he seem to be a good and experienced leader. alibe mbiri yakuba
@user-du9qs4tb6u2 ай бұрын
I love ❤❤ Dr chilupha chakwela ndiosakwanila Pau president zoona
@user-ql3of8rf4z2 ай бұрын
Azathu olilanu 😂
@user-oc6xd4tv9l2 ай бұрын
Following 🎉
@Harlod55662 ай бұрын
Uyu nzeru zirimo ndithu. Ndipo alibe nkhwidzi ndi munthu koma Chilungamo chokhachokha. Sungalamulire bwino opanda experience (UKADAULO) Walongosolanso bwino za chisankho ndi zina zambiri. Wa nzeru akuvomereza.Bingu anamumanga komaonani akuyamikira ng'ono wake Peter Muthalika. 🙄🙄🙄🙄🙄🙄🙄🙄🙄🤔🤔🤔🤔🤔🤔🤔❤️👍
@AustinChikaoneka-ow2rv2 ай бұрын
Come on Kaka Chilumpha you are the Leader.
@PreciousChizonga2 ай бұрын
I support your opinion Koma zoti pali Bola mwawiliwa ndiye kwaine ai Peter kulekerera zinthu two much ngati chakwera yemweyunso ndiye sindikusiyanitsa ndianthu okhutitsa mimba zao kuiwara udindo .
@user-gf6eh9ms5i2 ай бұрын
Dam truth DR Chilupha i love this
@Jermah51kennias2 ай бұрын
Apayu Legend nde mwayankhula momveka bwino okumva wamva
@ibrahimalfred65392 ай бұрын
Thokozani chiwaya you're doing the best man kept up this what we want to here man
Ali ndi mlandu wanji ndipo zopusa ndiziti galu iwe
@PreciousTepatepa2 ай бұрын
Very Genius
@HopeKhembo-qe7qs2 ай бұрын
💯% even a tac shop they need experience people what more a country
@dorcasmwale63282 ай бұрын
I agree
@zumuweasly47732 ай бұрын
The guy is retiring so fast....
@user-gj4li2gc8o2 ай бұрын
Nde a chilumpha mene mwakalambilamo mungakhaleso sogoleli ayi ndithu
@roxtonmbawa80122 ай бұрын
Majority rules , chakwera was chosen by majority ife titani nanga, cassim chilumpha adamangidwa ndi Dpp he must wait dpp to come back
@user-nf3ik3ff6y2 ай бұрын
Peter is good chakwela Achoke
@samuelsergio53432 ай бұрын
❤
@ChristopherMasangano2 ай бұрын
Following
@andymasingajunior2 ай бұрын
A Chilumpha adziwe kuti Democracy is very expensive, 2025 tivotanso katatu, ndipo mavoti achiwiriwo tidzapanga nthawi ya mvula.
@LawgiverSolomonАй бұрын
Ndipo palibe adzafike 50+1
@user-nn5fz5wj6n2 ай бұрын
❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤
@SupiaSamson-wb5ct2 ай бұрын
Wanena chilungamo cassim
@user-du9qs4tb6u2 ай бұрын
Kkkkkk koma kumeneko Panali pakamwa chabe 😂😂😂 koma chilupha auzeni
@timothymhone23402 ай бұрын
Kkkķk komaso
@user-hq6dq7zr1e2 ай бұрын
Ulemu wanu bwana Chilumpha
@user-pv9uk6sc3w2 ай бұрын
Tiyamike Thokozani Chiwaya chifukwa ukuyesetsa kulondola aliyense, ndipo ukukwana Thoko. A Mr. Chilumpha ali ndi mtima okonza Malawi mosakaika, koma akhwima, koma akunena zoona.
@user-xb4fo7tk6b2 ай бұрын
Thank you so much bwana, it really means a lot to me
@ElizabethMajiga2 ай бұрын
Chilungamo chabwanji ichii❤❤❤❤❤❤❤
@FatimaUmali-pc8sy2 ай бұрын
Uyu ndi munthu wa bwino Allah akudalitse mene mwayakhulilamu ndi zosowa kuyakhula chulungamo mwa uamikilaso Peter bingu pazomwe anachita pa Malawi
Akuti ine sindimagwila ku chipiku km cassim chilupha
@Boijeezymakan2 ай бұрын
Ndipo live
@user-co3wr3rn4h2 ай бұрын
Wayankhulatu chilungamo
@OmarManjawira-ex1yc2 ай бұрын
Gogo Cassim Chilupha concerd with this government,,,, from Chipiku to President 😂
@user-ee6be5kl5o2 ай бұрын
Munthu you akuyankhula za nzeru ndithu ulemu wanu kuyankhula kuposa pulezidenti chakwera
@goodvisionmedia20232 ай бұрын
Mr kulakhula momveka kwambiri
@LuciasZepete2 ай бұрын
Chakwera alibe nzeru ataaaa
@HopeKhembo-qe7qs2 ай бұрын
A MEC mukamalandila za anthu oimilila like MP and presedent please ask for experience please
@ChrisEnos-to5uv2 ай бұрын
Achilupha mukunena chilungamo
@KinosiKameta-ud1ps2 ай бұрын
Chilugamo nchowawa
@user-pv9uk6sc3w2 ай бұрын
Mr. Chilumpha mukusongosola chilungamo, Chakwera ndi chilima sadakonzeke komanso ni mbuli pa kuyendetsa Boma. Chakwera amapusha Wilber lomaso crerik ku Chipiku basi. Sadziwa chilichonse za boma.
@Dorah-zl9uf2 ай бұрын
😂😂😂
@peterchikwakwa84762 ай бұрын
It's true what chilumpha is saying, malawi we made a mistake
Osangopita kwa apule ndikukaunikila Pomwe akulephelapo bwanji
@ziyamporoma3772 ай бұрын
Uyu ukalamba wamufikadi mmafupa ndithu. Zoti Chakwera was leader of opposition sakudzika? Ku america akukutchulako did Trump hold a public office before the presidency?
@user-fd1tu6ku1r2 ай бұрын
Chakwera ndi Tambala Party ndi Anthu opanda Phindu
@user-ju7vc1uv7m2 ай бұрын
Atupele muluzi an akambapo kale
@odarm43342 ай бұрын
Akuti "sindimagwira ku Chipiku iyai" 😂😂😂😂
@frezarphiri34802 ай бұрын
😂😂😂😂😂 sanamangeko ndi toilet yomwe ku assembles 😂😂
@FrankBaison2 ай бұрын
Zoonadi chakwera sakukwanila kukhala president
@HopeKhembo-qe7qs2 ай бұрын
Vuto laku Malawi oimba Ati akhale MP.azisudzo MP
@jonathanNkhata-nl2de2 ай бұрын
Akut simagwira kuchipiku
@user-se8ze3fn3o2 ай бұрын
Chipiku boy 😅
@TrinityManeya2 ай бұрын
Zamzeru kwambili
@pierrekhabwiri38412 ай бұрын
Vuto lathu nd lot anafe sitimamvera sitimamvera akuluakulu kuteroko or apapa tikimva ngat mukut chakwera nd wabwino koma mmmmmhhhh mwa inuyo bwana muli mzeru koma ife omverafe mmmm
@user-gj4li2gc8o2 ай бұрын
Nkhalamba iwe unakhala 10 years unakwanisapo chani pa u vice president
@ChiyembekezoPhiri-sv8nw2 ай бұрын
Kkkkk so you can compare Malawi with USA mwaganiza bwanji kaka! Mwakalamba ingopumani akazi Anu Ali bwanji