BON KALINDO KUYANKHULA PAMBUYO PA CHIGAMULO CHAKU COURT 10 July 2024

  Рет қаралды 10,153

HOT 265

HOT 265

18 күн бұрын

Пікірлер: 65
@MuhajirinaSaid
@MuhajirinaSaid 16 күн бұрын
Keep it up mr Dc
@ForsterThawan
@ForsterThawan 16 күн бұрын
Aaaaaaaaa koma kalindo ndi munthu wankulu kwambili ndipo amayankhula saopa kanthu
@user-lz5yv4vj6h
@user-lz5yv4vj6h 16 күн бұрын
Kkkkk koma Born aaaa ndi president wanthudi ,l salute you sir
@josephinemisomali6840
@josephinemisomali6840 16 күн бұрын
Ndimadikira Dc kuti lero atichani apa nditha kukagona 😂😂😂 Boni kalindooooooooo!!!
@NelsonbastonMandela
@NelsonbastonMandela 15 күн бұрын
Kkkkl mpaka police 200 koma bon kalindo ndimunthu okwiya kwambiri 😂😂😂😂😂
@robertchitsulo8006
@robertchitsulo8006 16 күн бұрын
Bon kkkkkkkkk akuti aputa milandu yambiri iwe ndi 1 basi kkkkkk
@SamfrayGvng
@SamfrayGvng 14 күн бұрын
Eeeee ai ndagonja nanu big up a 🙋DC
@user-mk7fh5ml8s
@user-mk7fh5ml8s 15 күн бұрын
Mr kalindo ife tidalira inu basi❤❤❤
@user-jk8sh7fh2d
@user-jk8sh7fh2d 16 күн бұрын
Wakumuzi kwenikwenni za pa social media -zi saziziwa kuti inu muma -aimilira
@user-uc1pd1tc2x
@user-uc1pd1tc2x 15 күн бұрын
😂😂😂😂😂😂😂😂😂Nyau kumva pain 😂😂😂
@AufiThera
@AufiThera 15 күн бұрын
Kod Aku Germany aja bas angotithera ndalama mosemuja lipot osabwerensa aaaa ndiye angopita kwawo wapas amenewo iyaaa
@TougiedaAjam
@TougiedaAjam 15 күн бұрын
It's the Dc keep it
@PeterKathewera
@PeterKathewera 15 күн бұрын
Kodi kwanu sanakuvoteren bwanji😢😢
@AlickMakunganya-o4w
@AlickMakunganya-o4w 15 күн бұрын
Ichichi sichamasewera Adaaa😂😂
@PetroMatias
@PetroMatias 16 күн бұрын
🤝🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🤝🤝🤝🤝
@user-hh4wn4vf9e
@user-hh4wn4vf9e 15 күн бұрын
DC 🥰
@EvsonNgurube
@EvsonNgurube 15 күн бұрын
Bon kalindooooooo
@Homeofpeace321
@Homeofpeace321 15 күн бұрын
Za Imfa Ya Chilima Tisaopsezane, Ngati Simunamuphe Tiuzeni Kuti Chinachitika Ndichani? Ku MCP musabise zinthu zoti munapanga nokha, Chakwela Ukhale ndimanyazi Ubusa wake Uti Unkapanga iwe Okupha Nzako Chifukwa Chautsogoleli?
@AufiThera
@AufiThera 15 күн бұрын
Wanthu wanthu DC 💪
@user-hh4wn4vf9e
@user-hh4wn4vf9e 15 күн бұрын
DC ❤
@MariamJaffali
@MariamJaffali 15 күн бұрын
Ndodo ija ituluke DC tatopa ndi chakwera ife kkkkkkkkkkk the DC ❤❤❤❤
@sir-wanton-2001
@sir-wanton-2001 14 күн бұрын
Kkkkk chikumvesa kukoma a Malawi ambili
@user-fz3gu2ez1o
@user-fz3gu2ez1o 14 күн бұрын
Kkkkkkkk Mwana ovuta kulera Hehehehe
@MisheckAselo
@MisheckAselo 16 күн бұрын
Amafuna kukuipisirani Mr DC koma akunama 💪
@user-uc1pd1tc2x
@user-uc1pd1tc2x 15 күн бұрын
Bon Kalindo the DC (The most dangerous child)❤❤❤❤❤❤
@GracePhirie
@GracePhirie 15 күн бұрын
Mwana woipa kwambiri😂😂😂
@allansili-rc9gc
@allansili-rc9gc 16 күн бұрын
🤣🤣🤣🤣 mpaka a police 200 kkkkk
@williamchatha6139
@williamchatha6139 15 күн бұрын
The DC salute
@ShaibKudzinja
@ShaibKudzinja 16 күн бұрын
The DC, ndipo anthu tizamulilira kwambri mkului nd ntchto yakei akazasamira mkono
@ZexNkhoma-p8t
@ZexNkhoma-p8t 15 күн бұрын
The braval child of Malawi, Speak out without fear and favor! Bon kalindo, The DC...
@user-mi3fw1zg8b
@user-mi3fw1zg8b 15 күн бұрын
😂😂😂😂😂the DC machine
@kondwanimandala4575
@kondwanimandala4575 15 күн бұрын
Winiko the DC pachilungamo sumawopa iweyo umatha
@KhalideNerve-mu1eq
@KhalideNerve-mu1eq 15 күн бұрын
❤❤❤❤❤ more fire 🔥
@lazarousnamakhwa6549
@lazarousnamakhwa6549 15 күн бұрын
boni kalindo malawi 😂😂😂😂
@IbrahimYusufu-z9d
@IbrahimYusufu-z9d 15 күн бұрын
Bon Kalindo
@NorahMangasanja
@NorahMangasanja 16 күн бұрын
Mr Dc mumakwana inuyo tilinanu ife amalawi
@HaruunWalusa
@HaruunWalusa 15 күн бұрын
The DC
@moseskalande9853
@moseskalande9853 15 күн бұрын
zopanda ntchito zomwe ukulu inu mumalankhula
@nafejonga972
@nafejonga972 15 күн бұрын
Chizagwira zipolopolo😅😅 iwe ndi machine, wait to destroy them with you
@EmmanuelNgambi-y6h
@EmmanuelNgambi-y6h 15 күн бұрын
Umakwana DC
@user-zs6qc9dx8s
@user-zs6qc9dx8s 16 күн бұрын
The DC🔥
@user-ql8nf2vb8s
@user-ql8nf2vb8s 15 күн бұрын
It's plezident of poor people
@AustinBornface
@AustinBornface 16 күн бұрын
The DC!
@ArnoldKamanga-r6k
@ArnoldKamanga-r6k 15 күн бұрын
Uyu yekha timuteteza I swear
@PoxisNation-fe1kr
@PoxisNation-fe1kr 15 күн бұрын
The DC 😂😂😂
@OnexAliMwale
@OnexAliMwale 15 күн бұрын
Kulankhula wina aliyese atha kulankhula koma kuchita zakupsa...Bwana Bon kalindo akumalankhula koma ndi action yanji yomwe ikuchitika? We need kulankhula ndikuchita namaona progress..Mukatiuza zomwe mwapezazo kenako muzinenanso kuti tipanga izi pothana ndizimenezi...tisamangokhalira kumva mwana oopsa mmalankhulidwe, action nothing
@myheartforkids2876
@myheartforkids2876 15 күн бұрын
Inu mene mwayankhulamu mwapanga action yanji? Kkkkkkkkkk
@sir-wanton-2001
@sir-wanton-2001 14 күн бұрын
Kkkk mbuli ife timakonda DC
@OnexAliMwale
@OnexAliMwale 14 күн бұрын
@@myheartforkids2876 Amene amawatsata omenyera ufulawa atha kudziwa kuti nthawi ya Bingu kunali Mavuto Bamusi ndipo amati akanena amapanga action ndipo Mpaka Bingu anasintha machitidwe azinthu zina, nthawi ya Peter kunali Timothy Mtambo, za amenewu mukudziwa zomwe amachita, Koma Bwana Bon mmmm tiyeni tizingomva Mwana oopsa komanso kung'alura kenako tiseke osaona chisintha...I always appreciate for actions not talking that's why tonse Government tikudana nalo coz nawoso kulankhula amatha koma kukwanilitsa kukuwavuta
@RedrawLittleMushutula
@RedrawLittleMushutula 15 күн бұрын
DC mewafika
@williamalvis6028
@williamalvis6028 16 күн бұрын
The DC umakwana
@phindiswatshibo7101
@phindiswatshibo7101 16 күн бұрын
Chipangoline😂😂
@chipanganofackison5185
@chipanganofackison5185 15 күн бұрын
Zamanyi basi kape ndiweyo akanadakhala Ofuna kupha akanampha iweyo umatisokoneka mutu amakutuma ndindani? Umango uwanamizila anthu wosawuka ndidziko lanji lomwe kungapezeke wolemera wose?
@musaphiri317
@musaphiri317 15 күн бұрын
Iwe akupasa zingati koma inu ndi onvesachifundo kupusa uchisru
@SamKaposa-i5c
@SamKaposa-i5c 15 күн бұрын
Nyau imeneyi itayeni
@EvsonNgurube
@EvsonNgurube 15 күн бұрын
Matako ako nyau iwe
@sir-wanton-2001
@sir-wanton-2001 14 күн бұрын
Kape uyu
@moseskalande9853
@moseskalande9853 15 күн бұрын
Even ur voice doesn't sound like a leader
@FrankMulola
@FrankMulola 16 күн бұрын
😂😂😂😂😂
@samhussen708
@samhussen708 15 күн бұрын
😂😂
@brightkaunda920
@brightkaunda920 16 күн бұрын
Ati amangidwe ndamako
@user-uc1pd1tc2x
@user-uc1pd1tc2x 15 күн бұрын
😂😂😂😂😂Amangidwadi ndi amake a Chakwera 😂😂
@chifukanyo9447
@chifukanyo9447 15 күн бұрын
😂😂😂
@sir-wanton-2001
@sir-wanton-2001 14 күн бұрын
Kkkk
Lwasa afunye sente bupya,aguze benz ne rangerover
30:52
Kasuku Live
Рет қаралды 32 М.
BON   KALINDO LERO PA  26 JULY 2024 |
16:05
DZIWE TV
Рет қаралды 2,7 М.
I Can't Believe We Did This...
00:38
Stokes Twins
Рет қаралды 133 МЛН
Sigma Kid Hair #funny #sigma #comedy
00:33
CRAZY GREAPA
Рет қаралды 33 МЛН
Mom's Unique Approach to Teaching Kids Hygiene #shorts
00:16
Fabiosa Stories
Рет қаралды 28 МЛН
Самый Молодой Актёр Без Оскара 😂
00:13
Глеб Рандалайнен
Рет қаралды 10 МЛН
Reign Bamutadde, Kkooti Emutaddeko Obukwakkulizo
3:55
BBS Terefayina 2
Рет қаралды 196
LERO BON KALINDO WANG'ALULA NKULU WA ASILIKALI 26 July 2024
15:05
ZOMWE ZIDALI KU BALAKA 🙌🙌🙌🙌25 July 2024
27:52
HOT 265
Рет қаралды 10 М.
Times Exclusive featuring Bon Kalindo - 6 January 2024
1:03:20
Times 360 Malawi
Рет қаралды 240 М.
ZISAKHO ZAKU MANGOCHI ZODABWITSA ANTHU🙌🙌
28:38
HOT 265
Рет қаралды 20 М.
A Malawi Lyton Mangochi Musamukhulupilileso - Bon Kalindo
19:43
Nyasa VoiceBox
Рет қаралды 20 М.
Maloto A Bon Kalindo (Part 2) - Bon Kalindo
14:17
Nyasa VoiceBox
Рет қаралды 107 М.
I Can't Believe We Did This...
00:38
Stokes Twins
Рет қаралды 133 МЛН