BON KALINDO LERO PA 11 JULY 2024 |

  Рет қаралды 19,284

DZIWE TV

DZIWE TV

22 күн бұрын

Пікірлер: 117
@augustinechibbalazi8897
@augustinechibbalazi8897 20 күн бұрын
Bon Kalindo,Kamlepu Kaluwa,Comrade Ntanyiwa,Wanda Msiska and his friend,Brian Banda and others you are really philanthropic and patriotic. May God bless you abundantly.Religious,political, traditional and social leaders here in Malawi are all ordained to the mentality of cupidity hence very unable to transform Malawi philanthropically and patriotically.
@BlessingsMbawa
@BlessingsMbawa 19 күн бұрын
Bon kalindo iweyo umatha kulankhula bwino. Chifukwa kulankhula kwako umanena zoona zokhazokha kumvera chisoni amalawi munyengo zowawa zomwe tikudusamo kamba ka utsogoleri olephera wa chakwera. Osafooka , osatopa mpakana satana ameneyi tithana naye 2025 ino. Keep it up wakulu ndimakunyadirani kwambiri
@user-fi7ko7bl6f
@user-fi7ko7bl6f 20 күн бұрын
The DC mwana wayankhulira m Malawi mommuno osati mpakana kukabisala ku Zambia ayi chi Bon Kalindo chinatha mantha ndipo sichiopa Unyolo anta more 🔥🔥 Mr president waife anthu osauka😅😅😅😅
@AfricanKingdom-uv1qb
@AfricanKingdom-uv1qb 19 күн бұрын
God protect mr DC
@priscillamangata4023
@priscillamangata4023 19 күн бұрын
🤣🤣🤣🤣🤣 ngati Malawi ndiwandani Mr DC
@user-gm3cx2xn9o
@user-gm3cx2xn9o 19 күн бұрын
Ife si osauka ndipo sitisilira kukhala ndi president osauka😂😂😂😂😂
@JibuzahDrag
@JibuzahDrag 20 күн бұрын
Fire Mr president mumayakhula zilungamo zokha zokha
@ChristinaSinoyakapawo
@ChristinaSinoyakapawo 20 күн бұрын
Ndabwereza kawili nyimbo yoooo anaphaa mubale wake gwenembe chifwukwa cha udido
@ThompsonMakwakwa
@ThompsonMakwakwa 20 күн бұрын
Aaaaaaaaaaaaaa@ koma nde zafikapotu mpaka muchenga machende awo ndithu
@ShafieIdrissah
@ShafieIdrissah 19 күн бұрын
Bon kalindo dddccccc❤
@ishmaelcassim806
@ishmaelcassim806 20 күн бұрын
Mr bon kalindo you are number one. More fire Mr dc❤
@hajrazuwaja4993
@hajrazuwaja4993 20 күн бұрын
😂😂😂amangidwaso uyu ndithu sikusinja ndi gwenembe koma Mr the DC kkkkkkkk
@ChrissySalimu
@ChrissySalimu 20 күн бұрын
Sikusinja imweyo kkkkkk taimbaso Mr DC aifeeee❤❤❤
@julietmussa5103
@julietmussa5103 20 күн бұрын
Sikusinja ndi Gwenembe yemweyo....ana amphunzile
@AbdulsEdsan
@AbdulsEdsan 20 күн бұрын
Mr Kalindo great soldier
@JohnmarkNazombe-hi9xd
@JohnmarkNazombe-hi9xd 20 күн бұрын
Mwana wowopya kwambiri!!!!!!!!!❤❤❤❤❤❤
@ChifundoNinje
@ChifundoNinje 20 күн бұрын
We love you the DC
@AubreyBamus
@AubreyBamus 16 күн бұрын
My vote bn
@JosephPindani
@JosephPindani 20 күн бұрын
Km chakwela watopa m'chenga mpaka nd wa boma kkkkkk😅😅😅😅😅
@Moses51
@Moses51 20 күн бұрын
The Dc bon kalindo 🎉🎉🎉🎉
@user-cg5ml7ym4v
@user-cg5ml7ym4v 20 күн бұрын
Tili pa mbuyo panu DC ❤❤
@JuuuKomba
@JuuuKomba 20 күн бұрын
😂😂😂😂😂 malawi ndife makape timaopa muthu ot tamuvotela tokha
@user-qc5lh3xw2h
@user-qc5lh3xw2h 20 күн бұрын
Powerful Mr president ❤
@user-ln5hw7dn9g
@user-ln5hw7dn9g 20 күн бұрын
Ndakhalira kuseka😂😂😂😂😂😂 iweyo ndi wani
@user-fd7wj3mg2i
@user-fd7wj3mg2i 19 күн бұрын
Mulungu azikutetezera nkhondo mukuimenya
@Samu-q3z
@Samu-q3z 20 күн бұрын
❤❤❤❤smdc
@user-lr2wx5xd9d
@user-lr2wx5xd9d 19 күн бұрын
The DC!!!!!!!!!!!!!!!
@richardkumbambe-tg9qi
@richardkumbambe-tg9qi 20 күн бұрын
Great indeed. Let's all rise ip.
@JuvenileDebwe-bv8ow
@JuvenileDebwe-bv8ow 20 күн бұрын
kkkk koma chimwana chakwa njedza kkk
@WITTNESSMBOBADINHONJOLOM-bv4un
@WITTNESSMBOBADINHONJOLOM-bv4un 19 күн бұрын
Bon kalindo tili limodzi
@Lazarus-qo1sl
@Lazarus-qo1sl 20 күн бұрын
Kkkkkk wapolice samwa ambuye nditengeni
@chrisneySwanepoel-yu5vd
@chrisneySwanepoel-yu5vd 20 күн бұрын
God protect mr kalindo
@shamimmahomed6709
@shamimmahomed6709 20 күн бұрын
Bon kalindo yemweyo kuti wawawa!!!
@bamusmajawa1619
@bamusmajawa1619 20 күн бұрын
Mr Bon Kalindo on fire 🔥🔥💪
@thandothando6556
@thandothando6556 19 күн бұрын
Super super😂😂
@user-hh4wn4vf9e
@user-hh4wn4vf9e 20 күн бұрын
😂😂😂 koma ndaseka DC ayi taa sikusinja Kodi
@user-mi3fw1zg8b
@user-mi3fw1zg8b 20 күн бұрын
😂😂😂😂 Mr DC
@user-mx5cx3gl4h
@user-mx5cx3gl4h 20 күн бұрын
Osafowoka bon kalindo
@fatsanibanda5213
@fatsanibanda5213 20 күн бұрын
Yes iweeee ing'alure basi😂😂
@PeterMoosa
@PeterMoosa 20 күн бұрын
More fire mr winiko
@AlexNkhata-c8n
@AlexNkhata-c8n 19 күн бұрын
Zoona akunena B kalindo
@user-dk6yc8pl2m
@user-dk6yc8pl2m 20 күн бұрын
The Dc ❤❤❤❤
@user-fi7ko7bl6f
@user-fi7ko7bl6f 20 күн бұрын
Make mbuuu mwana mbuuuu 😅😅😅
@user-fi7ko7bl6f
@user-fi7ko7bl6f 20 күн бұрын
Tang'alulani the DC kuti atongwe-tongwe a MCP amve bwino lomwe. This Boniiii Kalindo the DC, mlowa mmalo mwa Solobala amene ananyongedwa pa makako nda agalu MCP ya Kamuzu ndi John Tembo
@RabsonSabit-nc5ds
@RabsonSabit-nc5ds 20 күн бұрын
Uyu ndi nyoooo
@user-tm6wl5tt3u
@user-tm6wl5tt3u 18 күн бұрын
Umakwana iweyo
@ChikumbutsoJohn-rs4tt
@ChikumbutsoJohn-rs4tt 20 күн бұрын
Bwana apolice atraffic akuonjeza bwerani mnseu wa Bunda every 200m atraffic ndie a area 3 amabwera 3koloko am kuyimba pa mnseu mmmmmmm Malawi
@PachaloShaba-pf5vw
@PachaloShaba-pf5vw 20 күн бұрын
Good boy
@user-vq6zr4tn8v
@user-vq6zr4tn8v 19 күн бұрын
Muma tiimila osatopa
@user-ng4ic8jo8b
@user-ng4ic8jo8b 20 күн бұрын
Koma iwe ndigalu kwambili
@user-sp4kn8rh2j
@user-sp4kn8rh2j 19 күн бұрын
Hahaha kwachema 🔥
@Chipilirodaniel1989
@Chipilirodaniel1989 19 күн бұрын
@AdiniKhama
@AdiniKhama 20 күн бұрын
Mr DC osafowoka
@JohnZyambo-q8h
@JohnZyambo-q8h 20 күн бұрын
❤❤
@JohnZyambo-q8h
@JohnZyambo-q8h 20 күн бұрын
🎉
@TiyanjaneMkwate-we8gu
@TiyanjaneMkwate-we8gu 20 күн бұрын
Kkkkkkkkk koma a Kalindo agogo anu ankakuuzani nthano ya sikusinja mukupita ku nzuzu , ndiye mwati ankakuwerengeranu mu chikangawa? Komanso mwati anaphana chifukwa cha udindo? Ndipaseni page ndiwerenge nawo basi . U are number 1
@WisdomMaseko-fi5sv
@WisdomMaseko-fi5sv 20 күн бұрын
Avu
@WisdomMaseko-fi5sv
@WisdomMaseko-fi5sv 20 күн бұрын
Lyton Mangochi bwerani yamanja ija kuno
@EmmanuelGasiten-fo5dr
@EmmanuelGasiten-fo5dr 19 күн бұрын
Ipondeni Fadah
@IssahAluba
@IssahAluba 20 күн бұрын
aaaaa zayambika liti tchega omwewu gati mwatopa nawo phandowo apatseni ena MCP is very nonsense iyaaa
@griviniakanjaula4456
@griviniakanjaula4456 20 күн бұрын
More fire mbuyanga alomwe alomwe nophiya
@JasperKaleni-dx6nn
@JasperKaleni-dx6nn 19 күн бұрын
😂😂the dc
@JeanBanda-zy6wu
@JeanBanda-zy6wu 20 күн бұрын
Koma ndiye mwafikapo mpaka kulesa anthu kuti asamavuule mchenga really? Nyumba zanuzo munamangila mchenga munakawoda ku America? Silly people
@frankdonovanntambira
@frankdonovanntambira 20 күн бұрын
Ndipo Boma Lamanyi ngati ili ine sindinalionepo Aaash!!
@SaidiMbawa-st6bj
@SaidiMbawa-st6bj 20 күн бұрын
A opposition zochita zamwo ndi zimodzimodzi
@stevejizaremu3396
@stevejizaremu3396 20 күн бұрын
The DC
@RichmanNkhoma
@RichmanNkhoma 20 күн бұрын
Mbambande me. Kalindo
@van-wykchilapondwa6981
@van-wykchilapondwa6981 20 күн бұрын
Great 👍
@irenioeugeniosumila6647
@irenioeugeniosumila6647 20 күн бұрын
Ulemu wano A Kalendo
@user-pv9uk6sc3w
@user-pv9uk6sc3w 20 күн бұрын
Kulephera kuja ndi kumeneku, anthu ndi okwiya kale , atopa ndi boma ili
@MemoryKamanga-jv4jh
@MemoryKamanga-jv4jh 20 күн бұрын
You are welcome Mr dc
@SarahMusama-eu7wt
@SarahMusama-eu7wt 20 күн бұрын
Atsala atigulitsa mphweyaa kwatsala
@FrankiePangan
@FrankiePangan 20 күн бұрын
😢😢😢😢
@oskidooscar7468
@oskidooscar7468 20 күн бұрын
Koma why sakuyamkhulapo za manganya ku mcp palibe audio olo imoz inakambapo za Mr usi
@SilenceChepiano
@SilenceChepiano 20 күн бұрын
DC ndimava kukoma mukatiyimilira
@TapiwaKhwisula
@TapiwaKhwisula 20 күн бұрын
Mo faya mr dc
@Martha-m6e
@Martha-m6e 20 күн бұрын
Mitu singwiradi.anthu onse anafa aja mwanzi wawo sukhara chete.
@JeanKambala-gm1zr
@JeanKambala-gm1zr 20 күн бұрын
Mwazi unja wakuchingawa ukuwayenda Mitu anthu amenewa mchenga wobwela ndibvula 😅😅😅😅
@JamilahChitulu
@JamilahChitulu 20 күн бұрын
😂😂❤
@StanleyChirwa-d6b
@StanleyChirwa-d6b 20 күн бұрын
Koma Chaka chamawa tikhapana ndithu
@charitykalua8507
@charitykalua8507 19 күн бұрын
The DC😂
@Aisha-db6ds
@Aisha-db6ds 20 күн бұрын
Eeeee koma ationjezadi apa ndiye yalakwa,, Tipindilana ndenvu mkamwa ulendo wake ndi umeneu
@GanieAlidih-gu7no
@GanieAlidih-gu7no 20 күн бұрын
Anapha zake chifukwa chaudindo
@phillgatoma4857
@phillgatoma4857 20 күн бұрын
😢😢😢😢😢😢
@KennethMchenga-j9c
@KennethMchenga-j9c 20 күн бұрын
Pliz a DPP tadzukani kodi mukunafuna amalawi atani
@dalitson3558
@dalitson3558 20 күн бұрын
Ndipo zomwe akupanga a Dpp akumabowa kwambiri anthu akuzunzika ndi boma Koma aliphee ngati akumetedwa
@IbrahimYusufu-z9d
@IbrahimYusufu-z9d 20 күн бұрын
Akufuna tidziwe kut tidapanga mistake.. ankatiuzatu paja
@dalitson3558
@dalitson3558 20 күн бұрын
@@IbrahimYusufu-z9d ndiye bola akazaluzanso asazalile chifukwa agalu a MCP akuwatakatu osusawa
@FrancisChimwaza-t7d
@FrancisChimwaza-t7d 20 күн бұрын
Iswani ndithu man wamkulu ndi mulungu basi
@scoltenroma6240
@scoltenroma6240 20 күн бұрын
Kuswa kuswa😂😂 akavote ndiamawo Oh yes 🔥🔥
@user-dp7bc7yy6s
@user-dp7bc7yy6s 20 күн бұрын
Km inuyo mumakwana kkkkkkkk the Dc
@lawrenceblacktealyson8015
@lawrenceblacktealyson8015 20 күн бұрын
I don't want to be Malawian anymore
@MecyMalothi
@MecyMalothi 20 күн бұрын
The D C!!!!
@SolomonNjolomole
@SolomonNjolomole 20 күн бұрын
Kodi achakwerawa mchiyani makamaka zikuyenda koma??
@ChikumbutsoJohn-rs4tt
@ChikumbutsoJohn-rs4tt 20 күн бұрын
Bwana ine office kuno ku Lilongwe tikupita kokayang'anira mayeso koma no allowances 😅
@PeterChilombo-ou2cd
@PeterChilombo-ou2cd 20 күн бұрын
kkk iwe usandiseketse no what?aa. wabodzaiwe
@ChikumbutsoJohn-rs4tt
@ChikumbutsoJohn-rs4tt 20 күн бұрын
@@PeterChilombo-ou2cd ok u can not believe it,maybe your side, koma kuno tili sanatipasebe za Theory subjects
@SolomonShaibuh
@SolomonShaibuh 20 күн бұрын
Ndkhulupilira kut a Malawi mistake iyiyi sitizachitanso
@RidsonChafulumirah-r2y
@RidsonChafulumirah-r2y 20 күн бұрын
DC
@muneeladan8580
@muneeladan8580 20 күн бұрын
Mafia
@isaacchiwaula731
@isaacchiwaula731 20 күн бұрын
Ubwino wake a Chakwera omwe mukuwanenawo sakuyankhani nkomwe, mumangobwebwetuka zaziii ngat ufulu omwe mumamenyera anthu osaukawo umathandizapo kalikonse, tikungogonabe ndinjala ngat mumati mukayankhula apa mumatipatsa ndalama, phindu lanu ndichani, ine ndiye nsaname zimandinyasa izizi, palibe chomwe munthu wanzeru angayamikire pazomwe mumayankhulazi, coz maboma onsewa zochitika ndizimodzi palibeso wabwino apa, n zonse izizi zilibe nzeru, nanga mpunga souseg zimenezo zikankhale zoyankhulira anthu osauka kapena zangolowa zidani zanu?? Zopusa
@StanleyChirwa-d6b
@StanleyChirwa-d6b 20 күн бұрын
Samayankhatu mosathepo mau ap😅😅😅
@HalisonSolomon
@HalisonSolomon 20 күн бұрын
IWEYO ndi opusa kwambiri ndi chakwera wakoyo ngati akutuma cadet mbuzi, ngati iwe ukidya ndi mcp usawanyase AMALAWI AKUVUTIKA , ndiye uzikayankhula mbwerera zako zankutuzo , ngati sizikusangalatsa amakutuma kuti uzimvera ndi ndani ulibe manyazi ? Cadet supit
@isaacchiwaula731
@isaacchiwaula731 20 күн бұрын
@@HalisonSolomon ukufuna ndikuyankhe? Born kalindo umamudziwa? Zomwe akumayankhula amayankhulira iweyo, it's wat u think? Ok kavotere amene ukumufunayo n uzandiuze kut zinthu tsopano zilibwino pamoyo wako. Kalindo sankatukwana DPP ndi Peter munthalika? Lero mwaiwala
@StanleyChirwa-d6b
@StanleyChirwa-d6b 20 күн бұрын
@@isaacchiwaula731 inu musokosa mungosiya kuverako bas sizokakamiza izi boss
@HalisonSolomon
@HalisonSolomon 20 күн бұрын
@@isaacchiwaula731 iwe sungamakhale KUMBUYO kwa mcp ngati sukuona momwe dziko lavundira ndiye kuduka mutu kumeneko , usiyamitse mene chakwera amatenga boma linali motani ndiye pano zilimotani ? Ndiye timusiye chakera alamuleso lidzakhala dziko? Anthu adzakhala ngati ndani, tiyeni tiganizire ana omwe taberekawa tisakhale ngati a police ndi asilikali amene asankha kigwira ntchito ndi chipano malo moteteza malamulo adziko,
@BudaEarth
@BudaEarth 18 күн бұрын
U na problematic
@chadreckchibwithala1493
@chadreckchibwithala1493 20 күн бұрын
DC PANTCHITO IFE WOZIWA ZINTHU WE KNOW KUTI ABONI KALINDO ALIPO PA NTCHITO YOSUTSA CHILICHOTSE NDE MUWONE ALOMWE AVEKERE EEE OOOO UUUU KUKUWA AGALU ACHILOMWE MKUNYA MCP IS GOING NO WAY 2030 WOOOOO CHAKWERA.
@JeanKambala-gm1zr
@JeanKambala-gm1zr 20 күн бұрын
Zosantheka Brazil ndipo idzankhala yazikwanje zomwe² mwaphela saulosinever again MCP achimwene
@HalisonSolomon
@HalisonSolomon 20 күн бұрын
2030 mcp ikakhala mnyumba mwa kwanu zopusa anthu opanda nzeru ngati akukudyetsani ndiye muphe anthu chifukwa choti mukudya ndi mcp yakuphayo yankhanza zachibwana
@Lazarus-qo1sl
@Lazarus-qo1sl 20 күн бұрын
The DC
New model rc bird unboxing and testing
00:10
Ruhul Shorts
Рет қаралды 27 МЛН
EVOLUTION OF ICE CREAM 😱 #shorts
00:11
Savage Vlogs
Рет қаралды 7 МЛН
Double Stacked Pizza @Lionfield @ChefRush
00:33
albert_cancook
Рет қаралды 97 МЛН
路飞太过分了,自己游泳。#海贼王#路飞
00:28
路飞与唐舞桐
Рет қаралды 29 МЛН
BON KALINDO LERO PA  31 JULY 2024 |
17:12
DZIWE TV
Рет қаралды 20 М.
A Michael Usi Inu Si A UTM - Lyton Mangochi
23:13
Nyasa VoiceBox
Рет қаралды 18 М.
KWAVUTA A UTM AKUNG'ALURA UKU MOSAOPA MUNTHU|
9:10
DZIWE TV
Рет қаралды 15 М.
EXCLUSIVE INTERVIEW WITH BON KALINDO
59:52
Zodiak Malawi
Рет қаралды 49 М.
ACHAKWERA KU DOWA PA MTENGO WANTHENGA 🤔🤔🤔
17:04
HOT 265
Рет қаралды 39 М.
New model rc bird unboxing and testing
00:10
Ruhul Shorts
Рет қаралды 27 МЛН