God is with Malawians and not with MCP which so called bloody party.
@kennedybandaСағат бұрын
You are doing business in the name of prophet. Stop telling false prophecies.
@HalisonSolomonСағат бұрын
AAAAAAAAA MA PROPHET AKE SI AZAKAZINOWA , MA PROPHET ANALI KALE ACHINA YOHANE, DANIEL KUNGOTCHULA OCHEPA, ANTHU AMENE AMAIMA PA CHOONADI. OSATI AWA OMETA MBALIWA CHONSECHO MALAMULO A MULUNGU AKUWADXIWA , MUKAKHUTA ZAKUMIDIMA KWANUKO MIZINAMIZA A MALAWI,. MUKULANDILAKUMENE MUNTHU WA MULUNGU SAPANGA ZANDALE, IYAAAAAAA ZA U SATANIKI BASI, NDIPO NDIWE MODZI AMENE UKUTENGERA ANTHU KU CHIONONGEKO , YOU SAID PEOPLE HAVE TO TRUST YOU LIKE WHO? INSTEAD TO TRUST IN GOD, FALLS PROPHET.
I am very disappointed in you,i have been following you all along,koma I have now realized that I have been following a very wrong person,God almighty should forgive you.
@HalisonSolomon3 сағат бұрын
IWETU USANAMIZE WANTHU IWEYO UMACHEZA NDI MULUNGU NGATI NDIWE NDANI ? ANAKANIKA MOSE KUCHEZA NDI MUKUNGU IWE NDI NDANI, SAMALANI NDINU AMENE MUKUNYOZETSA DZINA LA MULUNGU CHIFUKWA MUKUBISALIRA MDXINA LA MULUNGU MULI ASATANA, PALIBE CHINGAKUTHANDIZEN. KOMANSO USIYE KUGWIRITSA NTCHITO MAU OTI UMACHEZA NDI MULUNGU,SUNGA CHEZE NDI MULUNGU IWE ANAKANIKA YOSWA WHO IS YOU?
@BlessingsTembenu3 сағат бұрын
Mutu wanu sugwila ntchito bwino akulu,mwadya ndalama zingati? Zikusonyeza kuti infa ya achilima inakusangalatsani eti.musiye kuseweretsa mulungu coz God will punish you
@user-go5xy3cf1r3 сағат бұрын
Yankhulani anthu onse afika nenani munthu wa mulungu
@timothymacheka3 сағат бұрын
Munanena kuti chilima adzakhala president??
@user-ie4ci3zh7j3 сағат бұрын
Uuuuuuuuuu chokani apa mulibeso dzeru
@user-nr2bi5zm9f3 сағат бұрын
Iwe chitsiru kwambr , wasatanic iwe
@GeoffreyNyasulu3 сағат бұрын
Kucheza ndi Mulungu??? 😢. Kumbukilani Mneneri Elijah ndi Ahab pa phiri la Caramel.
@hendrixmwangata34523 сағат бұрын
Ukufuna kumubera chakwerayo sangawine
@JohnEzelohMagawa-fl8sw4 сағат бұрын
I can see that you are nothing but a full
@user-qq3ip1od6i4 сағат бұрын
We just lost a true statesman vp,, people are not happy wit Chakwela leaders. If you're true to your calling advice to step aside