But guys why can't we be like south Africans this too much chakwera wazolowela guys but why we Malawian we don't act guys akati boma ndife tomwe anthu onse akumalawi
Kupha ndi kumanga anthu, kodi ndale zimenezi bwanji kodi? Tilibe mu nthawi ya kamuzu 😢
@StevenTembo-mb7rm9 күн бұрын
Mr chakwera and your government bring back our freedom that our fathers and grandfathers fought for
@user-uc1pd1tc2x9 күн бұрын
Then Malawi timayenera kupanga mademo osausa koopsa zedi
@Malani419 күн бұрын
He is a great comedian
@AminaPhiri-pp9tw9 күн бұрын
Koma iwe chakwera bonikalindo usamupheso ngati mumene wachita ndi chilima uyambisa nkhondo midziko mo galu iwe
@user-pv9uk6sc3w9 күн бұрын
A chakwera ndi MCP yake sakudziwa kuti ku maiko ena anthu amamuuza President pamaso kuti itule pasi udindo. Tsopano a Malawi Bon Kalindo ndi Kamlepo Kalua kungolakhula choncho amangidwe! Aaaaaaaaah, useless government.
But chakwelayo anthu amene akuwamanga akulakwisa coz pano oziyipisilathu mbili munthu sazakhalaso president
@GeraldineSnyman8 күн бұрын
Komatu chotiuziwe iwe chakwela kenakoutasowe ndi iweyo sikalenso ayi
@trevorkasabikalyangu92559 күн бұрын
Please Release them. Peace
@YasinMusa-ym8lp9 күн бұрын
A yalukatu sanat mcp muona 2025 mutanosenu
@HappyAutumnTrees-cd9ye8 күн бұрын
Chonena ife tilibe 😭😭😭😭
@MathewsChitsulo9 күн бұрын
Chakwela ndi wakupha. Kodi nanga ndichifukwa chiyani akufuna kutseka anthu pakamwe by Force? He must not force us to keep quiet for the murder. How many people is he going to murder and how many times is he going to stop us looking for what killed Chilima and 8 others. He can do whatever is doing but he must remember that no matter how dark the night is, the don is still coming
@AubreyKadzuwa9 күн бұрын
Kd bomali ndi chan komatu a bwere wamoyo kumeneko
@AnnieBanda-rb2dk8 күн бұрын
manyi ake chakwera galu iwe chakwera ndeno oro umange anthu ukuona ngat oro umange anthu ndeno ukuwona ngat uwina galu iwe kachakwera, ubwereso kuno ku nkhotakota uzamange ine wava galu iwe ineso ndikumalengezaso kut wapha chilima ndiiweyo ndipo suzapeza voti kuno ku nkhotakota and nkhatabay galu iwe ubwereso kuno uzamange ine wava? galu opanda manyazi iwe l think inakubereka ndi ntchentche mayi wako ndi ntchentche ubwereso kuno uzamange ine galu iwe mayi anakubereka manyi awo galu iwee fiti yamunthu , ndikut oro umange anthu koma ndikubwerezaso unapha chilima ndiwe galu iwe chakwera ndikut wanapha chilima ndi chakweraaa
@MisheckAselo9 күн бұрын
Mumatero kumumanga akamanena chilungamo eee koma MCP, ameneu ndiye mutopa naye chifukwa mau achilungamo saopa gulu mutuluka Mr DC osaopa 🙏
@CatherineDesire9 күн бұрын
Akatero akufuna akampheso fiti dzachabe chobe
@chitchohistorical10369 күн бұрын
Malawi wanga mayooo 😭😭😭
@lonjebinga59208 күн бұрын
Akangopereka maumboniwo basi. They know the truth mesa?
When people say, MCP will remain that is according to the MCP we as Malawians know from the those old days when police cruisers were still in black painted colour with an eagle 🦅 mark on the left. Don't forget, with them killing is an inborn behaviour that they can't help it.
@AufiThera9 күн бұрын
Tizaima pachilunhamo ngat born kalindo pls don't killed him
@user-gi1gh9ry6h8 күн бұрын
?????? Boni kalindo asalakhole zowonadi kwa malawi 😂😂😂😂😂 shemu chakwela ndi mcp madafaka
And maganizo anga kuno ku mudzi kuno kulibe anthh azelu monga ngat momwe apanga zo fufuza za imfa y chilima ku pe mpa sadic kuti alowelerepo zomwe zikuchitika kumalawizi zandi kwana zed
@user-ww4ei5fb7d9 күн бұрын
Koma boma iri nkhanza zake, anthu akamati MCP ndi nkhanza ndi kupha adzikana? Anthu akanike kuyankhula mudziko la democracy? Mmmmmmmmm leading people with anger and emotions? 😅
@harryphiri90209 күн бұрын
Malawi is going to be like Zimbabwe no freedom at all becareful guys