Aaaaaaaaa koma kalindo ndi munthu wankulu kwambili ndipo amayankhula saopa kanthu
@user-lz5yv4vj6h16 күн бұрын
Kkkkk koma Born aaaa ndi president wanthudi ,l salute you sir
@josephinemisomali684016 күн бұрын
Ndimadikira Dc kuti lero atichani apa nditha kukagona 😂😂😂 Boni kalindooooooooo!!!
@NelsonbastonMandela15 күн бұрын
Kkkkl mpaka police 200 koma bon kalindo ndimunthu okwiya kwambiri 😂😂😂😂😂
@robertchitsulo800616 күн бұрын
Bon kkkkkkkkk akuti aputa milandu yambiri iwe ndi 1 basi kkkkkk
@SamfrayGvng14 күн бұрын
Eeeee ai ndagonja nanu big up a 🙋DC
@user-mk7fh5ml8s15 күн бұрын
Mr kalindo ife tidalira inu basi❤❤❤
@user-jk8sh7fh2d16 күн бұрын
Wakumuzi kwenikwenni za pa social media -zi saziziwa kuti inu muma -aimilira
@user-uc1pd1tc2x15 күн бұрын
😂😂😂😂😂😂😂😂😂Nyau kumva pain 😂😂😂
@AufiThera15 күн бұрын
Kod Aku Germany aja bas angotithera ndalama mosemuja lipot osabwerensa aaaa ndiye angopita kwawo wapas amenewo iyaaa
@TougiedaAjam15 күн бұрын
It's the Dc keep it
@PeterKathewera15 күн бұрын
Kodi kwanu sanakuvoteren bwanji😢😢
@AlickMakunganya-o4w15 күн бұрын
Ichichi sichamasewera Adaaa😂😂
@PetroMatias16 күн бұрын
🤝🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🤝🤝🤝🤝
@user-hh4wn4vf9e15 күн бұрын
DC 🥰
@EvsonNgurube15 күн бұрын
Bon kalindooooooo
@Homeofpeace32115 күн бұрын
Za Imfa Ya Chilima Tisaopsezane, Ngati Simunamuphe Tiuzeni Kuti Chinachitika Ndichani? Ku MCP musabise zinthu zoti munapanga nokha, Chakwela Ukhale ndimanyazi Ubusa wake Uti Unkapanga iwe Okupha Nzako Chifukwa Chautsogoleli?
@AufiThera15 күн бұрын
Wanthu wanthu DC 💪
@user-hh4wn4vf9e15 күн бұрын
DC ❤
@MariamJaffali15 күн бұрын
Ndodo ija ituluke DC tatopa ndi chakwera ife kkkkkkkkkkk the DC ❤❤❤❤
@sir-wanton-200114 күн бұрын
Kkkkk chikumvesa kukoma a Malawi ambili
@user-fz3gu2ez1o14 күн бұрын
Kkkkkkkk Mwana ovuta kulera Hehehehe
@MisheckAselo16 күн бұрын
Amafuna kukuipisirani Mr DC koma akunama 💪
@user-uc1pd1tc2x15 күн бұрын
Bon Kalindo the DC (The most dangerous child)❤❤❤❤❤❤