BON KALINDO 8 JULY 2024 BIG MAN WAFIKASO PA MONDAY

  Рет қаралды 19,594

Malawi Trends TV

Malawi Trends TV

18 күн бұрын

Пікірлер: 74
@JosephMichael-x7v
@JosephMichael-x7v 15 күн бұрын
Kungotiphera bon kalindo muzakhala nkhondo mmalawi
@MacleanKwacha
@MacleanKwacha 15 күн бұрын
Our president komaso mukudziwa kuti kulilongwe kuno kukuyenda anthu akuitanisa chiphaso chauzika,kumat akuchita kalembera oti pakamachitika zitukuko zaboma asamavutike kupita kwamfumu azingotenga mukaundula?Tifufuzileni mutiuze zoona.
@JamesEuginio
@JamesEuginio 15 күн бұрын
Bwana kalindo mugwirane mana ndi comrade mtambo chifukwa iwowo alibe tulo komaso ngati Malawi first itafuna kuima pa zisankho Malawi ambiri tikondwa inu bwana kalindo tikuona usogoleri mwa inu chifukwa kumuyankhulira mphawi yemwe alibe mawu sikophweka koma kuyankhulira olemera omwe pamapeto pake munthu amalipidwa choncho inu bwana timakupemphererani mulungu agwirise ntchito inu kuti satana achite manyazi kuno kumangichi makanjira
@EllenPhiri-xt8pt
@EllenPhiri-xt8pt 15 күн бұрын
Bon kalindo and antanyuwa bolaso munakangoimila u president that anthu amenewa angokhala chete akusekelela zomwe chakwelayu akuchitazi😢😢😢
@user-pv9uk6sc3w
@user-pv9uk6sc3w 15 күн бұрын
UTM, AFORD, DPP and UDF must make an alliance and win government, Chakwera out, useless government.
@inessmsiyambiri8517
@inessmsiyambiri8517 15 күн бұрын
Koma otsutsa akewa makape
@MikeArthur-jd2ij
@MikeArthur-jd2ij 15 күн бұрын
You are right
@JinishgiftMbalaka
@JinishgiftMbalaka 14 күн бұрын
Km za alliance zikumabweresa udani mmmm better aliyese azpangile yekha
@user-pv9uk6sc3w
@user-pv9uk6sc3w 14 күн бұрын
@@JinishgiftMbalaka vuto payekha payekha sangafike 50+1 yomwe yikufunika.
@MastonStanley
@MastonStanley 14 күн бұрын
Maganizo abhoo
@EllenPhiri-xt8pt
@EllenPhiri-xt8pt 15 күн бұрын
Keep it up mr DC
@watsonmhango8794
@watsonmhango8794 15 күн бұрын
Zoona Mr DC president wa Anthu osauka
@EVERSONGalatia
@EVERSONGalatia 15 күн бұрын
UTM PDP AFORD CFT PP and UDF must make alliance
@voicedumathindwa
@voicedumathindwa 15 күн бұрын
Mnthuyi ambuye amdalise akumenyadi ufulu
@BlessingswazaDyress
@BlessingswazaDyress 16 күн бұрын
Fantastic DC
@HenryKeyala
@HenryKeyala 15 күн бұрын
Loud and clear
@SigoMw
@SigoMw 15 күн бұрын
Onse mapulezidenti opuma Ali nkhwinthi ngati akumetetsa kwa kaondo ku 36, akupweteketsadi mtima chifukwa palibe akumveka kupatula inu akalindo. Ma radio ndi ma TV pa Malawi kulibe ife tikudalira inu akalindo, amtanyiwa ndi Wa bakili muluzi.
@user-ul1fb4yn5o
@user-ul1fb4yn5o 15 күн бұрын
Bon kalindo machine,, koma Aford, UDF, Aford komaso DPP khalan maso
@IssahAluba
@IssahAluba 14 күн бұрын
ndipo Pena gati useke president mpaka kuligawa dziko ai zikomo kuphandoko mulungu akudalitseni
@JefulyPesulo
@JefulyPesulo 15 күн бұрын
Keep up DC
@DavieMuziwo
@DavieMuziwo 15 күн бұрын
Best DC
@taneesharkamwendo8710
@taneesharkamwendo8710 14 күн бұрын
president wanga wanga vote yanga
@user-pn8lc7vq8b
@user-pn8lc7vq8b 15 күн бұрын
Kodi mesa a UTM anachita kuchokera ku zipani opositionizo? Akukolola zimene anafesa amenewo.
@MwanundaEmmanuel-nb5dk
@MwanundaEmmanuel-nb5dk 15 күн бұрын
Keep it up the dc
@Chiso2019
@Chiso2019 15 күн бұрын
Ine koma opposition yi.....imamunamizila kut akusokoneza ndi anankhumwa,nankhumwa anakuchokeraniko ife timayesa ziyamba kubebano koma manyaka okhaokha
@FaithDonald-ts2pp
@FaithDonald-ts2pp 15 күн бұрын
The dc❤
@peterchimatiro4093
@peterchimatiro4093 15 күн бұрын
The DC
@AndrewKonondo
@AndrewKonondo 15 күн бұрын
Bwana DC, ipatseni moto tili nanu, akapangaso chibwana zodzabera chisakhocho tidzangomenyanapo mmalawi muno, ndi mbuzi za anthu
@user-ri8em6my2e
@user-ri8em6my2e 15 күн бұрын
Koma azipani zotsutsa tapanganipo kanthu inuuuuuu Bon Kalindo ndiye akuyesetsa kukutsinani khutu ndipo CHAKWERA ndinduna zake akufuna kupitiliza kuba mubomali😢😢
@ChifundoNinje
@ChifundoNinje 15 күн бұрын
Abale a dpp mukutani
@CostanceLalli
@CostanceLalli 15 күн бұрын
This government must go out we don't need this mcp
@RobertKanaphwatiwa
@RobertKanaphwatiwa 15 күн бұрын
Ulemu wanu mr Kalindo tulutsani ndondo nthawi yakwana bwana
@MikeArthur-jd2ij
@MikeArthur-jd2ij 15 күн бұрын
Thus our DC 🔥
@ZettaImuranYunusu
@ZettaImuranYunusu 15 күн бұрын
Mr dc dziwani Izi... Zipani Izi DPP UDF AFORD ADD onsewo a kupanga zinthu zoti ayimile mu 2025 Ndipo inuyo musakayikenso ai
@ashrafffaque
@ashrafffaque 16 күн бұрын
Machine athu The DC
@user-bo1kt3nq6j
@user-bo1kt3nq6j 15 күн бұрын
Matiimilila DC Landilani ulemu wanu
@MuneerYusuf-py1lz
@MuneerYusuf-py1lz 15 күн бұрын
Komadi afasa kwambiri azuzeni
@trustchiwalo9225
@trustchiwalo9225 15 күн бұрын
Eiish!!
@AliciaMaphanga
@AliciaMaphanga 15 күн бұрын
Powerful the DC❤❤❤
@MacleanKwacha
@MacleanKwacha 15 күн бұрын
Ineyo ndkunena pano ,dzulo laliwisi moti akazanga achita kukana kuti mwina akufuna kubwera zisankho
@user-re7fo3be2z
@user-re7fo3be2z 15 күн бұрын
Awawa achoke a MCP
@PemphaChina
@PemphaChina 16 күн бұрын
From njedza village
@user-xt5in6nu2h
@user-xt5in6nu2h 15 күн бұрын
Ubwino wake achewawo ali m'boma
@DalitsoMatope
@DalitsoMatope 15 күн бұрын
Munthu uyi mulungu azimutetedza until mcp out of power,,,,Dpp ,,Afford,,udf,,,,why are you not listen to kalindo
@SmilingFishingRod-zc4wx
@SmilingFishingRod-zc4wx 15 күн бұрын
Nkhani yonveka bwino Nanga a Mwananveka muli kwanikiii? Monga inu.
@LameckBanda-ph2nh
@LameckBanda-ph2nh 15 күн бұрын
The DC ❤❤❤❤
@user-wu8kp7ui5j
@user-wu8kp7ui5j 16 күн бұрын
The DC 🔥🔥🔥🔥🔥
@user-wx1ri9xv3f
@user-wx1ri9xv3f 14 күн бұрын
🙏🙏🙏🙏🙏
@YasinMusa-ym8lp
@YasinMusa-ym8lp 16 күн бұрын
Dc ❤❤wi love you
@InnocentEdasi
@InnocentEdasi 15 күн бұрын
The DC 🔥💗🔥
@user-mv1wg2qd6i
@user-mv1wg2qd6i 15 күн бұрын
Machine ❤❤❤DC
@user-zr7wk4oq2x
@user-zr7wk4oq2x 15 күн бұрын
The DC🔥🔥🔥
@ThomasMlowoka
@ThomasMlowoka 15 күн бұрын
DC 💪💪
@siphiwenyirongo2568
@siphiwenyirongo2568 15 күн бұрын
Mmm
@user-rm2xv8ys1i
@user-rm2xv8ys1i 15 күн бұрын
❤❤❤❤
@user-eh1mg3ww6d
@user-eh1mg3ww6d 15 күн бұрын
Koma abambo inuyo mukuyesesa kunja kukacha mulungu apitilize kukusungani ndi moyo koma ndimati ndi pephe inuyo simungambise chipani chani ndi achina m,tanyiwa bakili TV tikuvitelanitu chifukwa mumaoneka ndinu amaso m,phenya
@mathewsnachuma8086
@mathewsnachuma8086 16 күн бұрын
Boooooooooooorn kalindoooooooooooooo
@osaukaonjoya
@osaukaonjoya 15 күн бұрын
Tokotani akolo
@user-sr4fe5bb2w
@user-sr4fe5bb2w 15 күн бұрын
Pita iweyo ku khothi ko Mesa umati ndiwe president
@inessmsiyambiri8517
@inessmsiyambiri8517 15 күн бұрын
Kape ukuti chani
@AlasonPaulo-ht7zb
@AlasonPaulo-ht7zb 16 күн бұрын
Azibambooooo
@RachealHarawa-xc9gs
@RachealHarawa-xc9gs 15 күн бұрын
Mulindimfundo zabwino
@CHIFUNDOCHINA-lp9lg
@CHIFUNDOCHINA-lp9lg 15 күн бұрын
KING
@user-ej6tw9do2r
@user-ej6tw9do2r 15 күн бұрын
Akufuna udindo uyu aaaaaa Popeza adamumana udindo. ndiye akuona kut aDPP azamupatsa?
@JamesEuginio
@JamesEuginio 15 күн бұрын
@@user-ej6tw9do2r ndiye ukuganiza kuti what way followard if akalindo akufuna udindo iwe iwe tanena chabwino mchiti?
@hanifahmponda8711
@hanifahmponda8711 15 күн бұрын
Ife UTM tsitiwelengela kuti chipani chotsusa ayi ichi ndi chipani cholamula boma ndi MCP itsewo alephelela lidzodzi kuyendetsa dziko NSONO A MCP KAYA APATSA NDALAMA KAYA TSAPATSA NDALAMA IDZO ZAWO AKUDZIWANI koma munthu wadzelu nsangasalale ndi munthu amene wapha bambo ako ndikumakuwudza kuti ndikutsamalilani bwino ana inu pomwe bombo wawoyo mumalephela kumutsamalila loko anawo bambo wawo ali moyo msimawathandidza UTM mistake yanu ndiyimene umalidze chipani chanu ndanena kuti kumalidza off course ifa ya CHILIMA yachepetsa mphamvu zanu mwina nsimukudziwa NDE MCP AMALAWI YAKWANO NDE OTSUNSA BOMA CHIHANA MUTHALIKA MAYI PATELO ATUPELE KALWUWA NDI ENA OTSE MUTSAKHELE CHETEEEEE KHALANI PAMODZI NDIKUPANGA CHIGANIDZO KUTI UKAMBELE MBELE AKUPANGANI A MCP NDI ARP muchita bwanji chifukwa kungopatsa pata kawili MCP kukhalatso boma amalawi OCHULUKA TiKUFA KOMATSO ULAMULILO UWU WACHIPANI CHIMODZI UDZAKHADZIKIKANO NDE MAMVUTO AKULU KU MALAWI
@DenisJamu
@DenisJamu 15 күн бұрын
Fadah
@SamsonWyson
@SamsonWyson 15 күн бұрын
Dccccc
@DavieMuziwo
@DavieMuziwo 15 күн бұрын
Best DC
@EmieMtendere
@EmieMtendere 15 күн бұрын
The DC
@ISSAHKAINGA-zz1op
@ISSAHKAINGA-zz1op 15 күн бұрын
ACHALUME KUTI CHUBWIIII
@FrancisGama-qb7ze
@FrancisGama-qb7ze 15 күн бұрын
The DC
@SemuKaunda
@SemuKaunda 16 күн бұрын
The DC
BON KALINDO 24 JULY 2024 KUSWANYA BASI PA WEDNESDAY
13:14
Malawi Trends TV
Рет қаралды 840
Mom's Unique Approach to Teaching Kids Hygiene #shorts
00:16
Fabiosa Stories
Рет қаралды 21 МЛН
Эффект Карбонаро и нестандартная коробка
01:00
История одного вокалиста
Рет қаралды 9 МЛН
Clown takes blame for missing candy 🍬🤣 #shorts
00:49
Yoeslan
Рет қаралды 38 МЛН
INTERVIEW YA BON KALINDO PA ZODIAK IYI NDIPO CHIKUKHADZULA
59:48
Malawi Trends TV
Рет қаралды 8 М.
ARRIVAL OF LUCIUS BANDA'S REMAINS😢
1:22:27
VILLAGE CHAMPION
Рет қаралды 94 М.
BON KALINDO AMAFUNA KUPHEDWA KU PARLIAMENT
38:53
TIDZIWE TV
Рет қаралды 66 М.