I wish to see change for Malawian with alliance for democracy god bless you
@Nganya96Ай бұрын
Talk is free, mvura ikagwa kumachuluka zolilalira😂😂😂😂😂😊
@user-ve4zn2ne1kАй бұрын
Big up bro mumakwana ndinu big wa ma biggy ife tilindi inu even wina afune asafune munthu wakulu kwambiri mutambo❤❤❤❤
@TiyanjaneMkwate-we8guАй бұрын
Opusa uyu, mavuto tikuwaonawa anatipalia ndi iyeyo. May GOD punish him.
@MarymahendraАй бұрын
I want to see Malawi and change the present state like Chikwara is not doing well enough in four years time he killed 18people so please don’t be chose him may god bless Malawi xx
Musapuse naye Mtambo ndi nazikambe kapena kuti bilimankhwe
@JohnFrank-cg1yhАй бұрын
Izi ndi zoona anthu akale andale must go chifukwa ambiliwa ali ndi magazi m'mazi ndie zazitukuko sizingatheke, koma azingoganiza zothana ndi ana asogoleri am'mawa
@inessmsiyambiri8517Ай бұрын
Unalipilidwa kale mtambo wadyera
@ShelifibraheemАй бұрын
Bilimangwe Ali pa mpando wa blue tsopano
@CharlotteMushimiyimana-g6bАй бұрын
Zona
@EdwardKachinjika-c8qАй бұрын
Mose wake uti naweso usanamize wanthu iweyo
@AshimayeGamaАй бұрын
Ife sitidza khululupilaso andale ayi Bola dpp sina gwetsepo ndalama ayi
@JohnJohn-og8rtАй бұрын
Nkondo ilipo apa ukuvunika dpp kapena UDF afodi tikwavuna koma apapa ayi sangate
Very stupid info iyeyu analiko komwe ngoziyo ikachitikira matako ake
@SaidiMbawa-st6bjАй бұрын
Kodi Chilima ndi chida choyakhulira zandale kodi abale
@johnbullyohanittokasikizim7127Ай бұрын
Kodi munamupha ndinu?
@joebrown1158Ай бұрын
Iwe mwana wanjoka
@inessmsiyambiri8517Ай бұрын
Simwamupha dala cholinga tikhale mchonena
@joebrown1158Ай бұрын
@@inessmsiyambiri8517 you need someone to interpret for you people will not gonna stop to speak about chilima until the truth must prevail ngati wuli mvali yomweyo ya kupha nawo ndiwe watsoka
@kensonmbewe6692Ай бұрын
We Malawians are tired of you people, mukametana kuseriko mumabwera poyera kudzapangana black mail, timakidziwani ma politicians a Ku Malawi. Now we need a new blood, a new gene, we want someone selfless and bold to help Malawians not you people