Bon Kalindo,Kamlepu Kaluwa,Comrade Ntanyiwa,Wanda Msiska and his friend,Brian Banda and others you are really philanthropic and patriotic. May God bless you abundantly.Religious,political, traditional and social leaders here in Malawi are all ordained to the mentality of cupidity hence very unable to transform Malawi philanthropically and patriotically.
The DC mwana wayankhulira m Malawi mommuno osati mpakana kukabisala ku Zambia ayi chi Bon Kalindo chinatha mantha ndipo sichiopa Unyolo anta more 🔥🔥 Mr president waife anthu osauka😅😅😅😅
@AfricanKingdom-uv1qb19 күн бұрын
God protect mr DC
@priscillamangata402319 күн бұрын
🤣🤣🤣🤣🤣 ngati Malawi ndiwandani Mr DC
@user-gm3cx2xn9o19 күн бұрын
Ife si osauka ndipo sitisilira kukhala ndi president osauka😂😂😂😂😂
@JibuzahDrag20 күн бұрын
Fire Mr president mumayakhula zilungamo zokha zokha
@ChristinaSinoyakapawo20 күн бұрын
Ndabwereza kawili nyimbo yoooo anaphaa mubale wake gwenembe chifwukwa cha udido
@ThompsonMakwakwa20 күн бұрын
Aaaaaaaaaaaaaa@ koma nde zafikapotu mpaka muchenga machende awo ndithu
@ShafieIdrissah19 күн бұрын
Bon kalindo dddccccc❤
@ishmaelcassim80620 күн бұрын
Mr bon kalindo you are number one. More fire Mr dc❤
@hajrazuwaja499320 күн бұрын
😂😂😂amangidwaso uyu ndithu sikusinja ndi gwenembe koma Mr the DC kkkkkkkk
@ChrissySalimu20 күн бұрын
Sikusinja imweyo kkkkkk taimbaso Mr DC aifeeee❤❤❤
@julietmussa510320 күн бұрын
Sikusinja ndi Gwenembe yemweyo....ana amphunzile
@AbdulsEdsan20 күн бұрын
Mr Kalindo great soldier
@JohnmarkNazombe-hi9xd20 күн бұрын
Mwana wowopya kwambiri!!!!!!!!!❤❤❤❤❤❤
@ChifundoNinje20 күн бұрын
We love you the DC
@AubreyBamus16 күн бұрын
My vote bn
@JosephPindani20 күн бұрын
Km chakwela watopa m'chenga mpaka nd wa boma kkkkkk😅😅😅😅😅
@Moses5120 күн бұрын
The Dc bon kalindo 🎉🎉🎉🎉
@user-cg5ml7ym4v20 күн бұрын
Tili pa mbuyo panu DC ❤❤
@JuuuKomba20 күн бұрын
😂😂😂😂😂 malawi ndife makape timaopa muthu ot tamuvotela tokha
@user-qc5lh3xw2h20 күн бұрын
Powerful Mr president ❤
@user-ln5hw7dn9g20 күн бұрын
Ndakhalira kuseka😂😂😂😂😂😂 iweyo ndi wani
@user-fd7wj3mg2i19 күн бұрын
Mulungu azikutetezera nkhondo mukuimenya
@Samu-q3z20 күн бұрын
❤❤❤❤smdc
@user-lr2wx5xd9d19 күн бұрын
The DC!!!!!!!!!!!!!!!
@richardkumbambe-tg9qi20 күн бұрын
Great indeed. Let's all rise ip.
@JuvenileDebwe-bv8ow20 күн бұрын
kkkk koma chimwana chakwa njedza kkk
@WITTNESSMBOBADINHONJOLOM-bv4un19 күн бұрын
Bon kalindo tili limodzi
@Lazarus-qo1sl20 күн бұрын
Kkkkkk wapolice samwa ambuye nditengeni
@chrisneySwanepoel-yu5vd20 күн бұрын
God protect mr kalindo
@shamimmahomed670920 күн бұрын
Bon kalindo yemweyo kuti wawawa!!!
@bamusmajawa161920 күн бұрын
Mr Bon Kalindo on fire 🔥🔥💪
@thandothando655619 күн бұрын
Super super😂😂
@user-hh4wn4vf9e20 күн бұрын
😂😂😂 koma ndaseka DC ayi taa sikusinja Kodi
@user-mi3fw1zg8b20 күн бұрын
😂😂😂😂 Mr DC
@user-mx5cx3gl4h20 күн бұрын
Osafowoka bon kalindo
@fatsanibanda521320 күн бұрын
Yes iweeee ing'alure basi😂😂
@PeterMoosa20 күн бұрын
More fire mr winiko
@AlexNkhata-c8n19 күн бұрын
Zoona akunena B kalindo
@user-dk6yc8pl2m20 күн бұрын
The Dc ❤❤❤❤
@user-fi7ko7bl6f20 күн бұрын
Make mbuuu mwana mbuuuu 😅😅😅
@user-fi7ko7bl6f20 күн бұрын
Tang'alulani the DC kuti atongwe-tongwe a MCP amve bwino lomwe. This Boniiii Kalindo the DC, mlowa mmalo mwa Solobala amene ananyongedwa pa makako nda agalu MCP ya Kamuzu ndi John Tembo
@RabsonSabit-nc5ds20 күн бұрын
Uyu ndi nyoooo
@user-tm6wl5tt3u18 күн бұрын
Umakwana iweyo
@ChikumbutsoJohn-rs4tt20 күн бұрын
Bwana apolice atraffic akuonjeza bwerani mnseu wa Bunda every 200m atraffic ndie a area 3 amabwera 3koloko am kuyimba pa mnseu mmmmmmm Malawi
@PachaloShaba-pf5vw20 күн бұрын
Good boy
@user-vq6zr4tn8v19 күн бұрын
Muma tiimila osatopa
@user-ng4ic8jo8b20 күн бұрын
Koma iwe ndigalu kwambili
@user-sp4kn8rh2j19 күн бұрын
Hahaha kwachema 🔥
@Chipilirodaniel198919 күн бұрын
❤
@AdiniKhama20 күн бұрын
Mr DC osafowoka
@JohnZyambo-q8h20 күн бұрын
❤❤
@JohnZyambo-q8h20 күн бұрын
🎉
@TiyanjaneMkwate-we8gu20 күн бұрын
Kkkkkkkkk koma a Kalindo agogo anu ankakuuzani nthano ya sikusinja mukupita ku nzuzu , ndiye mwati ankakuwerengeranu mu chikangawa? Komanso mwati anaphana chifukwa cha udindo? Ndipaseni page ndiwerenge nawo basi . U are number 1
@WisdomMaseko-fi5sv20 күн бұрын
Avu
@WisdomMaseko-fi5sv20 күн бұрын
Lyton Mangochi bwerani yamanja ija kuno
@EmmanuelGasiten-fo5dr19 күн бұрын
Ipondeni Fadah
@IssahAluba20 күн бұрын
aaaaa zayambika liti tchega omwewu gati mwatopa nawo phandowo apatseni ena MCP is very nonsense iyaaa
@griviniakanjaula445620 күн бұрын
More fire mbuyanga alomwe alomwe nophiya
@JasperKaleni-dx6nn19 күн бұрын
😂😂the dc
@JeanBanda-zy6wu20 күн бұрын
Koma ndiye mwafikapo mpaka kulesa anthu kuti asamavuule mchenga really? Nyumba zanuzo munamangila mchenga munakawoda ku America? Silly people
@frankdonovanntambira20 күн бұрын
Ndipo Boma Lamanyi ngati ili ine sindinalionepo Aaash!!
@SaidiMbawa-st6bj20 күн бұрын
A opposition zochita zamwo ndi zimodzimodzi
@stevejizaremu339620 күн бұрын
The DC
@RichmanNkhoma20 күн бұрын
Mbambande me. Kalindo
@van-wykchilapondwa698120 күн бұрын
Great 👍
@irenioeugeniosumila664720 күн бұрын
Ulemu wano A Kalendo
@user-pv9uk6sc3w20 күн бұрын
Kulephera kuja ndi kumeneku, anthu ndi okwiya kale , atopa ndi boma ili
@MemoryKamanga-jv4jh20 күн бұрын
You are welcome Mr dc
@SarahMusama-eu7wt20 күн бұрын
Atsala atigulitsa mphweyaa kwatsala
@FrankiePangan20 күн бұрын
😢😢😢😢
@oskidooscar746820 күн бұрын
Koma why sakuyamkhulapo za manganya ku mcp palibe audio olo imoz inakambapo za Mr usi
@SilenceChepiano20 күн бұрын
DC ndimava kukoma mukatiyimilira
@TapiwaKhwisula20 күн бұрын
Mo faya mr dc
@Martha-m6e20 күн бұрын
Mitu singwiradi.anthu onse anafa aja mwanzi wawo sukhara chete.
IWEYO ndi opusa kwambiri ndi chakwera wakoyo ngati akutuma cadet mbuzi, ngati iwe ukidya ndi mcp usawanyase AMALAWI AKUVUTIKA , ndiye uzikayankhula mbwerera zako zankutuzo , ngati sizikusangalatsa amakutuma kuti uzimvera ndi ndani ulibe manyazi ? Cadet supit
@isaacchiwaula73120 күн бұрын
@@HalisonSolomon ukufuna ndikuyankhe? Born kalindo umamudziwa? Zomwe akumayankhula amayankhulira iweyo, it's wat u think? Ok kavotere amene ukumufunayo n uzandiuze kut zinthu tsopano zilibwino pamoyo wako. Kalindo sankatukwana DPP ndi Peter munthalika? Lero mwaiwala
@StanleyChirwa-d6b20 күн бұрын
@@isaacchiwaula731 inu musokosa mungosiya kuverako bas sizokakamiza izi boss
@HalisonSolomon20 күн бұрын
@@isaacchiwaula731 iwe sungamakhale KUMBUYO kwa mcp ngati sukuona momwe dziko lavundira ndiye kuduka mutu kumeneko , usiyamitse mene chakwera amatenga boma linali motani ndiye pano zilimotani ? Ndiye timusiye chakera alamuleso lidzakhala dziko? Anthu adzakhala ngati ndani, tiyeni tiganizire ana omwe taberekawa tisakhale ngati a police ndi asilikali amene asankha kigwira ntchito ndi chipano malo moteteza malamulo adziko,
@BudaEarth18 күн бұрын
U na problematic
@chadreckchibwithala149320 күн бұрын
DC PANTCHITO IFE WOZIWA ZINTHU WE KNOW KUTI ABONI KALINDO ALIPO PA NTCHITO YOSUTSA CHILICHOTSE NDE MUWONE ALOMWE AVEKERE EEE OOOO UUUU KUKUWA AGALU ACHILOMWE MKUNYA MCP IS GOING NO WAY 2030 WOOOOO CHAKWERA.
@JeanKambala-gm1zr20 күн бұрын
Zosantheka Brazil ndipo idzankhala yazikwanje zomwe² mwaphela saulosinever again MCP achimwene