Kwa APM yekhayo ndiye sangamukwanise dinner and dance ndi imeneyo koma Peter Muthalika yekhayo ku dinnerko Peter Muthalika akudziwa zokachita ifa ya Bingu Muthalika ndi ifa za anthu padege ukumupasa phunziro Peter amandisangalasa ndi omvera malangizo awanthu ngati Inu Amtanyiwa ndi Bakili Muluzi TV 🔥
Mwachita bwino Comrade mtanyiwa Tili nawenawe sitingakutaye
@RobertNedson14 сағат бұрын
Ambuye apitilize kukudalitsani 🙏🙏🙏🙏musafooke chonde chonde mulungu ali mbali yanu ndi ife ofuna mtendere ndiochitila chifundo malawi aliyese amen!🙏🙏🙏🙏
@AlexMbewe-p7y26 күн бұрын
NDIPO SIZITHEKA AYI MULUNGU ALI KOMWEKO AMENEUJA SANGAKWANISE CHAKWERA KWAKE KWATHA NDIPO ALI NDI THAWI YOCHEPA MULUNGU AMULANGA ANANGOKHALA BUSA KOMA NDICHIGAWENGA CHACHABECHABE BUT I BELIEVE GOD IS THERE TO PROTECT PETER WA MUTHALIKA
@macdonaldkorea292826 күн бұрын
Or nkhope ya Chakwerayo ikuchitakuonetsa kut ndinkhandwe yoopsa....asapotilidze.konse aidya malawi yonse
@StelliaSangaya22 күн бұрын
Zoonad
@Emmanuelisraelsimbi26 күн бұрын
Koma ngati mgwirizano watha ndiye tikhale chisankho tu coz utsogoleri wu unasankhidwa pansi pa mgwirizano wa Tonse. Lets vote guys
@user-dn3gp6yi4y27 күн бұрын
Kumeneko ndiye ku mafelano kuja sopano koma anthu awa akuti bwanji ndi dziko lathu cholinga chawo ndi chani? Komaso asilikali athu angoti ziiiii kumangowonelela dziko likuwinengeka koma zoti abale awo ndi makolo awo ku mamamidziku akuvutika iwowo sakuziwa kodi? Nanga chomwe akumakhalila chete ndi chani ? Chakwela kwake kwatha ife tikufuna mtendele mu dziko musakomedwe ndi ndalama komaso omwe akudya ndalama za magazizi si asikali onse pali omwe akumadya enanu dzukani kutha ndi boma lopusali lakupha la mabodza komaso pa katangale azathu aku mangochi tetedzani PM kumeneko akaziwika anthuwo apondeni or kuwapha kumene np afela zintchito zawo
@VeronicaChirwa-ct4os26 күн бұрын
Asilikali a Malawi amawoneka kuti ndi opepera safuna kuthandiza Zika za Malawi akowopa kuyimbira anthu akulemekeza zigawenga zi Achina Chakwera
@HamzaMkwanda-bh8dc26 күн бұрын
We don't have any police in our country
@ChifundoNinje26 күн бұрын
Plz plz achisale amunkhitho plz maso ndinu kt amene mumapeleka chitetezo Kwa Pam
@preciouskadembo193226 күн бұрын
Dr Bakili Muluzi amkatuza koma ife aMalawi kusamva
@user-tw2zf7bj3e26 күн бұрын
May Allah almighty protect Apm 🤲 amiina
@AndrewDinala-d9j26 күн бұрын
Yes
@ephraimphalawala472026 күн бұрын
In Jesus name, God protect APM
@PeterJames-i8y26 күн бұрын
Mulungu amene anapulumutsa shadrec ,Mishec ndi abitinego kuphatikiza Daniel mudzenje lamikango apulumutsenso azitsogoleri amene atsalawa. kuti kudziwike kuti kumwamba kuli mulungu wamoyo amene sagona komaso saphethira amawona chilichose cha pasi pa thambo. mulungu apitilize kuulula zisisi pa ana ake amen.
@VungaQueen26 күн бұрын
Amen ❤❤
@wangachindeya857726 күн бұрын
Amen
@TamikaKaponya20 күн бұрын
Amen
@salimmkumakumakitombi-yc7pw27 күн бұрын
Uthenga upite kwa Norman chisale .onesetsani kuti chitetedzo chakhwimisidwa pa gate
@harrietmkusangombe26 күн бұрын
God have mercy on our country
@AhmadShariff-bk3rr27 күн бұрын
Mission impossible
@OnenessLestas26 күн бұрын
Zamaboza basi mulungu akuwoneni
@ephraimphalawala472026 күн бұрын
Prayer Malawi
@user-pv9uk6sc3w26 күн бұрын
End of chakwera and MCP, achepa, wapha uja Chilima wakwana basi. Thanks to Limpopo FM.
@IbrahimPhiri-ky5jk26 күн бұрын
Awili aziwika kale tikuimbolani kuti muziwe zosatila anafika pa asoko ndiye atawapo koma tikuwalondolola anyani amenewa komanso mangochi boys ili paliponse 💯
@FrankSpison-o7o26 күн бұрын
Lord have mercy on us
@wangachindeya857726 күн бұрын
Amen
@user-bd5kw8oq1r26 күн бұрын
Koma apa pali anthu odwala amene amakhulilupilila social media dziko lathadi basi munthu kungodzuka kupanga plan yoyipitsa munthu basi the opposite is true inu ndi amene mukufuna chakwera ataphedwa mu nthawi ya DPP anthu amaphedwa ambili apa lero iliso layipa bndiyetu sankhani yesu osati satana mudzakondwa
@PatrickSomanje26 күн бұрын
I love u mr khanga osawopa ngwilanani manja pls
@user-pt8wb4vw6r26 күн бұрын
Inu antanyiwa mwina inuyo ndinu mmapha anthu ndiye mzinamizila ena ndinu zizsilu ndi maboza anuwo
Mulungu ndiwamphavu yonse Nothing can happen to them in the name of Jesus
@MatemangaMoyo26 күн бұрын
Limpopo FM ndi bakili muluzi tv, mulungu akupaseni moyo wautali
@Janaphiri27 күн бұрын
Munthalika wakuti sangalanulire Dziko la Malawi ali ndi ntchito yanji? Za fodya basi Kodi mwasiya za Tea mwayamba za chamba eti
@user-mi2xf3sw1i26 күн бұрын
Ku kholo kwa amako wamva
@dalitson355826 күн бұрын
Pantumbo pa mayi wako galu iwe
@WisdomMaseko-fi5sv26 күн бұрын
Koma mtanyiwa ndi masewero ako ukuzuza anthu kwabasi ona ena ayamba kale kupempherera APM kkkkk
@kensonmbewe669224 күн бұрын
I think this is a sign that we have so many satanists in Malawi, we need God, anthu afika pongoyankhula zimene akugani as long as it will black mail Chakwera, how can you feel if that happens to your father. Too bad
@nyanguoipa699626 күн бұрын
Anthu amenewo asamale mangochi sigawa ma sweet
@AREFRIEDNELSON26 күн бұрын
MCp ndichigawenga kuchokela ma 90s nde wina iziti chakwera Alobwino walowa nzwiwanda wangofika pa misara
@ChristopherManase-s1f26 күн бұрын
Eeeee koma ma cadet muli pa ntchito. Kkkkkk
@adrianobrigida340226 күн бұрын
Chigawengacho Chichewa Chakwera chikutseweretsa miyoyo ya wanthu.
@kidneyblessingschilinguloj729226 күн бұрын
Keep it up
@piliranimalama609026 күн бұрын
Anthu ndiye kuwadodatu ndi mabodza
@FamousJohnathan26 күн бұрын
Yanjiru simatani..?
@WilliamMasauko-su1wx26 күн бұрын
Siiswa
@JohnFrank-g6e14 күн бұрын
Ndi Ana awa zomwe akufuna sizitheka komwe in the name of Jesus
@macdonaldkorea292826 күн бұрын
Tiyamike kut okonda dziko ngati achina Mtanyiwa alipo ambiri....chifukwa chaichi choipa sichibweredzedwa....a Gadama, Matenje ndiena monga a Chilima ndiena aja akwana, pa Muthalika pokha usayerekedze ndithu iwe Chakwera (kungokhala anthu amagazi basi) Bakili Muluzi amkanenatu kut MCP siyoyanjana nayo lero ndiiyo itangolawa mpandowo basi kupha kwadzuka ASAAAAA
@cliftondad381625 күн бұрын
Zinazi zalowa fodya zinthu.. apa nde trust pa nkhani zanu ndachosa.... Maboza
@user-od6eo5zc4h26 күн бұрын
Mudzina la yesu christu mnazaleti mutetezelnini Peter mutalika kulikonse komwe kuli iye
@christophergibson7226 күн бұрын
Inu munthu watha kale uyu mufuna mudanitse basi
@JosephyMakunganya27 күн бұрын
Nkhope za Rwandans zimadziwika asalowe dara kumeneko
@EliasKawuwa26 күн бұрын
A Ntanyiwa tengani ndi inuyo dzikoli,musawauze azanu kuti atenge koma inuyo, a Bon Kalindo, wa Bakili Muluzi TV,atenge dzikoli,kuti kunyoza,ndikutukwana kusiye, kumangonyoza basi, zambiri zimene mumanena ndizabodza kwambiri, zonse akunena za Peter Muntharika ndi zabodza zimenezo, kungofuna kudzionetsa kuti achina Peter Muntharika awaone kuti akupanga za iwowo,kuti DPP ikadzawina adzawatole,adzadyetse mimba zawo
Umakwana ntanyiwa koma akangopha muntalika nafe tipha ndimiyala chakwerayo
@GraceMbengo25 күн бұрын
We pray for God's intervention. Mission iyi Ambuye alowererepo.
@chadreckchibwithala149326 күн бұрын
koma mmm ntanyiwa boza ngati mnthu wa nkazi aaaa mnthu oti si wa dpp akagula ticket mnthu wachilendo aaa
@kangungufoundation202025 күн бұрын
Kodi amalawi bingu anakulakwirani chani?? Munamuchotsa mwachipongwe, peter uyu mukuti peter ndimunthu amene munamuchotsa mwa chipongwe again kungoni peter ndi chitsiru akuloranso kuti azapangidwenso chipongwe, saulos chilima zana zanali mumamutukwana limodzi ndi chakwera nde poti lero wamwalira wasanduka wabwino amalawi mulibe nzeru you deserve what is happening and there is no way out until you change, you will reap what you sowing
@user-uk1tt7ho9t26 күн бұрын
May Lord for everything please protect our beloved president