapansi kunalibe mu syllabus ya mcp
@basiliojeremias6200
@basiliojeremias6200 2 жыл бұрын
Ndipo kwamenkruma akufana khope ndi Kamuzu banda
@lamecknyadani1905
@lamecknyadani1905 10 ай бұрын
Kamuzu Banda tamuchosa mu history ya Malawians kkkkk
@bobkenneth2947
@bobkenneth2947 9 ай бұрын
He was not a Malawian citizen
@dastahchikwekwe7864
@dastahchikwekwe7864 3 жыл бұрын
Who can say the trueth about kamuzu banda ok it seems like he was not amalawan by his language mama may be can know if he was not a malawian it's so shame to malawian
@dorikakamwendo6970
@dorikakamwendo6970 3 жыл бұрын
Anali Foreigner uyu
@chelseajackson3200
@chelseajackson3200 3 жыл бұрын
The government should take Kadzamila, Kazombo, Mzaza family to courts on supporting Kamuzu. They leave on the stolen money that kamuzu store from taxpayers.
@wizahsimbeye3227
@wizahsimbeye3227 3 жыл бұрын
Kodi bwanji osafusa za Cecilia Kadzamila za Kamuzu Banda Mesa she is alive you are now too much on Kamuzu Banda. Kwame Ncluma was a nationalist nde why Kamuzu Banda was if he Kamuzu was supporting azungu a Ku RSA?
@memoryfrancisco6558
@memoryfrancisco6558 3 жыл бұрын
Cecilia kadzamira sanganene chilungamo. Ndi magulu okhaokhawo amene anakhala akubisa chilungamo for 31 years. So don't expect any truth from that evil woman. Everything she can speak out on her mouth can be all lies
@peteruko
@peteruko 3 жыл бұрын
Zipumi? Lol !😂
@edwingondwe2860
@edwingondwe2860 3 жыл бұрын
Pitirizani kutiuza za mbiri zobisika
@johnchavula3282
@johnchavula3282 Жыл бұрын
nice
@emmainvestmentgroupofcompa3355
@emmainvestmentgroupofcompa3355 3 жыл бұрын
Kukafukla kumumenya ndikupanga deported. Gana or kungomutaya ku shire
@peterarvaszulu5069
@peterarvaszulu5069 2 жыл бұрын
Why was kamuzu Banda not arrested posthumously for the evils he caused on innocent people
@umaliisah6920
@umaliisah6920 3 жыл бұрын
We follow u
@Sikhakhane2
@Sikhakhane2 10 ай бұрын
He was really devil 😈 this man
@stevenchirwa5028
@stevenchirwa5028 Ай бұрын
Straight to jail
@charlesmuyaya8839
@charlesmuyaya8839 3 жыл бұрын
What you are talking is making sense somehow. Analephera bwanji kulankhula chilankhulo cha makolo ake for the rest of his life.
@eltonmpiro8738
@eltonmpiro8738 3 жыл бұрын
Samalakhula even chichewa?
@charlesmuyaya8839
@charlesmuyaya8839 3 жыл бұрын
@@eltonmpiro8738 inde kaya sankalankhula Chichewa. Anangolankhula kamodzi komanso chochita kuwerenga choonera pa bukhu
@memoryfrancisco6558
@memoryfrancisco6558 3 жыл бұрын
Anali foreigner
@charlesmuyaya8839
@charlesmuyaya8839 3 жыл бұрын
@@ishmaelchiponda5471 akanakhala kuti ankadziwa kulankhula Chichewa ndie bwezi atalemba ntchito interpretor? Kodi mukuona ngati munganamizenso munthu lero? Anthu anapenya masiku ano ndipo akudziwa kuti Kamuzu Banda anali foreigner
@charlesmuyaya8839
@charlesmuyaya8839 3 жыл бұрын
@@ishmaelchiponda5471 ndie unamuona Mandela atalemba ntchito interpretor omasulira chizulu pa msonkhano wake? Kapena unamuona Mugabe atalemba ntchito interpretor omasulira Chishona? Mandela and Mugabe were speaking English poyenera kulankhula English, koma ankapanga communicate ndi anthu a kumidzi mchilankhulo chawo. Not this Kamuzu Banda who was speaking English to the rural masses where there was more uneducated people
@duncankamanga3461
@duncankamanga3461 3 жыл бұрын
Kodi tikungomva kuti kale kunali ulamulilo wa chipani chimodzi,ngakhale munthawi ya atsamunda,koma tikamamva mbiri tikumvamo kuti zipani zina zinaliko.ziwona zenizeni ndi ziti?
@duncankamanga3461
@duncankamanga3461 3 жыл бұрын
Okay ndamvetsesa ndiye kuti zipanizo zinali zosabvomelezeka kuno Ku malawi. Chabwino
@tritondiver3449
@tritondiver3449 2 жыл бұрын
Kamudzu tsadali Malawi
@tonyomondi2683
@tonyomondi2683 3 жыл бұрын
Please narrate in English so that others can understand
@alexanderkaunda9554
@alexanderkaunda9554 3 жыл бұрын
Amalawi ndi kuwudzeni vuto ndilakuti amalawi tulo (1)kuopa kwambili asilikari ndi apolice ndi chifukwa mbudzi dzikakhala pampando dzimagwilisa ntchito asilikali ndi apolice kuophyedza anthu ( tithokodze asilikali apano chifukwa akuona m'mene dziko likuyendela pomalidza chakwera ndi chilima musamale
@alexanderkaunda9554
@alexanderkaunda9554 Жыл бұрын
That is point kuopa kwambili apolice ndi asilikali komaso naonso ndi osauka
@piperharder7436
@piperharder7436 3 жыл бұрын
Kamuzu analidi jabulosi koma za nkazi wake panopo zli pati
@chelseajackson3200
@chelseajackson3200 3 жыл бұрын
The reporter needs to go to Ghana and dig out Kamuzu village, his relatives & friends on identity issues. I for one believed that kamuzu was never a malawian.
@charlesmuyaya8839
@charlesmuyaya8839 3 жыл бұрын
@@rickchipo4140 it's true story kungoti amalawi ambiri anapusitsidwa mu ulamuliro wa MCP. Kamuzu Banda was not a Malawian.
@chelseajackson3200
@chelseajackson3200 3 жыл бұрын
People in the clan of Kazombo, JZT, Kadzamila, Mzengereza know the truth but love of money/benefits they keep quite. If Muluzi had genuine love for the country, he could have challenged Kamuzu on this but alas, kuba basi.
@louiskagona
@louiskagona 2 жыл бұрын
Zinachitika basi. He ruled Malawi with integrity Than enawa
@drjoetheu
@drjoetheu 3 жыл бұрын
The more the narrator points to Kamuzu's background as a Ghanaian, the more he is losing credibility because he is using very lame arguments. For example, he uses the similarity of foreheads in Kamuzu's picture and that of Kwame Nkruma's. This is a very weak argument which may not stand serious critical examination . He keeps referring to knowledge of a foreign language and failure to speak one's mother tongue as another very strong proof that one is not from his claimed motherland; again another weak argument. As he continues to use such weak arguments, he begins to lose followers who may have been convinced in earlier episodes. For one, I have followed the few times that Kamuzu spoke Chichewa and Chitumbuka and on all occasions I was convinced beyond doubt that his accent was that of one from Kasungu-for example; he pronounced "weni weni" as "wene wene". In Malawi, this kind of pronunciation is common in Kasungu. People from Kasungu are usually very good at Chitumbuka as well. He seemed to speak very good Chitumbuka. This to me more than pin points his home village, right in Kasungu. Please revisit these points and reconsider your points when making arguments on Kamuzu's Malawian origin and other historical arguments in general. Otherwise, this is a good initiative with so far reasonable output.
@charlesmuyaya8839
@charlesmuyaya8839 3 жыл бұрын
Kamuzu Banda was not speaking Chichewa or even chitumbuka. Don't cheat people here. Even me I can teach someone chizulu just by reading like the way Kamuzu was reading at the podium. That doesn't mean he was speaking Chichewa or chitumbuka. Where in the world Kamuzu Banda spoke Chichewa or chitumbuka without reading on the paper? Inu mukunena zoonera pa likasa lochita kulemberedwa?
@g_deonm5793
@g_deonm5793 3 жыл бұрын
The narrator posses a good argument a good point. I like his points, even if they may not stand to prove his point beyond reasonable doubt in the court of law but they provoke ones thinking and provide alternative reasoning. We are enjoying this...!
@charlesmuyaya8839
@charlesmuyaya8839 3 жыл бұрын
@@qonttransportltd7027 olo mutsutse Kona zomwe akunena munthuyu ndi zoona. Amfumu a Mwase ake ati amene ankalemberana makalata ndi Kamuzu? Iweyo ukunena zimenezo potengera mabodza amene unkanamizidwa ndi a MCP koma choti udziwe nchakuti Kamuzu Banda anayamba kudziwika ndi anthu Ku Malawi kuno mzaka za man 1950s. Zina zonse zimene umamva zokhudza Kamuzu it's just a makeup by MCP gurus for you to believe that he was indeed a Malawian. Zoti ziliro mumba ankadziwana ndi Kamuzu ndi zabodzanso, don't believe those lies. Ziliro mumba died in 1945 and he don't know Kamuzu. Zomwe ukunenazo ukunena potengera information imene ankakunamiza a Kamuzu Banda was not a Malawian and that's why he was making sure to block everyone to write his biography. Mnthawi yake kunali ulamuliro wa chipani chimodzi and he denied access to information regarding his biography. He was not even speaking Chichewa don't cheat us here. Tell us that Kamuzu was just reading Chichewa chimene ankachita kulemberedwa ndi ma advisors ake. We have the videos and there was nothing like speaking Chichewa.
@charlesmuyaya8839
@charlesmuyaya8839 3 жыл бұрын
@@qonttransportltd7027 iwe ngombwambwanadi eti. Unayamba utayiona degree ya Kamuzu Banda kuti inali ndi dzina la Kamuzu Banda? Degree yake ya za udokotala anapangira mdziko la United States of America not Britain. And ankalephera kuwaonetsa anthu. In 1959 MP Mr Whitewick anamuuza kuti aonetse macertificate ake ngati anali ndi dzina la Kamuzu Banda, Kona Kamuzu sanaonetse. Komanso atangobwera kumene able ake adamukana Ku kasungu ponena kuti amene uja sanali Kamuzu. And you know kuti anthu amenewa anachita kutsekedwa pakamwa ndi ndalama at that time. There was an old woman there who claim that Kamuzu anali ndi chipsera Kunkhope kwake pomwe uyuyu analibe. Ngakhale pomwe anali president, he detained alot of people amene anali able ake Ku kasungu ngati njira imodzi yowaopseza kuti asaulure.
@memoryfrancisco6558
@memoryfrancisco6558 3 жыл бұрын
@@qonttransportltd7027 mmmh, palibepo za u cadet apa nanu. Kuzolowera kudana ndi chilungamo basi. Instead of bringing real argument basi waganiza kuti uzitchula macadet. Kungosonyezeratu kuti cadet ndi iweyo amene ukufuna kumanamiza anthu pano kuti Kamuzu anali mmalawi
The low-minded Kamuzu Banda and his tribalism ideas
26:50
Bakili Muluzi TV
Рет қаралды 22 М.
Tanzania Vs Malawi Lake Dispute PART 2
20:42
Bakili Muluzi TV
Рет қаралды 48 М.
你们会选择哪一辆呢#short #angel #clown
00:20
Super Beauty team
Рет қаралды 14 МЛН
That's how money comes into our family
00:14
Mamasoboliha
Рет қаралды 7 МЛН
Tom & Jerry !! 😂😂
00:59
Tibo InShape
Рет қаралды 65 МЛН
Children deceived dad #comedy
00:19
yuzvikii_family
Рет қаралды 8 МЛН
Malawian President who had mental illness.
18:14
Bakili Muluzi TV
Рет қаралды 27 М.
THENGO MALOYA ON CABINET CRISIS
30:42
Joab Frank Chakhaza
Рет қаралды 9 М.
African President who was killed in 2021 (Idris Déby Biography)
17:49
Bakili Muluzi TV
Рет қаралды 30 М.
Who killed Evison Matafale?  Adaferanji Evison Matafale?
21:20
Bakili Muluzi TV
Рет қаралды 142 М.
Leonard Dembo Biography, Facts & Death
20:41
Bakili Muluzi TV
Рет қаралды 31 М.
Mbiri ya Mama Cecilia Kadzamira
29:43
Bakili Muluzi TV
Рет қаралды 206 М.
ONCE UPON A TIME in GHANA [  GHANAIAN MOVIE ]
56:51
TWI NATION TV
Рет қаралды 8 М.
你们会选择哪一辆呢#short #angel #clown
00:20
Super Beauty team
Рет қаралды 14 МЛН