No video

Nkhanga zaona Chakwera watumiza Asilikali kuti Akamuphe Peter Muthalika lero.

  Рет қаралды 102,225

Jay Kawere Mw

Jay Kawere Mw

28 күн бұрын

Пікірлер: 436
@johnmpatama1461
@johnmpatama1461 27 күн бұрын
This is the beginning of the end of Chakwera government.
@user-mr2mh4gq8w
@user-mr2mh4gq8w 26 күн бұрын
AMbuye mutisogolere Peter ndi salimo 91 ambuye mupase I mzimu wachiziwitso
@user-ev6bi7jr7g
@user-ev6bi7jr7g 27 күн бұрын
Ndiye MCP tikuidziwa ife ndimeneyo ndale zake ndi zakupha
@stephankamyata3862
@stephankamyata3862 26 күн бұрын
Achisale pls motsongozedwa ndambuye protect our APM
@augustMag
@augustMag 26 күн бұрын
Kwa APM yekhayo ndiye sangamukwanise dinner and dance ndi imeneyo koma Peter Muthalika yekhayo ku dinnerko Peter Muthalika akudziwa zokachita ifa ya Bingu Muthalika ndi ifa za anthu padege ukumupasa phunziro Peter amandisangalasa ndi omvera malangizo awanthu ngati Inu Amtanyiwa ndi Bakili Muluzi TV 🔥
@miketholiwa1762
@miketholiwa1762 25 күн бұрын
Asamale kwambiribe koma
@user-ky4ce9gb6j
@user-ky4ce9gb6j 25 күн бұрын
Eti
@user-ky4ce9gb6j
@user-ky4ce9gb6j 17 күн бұрын
@@augustMag ndipo kwambiri tu mmm
@BrownMainje-sh7hj
@BrownMainje-sh7hj 26 күн бұрын
Shame on MCP
@ExcitedBreakingWaves-oh3zb
@ExcitedBreakingWaves-oh3zb 26 күн бұрын
Ngati iyeyo akuphanso Pieter nayenso ayenera kusogozana naye.
@user-ky4ce9gb6j
@user-ky4ce9gb6j 25 күн бұрын
Ndipo kwambiri tu mmm
@MayamikoBanda-jh8bn
@MayamikoBanda-jh8bn 26 күн бұрын
I love the way momwe mumachenjeza Malawi kwa zigawenga . Ndiye nimamutsatilani kwambiri pa KZfaq Kono ku Zambia
@MaggieMujuma
@MaggieMujuma 26 күн бұрын
Eeeee mayo ndalama yanga ine Peter munthalika iwe ndi Wilson msemanjira iwe anthu okuba inu
@chimeraJonathan
@chimeraJonathan 24 күн бұрын
L
@AiameAdamo-su1nt
@AiameAdamo-su1nt 27 күн бұрын
I'm here following you step by step each and everyday.
@PhilipMatolino
@PhilipMatolino 27 күн бұрын
Kom guyz chakwera khani ndiyotu wina kungofanso kukhala ma demo anyooo!! Mwatitola mcp kwambiri
@cynthiakananji1608
@cynthiakananji1608 27 күн бұрын
Ndipo apitilira Aku Kenya kuvutatu owo
@KhalideNerve-mu1eq
@KhalideNerve-mu1eq 27 күн бұрын
Mission impossible God is watching 😢
@KennedyPhiri-h9h
@KennedyPhiri-h9h 26 күн бұрын
Thanks for your information Mr Limpopo FM 🙏 we always with you
@louisgolden
@louisgolden 26 күн бұрын
May Allah protect APM
@user-ew4dm8yy3b
@user-ew4dm8yy3b 26 күн бұрын
Achisale motsogozedwa nd mulungu please protect apm
@chrisschikozera7271
@chrisschikozera7271 26 күн бұрын
That's end of mcp in this country again.....God ll protect Amp
@lovenessmuthiya3513
@lovenessmuthiya3513 26 күн бұрын
May God protect APM
@user-be5fc3ed1i
@user-be5fc3ed1i 26 күн бұрын
Nyimbo imeneyo ntanyiwa ukamabwera pa Limpopo FM usayisiye chonde Limpopo FM moto kuti buuu 🔥🔥 🔥🔥🔥
@JosephyMakunganya
@JosephyMakunganya 27 күн бұрын
Apa ndiye alimbana ndi achina chisale 🔥🔥 Malawi wafika posauzana
@CharlesMaloya
@CharlesMaloya 26 күн бұрын
Chakwela and Rwanda foreigner based in Malawi you will get what you want warning to Rwanda you will see
@salimmkumakumakitombi-yc7pw
@salimmkumakumakitombi-yc7pw 27 күн бұрын
APM SANGAPITE NGATI CHIWETO .YEMWE UJA MUNAPANGA UJA BANSI .. APM ATUPELE CHIHANA ANTHU AWAWA SANGAPANFIDWE NTINTINI NEVER
@user-ky4ce9gb6j
@user-ky4ce9gb6j 25 күн бұрын
Eti
@AjibuTwalibu
@AjibuTwalibu 26 күн бұрын
Mwachita bwino Comrade mtanyiwa Tili nawenawe sitingakutaye
@RobertNedson
@RobertNedson 14 сағат бұрын
Ambuye apitilize kukudalitsani 🙏🙏🙏🙏musafooke chonde chonde mulungu ali mbali yanu ndi ife ofuna mtendere ndiochitila chifundo malawi aliyese amen!🙏🙏🙏🙏
@AlexMbewe-p7y
@AlexMbewe-p7y 26 күн бұрын
NDIPO SIZITHEKA AYI MULUNGU ALI KOMWEKO AMENEUJA SANGAKWANISE CHAKWERA KWAKE KWATHA NDIPO ALI NDI THAWI YOCHEPA MULUNGU AMULANGA ANANGOKHALA BUSA KOMA NDICHIGAWENGA CHACHABECHABE BUT I BELIEVE GOD IS THERE TO PROTECT PETER WA MUTHALIKA
@macdonaldkorea2928
@macdonaldkorea2928 26 күн бұрын
Or nkhope ya Chakwerayo ikuchitakuonetsa kut ndinkhandwe yoopsa....asapotilidze.konse aidya malawi yonse
@StelliaSangaya
@StelliaSangaya 22 күн бұрын
Zoonad
@Emmanuelisraelsimbi
@Emmanuelisraelsimbi 26 күн бұрын
Koma ngati mgwirizano watha ndiye tikhale chisankho tu coz utsogoleri wu unasankhidwa pansi pa mgwirizano wa Tonse. Lets vote guys
@user-dn3gp6yi4y
@user-dn3gp6yi4y 27 күн бұрын
Kumeneko ndiye ku mafelano kuja sopano koma anthu awa akuti bwanji ndi dziko lathu cholinga chawo ndi chani? Komaso asilikali athu angoti ziiiii kumangowonelela dziko likuwinengeka koma zoti abale awo ndi makolo awo ku mamamidziku akuvutika iwowo sakuziwa kodi? Nanga chomwe akumakhalila chete ndi chani ? Chakwela kwake kwatha ife tikufuna mtendele mu dziko musakomedwe ndi ndalama komaso omwe akudya ndalama za magazizi si asikali onse pali omwe akumadya enanu dzukani kutha ndi boma lopusali lakupha la mabodza komaso pa katangale azathu aku mangochi tetedzani PM kumeneko akaziwika anthuwo apondeni or kuwapha kumene np afela zintchito zawo
@VeronicaChirwa-ct4os
@VeronicaChirwa-ct4os 26 күн бұрын
Asilikali a Malawi amawoneka kuti ndi opepera safuna kuthandiza Zika za Malawi akowopa kuyimbira anthu akulemekeza zigawenga zi Achina Chakwera
@HamzaMkwanda-bh8dc
@HamzaMkwanda-bh8dc 26 күн бұрын
We don't have any police in our country
@ChifundoNinje
@ChifundoNinje 26 күн бұрын
Plz plz achisale amunkhitho plz maso ndinu kt amene mumapeleka chitetezo Kwa Pam
@preciouskadembo1932
@preciouskadembo1932 26 күн бұрын
Dr Bakili Muluzi amkatuza koma ife aMalawi kusamva
@user-tw2zf7bj3e
@user-tw2zf7bj3e 26 күн бұрын
May Allah almighty protect Apm 🤲 amiina
@AndrewDinala-d9j
@AndrewDinala-d9j 26 күн бұрын
Yes
@ephraimphalawala4720
@ephraimphalawala4720 26 күн бұрын
In Jesus name, God protect APM
@PeterJames-i8y
@PeterJames-i8y 26 күн бұрын
Mulungu amene anapulumutsa shadrec ,Mishec ndi abitinego kuphatikiza Daniel mudzenje lamikango apulumutsenso azitsogoleri amene atsalawa. kuti kudziwike kuti kumwamba kuli mulungu wamoyo amene sagona komaso saphethira amawona chilichose cha pasi pa thambo. mulungu apitilize kuulula zisisi pa ana ake amen.
@VungaQueen
@VungaQueen 26 күн бұрын
Amen ❤❤
@wangachindeya8577
@wangachindeya8577 26 күн бұрын
Amen
@TamikaKaponya
@TamikaKaponya 20 күн бұрын
Amen
@salimmkumakumakitombi-yc7pw
@salimmkumakumakitombi-yc7pw 27 күн бұрын
Uthenga upite kwa Norman chisale .onesetsani kuti chitetedzo chakhwimisidwa pa gate
@harrietmkusangombe
@harrietmkusangombe 26 күн бұрын
God have mercy on our country
@AhmadShariff-bk3rr
@AhmadShariff-bk3rr 27 күн бұрын
Mission impossible
@OnenessLestas
@OnenessLestas 26 күн бұрын
Zamaboza basi mulungu akuwoneni
@ephraimphalawala4720
@ephraimphalawala4720 26 күн бұрын
Prayer Malawi
@user-pv9uk6sc3w
@user-pv9uk6sc3w 26 күн бұрын
End of chakwera and MCP, achepa, wapha uja Chilima wakwana basi. Thanks to Limpopo FM.
@IbrahimPhiri-ky5jk
@IbrahimPhiri-ky5jk 26 күн бұрын
Awili aziwika kale tikuimbolani kuti muziwe zosatila anafika pa asoko ndiye atawapo koma tikuwalondolola anyani amenewa komanso mangochi boys ili paliponse 💯
@FrankSpison-o7o
@FrankSpison-o7o 26 күн бұрын
Lord have mercy on us
@wangachindeya8577
@wangachindeya8577 26 күн бұрын
Amen
@user-bd5kw8oq1r
@user-bd5kw8oq1r 26 күн бұрын
Koma apa pali anthu odwala amene amakhulilupilila social media dziko lathadi basi munthu kungodzuka kupanga plan yoyipitsa munthu basi the opposite is true inu ndi amene mukufuna chakwera ataphedwa mu nthawi ya DPP anthu amaphedwa ambili apa lero iliso layipa bndiyetu sankhani yesu osati satana mudzakondwa
@PatrickSomanje
@PatrickSomanje 26 күн бұрын
I love u mr khanga osawopa ngwilanani manja pls
@user-pt8wb4vw6r
@user-pt8wb4vw6r 26 күн бұрын
Inu antanyiwa mwina inuyo ndinu mmapha anthu ndiye mzinamizila ena ndinu zizsilu ndi maboza anuwo
@GRACIOUSKENAN
@GRACIOUSKENAN 25 күн бұрын
Ntanyiwa ndiwe one, continue ,tilibe asilikali angakhale police, kulibe ndattttiii aaaaaaa !!!!!! Agalu alipowo ntchito ndi zigololo bas😰😭😭
@vituveggah7619
@vituveggah7619 26 күн бұрын
Osazamuphwekesa comrade
@AndrewChilambo
@AndrewChilambo 26 күн бұрын
Antanyiwa pitilizani kuchenjeza amalawi zazigawenga za mcp
@AiwaMedia-sh6vx
@AiwaMedia-sh6vx 27 күн бұрын
Limpopo FM and BAKILI MULUZI TV mukuyesetsa ndithu kutitsegula mmaso koma amene alikutsogolo kwathu n'gokhumudwitsa. A Opposition aliko????
@GrinTemboh
@GrinTemboh 26 күн бұрын
Continue with good news we always listen u ukutimvetsa kukoma ntanyiwa
@benjaminjobo3525
@benjaminjobo3525 26 күн бұрын
Nyimboyi ndaikonda Antanyiwa cain ndi abelo
@tiwongehojaney5873
@tiwongehojaney5873 26 күн бұрын
God will protect Peter ❤❤❤😢😢
@ThivadoartistDyson
@ThivadoartistDyson 26 күн бұрын
Akangopha peter l tell you chakwela we come by the trip cross the country kukathana ndi iweyo alu continue.
@user-ky4ce9gb6j
@user-ky4ce9gb6j 25 күн бұрын
Ndipo kwambiri tu mmm
@kennethkaunda3636
@kennethkaunda3636 26 күн бұрын
Can I come to Malawi and show my position to chakwera government?
@user-sw8bb3iz7x
@user-sw8bb3iz7x 25 күн бұрын
God protect APM
@AleksaWilliams-qc6cn
@AleksaWilliams-qc6cn 27 күн бұрын
Yoo alipachintchito eti
@BlessMnyenyembe
@BlessMnyenyembe 27 күн бұрын
Thanks
@AllanKamphata
@AllanKamphata 26 күн бұрын
Mwasowa nkhani, akaphe nkhalamba ngati imeneyi
@BenPhillip-fw8hi
@BenPhillip-fw8hi 26 күн бұрын
Mmmm
@FrolenceKochelannkhata
@FrolenceKochelannkhata 26 күн бұрын
Ndipo inu!mabodza basi
@user-vq5fe6mo6o
@user-vq5fe6mo6o 20 күн бұрын
Nipamene wina akt chakwera 😢😢koma zowawa izi menyeren nkhondo Ambuye titan padziko pano
@UsenLashid
@UsenLashid 26 күн бұрын
Mulungu ndiwamphavu yonse Nothing can happen to them in the name of Jesus
@MatemangaMoyo
@MatemangaMoyo 26 күн бұрын
Limpopo FM ndi bakili muluzi tv, mulungu akupaseni moyo wautali
@Janaphiri
@Janaphiri 27 күн бұрын
Munthalika wakuti sangalanulire Dziko la Malawi ali ndi ntchito yanji? Za fodya basi Kodi mwasiya za Tea mwayamba za chamba eti
@user-mi2xf3sw1i
@user-mi2xf3sw1i 26 күн бұрын
Ku kholo kwa amako wamva
@dalitson3558
@dalitson3558 26 күн бұрын
Pantumbo pa mayi wako galu iwe
@WisdomMaseko-fi5sv
@WisdomMaseko-fi5sv 26 күн бұрын
Koma mtanyiwa ndi masewero ako ukuzuza anthu kwabasi ona ena ayamba kale kupempherera APM kkkkk
@kensonmbewe6692
@kensonmbewe6692 24 күн бұрын
I think this is a sign that we have so many satanists in Malawi, we need God, anthu afika pongoyankhula zimene akugani as long as it will black mail Chakwera, how can you feel if that happens to your father. Too bad
@nyanguoipa6996
@nyanguoipa6996 26 күн бұрын
Anthu amenewo asamale mangochi sigawa ma sweet
@AREFRIEDNELSON
@AREFRIEDNELSON 26 күн бұрын
MCp ndichigawenga kuchokela ma 90s nde wina iziti chakwera Alobwino walowa nzwiwanda wangofika pa misara
@ChristopherManase-s1f
@ChristopherManase-s1f 26 күн бұрын
Eeeee koma ma cadet muli pa ntchito. Kkkkkk
@adrianobrigida3402
@adrianobrigida3402 26 күн бұрын
Chigawengacho Chichewa Chakwera chikutseweretsa miyoyo ya wanthu.
@kidneyblessingschilinguloj7292
@kidneyblessingschilinguloj7292 26 күн бұрын
Keep it up
@piliranimalama6090
@piliranimalama6090 26 күн бұрын
Anthu ndiye kuwadodatu ndi mabodza
@FamousJohnathan
@FamousJohnathan 26 күн бұрын
Yanjiru simatani..?
@WilliamMasauko-su1wx
@WilliamMasauko-su1wx 26 күн бұрын
Siiswa
@JohnFrank-g6e
@JohnFrank-g6e 14 күн бұрын
Ndi Ana awa zomwe akufuna sizitheka komwe in the name of Jesus
@macdonaldkorea2928
@macdonaldkorea2928 26 күн бұрын
Tiyamike kut okonda dziko ngati achina Mtanyiwa alipo ambiri....chifukwa chaichi choipa sichibweredzedwa....a Gadama, Matenje ndiena monga a Chilima ndiena aja akwana, pa Muthalika pokha usayerekedze ndithu iwe Chakwera (kungokhala anthu amagazi basi) Bakili Muluzi amkanenatu kut MCP siyoyanjana nayo lero ndiiyo itangolawa mpandowo basi kupha kwadzuka ASAAAAA
@cliftondad3816
@cliftondad3816 25 күн бұрын
Zinazi zalowa fodya zinthu.. apa nde trust pa nkhani zanu ndachosa.... Maboza
@user-od6eo5zc4h
@user-od6eo5zc4h 26 күн бұрын
Mudzina la yesu christu mnazaleti mutetezelnini Peter mutalika kulikonse komwe kuli iye
@christophergibson72
@christophergibson72 26 күн бұрын
Inu munthu watha kale uyu mufuna mudanitse basi
@JosephyMakunganya
@JosephyMakunganya 27 күн бұрын
Nkhope za Rwandans zimadziwika asalowe dara kumeneko
@EliasKawuwa
@EliasKawuwa 26 күн бұрын
A Ntanyiwa tengani ndi inuyo dzikoli,musawauze azanu kuti atenge koma inuyo, a Bon Kalindo, wa Bakili Muluzi TV,atenge dzikoli,kuti kunyoza,ndikutukwana kusiye, kumangonyoza basi, zambiri zimene mumanena ndizabodza kwambiri, zonse akunena za Peter Muntharika ndi zabodza zimenezo, kungofuna kudzionetsa kuti achina Peter Muntharika awaone kuti akupanga za iwowo,kuti DPP ikadzawina adzawatole,adzadyetse mimba zawo
@user-gd6zb2bv8f
@user-gd6zb2bv8f 25 күн бұрын
CHAKWERA tamachita manyazi zinazi popanga, nawenso Manganya ndiwe katukule, Mulungu wakumwamba, achite nanu mwapadera ndipo asakusiyani chonchi
@patrickkusailemp3769
@patrickkusailemp3769 26 күн бұрын
Longlive APM ..God is in control !!
@ibrahimalex7137
@ibrahimalex7137 27 күн бұрын
We're here my brother ❤
@MalawianMediafm97
@MalawianMediafm97 26 күн бұрын
🤣🤣🤣🤣 this is Comred ntanyiwa on Lipompo FM
@AbdulmajeedJbanda-oz3jv
@AbdulmajeedJbanda-oz3jv 26 күн бұрын
Timakunyadilani big
@MuhammadBAKILI-kl2mj
@MuhammadBAKILI-kl2mj 26 күн бұрын
🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏yomweyo chikangawa
@GodifureRifa
@GodifureRifa 26 күн бұрын
Mulungu mumutetezere peter muthalika kulikose komwe apita 🙏🙏🙏
@SmileMalanda
@SmileMalanda 26 күн бұрын
Akuluwa misala chani kapena mwaz wachilima nd anthu ena aja zikuwazunguza😂😂😂
@NDIZOTHEKABANDA
@NDIZOTHEKABANDA 26 күн бұрын
Mabozatu amenewo
@mellipherjohn7158
@mellipherjohn7158 26 күн бұрын
mumakwana bwana wanthuu🎉🎉🎉
@marryphili5419
@marryphili5419 25 күн бұрын
Shame you chakwera fiti Yopanda manyazi wunapha chilima Pano wayamba kusaka Peter wupha anthu angati iwe
@AgnessMita
@AgnessMita 25 күн бұрын
Ambuye akutetezeleni APM
@MaureenBanda-t2q
@MaureenBanda-t2q 26 күн бұрын
Asiyeni akafa ndiiwowo ili ndi dziko
@user-gm3cx2xn9o
@user-gm3cx2xn9o 23 күн бұрын
Inu anthu akungofuna kutchuka ndiye inu muli busy 😂😂😂😂😂
@BenjaminCharlie-md3fk
@BenjaminCharlie-md3fk 22 күн бұрын
Umakwana ntanyiwa koma akangopha muntalika nafe tipha ndimiyala chakwerayo
@GraceMbengo
@GraceMbengo 25 күн бұрын
We pray for God's intervention. Mission iyi Ambuye alowererepo.
@chadreckchibwithala1493
@chadreckchibwithala1493 26 күн бұрын
koma mmm ntanyiwa boza ngati mnthu wa nkazi aaaa mnthu oti si wa dpp akagula ticket mnthu wachilendo aaa
@kangungufoundation2020
@kangungufoundation2020 25 күн бұрын
Kodi amalawi bingu anakulakwirani chani?? Munamuchotsa mwachipongwe, peter uyu mukuti peter ndimunthu amene munamuchotsa mwa chipongwe again kungoni peter ndi chitsiru akuloranso kuti azapangidwenso chipongwe, saulos chilima zana zanali mumamutukwana limodzi ndi chakwera nde poti lero wamwalira wasanduka wabwino amalawi mulibe nzeru you deserve what is happening and there is no way out until you change, you will reap what you sowing
@user-uk1tt7ho9t
@user-uk1tt7ho9t 26 күн бұрын
May Lord for everything please protect our beloved president
@CatherineDesire
@CatherineDesire 22 күн бұрын
Asilikali nanuso bwanji otsangomupha iyeyo wakutumani Kodi anzako sakufuna moyo
@JabiluWaiti
@JabiluWaiti 25 күн бұрын
Mmmm koma akachoka kwa Peter abwera kwa inu a UDF inunso mukuyenera kukhala osamala
@user-kc7sd3te3d
@user-kc7sd3te3d 27 күн бұрын
Kodi asirikali athu bwanji ku Malawi uko mwangokhala pheeee 😂😂😂
@gladysbonongwe1038
@gladysbonongwe1038 26 күн бұрын
Kulandira ndalama
@CharlesMaloya
@CharlesMaloya 26 күн бұрын
Adadya chimbanzi
@user-zs7yq3tj7n
@user-zs7yq3tj7n 26 күн бұрын
Asiya chilungamo asogoza ndalama.
@patrickndojime1632
@patrickndojime1632 26 күн бұрын
Koma aPrasident opuma ananenatu kuti Doom sumafayira mkamwatu ndizitu pano tubwelera ku ulamuliro wa chipani chimodzi
@user-gm3cx2xn9o
@user-gm3cx2xn9o 23 күн бұрын
Anthu akamatenthedwa zolankhula zake zimakhala ngati zingatheke 😂😂😂😂 mulira simunati
@user-je6wk8ew6g
@user-je6wk8ew6g 26 күн бұрын
Moti chikangawa yalusa sikugawanso masweet 🤣🤣🤣🤣 atimaliza
@MuhammadBAKILI-kl2mj
@MuhammadBAKILI-kl2mj 26 күн бұрын
My bsst ladio station limpopo
@user-bh2ei4os8w
@user-bh2ei4os8w 26 күн бұрын
Iyiyi ndiye akufuna Kenya Kenya tsopano 🏹🏹🏹
MOSES KUNKUYU MUTU SUKUKOKA UKU KWANUNKHA UTSI
40:43
LIKI-LIKI TELEVISION
Рет қаралды 9 М.
Amazing weight loss transformation !! 😱😱
00:24
Tibo InShape
Рет қаралды 68 МЛН
A little girl was shy at her first ballet lesson #shorts
00:35
Fabiosa Animated
Рет қаралды 18 МЛН
MISS CIRCLE STUDENTS BULLY ME!
00:12
Andreas Eskander
Рет қаралды 21 МЛН
FULL INTERVIEW: Donald Trump takes questions from NABJ panel
35:47
ABC News
Рет қаралды 1,2 МЛН
FULL SPEECH: Donald Trump speaks before the NABJ in Chicago
36:28
FOX 32 Chicago
Рет қаралды 402 М.
MALAWI COURT.... TAMVANI IZI ABALE 🤔
20:45
Jimmy
Рет қаралды 63 М.
Amalawi ndi mbuli, asiye kudzudzula Chakwera;
7:24
Bakili Muluzi TV
Рет қаралды 64 М.