Omwalira apezeka wa moyo

  Рет қаралды 70,199

Malawi Lovers 🇲🇼

Malawi Lovers 🇲🇼

11 ай бұрын

Пікірлер: 68
@SaidShop-nf3qu
@SaidShop-nf3qu 3 ай бұрын
Abare Kodi busayo ndingapeze bwanji abare ndiarogo mwaambuye chonde ndithandizeni
@user-eu9xe6wl8b
@user-eu9xe6wl8b 9 ай бұрын
Great work prophet❤🎉
@user-yy6rj5lc4i
@user-yy6rj5lc4i 11 ай бұрын
Pano zithu sizili bwino ndimakhala ndikuva nkhani zimenezi kwambiri chomwe chimandipasa kulimba mtima kuti ndizoona ndithu ndipo satana akugwilisa ntchito anthu oipa mtima awa kumaononga miyoyo ya anthu kumalimisa muminda.Ambuye atichitire chifundo kwambiri
@IvvyMakuluni
@IvvyMakuluni 11 ай бұрын
Mpimpimpi!!!!!mwabisapo chani a Zulanga....mesa mufuna anthu tidzidziwa chilungamo 😅😅😂
@user-lc7ji1gn9w
@user-lc7ji1gn9w 10 ай бұрын
😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂 kma ndaseka
@nimrodkapingatheu5475
@nimrodkapingatheu5475 25 күн бұрын
Anthu awawa anazonzedwa ndi ukulu wa Mulungu.. si azibusa ongofuna kunjoya mmacarpet wa....
@tonyteixeira2463
@tonyteixeira2463 17 күн бұрын
Tolo Thoko😅
@hawabanda-xs5fx
@hawabanda-xs5fx 10 ай бұрын
Anakakhala azibusa ena bwezi Ali pa screen mulungu apitilize kuwakhuza abusa in Jesus Christ
@user-lz1ry1sm4j
@user-lz1ry1sm4j 8 ай бұрын
Too bad. The name of the Lord is a strong tower
@BdhfbHdhe-pd7nh
@BdhfbHdhe-pd7nh 11 ай бұрын
Ukulu wa Mulungu tauona
@Felix-ln4ql
@Felix-ln4ql 14 күн бұрын
Koma padziko pano pakuchitika zinthu eeh ndagoma
@MadalitsoHope
@MadalitsoHope 9 ай бұрын
Zamphavu 🙏👏 prophet
@collinstrevor
@collinstrevor 11 ай бұрын
Ukulu wambuye uwonekere afiti ayaluke sambitu kumampha makolo anzawo
@richsambakusi424
@richsambakusi424 10 ай бұрын
Azibusa ngat awa mulungu azipitiliza kuwadalisa
@rachealphiri3416
@rachealphiri3416 10 ай бұрын
It happened in Zambia twice
@ephraimphiri5789
@ephraimphiri5789 10 ай бұрын
Nope, it's happened in Zambia more than seven times 'just on TV' about 5-7 years ago...and many more times in the rural areas...
@esthermakwinja3207
@esthermakwinja3207 10 ай бұрын
Ambuye akantheni afiti on se dziko lilongosoke
@CatherineDesire
@CatherineDesire 29 күн бұрын
Ndingampedzeko bwanji mbusa amenei?
@MussaIbla
@MussaIbla 11 ай бұрын
Eish zovesa chisoni kwambiri
@JohnChibalo-wf8gr
@JohnChibalo-wf8gr 11 ай бұрын
Adzibale anga.nsanje to chitipa kwainu nonse mukumapanga masalamusi amenewa kodi mumafuna kuti mupedze chani ? Kodi umakhala umphawi ? kapena kukhwima ? Tiyeni tiyike chikhulupiliro chathu pa mulungu tiyeni tigwire ntchito ndikumapempha kwa mulungu zomwe tikufuna koma tisamafike mpaka pomapha nzanthu muchifukwa chofuna kukhupuka kodi zimenezi kwainu mwapanga idzi zikanakhala kuti mwachitidwa inu kapena mwana wanu mukanamva bwanji ? Nchitidwe uwu utheretu kumalawi inu mukupha anzanu inuyo ndiye mudzapita kuti ? 😂😂😂😂
@josephnanyanga2012
@josephnanyanga2012 8 ай бұрын
koma akutipweteka anthu wokupha azawowo because amatitengera anthu wotitimawadalira andipaseko namba prophet please
@user-zc9ku5fw4n
@user-zc9ku5fw4n 5 ай бұрын
Ndipo ineyo ndipemphero Langa Kwa onse akupanga nchiiiitidwe opha anzawou adzafe mozinzika.ndili munyengo zomwezi nane Ambuye andochitire chifundo Mwana wanga azauke,🙏
@user-lc7ji1gn9w
@user-lc7ji1gn9w 10 ай бұрын
Nde mabeluwo kut zinveke bwanji ukubisa chani aaaaa kangaude watani kod😮
@adamusaidih8570
@adamusaidih8570 11 ай бұрын
Kkkkkkkkk km ku Malawi gyz kuli ufuti
@chimwemwemaquesuwell5841
@chimwemwemaquesuwell5841 10 ай бұрын
Choonde tipatseniko nambala yá openphererawo
@user-rv8gi4ro6r
@user-rv8gi4ro6r 11 ай бұрын
Nkhani ndi yakuti mulungu wakwiya
@oswardmwale216
@oswardmwale216 9 ай бұрын
Aaaa bwanji simunafukule kumaliza mpaka kupeza bokosi kuti muone ngati mafupa alipo
@mordecaikachale2497
@mordecaikachale2497 11 ай бұрын
Abel siyani kuliza ma bell 🔔 kubisa mawu ena Pano ndinyengo zoti zibisika za anthu tiziziwa basi
@JosophineSolobala-hp5ds
@JosophineSolobala-hp5ds 4 ай бұрын
So sad alot of our relatives akugwilitsidwa ukapolo somewhere ife kumat anamwalila😢😢
@dondamissonchdziwe3958
@dondamissonchdziwe3958 11 ай бұрын
Ndi zoona wanthu ambiri sakufa akuma phedwa ndi asatanic m'modzi wa iwo ndi INE inenso ndinaphedwa koma ndina zuka koma munali mu 2015 moti m'mene ndina zukira kunyumba kwa achibale ku Malawiko sindinabwere ndikuopa Kuti mwina achibale sangandirandire koma panopa ndiri ndi Wana awiri chidzukire ineyo ambuye yesu akandithandiza ndizafika kunyumba chifukwa ndina chosedwa kumeneko ndi Wanthu wena awiri woyera mpakana pano wa nthu anandi chosa kumeneko amabwera mpakana pano ndimacheza nawo dziko Lino lapansi likudabwisa kwambiri pempherani kwambiri ambuye yesu afika nthawi iriyonse nanga m'mene ndiriri ine munga ndiziwe kuti ndine odzuka panopa ndiri ku Mozambique malire ndi zimbabwe kunyumba ndiku Mulanje kwa nkanda ku kambenje
@peterbakuwo1249
@peterbakuwo1249 11 ай бұрын
🙆🙆🙆🙆
@adamusaidih8570
@adamusaidih8570 11 ай бұрын
Kkkkkkkkk km ase srias wava kkkkkk
@oliviaolivia4979
@oliviaolivia4979 11 ай бұрын
Koma ambuye akuchitole. Chifundo mupite kwanu akakulandila
@mbawabuliyan9704
@mbawabuliyan9704 11 ай бұрын
Akulu inu bwanji Nkhani yanuyo ndiyoopsa kwambiri osabwela poyela nayo bwanji
@florencebonga3211
@florencebonga3211 10 ай бұрын
Ambuye alandile ulemu 🙏
@liki-likiladies---lilongwe6963
@liki-likiladies---lilongwe6963 11 ай бұрын
Divine postmortem
@BlessingsBanda-qn7xr
@BlessingsBanda-qn7xr 11 ай бұрын
Koma anthu ndinu otamba Ana anjoka koma mulungu adzaweruza . Jehovah inu inu ndinu choonadi ndi moyo kazitikhululukirani machimo athu
@CatherineDesire
@CatherineDesire 29 күн бұрын
Amenewa NDE adzibusa a Mlungu not a "can I prophecy!)a busa a receive receive,ma agent a satanic ulaliki ukhare wa ndrama otsati wachipulumutso?
@CostaCasimiro
@CostaCasimiro 7 ай бұрын
Blassa semanal agovati ndi agedo
@user-dt8nr1zx6e
@user-dt8nr1zx6e 11 ай бұрын
Taona nawo zikomo
@AmusedSakura-dx1nw
@AmusedSakura-dx1nw 6 ай бұрын
Lord have mercy
@BaxterChipofya
@BaxterChipofya Ай бұрын
Akafukule manda akapange check ngati mafupa palibed
@KINGMANMAKALA-hb9gs
@KINGMANMAKALA-hb9gs 11 ай бұрын
😂😂😂😂
@JusticeMakwinja
@JusticeMakwinja 3 ай бұрын
Tikufuna busayo ndithu
@ChisomoKapanda-jg2uf
@ChisomoKapanda-jg2uf 10 ай бұрын
Ati amangonda ngati edzi kulankhula kwabwanji uku
@BdhfbHdhe-pd7nh
@BdhfbHdhe-pd7nh 11 ай бұрын
Abelo ukutiona kupusa
@user-zk5nu5fh6l
@user-zk5nu5fh6l 10 ай бұрын
Izi ndi zowona ndinaziwonapo ndi maso anga
@BaxterChipofya
@BaxterChipofya Ай бұрын
Asakhale anyamata okhwima awa akanafukula mpaka pansi to prove that A = B
@josephnanyanga2012
@josephnanyanga2012 8 ай бұрын
ndikupephako namba ya pulofetiyo ndikupepha
@YusufMolesi-vr4pn
@YusufMolesi-vr4pn 10 ай бұрын
Hy
@user-ek7vg7ld8h
@user-ek7vg7ld8h 9 ай бұрын
chifukwa chan anthu akungozuka ku Malawi kokha?
@AleksaWilliams-qc6cn
@AleksaWilliams-qc6cn 10 ай бұрын
Shame😢
@mcsellahntv6896
@mcsellahntv6896 10 ай бұрын
Ndiye wina amvekele ufiti kulibe. Ur mad.
@user-ux8qz1tg7l
@user-ux8qz1tg7l 10 ай бұрын
Number ya abelo pls pls ol ya abusa
@SaidShop-nf3qu
@SaidShop-nf3qu 3 ай бұрын
Gati mwaipeza number chonde tigawireni number yabusawo
@hawabanda-xs5fx
@hawabanda-xs5fx 10 ай бұрын
Abusa achilungamo achochi akusowa tikungolimbana ndi ama jecket mtwn
@rooseveltmtemula2643
@rooseveltmtemula2643 9 ай бұрын
😂😂 Paja timafera ma jekete... Koma awawa voice yawo ikuchita kumveka kuti ndi a prophet di
@patriciacraiton-sf5vu
@patriciacraiton-sf5vu 8 ай бұрын
😂😂😂😂
@AriohChauluka-lm9oo
@AriohChauluka-lm9oo 10 ай бұрын
M
@mbawabuliyan9704
@mbawabuliyan9704 11 ай бұрын
Family imeneyi kuli Anthu ochepa pakufunika afufuze bwino kwambiri munthu akupanga zimenezo aziwike
@patrickjaenda8288
@patrickjaenda8288 11 ай бұрын
Zomvesa chisoni kwambili
@user-fq3jz4hl4c
@user-fq3jz4hl4c 10 ай бұрын
Chonde chonde ine kwathu ku Mangochi ndikufuna phone number ya abusa wo please ndili ndi mavutho nso ine yo
@rooseveltmtemula2643
@rooseveltmtemula2643 9 ай бұрын
Ineso ndikuifuna ngati munaipeza please share
@marthacassam
@marthacassam 10 ай бұрын
Zaulendo uno tiona zithu
Kangawude Amuna folo
26:38
Malawi Lovers 🇲🇼
Рет қаралды 49 М.
A Michael Usi Inu Si A UTM - Lyton Mangochi
23:13
Nyasa VoiceBox
Рет қаралды 3,3 М.
Looks realistic #tiktok
00:22
Анастасия Тарасова
Рет қаралды 106 МЛН
ZIKUCHITIKA - Anthu Awiri omwe anamwalira zaka zapitazo apezeka mu mb'oma la Balaka
51:27
Continu.. Part 2
37:28
Malawi Lovers 🇲🇼
Рет қаралды 140 М.
Mbewe Steve ulaliki Manondo
9:25
Zion City Malawi Channel 2
Рет қаралды 44 М.
Mwa Atupele Muli Utsogoleri - Concerned Citizen
24:16
Nyasa VoiceBox
Рет қаралды 328
Gwanda's Funeral - Last Sermon
25:21
Edson Gunsalu
Рет қаралды 153 М.
CRUISE 5 WITH BLACK MISSIONARIES
1:05:27
Joab Frank Chakhaza
Рет қаралды 78 М.
kangaude
33:06
Malawi Lovers 🇲🇼
Рет қаралды 16 М.
AMENYEDWA NDI MBAMA YACHIKWANJE KUMALO OBISIKA ndipo zadzetsa ulumari kumaloko.
46:18
ma banja awiri aphedwa ndi anthu olusa powaganizira kuti ndinfiti ku tsangano ndi Angonia .
12:49