M C P -- Malawi Congress Party M C P = Malawi Chikangawa Party 👹👹👹🔨⚒️⛏️
@AndrewMagombo4 сағат бұрын
Mesa ife tudalira inu n TV bakili❤❤❤
@user-xi2vo4gc4u4 сағат бұрын
Ku Malawi aku shooter ma movie rekani amenyane
@Bonisiwentamo4 сағат бұрын
❤Zowona acc muthu ameneyu AChoke
@ShentrycChinoko4 сағат бұрын
Chikamabodza chabwela zotani kukamwa ngati manyi
@FrancisDay-br7xb43 минут бұрын
Pain MCP
@FrankMulela-qt1wi4 сағат бұрын
Number yotumizila zinthu kwantanyiwa plz
@NisharChibisa5 сағат бұрын
Mumakwana
@ShentrycChinoko5 сағат бұрын
Muyiyambe muwone utsi ntanyawa Ali kunja athawa ataba mbuzi kumalawi
@GraceZumazuma5 сағат бұрын
Koma Malawi walowa chibwana chakwera anapita ku sukulu koma?pano akusekedwa ndi anthu akunja omwe
@ShentrycChinoko5 сағат бұрын
Atanyiwa pathako pako
@ShentrycChinoko4 сағат бұрын
Yess
@ShentrycChinoko4 сағат бұрын
Zowonadi mchutsuludi chimenechi
@user-qv3bc4rv7q5 сағат бұрын
Afuna abe ndalamazo
@RobertLuka-wy9cl5 сағат бұрын
Alandila mabazi nawonso ndi achinyengo
@hanifahmponda87115 сағат бұрын
Aaaa galu wa MCP ngati munthu oyipa dzedi modzi wake ndiameneyi APA DZOTI BOMA LABWELETSA FUTI ZA TUNDU WA PISTONS 400 KUCHOKELA KU ISRAEL SAKUNENA KOMATU MUTSAPHE MUNTHU MALAWI MUYIMVA KUWAWA CHIFUKWA ISRAEL YAMAGADZI NDE MUKUYIKOKELA NDALA KU MALAWI MWAPHA CHILIMA PANOTSO KUMAPHELABE ANTHU ENA KOMA MCP MWATAYILATU KOMA MULUNGU SI MUNTHU
Ntanyiwa iweyo ndi number one radio yako timainyadira kom athu athawa ziko lili rawo kom kumeneko moto kuti buuuuu mumtimamo angokhuta mphuma lokhalokha km mulimba Ntanyiwa woyeee
@user-ht7vs3dp2u5 сағат бұрын
Kom Boma ili mmmmm chazelu balibes chomwe ndikuona ine mulungu atimenyere khondo
@SueWahna5 сағат бұрын
Anakodza bwanji date asanawunikile
@CadTafa26 сағат бұрын
Apolici a malawi a kuzishipisa
@MoffatChiwaya-i5k6 сағат бұрын
Good job continue informing the nation,we are proud of you
@user-ks3uw8gj8h6 сағат бұрын
Akatero Mulungu wanthu wayamba kuvumbulutsa poyera, koma wina ayaluka sumungamawononge ma tax anthu ndi za Zii, tingopita ku nkhalango ya ku state house komweko
@FatimanickisJaffer6 сағат бұрын
Am waiting good news not bad news 😔😔😔😔😔
@ShaolinThomas-ow8yn6 сағат бұрын
Inuyo mulungu adzingokuonjexelani moyo wautali basi ,chifukwa mukutimvetsa kukoma