Zoonadi Amalawi kudalira munthu dziko kumangogwa mungongole kuti dziko liyende kupepha pepha basi Malawi wafikapo ndi ngongole mmmmmhu Mau awa atisinthe zikomo father Elizey Munthalika Ambuye apitilize kukupani nzeru 🙏
@marthansaliwa77324 ай бұрын
So Powerful. Thank you so much man of God
@alicemalika6774 ай бұрын
May the Almighty God have mercy upon us . To do according to the Word
@greychizaka40884 ай бұрын
Live long brother. Message worth for my brain❤
@AndrewMandala-yz8ri4 ай бұрын
Powerful msg father wakumva wamva osamva sazamva
@AhmadumkomaTambala-lr9gp4 ай бұрын
Emen my father
@user-ig7dv8rp7r4 ай бұрын
Amen 🙏
@ShumHannah-yd9jg4 ай бұрын
😂 A LOUDER AMEN ❤😂
@emilynthite654520 күн бұрын
Mulungu akudalitse a ntalika
@johnkambala6924 ай бұрын
Ngati achokela kwa Mulungu alemekezeke, koma aaah panopa azitumiku akulalika zumumtima mwao. Zachisoni
@HarrisonMwanga-xy4sc3 ай бұрын
Malawi imadalila anthu mu ulamulilo wa democracy, poyambapo,sitimadalila,mbavazi, ndipo tinalibe nazo ntchito, chifukwa aliyese zithu zimayenda koma chifukwa cha boza ndi zina la democracy.lero, amalawi tikuitanidwa ndi maina amitundu.