Anakawatenga kulilongwe kukawavinisa ku mangochi... Amangochi sangapange manyi ngati awa
@user-oq5rg5mz7q2 ай бұрын
Nkazi wayine never kupita kusongano wa MCP
@user-fm8ed7eo3i2 ай бұрын
Mmmmmmmm moto wake uti poti akufuna kuti awadyere ndalama zomwe akubanzo, ndi wa kumangochinso
@usumanidaudi2 ай бұрын
Inuso a hanifa mwayamba kujama ya mcp anthu atatuwo paka kwawonesa apa muzawona apm pa 12 pano
@owenskabazanechiumia35432 ай бұрын
Koma ndiye Umphawi ndivuto lalikulu, Komanso Kamuzu anatipusitsa Azimayi achimalawi ndiotengeka ndi zaziii Anthu akuwawona awawika mumavuto ndiiwowo, koma nkuapasa so sapoti kuti apitilize kugwetsa Malawi mpaka tione K20000 note zomvetsa chisoni pa Mangochi apo.
@user-jn7bt1uy5s2 ай бұрын
Nambo kwereko
@user-pt8wb4vw6r2 ай бұрын
Mcp mito kuti buuuu❤❤❤
@user-gj4li2gc8o2 ай бұрын
Pa Malawi mpovuta ena akulila ena avotela yemweyo chakwera
@BerlindaJetel2 ай бұрын
Kkkk etietii zomvesa chisoni
@hawakumchengtokusonsoja11 күн бұрын
Bom iro
@charlesnanthambwe18322 ай бұрын
Mbuzi za dzimayi
@FaisonLukiyo2 ай бұрын
Auawo sagwira ntchito
@APOSTLEBJ-tc5fp2 ай бұрын
Ayao alibe nzeru alibe kaya chifukwa cha umbuli wosapita ku school kaya.mcp idapha ndi kuwocha nyumba za anthu aku mangochi ku malindi kwa amoto pofuna kumupha chipembere koma lero ayao ndikumasapota mcp zoona?
@BonganiCharles-ju4ty2 ай бұрын
Azimayi angododoloka zili zonse maka achiyao eeeee mavuto kufika kunyumba kungo ona poto wauma
@LovelyBlini-cu3iu2 ай бұрын
Ena ndi obwela MCP ndiyochenjera apasidwa ma 5pin adyeleni
@user-dh8ml4bv4w2 ай бұрын
Azimayi Ali ndiivuto kutengeka zaziiii
@hanifahmponda87112 ай бұрын
Aaaaa mangichi
@user-ww9rj2wx8d2 ай бұрын
Zakutumbo basi kusowa zochitatu uku hiyaaaa
@user-ti2ct8ts8d2 ай бұрын
Zitsiru kuvinila chitsilu chinzawo
@edenngoma82142 ай бұрын
Waiting
@innocentissah26362 ай бұрын
Zitsiru kuvinira mbava ngati akudya mmakwawo
@salimmkumakumakitombi-yc7pw2 ай бұрын
Ayao a 2 sim awa not a 1 sim .muyao wa original angamasapote idzi
@APOSTLEBJ-tc5fp2 ай бұрын
Koma zakuti sugar akugulitsa K6000 akuziziwa koma ayaowa?