Ine ID yanga ikangopanga expire ulendo ndingosaka kolowela. Malawi wandikanika🙌🏾
@chimwemwekamwana787Ай бұрын
Sindizasiya kumvera limpompo... Kumvera bakili muluzi tv.. born kalindo....❤❤❤❤
@vincentgerald9172Ай бұрын
Inense
@Homeofpeace321Ай бұрын
Chakwela amasankhila dala achewa maudindo aku army ndikupolisi kuti amuthandize kupha chilima, zonsezo tikuzidziwa
@DannieChimenyaАй бұрын
Limpopo Fm 🔥🔥🔥🔥ndipo timakutsatilan kwambili pitilizan kutiwuza zoona tililimodzi
@IsaacTsindeАй бұрын
Amenewa alawa kulamula komaliza...
@stelliamkupa693Ай бұрын
Ing'aluleni basi
@JamesChiphwanya-tb3tqАй бұрын
Inetu ndikuti ndikanakhala banja la vice president sindikanalola kuti boma litengepo mbali maliro amenewa komaso Malawi zukani iyi sikhani yokhala chete
Ndimaona ngati tisadzavoteso kungomutenga peter kumuika pampandopo basi galu ameneyu achoke basi😢😢
@user-pl8kw3dc9dАй бұрын
Koma achilima aphedwa maliro owawa chifukwa cha mpando 😭😭😭
@ToothyWebbАй бұрын
Tipite ku zambia konko tikawathothole bwanji?
@MphatsoWilliam-dh5ouАй бұрын
Ulemu Boss mtanyiwa osaopa
@JimmyKapunzaАй бұрын
May you God please protect this guy of Limpopo FM
@braveglorymwanzagolah4899Ай бұрын
Kung,galula basi osaopa
@stelliamkupa693Ай бұрын
Ipondeni fadah
@garnetphiriАй бұрын
I support you Mtanyula that Chilima and others are just killed even the the speech of Nankhumwa mmene amakhazikisa chipani chake anati ,akulu akulu ena asogoleli azipani anati agwesa athana nawo ndipo sadzaima pachisankho cha 2025
@JeanKambala-gm1zrАй бұрын
Tinkangonva mbuyomo Kuti MCP ndichipani chakumpha Koma tazionela ndimaso
Mulungu azikutetezerani kwa Adani chifukwa dziko limadana ndianthu achilungamo ngati Inu alimpopi FM mumatinvesa kukoma kobasi
@MesiyaChazingaАй бұрын
Tikumbukile za udasi chinamuchitikila ndichani yudasi atagulisa yesu anasowa ntendele mapeto ake anadzimangilila yekha mulungu sanyozedwa
@ToothyWebbАй бұрын
Zikomo comrade mtanyiwa.
@IsaacTsindeАй бұрын
Nkhondotu iyi
@amosbula1249Ай бұрын
Mbendera yathu ndi imeneyi. Dead but lives on.
@DavidJackson-ox4xmАй бұрын
The best Radio station in central Africa
@AlinafeChimoto-pp7wpАй бұрын
Athu ngati inu dziko lingayende bwino bwanji
@mayesojameskateteАй бұрын
Big up brother ❤❤
@TracyTomuАй бұрын
Koma Kwa kalindo alimbetu Amasamba mankhwala chimasanduka chilombo kkkkkk
@user-mc1ig1ex4vАй бұрын
The closure of Israel embassy, is the best solution for Malawi. We are at risk of loosing our identity as Malawi. Comrade Ntanyiwa, the DC and other activitis have opened all the hidden corners exposing the ruling government to have captured the state using Israel and Rwanda of course. Malawi wake up and get things done
@RobertChisenga-ci2mqАй бұрын
Thawi imeneo akulimbana ndi Peter muthalika,mau a chilima Osaziwa chakwela ndiye fisi wake adaziyamba yekha
@pemphokatembe443Ай бұрын
Mwaona mmm dziko 🙌
@SolomonBewulaАй бұрын
Osaopa
@PatrickMailosАй бұрын
Chakwera wapha chilima 😭😭😭 umboni ulipo
@ChimwemweKondowe-nj4lxАй бұрын
Ululani big Man. Ayaluke anthu amenewa
@user-jn4wu3ii5nАй бұрын
Limpopo . Go ahead. Umakwana ntanyiwa
@NgongireMwakasungulaАй бұрын
Tingoyambisa nkhondo basi tatopa ndi mcp tisatile chilima
@peternashyo9850Ай бұрын
MCP paulendo, timaona ngati za achina Gadama zija anasiyatu, ooooh!.
@DavidJackson-ox4xmАй бұрын
Mmmmm MCP ndiyoipa kwambiri
@nyanguoipa6996Ай бұрын
Timakunyadilani big man
@collennyadile8179Ай бұрын
Peter muntharika akufuna azamuphe tikamayandikila ku mavoti cholinga anthu azasowe mtengo wogwira tiyeni tidzuke MCP ndi chipani cha magadzi
boma lolamula zigawenga ili ndi mbava zokha zokha amabisara mu ubusa mbuzi za anthu
@user-mj2te7vl6pАй бұрын
Mufunirani umboni wina please
@thulanimpphiri6873Ай бұрын
Lipopo fm 1 Anthu analakwisa kwambiri amene anavotera mcp ndipo tivutika ngati kale. Anthu ena anavutika kutichosa mukamwa mwa ng'ona 1994 koma kupupuluma ife amalawi ndikuvotereso ng'ona
@ZamwanoАй бұрын
This is comred muthanyiwa on lipompo fm
@JustinLipipaАй бұрын
Crocodile party MCP
@user-gr2vr6yw8bАй бұрын
Ndikutsatila ndithu😭😭😭
@hanifahmponda8711Ай бұрын
Komato MCP akamwalila muthalika ndi DC kalindo.iiiiiii kaya malawi apa ifa achilima mwadziyika pamoto nde muphetso aaa nkhondo imeneyi chakwela iwe ndi galu nsono police adzichita kulondola anthu kuti ayankhula chiyani ndikuwona ngati ma Israel nde mulungu wanu aaa mulungu wamoyo sagongo GOD BLESS MALAWI
@StellaMike-og3wfАй бұрын
Ife tili pano kutsatira chilungamo dziko ndilatonse ili
@EnetChiombaАй бұрын
😢😢😢 eee koma nkhani zake zovuta
@sweeneykamwendo6251Ай бұрын
Mcp sizatheka... Malawians made a huge mistake
@SolomonNjolomoleАй бұрын
Pafupi ndi tower kmso mudzi anthu akuona km akuti kasakeni mu nkhalango zomvetsa chisoni kwambiri. 😢😢😢
@mlomwegomiwa1223Ай бұрын
Ife tizigona pompano bas
@jamesgama5489Ай бұрын
Koma nde kundende kudzaza but we are in democratic country we are not in one party system
@user-zc4wl5pc3mАй бұрын
😮😮
@marthansaliwa7732Ай бұрын
Mwazi wa Abel umulilire Kain. There should be no peace in the camp of the enemy
@user-ct9dx7mw9oАй бұрын
Following
@RaphaelJordanNyirendaАй бұрын
This world
@user-co3wr3rn4hАй бұрын
By public demand tiyeni a Malawi tisawope tisafooke tiyen tipange zothela amutuluse wa police ameneyo
Amalawi wake up chakwera atitha ndithu amanena zoona Kuti chikomekome chakhuyu mukati Muli Nyerere chakwera khope mawu achikoka Koma ndi fiti yotheradi shame on you chakwera
@chadreckchibwithala1493Ай бұрын
waboza iwe ndege yagwera pafupi ndi tower ya chikangawa malo otchedwa nkhunga not pafupi ndi mizi ayi
@ERICBISHOPJEREАй бұрын
It doesn't matter nawe. What matters is there were people next to what the whole thing happened. So someone should know exactly on what has happened.
@mishecksipolo7153Ай бұрын
Shut up,ndiye wqpangapo chqni with your information? Ukufuna Anthony asalankhule?