Kodi uyu ndi bambo wandani uyu 🙌🙌 no wonder soap wina amangokula alibedi thovu ndaonela👆
@user-is5dl7np9g2 ай бұрын
Mwangokula madala Koma mzeru Zanu sizikusiyana ndi Za mbuzi, malawi mmene ikumvetsela cisoni panomu inu mungamalankhule mwauchitsiru chomcho??? Kuchikwawa!!!!
@user-hm9nc7lz6e2 ай бұрын
Madala ndinu achisiru kwabasi ndipo mulibe nzeru kukamwa kotambalalako 100 years adzidzalamula ana ako osati amalawi ea ife
@user-pv9uk6sc3w2 ай бұрын
Pamtumbo pa bambo uyu, tatopa ndi zimenezi, agalu achabe chabe. Anthu akuba awa, umoyo wa anthu pa ground sulibwino. Kwavuta ku Malawi sizinachitikenso ku Malawi, chitsilu ichi.
Mbava za a MCP izi choncho dziko lingatukuke ,Malawi ali moto ngati Boma ili litapitilira ndipo dziko pa Malawi padzakhala umphawi wananu kobasi
@hambalisaeedphiri2 ай бұрын
Munthu amatero poyankhula akasuta chamba ,mdziko muno muli njala ndi zimene akuganiza apa si misala imeneyo
@user-qp9bn5ed5n2 ай бұрын
Mwaredzera kachaso chani galimoto zachani mmalo momagura chimanga nkumasunga galunso iwe eti nyani
@khalifajalih19602 ай бұрын
Kod mchikumbeyu fodya wake wagulisa?
@GraceLimani-zw7dx2 ай бұрын
Ndiye akufuna kugwira ntchito kwanuko ndani zopusa eeeee mwawelengera kale ndalama zopeza pa mwezi kkkkkk
@FelixLivison-eg2hf2 ай бұрын
Zonsezi ndi nkhani yakulephela basi
@YusufuKaifa-fr4wt2 ай бұрын
4yers mwapanga palibe mwedzi yokha ndiyo yatsala mungapange zithu zochuluka choncho kkkkkkkkkk ndakayika bodza ili leni leni anthu akufa malawi muno ndi mavuto Akusangalala ndi omwe ali ku boma wo basi ndifukwa chake alindi phavu yoyakhura chonchi akhuta khuta uko ndi kuma phwetsera pa TV is nothing this is funny seriously
Iwedi ndi olimbantimadi mbuzi ya munthu anthu akufa ndi njala iwe ukufuna kugulila ma quantum a mcp machende ako
@user-yg9rs7tp2x2 ай бұрын
galu ameneyu ndiye ndani?
@Spaw-BTheGogoBoy2 ай бұрын
Nde zopusazo zimenezo inu simungatukule dziko munakanika kale mukapume
@Brandinah-we2dp2 ай бұрын
Afuna sugar tizizagula pa 20 000 awa 😂😂
@charlesgunda18732 ай бұрын
Kkkkkk this man is dreaming can someone wake him up
@victorauwana72582 ай бұрын
Mu anthu 10 kulilongwe 4 mwa iwo amagwa khunyu ... Here is the example 😅
@eliaskhofielias81522 ай бұрын
😂😂😂 nthawi mkachitsiludi. nanga nthawi yonseyi munali nayoyi mumatani kuzipanga?ntchewa akulira akudziwa kwake kwatha mamama ntima ukumuwawa kut zoonadi Chaka chamawa tikutulukadi m'boma ili tikumadya bwinoli.koma osananama achewa munatasa nazo ndalama zathuzi.koma Aaah kwanu kwatha basi no more mcp next year even mugule anthu you will never get more votes.