We need to know that mulungu akamayankhula ndiye kuti akutikonda. Olo mu bible atsogoleri amalangizidwa ndi ma prophet.izi sizachilendo..komanso ma prophet omwe ayitanidwa kulakira the pure gospel of God alipo..uyu calling yake is to give counsell to the goverment. Zinthuzi zimafunika kuzimvetsa..Liabunya sakunama.
@user-dd5kb4iv3z6 ай бұрын
Mtima wanjiru, munthu wa Mulungu mabodza,mwana wa satana iwe, a professor timakonda ndife, pita ukalalikire anthu akumidima
@GraceLimani-zw7dx27 күн бұрын
Munali so kwa chakwera pompano aprophet
@GodfreyjcBinguh4 күн бұрын
Chitsiru Ichi sadziwa pano Kuti mulungu akulilira Moyo wakoyo fiti iwe .do you knew Kuti nthawi yatha pompano okudzayo akudza.mulungu akusithe chifukwa yemwe ndimudziwa akuva chisoni ndi dziko
@tisuhmakhwah70855 ай бұрын
Ubwino wake opemphelanu takuonani zochita zanu nde sitingamvela zakozo..iwe si Mulungu.. Auze anthu za ufumu wa Mulungu ..lalikilani kut anthu tilape pliz..mukupangazi ndi gospel ya ntundu wina..kukuyang'ana mmaso mwakomo I 've lead your mind..
@sylessmaduka46616 күн бұрын
Munapereka chitsanzo cha Sauli ndi David. Nde munazatinso 2019 Peter atawina inu munkauzabe anthu kuti Chakwera ndi amene anawina mpakana 2020 zinaonekadi poti Mulungu mau ake sapita pachabe. Now tikaona za David sanakakamize ayi, sankamemeza anthu kuchita chipolowe mpakana nkutenga ufumu, ndi Sauli amene ankalimbana ndi David koma David sankabwenzera pomwe zinazi ndibwino musafananize chifukwa zinali zokakamiza. Komanso Mulungu kunena zoona mene zinthu zikuchitikira ku Malawi kuno olo munthu oti sawerenga mau a Mulungu sangavomereze kuti Mulungu anatisankhira mtsogoleri. Kodi zikuchitika ku Malawi kuno ndi mdalitso kapena thembelero? Izizi kupanda kusamala mayiko ena atengera chitsanzo pa Malawi kuti Mulungu siomuseweretsa.
@user-zm4vy5rs4v5 ай бұрын
Ndizowona munthu si pitalayekhayu anzake achitepo
@user-si7po9sd5i6 ай бұрын
Akunama uyu
@johnkumbanga33696 ай бұрын
What are you trying to say mr prophet?
@user-qv4ko6ps4j5 ай бұрын
Ukayang'anatu ndi diso la uzimu zimu koma uli mwana wa njoka,,,,,,,,,alosi onyenga inu mmodzi wa Satanism iwe mmmmmmmmmmmmm ngati mwadya ndalama za uyo mukumuti ndi ofatsayo nonse ana anjoka,,,,,,,,,,,,,,,ofatsa wake tsiluyo!
@user-qq3ip1od6i5 ай бұрын
Wabodza iwe,, busy wit politics rather than kulalikila uthenga wabwino,, busy kuchita predict zoipa za moyo Wa wina
@samsonhavenoyayshonga26096 ай бұрын
What he saying is not from God,he trie to be a politician
@NevesonChirwa-tt5eg6 ай бұрын
Iwe prophet iwe ndiwe wa chamba kwambiri wamva?osangojoina ndale bwanji?Anzako a Mbewe adayambaso choncho koma pano si awo anayambitsa chipani.
@MisheckChapomba-lr8kz6 ай бұрын
Akunenazo ndi zoona Koma osati zachokela Kwa Mulungu ayi God has nothing to do with this satanic parties
@MuhammadSamson-yz1kl5 ай бұрын
Kkkkkkkk forsake kagwere uko iwe wasuta chamba
@user-pt2ok1kr1o6 ай бұрын
Zachikunja izi auzeni anthu za yesu.
@user-ti2ct8ts8d6 ай бұрын
Just start politics Mr prophet than Malo mumatiuza mawu a mulungu.
@EllenLuwanika-tl5ck2 ай бұрын
Man of God stimuli kumalawi eti anthu akuvutika kuno