Akubanja nkhani musayisiye chomcho apolice azolowela kudya ziphuphu akuma tulutsa zigewenga chifukwa cha ndlama funani lawyer basi
@SuwemaHafizaayami-gy2hnАй бұрын
Sorry for the loss mama zosakhala bwino koma abale dzikoli iiiiii😢😢😢
@morgansilungweАй бұрын
pakuchitika zachinyengo mama.kasumeni kuma bungwe ndi ma lawyer aboma aja akuthandizeni.dziko lathu linawola koopsa maka kwa anthu osauka
@user-ks3uw3pq7d2 ай бұрын
Ndawona kwa thu after long time
@user-uf4db7im7dАй бұрын
Kayiperekeni nkhani ku mabungwe osachedwa apa ayi
@APOSTLEBJ-tc5fp2 ай бұрын
Malawi police God will punish you and judge you harshly.
@damianokachingwe35312 ай бұрын
Akubanja pepan kwambr km limban mtima muitane a police ku headquarters ku area 30 Lilongwe akuthandizen nawonso akalephera pitan ku court direct.Musalole wa police kukupusitsani mu njira iliyonse .
@HenryGulani-fq5js2 ай бұрын
Kom Ku Malawi kwachuluka katangale ine ndili Joz ndichitapo Kathu ndikuimbilani chimene chikufunika kungomuona wamodziyo ndi kumutema Tema batsi
@RoyNamwiliАй бұрын
Police ya 2020 mpaka pano ziphuphu zokhazokha. A khoti atulutsa bwanji chigawenga mu ceil ya police before hearing? Mupite Kwa ma lawyer aboma muthandizidwe.