NTHAWI YA UMBULI KUIMBIRA MFITI MMANJA SH.ABOU SUFIAN KHATWEEB DAWOOD

  Рет қаралды 1,652

Qassim cedrick

Qassim cedrick

Ай бұрын

Пікірлер: 15
@UseniMailosi
@UseniMailosi 23 күн бұрын
Ameen inshaah Allah
@Musa-cz1nm
@Musa-cz1nm 22 күн бұрын
Ma shaallah ma shaallah ma shaallah
@MariamJaffali
@MariamJaffali 21 күн бұрын
Naam sheikh ma shaa Allah ndipo anthu amaopa kukhala kuqibula Allah awakhululukire zofooka zawo
@user-gk6bf7xe9g
@user-gk6bf7xe9g 23 күн бұрын
❤❤❤❤
@user-lf5qw7mk3h
@user-lf5qw7mk3h 13 күн бұрын
Km this kind of lecturing sometimes zumandikhuxa bwanj Mmalo moti muzapephelera amzanu chikhululuko bas muli busy achibekete Panopat kumalawik kuli zambil zoti kalel sizimachitikai inuo ophuziran muthawi yanu samasephan pakhan ya eid km lero ikangofik mumangotukwanizana apa Be humble muziwapephera amzanu chikhululuk jaman kozan zomwe zilipoz pano a a jaman
@user-rl5zq1qr4d
@user-rl5zq1qr4d 18 күн бұрын
Ulaliki wabwino ndithu koma kuchula mbiri ya munthu omwalira kuti anali wa shirik its very unfortunate mukanangokhonza zimene inu munaziwona kuti ndizolakwika in directily not directily nkutheka ena analowa chisalam kuchokera kuzimene iye amapangazo inde tiwalemekeze ndi amene anasunga deen inu ozindikiranu musanabwere choncho tiyeni tiwapemphere chikhululuko osati kuwapepusa MAY ALLAH SHOWERS US ALL WITH BLESSINGS FOR BEING MUSLIMS
@MoneyTiririMgwagwa
@MoneyTiririMgwagwa 18 күн бұрын
Zoonadi kuzuzula kwa bwino
@IsmaelBilal-lh1pi
@IsmaelBilal-lh1pi 23 күн бұрын
Tiyeni tiwapangile ma duwah mwina kutheka amaizichita mu umbuli. Allah awakululukire chifukwa anatisungira Deen
@Qassimcedrick
@Qassimcedrick 21 күн бұрын
Amee
@MoneyTiririMgwagwa
@MoneyTiririMgwagwa 18 күн бұрын
Munakakamba zoonadi koma osatchula muthu ngat inu mwazindikila muchoonadi munakalalikila pazomwe inu mwazindikila ndi mene mwaphuzilila
@AdamYas-ec9oc
@AdamYas-ec9oc 5 күн бұрын
Uyu sadayange mafuso amene ana fusidwa komaso tingopemba allah kuti abwelere kudarassa chifukwa hukum ya deen mutu mwawu mulibe
@JohnAsendi
@JohnAsendi 22 күн бұрын
Koma amwene ndi makusati mukulankhulana kwanu kwaonesa kuti wabwera kuzalimbana ndi anthu omwe anaphunzira kale kodi tizinena kuti muli PA chiwongoko ndiinu choti muziwe ndi chakuti dini ndi ntchito sizingagwilizane mupite Kwame e mukuwanyozawo samalandila ndalama kutha kwamwezi pomwe Ena inu mumalandila ndiye kumati uza zabwino zomwe akuchita ungokhala zonse ndizolakwika alibe zabwino zomwe akuchita
@Qassimcedrick
@Qassimcedrick 21 күн бұрын
Sheikh kodi mitiuza mu Quran pomwe aletsa kulandira ndalama ukagwira ntchito ya Deen pakati panu ndi ife pali Quran ndi MA hadith atumiki basi palibe zokangana
@JohnAsendi
@JohnAsendi 21 күн бұрын
@@Qassimcedrick mumalandila ndiinu ingo ndiuzani lembalo mu qraan
@JohnAsendi
@JohnAsendi 21 күн бұрын
@@Qassimcedrick mumalandila ndiinu ingo ndi uza lemba mu quraan
EP 2 KODI SINAKWANE NTHAWI
14:20
SHEIKH ABOU SUFIAN KHATWEEBU DAWOOD
Рет қаралды 1,7 М.
No empty
00:35
Mamasoboliha
Рет қаралды 9 МЛН
Summer shower by Secret Vlog
00:17
Secret Vlog
Рет қаралды 13 МЛН
Kuganiza Mwangwiro - Kuvomereza Ukalamba
27:23
Sheikh Mustahab Ayami
Рет қаралды 1,6 М.
ABANTU ABAAKOLIMIRWA MU QURAN NE MU HADITH -  SHEIK NUMAN MUHAMMAD MBOGO
58:17
Sheikh Numan Muhammad Mbogo
Рет қаралды 619
KUWACHEPETSA MACHIMO OMWE ALLAH ANAWAKUZA  SH ABOU SUFIAN KHATWEEB DAWOOD
36:36
SHEIKH ABOU SUFIAN KHATWEEBU DAWOOD
Рет қаралды 5 М.
PEWANI KUWADA ABWENZI A ALLAH SHEIKH ABOU SUFIAN KHATWEEB DAWOOD
11:59
KHALAN CHETE MMENEMO
25:51
SHEIKH ABOU SUFIAN KHATWEEBU DAWOOD
Рет қаралды 4,8 М.