Big man ukamalankhula ngati usasiye koma mvuto mumachepetsa mphindi..anyway we proud of you may almighty Allah protect you
@dicksonhangiwa7847Ай бұрын
Ndimaona ngati vuto limeneli ndi ndekha, ndimangofunabe aziyankhula ,,
@harrisbanda5891Ай бұрын
Dat's true bro, amandiwelengela bwino kwambiri and he deserves to be a Journalist, osati ma Journalists enawa ukamawelenga khala ngati ali mmadzi or m'botolo , nthawiyo nde imachepadi Biggy pangani zoiwonjezela ndithu izifikira kuma 25 mnts please
@harrisbanda5891Ай бұрын
Journalist olimba mtima uyuu, big up Mr Biggy, amalawi tonsefe tili pambuyo panu kuphatikizapo tonse alliance yonse timakukondani
@harrisbanda5891Ай бұрын
Keep it up Mr BK tv, mumuphunzitsenso chawezi banda how to be a Journalist, azisiyanisa kukhala mtolankhani ndi politician, he doesn't differentiate a word between JOURNALIST and POLITICIAN
@HopefulCoralReef-tx4vxАй бұрын
Zoona zake man
@NicholasJames-cb7duАй бұрын
Mumativetsa kukoma kwambiri pitilizan watching from port Elizabeth RSA
@FelixMcDonardАй бұрын
Bakili muluzi ndi number one we all love ♥️♥️ you
@user-tn5eq9fp2zАй бұрын
Best tv Ever and not only in malawi but the whole world ❤❤ keep it up big man and fear nobody
@maggiekamphinda5699Ай бұрын
Osamasewela ndi Israel
@chigokhalid9420Ай бұрын
Inna Lillah wa Inna ilayih rajiuna
@jameskachulu8141Ай бұрын
Wina ndiye aziti timange bakili muluzi TV
@LongiMtimabiiАй бұрын
Ndipo Anya akamange kunkuyu okupha komanso mbava
@StevoZimbaАй бұрын
Kutumpa uko
@DjAmfumuАй бұрын
eti sichamba chimenecho nsanje basi ngati alephela osangosiya dziko bwanji, ndinanso angathe zomwe Bakili muluzi TV IKUPANGA or ku bomako ngati ali anzelu bwanji osatsegulanso channel yawo bwanji
@user-xd1cm7tm7tАй бұрын
Chocho azit akumangen azitiwuza nkhani ngat zimenezo ndi ndan
@patrickphiri5334Ай бұрын
Imagine ayi
@patrickphiri5334Ай бұрын
This is the only channel I get the news yodalilika
@innocentchirombo2073Ай бұрын
Ipondeni fadah ❤❤
@JamesbhekiGama-gt5oeАй бұрын
We understand we enjoyed for everything what your saying and thank very much keep it up your big man
@JAMESZIMBIRIАй бұрын
Ineso amandisangalatsa mkuluyi
@jameschibisa1433Ай бұрын
You are the best baba continue with the story we love you bakili muluzi tv for life
@user-eb7px2ex2qАй бұрын
Mwayankhula monveka ngt Aljazeera big up
@AjeliMwАй бұрын
Bakili muluzi tv we proud of you ndipo zomachepetsa mphindizi zimangoona kuchitika koma mmene ndimanvela kukoma mkamanvela nkhan zanu ngat zisamathe
Am your big fan yes ofcourse but today i would like send some special respect always stay safe and strong 💪
@user-et5nz4vz2vАй бұрын
Respect boss Best TV ever
@user-be5fc3ed1iАй бұрын
Mkammanga wa Bakili Muluzi tv ife tizanvera kwa ndani? Ameneyu si mnthu wamba ndiye amaunika zomwe zimachitika paziko lapansi. Ulemu wanu boss tiri pano ife kumvera kwa Inu zikachitika tiponyereni .the best Tv in the world not zinazi
@tisamulangala5570Ай бұрын
Watching from state house Malawi 🇲🇼
@user-fp5qn5ci2vАй бұрын
Nde wina wazimphonongolo mphuno aziti aseka Bakili Mulauzi TV
I also lo Bakili TV ndi ower wake paukadaulo wake maka kufufuza khani ndikudzieisa mtundu wa a malawi
@user-ng7re9sp1gАй бұрын
Watshing from durban
@user-mz4tk1pw3fАй бұрын
Inna lillah Wa inna ilayih rajiuna ulem wanu big koma ndadandaura imfa imeneyi kwambiri
@JamesbhekiGama-gt5oeАй бұрын
Mfwentu syabonga kakhulu akuwande Tina e RSA Siti thank you
@staceycossam5933Ай бұрын
Kkkkkkkkk
@staceycossam5933Ай бұрын
Awe my bro
@staceycossam5933Ай бұрын
Number kkkkkkkk
@PangolinimwАй бұрын
❤❤❤❤💪💪 my best tv
@user-pt1fy3qg4uАй бұрын
Never give up bro ❤
@user-to5of3ks3gАй бұрын
Nice story bro
@uchizJoelMumbaАй бұрын
Tamatiuzani zimenezi osati Zija zomalimbana ndi boma anthu andale asakugilitseni tchito ndi anthu oipa kwambili
@Littlefair7Ай бұрын
Raisi amasokoneza mtendere padziko lapansi, amathandiza magulu azigawenga, lero zinthu zadula padziko lonse chifukwa cha gulu lake la Houlthi limene lasokoneza the Red sea route. Asilamu ndi anthu osafunika padziko.
@christophermkhize1991Ай бұрын
Ine pano pheeee kumbetsela inuyo big man ipondeni fadah ulemu wanu
@wilsonsawasawa3794Ай бұрын
Good narration
@chrisboyce2Ай бұрын
Zoonadi ABWINO sakhalitsa 😢 Kusiya wathuyo kuno kuti azingotibera bas kaya ameneyu ikumuphonya pati anakapitaso naye ife tipume kumudzi kuno..
@user-dh8ml4bv4wАй бұрын
Kkkkk
@user-gx5ht9gm3zАй бұрын
WANING TO CHAKWEL NAYESO ONE DAY ITS ONE DAY TSIKU LAKE LIKUBWEL